BON KALINDO 24 JULY 2024 KUSWANYA BASI PA WEDNESDAY

  Рет қаралды 20,098

Malawi Trends TV

Malawi Trends TV

Күн бұрын

Пікірлер: 76
@KelvinLaudon
@KelvinLaudon 2 ай бұрын
Kuyankhula ndiye mukuyankhula koma anthuwa kusamva big up kalindo your the genuine the DC
@MaxonKambazithe
@MaxonKambazithe 2 ай бұрын
Ngati inuyo a DPP, UDF AND AFORD simugwizana mutaphe matiparty ndinu mutizunzisa koopsya pamene bolani inuyo muli ni ndalama muzatha kuthawa koma ifeee tizangosowa Ngati mmene zinkachikira mu mcp yapitayo😭😭😭😭😭😭 tikulira kodi kumwera kuno singathe kukhala nigwizano wa zipani kupanga chimozi please akaliyati apm,Atupele choonde choonde pangani chimozi zukani tikutha tonse muno please
@AugustineMwamadi
@AugustineMwamadi 2 ай бұрын
Chisankho nthawi zambiri zimatengera amene waimirayo kuti ndi ochuka bwanji kuderalo chisanzo BT wawina wa independent kusonyeza kuti iyeyo ndi amene anali popular mangochi wawina uja ngakhale akanaima pa yekha still akanawina sanabvotere mcp amubvotera munthuyo chimodzi modzi chisankho Cha 2020 anthu anavotera mcp chifukwa Cha chilima namukonda amb
@AffectionateGeyser-fm7dl
@AffectionateGeyser-fm7dl 2 ай бұрын
Zoona ma candidate ena imakhala character siyabwino ndiye anthu savotera the problem is not the party but candidate
@BenPhiri-r8j
@BenPhiri-r8j 2 ай бұрын
Next year MCP might win opposition hasn't been active chiloweleni, so voting ndikumudzi ambiri amayenera kupangidwa convince
@KunyengaMoyo
@KunyengaMoyo 2 ай бұрын
Simukunama opposition ikugona, kmanso Madera omwe avotera MCP mitu yawo sigwira kuno ku Thyolo MCP taikana
@PromiseBonya
@PromiseBonya 2 ай бұрын
Otsusaw akubowa ndipo akupsesa mtim ochenjeza schenjeze bwanji KT amve anthu away eshiiiii
@TanishaLiffa
@TanishaLiffa 2 ай бұрын
The DC 💪
@inamrigala
@inamrigala 2 ай бұрын
apepetula zisilu izi zitayen bon
@HalisonSolomon
@HalisonSolomon 2 ай бұрын
KALINDO NDIYE AKUYANKHULA KOMA KUSAMVA KWA ANTHU OSUSA AGONA AKUFUNA KUWINA ZASANKHO KOMA ALI NDWIIIIII.NGATI AKUMETESA , AKUFUNA KUMENYEREDWA NKHONDO CHONSECHO ANGOKHALA
@BrightNkhoma-xz4bg
@BrightNkhoma-xz4bg 2 ай бұрын
Bon Kalindo 🇲🇼🙏
@FrankMwachande
@FrankMwachande 2 ай бұрын
😂kkk kukhunuka inuyo a opposition seriously .
@DavidJackson-ox4xm
@DavidJackson-ox4xm 2 ай бұрын
The DC'S mwana woooopsa kwambiri akhalise Malawi
@ChimwemweKondowe-nj4lx
@ChimwemweKondowe-nj4lx 2 ай бұрын
Vuto option yikugona kwambiri. Munthu oti akudziwa zoti atha akumenyedwa ndeu, amakonzekera kwambiri, lero ndi izo
@JeniferNyankhomaMndalasini
@JeniferNyankhomaMndalasini 2 ай бұрын
11:07
@MsondaBanda
@MsondaBanda 2 ай бұрын
The Minister Boni Kanindo, you see yourself how these options their mind is just to tuka each other , so it's not solution, Bon you are a big Minister
@ChomboNgosi
@ChomboNgosi 2 ай бұрын
Bon kalindo anayamba kale kuyakula koma position yili ziiii yikutibowaso bwanji😊
@FrankMwachande
@FrankMwachande 2 ай бұрын
True story the DC😢
@EllenPhiri-xt8pt
@EllenPhiri-xt8pt 2 ай бұрын
Koma chilima timuliladi mpakamkapa chifukwa ndiyekhayo anakakhala active analidi msikilikali wa anthu osauka a DPP,UDF,AFORD alibe nazo ntchito iwowo bola zawo zilibwino sagona ndinjala koma akupha ife amalawi osawukafe eeeeeh koma achilima munatisiliyanji ifeee😢😢😢😢😢
@enocklimani1750
@enocklimani1750 2 ай бұрын
The Dc
@AndrewChiponga
@AndrewChiponga 2 ай бұрын
Ase karindo ndi doro maguys chisakho chizavuta chaka chamawa apapa zaonesa kuberedwa
@samanthamuller7643
@samanthamuller7643 2 ай бұрын
awa olo apange zonela anthu akumudzi ananaminza zachimanga koma akumangochi anthu opunsa kwabasi musapangeso zimenezo ku mp ndikuwuzeni ine ndiwina ndipo mangochi zizayivutisa tikawina inu mukavotera mcp yanuyo muziwa Malawi musayelekeze mistake ina mulilanayo anthu awa mene tikuvutikira pano inu zowona kwavutera kodi mvuto lanu ndichani inu achiyao mumazichemelera kuti inu ndaya odzindikira apa mwatani ìnu inu munali ndi mvuto lanji inu ❤Dpp UDF ilikoko zowona inu
@dinchisale
@dinchisale 2 ай бұрын
Akugonadi too much chifukwa amafuna mipando ya u Prezident,
@blessingsnyalo-rp9ko
@blessingsnyalo-rp9ko 2 ай бұрын
A opposition ndizisilu zawanthu😅😅
@dalitson3558
@dalitson3558 2 ай бұрын
A opposition machende awo zoti amalawi akuvutika sakusamala what kinds of opposition parties are these , atikwana kwambiri
@GeraldChisokeza-er5cf
@GeraldChisokeza-er5cf 2 ай бұрын
Auzen adziwe
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 2 ай бұрын
Amalawi apapa a opposition,'wa asatipusise coz dzikoli ndilathu, tiyeni tipange mademo ochosa akhwakhwananda amenewa m'boma mosogozedwa ndi Bon Kalindo, President wathu wa amphawi basii, opposition leaders are scared to be jailed and killed
@FWhite-w3l
@FWhite-w3l 2 ай бұрын
Opposition yonse ndiyausilu mwina akuziwana mpatumbo pa opposition
@KennedyKanyama-ce8lb
@KennedyKanyama-ce8lb 2 ай бұрын
Zaoneselatu kuti DPP yatha. Udf yatha. UTM yatha. Afford yatha. Nanga ichi ndichani? Zoona awawa mmene akudzudzira zikoli alipo angawavotere?
@YamieManda
@YamieManda 2 ай бұрын
Wasowa chonena mkulu iwe ,,athu amawona wokha zothandiza osati zopanda tsogolo zanuzo.mcp mpakanampakana bacedwani mkutukwana kwanuko
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 2 ай бұрын
😂😂😂😂😂😂 boma ilooo , mcp oyeeeeeee 😂😂😂😂😂, mumkatitu mukufuna boma la anyamata oganiza Booo kkkkkkkkkkk chakwela mukati ndi m'busa owopa MULUNGU 😂😂😂, lero ndebwa?, muchiwonatu inuu simunati , ife tinaziona kale nkhanza zawo zinatikwana kale mdzaka zimenezooo, mchifukwa chake timasamza evrytime tikangomva za dzina la chikangawa mcp crocodile dancer party 😂😂😂😂😂, ine lero ndiye ndingoti chakwela yemweyoo , kuti waa waa waa 😂😂😂
@JohnAsendi
@JohnAsendi 2 ай бұрын
Tivomeleze kuti ngati osapanga n'gwilizano ndithu sitingaboole PA Chakwera ochenjera PA sosho midiya shiti
@justinmalala-e4o
@justinmalala-e4o 2 ай бұрын
Koma akudziwa ndalama zomwe chakwela ndi mcp yakeyo awononga chifukwa cha mpando waung'ono ngati umenewu ? Mcp ikufuna anthu aziyesa ngati akukondedwa. Chipani chanzeru sichingaononge ndalama zambilimbili chifukwa cha zinthu zofoila.
@ishmaelsiffah9900
@ishmaelsiffah9900 2 ай бұрын
Amene amaimila ku Mwasa ward pa ticket ya DPP ndimunthu osowa khalidwe anthu sanamuvotele chifukwa chachimenecho,iye uja ndiwaguru la Bam Bam lija limasokoneza pam baluku limamenya anthu lija pomwe uyu anaimila mcp ndimunthu wabwino kwambiri,fact yankhani imenei ndi imeneyo basi,tikamakamba za Bam Bam ndi guru la anthu lomwe linapangidwa kuchokera ku dzina la film ina yake ya anthu osokoneza aku Mexico ena amati B13,anthu amenewa ngati mukukumbukira mmbuyo muja ndi aja anamenya ndikubvula a UTM aja ameneo
@sinethembangubo3718
@sinethembangubo3718 2 ай бұрын
The DC bon kalindo avery dangerous child
@NelsonNdeke
@NelsonNdeke 2 ай бұрын
Opposition is sleeping indeed ali ziiiii!
@GeorgePhiri-ub2of
@GeorgePhiri-ub2of 2 ай бұрын
Or zipani zonse zitasokhana sizingawinen inuyo mcp mmangodananayo chabe ndiye ubwino wake mulungu samakhala kwanu mbuzi inu simunati mulila shupit
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 2 ай бұрын
Opposition leaders osapita kukhoti kukatenga chiletso choti achikangawa akuphwanya malamulo oyendetsela zisankho, nrb sikupanga bwino ndi mabungwe ena ambiri, instead mwangopindilila michila yanuyo mma trouser mwanu , mukufuna kuti amalawi atani komanso mukufuna kuti amalawi awomboledwe kumoto wachikangawu ndindaniiii?
@dondamissonchdziwe3958
@dondamissonchdziwe3958 2 ай бұрын
Eya zivoterani MCP ikumalizani kuku phani Nonse Wanthu opanda mzeru
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 2 ай бұрын
Opposition leaders osamva malangizo awanthu yamtundu wanji?, eish!, bon Kalindo, mtanyiwa alongside bakili muluzi tv akutivumbulusila zinsinsi zomwe asatanic'wa akuchita pobela zisankho , koma inuyo a opposition mwangoti machende phwii osatengapo action iliyonse y?, i think muli gulu limodzi ndila chikangawa inuu and musamawapusise amalawi agalu 🐕🐕🐕 osusa inu, chikangawa yomweyo galu iwee 🐕🐕🐕
@JonaZimpita
@JonaZimpita 2 ай бұрын
Chistilu uyu More Fare MCP wina afune asafune 2030 walila chokweza B,K
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 2 ай бұрын
Bon Kalindo please, pangani mademo oti tichotse guleyu pampando wa u President, munamulemba ntchito ndinu ndipo wayesedwa mayeso and wapezeka kuti walephela , mabwana akefe tikuti achoke basi , awoposition anamachende 😂😂😂
@GeorgePhiri-ub2of
@GeorgePhiri-ub2of 2 ай бұрын
Ndipo inuyo okonda zotukwananu mukhaula mulimbana ndi ma bgy
@MathiasJoseph-xv1hj
@MathiasJoseph-xv1hj 2 ай бұрын
Uwundiuthenga waukulu ku opposition sure
@EusébioLucianoGaiondo
@EusébioLucianoGaiondo 2 ай бұрын
Bon kalindo 🔥🇲🇿
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 2 ай бұрын
Please bon Kalindo, mademo omwe mupangise akhale ochosela chakwela satana ameneyu pampando, atmalizatu amalawife satana ameneyu 👺👹👿☻
@PatrickMkonongo
@PatrickMkonongo 2 ай бұрын
🎉
@DalitsoMatope
@DalitsoMatope 2 ай бұрын
Adad mukugonatu
@IshmailiMkoz
@IshmailiMkoz 2 ай бұрын
Mmera poyamba
@GeorgePhiri-ub2of
@GeorgePhiri-ub2of 2 ай бұрын
Akulu akulu timanena nthawi zonse sosho midia singasinthe kanthu ndale ndi pagiraundi inu mmakhala bze kupeka maboza pano azanu alibze pa galaund mungawine? taonani kularonga anakumenyani 3 zilo koma simabva mukhaula ndipo simunati mcp simungaichose boma
@HastingsNkhoma-q9c
@HastingsNkhoma-q9c 2 ай бұрын
Zoona a opposition akugona
@HappyAbyssinianCat-xt2bm
@HappyAbyssinianCat-xt2bm 2 ай бұрын
Ndpo ndi zoona atsogoleri athu akugona kwambiri kupanga masewera mcp ikhoza kutenga boma, ndpo akatenga boma tizavutika kwambiri, kulankhura ndye anthu mukulankhura km atsogoleri sakumva
@TrizaGeorge-q8w
@TrizaGeorge-q8w 2 ай бұрын
Koma tipephele mulungu asithe nyengo ya ziko lathu posawelengela kuti zikoli ndi la Chakwela koma mulungu azilemekeze yekha kusitha ziko lathu
@ziyamporoma377
@ziyamporoma377 2 ай бұрын
Mau oti “zinthu sizikuenda” is not a political strategy pitani mukawafunse anzanu ku Zimbabwe 🇿🇼…..ndaletu ndikufikira anthu Pa ground osati Pa social media 🤣🤣mulira simunati
@Lee-lee-w1r
@Lee-lee-w1r 2 ай бұрын
Kuyankhula motumbwa chonchi ndikomwe kudachotsetsa DPP mu boma. President wakoyo is even very far from the ground pomwe ukupanenapo. Mutha kuyankhula motumbwa chonchi chifukwa nzachidziwikile kuti chaka cha mawa mukuzalowa mboma mwachinyengo. Koma choti udziwe nchokuti muzachoka mboma muli ndi nkhope zamanyazi kwambili
@ziyamporoma377
@ziyamporoma377 2 ай бұрын
@@Lee-lee-w1rAnkolo mwanvako olo mfundo imodzi from opposition other than kungoti ‘sizikuenda’? Akakhala ma activist ndekumangotukwa daily. Boma ndilomweli basi mufune musafune 🤣
@DeenesNurudMeke
@DeenesNurudMeke 2 ай бұрын
Zomvesa chisoni tu kwambiri esh
@mayesojameskatete
@mayesojameskatete 2 ай бұрын
The D.C. ❤❤❤
@Pangolinimw
@Pangolinimw 2 ай бұрын
Mangochi athu ake alibe selu
@YoungScott-p7e
@YoungScott-p7e 2 ай бұрын
Anthu aku opposition ndi opusa kwambiri
@DeenesNurudMeke
@DeenesNurudMeke 2 ай бұрын
Ndipo kwambiri
@AlbertMatola-u9r
@AlbertMatola-u9r 2 ай бұрын
Zosusa zomwezo 😂😂😂
@Chiso2019
@Chiso2019 2 ай бұрын
Ndipo zoona zikunenedwa apa.....ndi mcp woyeeeeeeee .....kugona too much ku opposition
@MaxonKambazithe
@MaxonKambazithe 2 ай бұрын
Zoona mangochi ndichiani chachika anthunu bwanji nzeru mulibe mukunyengedwa ni deya kodi kumpoto anachita kubera koma inuyo a DPP, UDF, AFORD anthu opanda chikondi chisoni ni wanthu mwandiliza kwambiri mukukonda ndalama osakonda anthu mwatikhumudwitsa kwambiri
@DONNEXKhama-bk1gy
@DONNEXKhama-bk1gy 2 ай бұрын
Zikupwetekesan Mutu izi zitayen
@PhilipMatolino
@PhilipMatolino 2 ай бұрын
The DC zoona ? Apo ndie akubeladi ansaaaa!
@chrisgremu740
@chrisgremu740 2 ай бұрын
Vuto anthunu MCP simuidziwaa
@chrisgremu740
@chrisgremu740 2 ай бұрын
Munyeraaaa
@tingamasi106
@tingamasi106 2 ай бұрын
Tikanyera iwe utiseta
@MatthewLameck
@MatthewLameck 2 ай бұрын
MCP boma ilo 2030 wooooo💃💃💃
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 2 ай бұрын
Government less chikangawa Idiot 😡, tikuchotsani b4 2025 asatana akupha inuu👺👹👿☻
@DeenesNurudMeke
@DeenesNurudMeke 2 ай бұрын
Palibe zimenezo mukunama
@Lee-lee-w1r
@Lee-lee-w1r 2 ай бұрын
Ndipotu zoti muzawina sizachilendo chifukwa tikudziwa muzapanga chinyengo komatu muzaphana agalu inu
@FrancisMakuluni
@FrancisMakuluni 2 ай бұрын
Ndipo live
@YasinMusa-ym8lp
@YasinMusa-ym8lp 2 ай бұрын
Abela mcp koma
Times Exclusive featuring Bon Kalindo - 6 January 2024
1:03:20
Times 360 Malawi
Рет қаралды 256 М.
Who’s the Real Dad Doll Squid? Can You Guess in 60 Seconds? | Roblox 3D
00:34
Running With Bigger And Bigger Lunchlys
00:18
MrBeast
Рет қаралды 137 МЛН
Akweza cement ndi mafuta ophikira kuti apeze ndalama za campaign
9:31
Bakili Muluzi TV
Рет қаралды 48 М.
Pastor Alexander Kambiri "Moto wapathupi umaunva wekha"
18:12
Twin K TV
Рет қаралды 72 М.
LIVE:   DP Gachagua's impeachment trial at Senate
Nation
Рет қаралды 1,4 М.
EXCLUSIVE INTERVIEW WITH BON KALINDO
59:52
Zodiak Malawi
Рет қаралды 93 М.
Who’s the Real Dad Doll Squid? Can You Guess in 60 Seconds? | Roblox 3D
00:34