The Minister Boni Kanindo, you see yourself how these options their mind is just to tuka each other , so it's not solution, Bon you are a big Minister
@ChomboNgosi2 ай бұрын
Bon kalindo anayamba kale kuyakula koma position yili ziiii yikutibowaso bwanji😊
@FrankMwachande2 ай бұрын
True story the DC😢
@EllenPhiri-xt8pt2 ай бұрын
Koma chilima timuliladi mpakamkapa chifukwa ndiyekhayo anakakhala active analidi msikilikali wa anthu osauka a DPP,UDF,AFORD alibe nazo ntchito iwowo bola zawo zilibwino sagona ndinjala koma akupha ife amalawi osawukafe eeeeeh koma achilima munatisiliyanji ifeee😢😢😢😢😢
@enocklimani17502 ай бұрын
The Dc
@AndrewChiponga2 ай бұрын
Ase karindo ndi doro maguys chisakho chizavuta chaka chamawa apapa zaonesa kuberedwa
Akugonadi too much chifukwa amafuna mipando ya u Prezident,
@blessingsnyalo-rp9ko2 ай бұрын
A opposition ndizisilu zawanthu😅😅
@dalitson35582 ай бұрын
A opposition machende awo zoti amalawi akuvutika sakusamala what kinds of opposition parties are these , atikwana kwambiri
@GeraldChisokeza-er5cf2 ай бұрын
Auzen adziwe
@harrisbanda58912 ай бұрын
Amalawi apapa a opposition,'wa asatipusise coz dzikoli ndilathu, tiyeni tipange mademo ochosa akhwakhwananda amenewa m'boma mosogozedwa ndi Bon Kalindo, President wathu wa amphawi basii, opposition leaders are scared to be jailed and killed
@FWhite-w3l2 ай бұрын
Opposition yonse ndiyausilu mwina akuziwana mpatumbo pa opposition
😂😂😂😂😂😂 boma ilooo , mcp oyeeeeeee 😂😂😂😂😂, mumkatitu mukufuna boma la anyamata oganiza Booo kkkkkkkkkkk chakwela mukati ndi m'busa owopa MULUNGU 😂😂😂, lero ndebwa?, muchiwonatu inuu simunati , ife tinaziona kale nkhanza zawo zinatikwana kale mdzaka zimenezooo, mchifukwa chake timasamza evrytime tikangomva za dzina la chikangawa mcp crocodile dancer party 😂😂😂😂😂, ine lero ndiye ndingoti chakwela yemweyoo , kuti waa waa waa 😂😂😂
@JohnAsendi2 ай бұрын
Tivomeleze kuti ngati osapanga n'gwilizano ndithu sitingaboole PA Chakwera ochenjera PA sosho midiya shiti
@justinmalala-e4o2 ай бұрын
Koma akudziwa ndalama zomwe chakwela ndi mcp yakeyo awononga chifukwa cha mpando waung'ono ngati umenewu ? Mcp ikufuna anthu aziyesa ngati akukondedwa. Chipani chanzeru sichingaononge ndalama zambilimbili chifukwa cha zinthu zofoila.
@ishmaelsiffah99002 ай бұрын
Amene amaimila ku Mwasa ward pa ticket ya DPP ndimunthu osowa khalidwe anthu sanamuvotele chifukwa chachimenecho,iye uja ndiwaguru la Bam Bam lija limasokoneza pam baluku limamenya anthu lija pomwe uyu anaimila mcp ndimunthu wabwino kwambiri,fact yankhani imenei ndi imeneyo basi,tikamakamba za Bam Bam ndi guru la anthu lomwe linapangidwa kuchokera ku dzina la film ina yake ya anthu osokoneza aku Mexico ena amati B13,anthu amenewa ngati mukukumbukira mmbuyo muja ndi aja anamenya ndikubvula a UTM aja ameneo
@sinethembangubo37182 ай бұрын
The DC bon kalindo avery dangerous child
@NelsonNdeke2 ай бұрын
Opposition is sleeping indeed ali ziiiii!
@GeorgePhiri-ub2of2 ай бұрын
Or zipani zonse zitasokhana sizingawinen inuyo mcp mmangodananayo chabe ndiye ubwino wake mulungu samakhala kwanu mbuzi inu simunati mulila shupit
Koma tipephele mulungu asithe nyengo ya ziko lathu posawelengela kuti zikoli ndi la Chakwela koma mulungu azilemekeze yekha kusitha ziko lathu
@ziyamporoma3772 ай бұрын
Mau oti “zinthu sizikuenda” is not a political strategy pitani mukawafunse anzanu ku Zimbabwe 🇿🇼…..ndaletu ndikufikira anthu Pa ground osati Pa social media 🤣🤣mulira simunati
@Lee-lee-w1r2 ай бұрын
Kuyankhula motumbwa chonchi ndikomwe kudachotsetsa DPP mu boma. President wakoyo is even very far from the ground pomwe ukupanenapo. Mutha kuyankhula motumbwa chonchi chifukwa nzachidziwikile kuti chaka cha mawa mukuzalowa mboma mwachinyengo. Koma choti udziwe nchokuti muzachoka mboma muli ndi nkhope zamanyazi kwambili
@ziyamporoma3772 ай бұрын
@@Lee-lee-w1rAnkolo mwanvako olo mfundo imodzi from opposition other than kungoti ‘sizikuenda’? Akakhala ma activist ndekumangotukwa daily. Boma ndilomweli basi mufune musafune 🤣
@DeenesNurudMeke2 ай бұрын
Zomvesa chisoni tu kwambiri esh
@mayesojameskatete2 ай бұрын
The D.C. ❤❤❤
@Pangolinimw2 ай бұрын
Mangochi athu ake alibe selu
@YoungScott-p7e2 ай бұрын
Anthu aku opposition ndi opusa kwambiri
@DeenesNurudMeke2 ай бұрын
Ndipo kwambiri
@AlbertMatola-u9r2 ай бұрын
Zosusa zomwezo 😂😂😂
@Chiso20192 ай бұрын
Ndipo zoona zikunenedwa apa.....ndi mcp woyeeeeeeee .....kugona too much ku opposition
@MaxonKambazithe2 ай бұрын
Zoona mangochi ndichiani chachika anthunu bwanji nzeru mulibe mukunyengedwa ni deya kodi kumpoto anachita kubera koma inuyo a DPP, UDF, AFORD anthu opanda chikondi chisoni ni wanthu mwandiliza kwambiri mukukonda ndalama osakonda anthu mwatikhumudwitsa kwambiri
@DONNEXKhama-bk1gy2 ай бұрын
Zikupwetekesan Mutu izi zitayen
@PhilipMatolino2 ай бұрын
The DC zoona ? Apo ndie akubeladi ansaaaa!
@chrisgremu7402 ай бұрын
Vuto anthunu MCP simuidziwaa
@chrisgremu7402 ай бұрын
Munyeraaaa
@tingamasi1062 ай бұрын
Tikanyera iwe utiseta
@MatthewLameck2 ай бұрын
MCP boma ilo 2030 wooooo💃💃💃
@harrisbanda58912 ай бұрын
Government less chikangawa Idiot 😡, tikuchotsani b4 2025 asatana akupha inuu👺👹👿☻