BON KALINDO LERO PA 12 JULY 2024 | KUPITILIRA KUNG'ALURA |

  Рет қаралды 32,541

DZIWE TV

DZIWE TV

Күн бұрын

Пікірлер: 148
@RonaldBanda-n5e
@RonaldBanda-n5e 2 ай бұрын
Thanks sir for ur update
@loycekachy3370
@loycekachy3370 2 ай бұрын
Wamisala anaona nkhondo,,lero Bon kalindo mukumuyamikila koma mmene munkamunyozela siizi😂😂😂😂
@StanleyChirwa-d6b
@StanleyChirwa-d6b 2 ай бұрын
Ati amakutengan ngat manyi😂😂😂😂 chi booooniiiiii kalindoooo
@TaongaChibuwu
@TaongaChibuwu 2 ай бұрын
Zikomo bwana DC UTM yitulukedi kumeneko iyime pa yokha basi
@fosternyirenda-wo4eb
@fosternyirenda-wo4eb 2 ай бұрын
Good advice sir.
@JonesMwera
@JonesMwera 2 ай бұрын
Uyu ndiye activits yemwe timamudziwa, Bon kalindooooooo!! Mwana owopsa kwambiri.
@DarlingtonKamando
@DarlingtonKamando 2 ай бұрын
Your the best the DC bon kalindo❤
@MaxWell-d7o
@MaxWell-d7o 2 ай бұрын
Yomweyo fadaa🎉
@HenryMbawa-v9u
@HenryMbawa-v9u 2 ай бұрын
🎉🎉🎉 following
@stelladolizyi
@stelladolizyi 2 ай бұрын
Kuyankhula mopanda mantha ngati wakhalira mfuti Bon kalindo 😮😮
@OscarChizula-qr4bi
@OscarChizula-qr4bi 2 ай бұрын
Ndpo inu
@ChikondiKachaso-ox5ng
@ChikondiKachaso-ox5ng 2 ай бұрын
Bon kalindo amalankhula zoona zokhazokha koma anthufe timangoti ndi wama comedy let's support him as malawians
@ellensambo6323
@ellensambo6323 2 ай бұрын
Uyu ndiye ❤
@OscarChizula-qr4bi
@OscarChizula-qr4bi 2 ай бұрын
Salute
@BlessingsMpondaphiri
@BlessingsMpondaphiri 2 ай бұрын
Good advise Mr born kalindo thank you 😅
@KhondanKhondan
@KhondanKhondan 2 ай бұрын
Kalindo amatha kwambili❤
@SmileMalanda
@SmileMalanda 2 ай бұрын
The DC🔥🔥🔥
@KondwaniMwasinga-rs6kv
@KondwaniMwasinga-rs6kv 2 ай бұрын
Born kalindo🔥🔥🔥🎷🎷
@yamikanikamboyi8686
@yamikanikamboyi8686 2 ай бұрын
The DC
@AubreyTrust
@AubreyTrust 2 ай бұрын
God bless you Kalindo
@BlessingsPhiri-fv5gs
@BlessingsPhiri-fv5gs 2 ай бұрын
Umakwana
@SanudiKambona
@SanudiKambona 2 ай бұрын
I love you so much
@SolomonMbewe
@SolomonMbewe 2 ай бұрын
DPP+UTM+UDF+AFORD.... MCP out 2025..
@JosephLunga-e7q
@JosephLunga-e7q 2 ай бұрын
Always your the best all the time mr president Bonie Kalindo
@AlinafeSolomoni
@AlinafeSolomoni 2 ай бұрын
True
@DoricaGoweka
@DoricaGoweka 2 ай бұрын
President wathu wathu,Mr Kalindo lero ndilomwe tidziwedi kuti UTM ipitilira ndipo SKC waphera chilungamo.
@jeladiaustain
@jeladiaustain 2 ай бұрын
❤❤❤❤❤❤❤
@ArnoldKamanga-r6k
@ArnoldKamanga-r6k 2 ай бұрын
Tikumupemphani a Born kalindo bwelelani ku UTM please
@LuundoJohnkabage
@LuundoJohnkabage 2 ай бұрын
Ndipo president akakhale iyeyu ndimunthu wamaso mphenya❤❤we love him❤
@justinmalala-e4o
@justinmalala-e4o 2 ай бұрын
What if mrs Chilima is not a politician? Komanso akuti anthu azilowa kuchipinda ndi candle nkumakatchula dzina la Chilima kodi Chilimayo wasandukano mulungu?
@priscillamangata4023
@priscillamangata4023 2 ай бұрын
President wathu Mr DC
@PatrickSomanje
@PatrickSomanje 2 ай бұрын
U always stand in true mr Bon l love u more than
@JamesMatupi
@JamesMatupi 2 ай бұрын
Ndiwamisala daily ma audio Iya ndimbuzi President osauka kwanu konko
@MathewsChitambe
@MathewsChitambe 2 ай бұрын
Uzifuse wekha kut ndi angat omwe akumuyamikila,? Nanga omwe akumunyoza n angat?
@JamesMatupi
@JamesMatupi 2 ай бұрын
@@MathewsChitambe zako zimenezo cadet ine ayi ok. Your opinion is not my opinion. Ine yanga ndi MCP basi
@GeraldChikalema
@GeraldChikalema 2 ай бұрын
In short Utm ibwerere ku DDP....tigwetse vinyau tikinze dziko
@valenceemmanuel74
@valenceemmanuel74 2 ай бұрын
Like this guy or not , but he is very sharp
@MasterBlack-r2n
@MasterBlack-r2n 2 ай бұрын
boooooon kalindo!
@AlbertEngelbercht
@AlbertEngelbercht 2 ай бұрын
Kalindo is trying his best,chikufunika osusa agwirane manja!,ku UTM apereke mpata kapena position imene Mary chilima angatenge icho chiperekeranso mphanvu ina yapadera muchipani.
@GoodsonfahardMaganga-qc2qk
@GoodsonfahardMaganga-qc2qk 2 ай бұрын
Big up to you 🎉🎉🎉🎉🎉 umatha kung'alura
@macfordmbama7862
@macfordmbama7862 2 ай бұрын
Good advice
@TalazanGamah
@TalazanGamah 2 ай бұрын
Powerful spetch
@ListonFrancis
@ListonFrancis 2 ай бұрын
Mbambande Bon Kalindo
@HassaniHassani-yr2rf
@HassaniHassani-yr2rf 2 ай бұрын
THE DC PANGOLINI 💪💪💪💪💪
@HawaHussein-d4l
@HawaHussein-d4l 2 ай бұрын
Mumaitha bwana d c ndi more pachilungamo😊
@anicakandiado
@anicakandiado 2 ай бұрын
Kulankhula mwachilungamo. UTM tsegulani maso. Tulukani mu tonse alliance monga akunenela Bon Kalindo please. A MCP asakupusitseni ife tili mbali yanu ndi SKC osaopa, osatopa, osafooka 💪
@MathewsChilenje
@MathewsChilenje 2 ай бұрын
Umaitha bon
@OmegaChingamuka
@OmegaChingamuka 2 ай бұрын
Koma Mai kaliyati ndi kagulu kanu choonde nvelani kulira kwa anthu ngati ku UTM kuli anthu olimba nde ndinuyo mumakhala chifupi ndi Chilima musakomedwe ndi ndalama mukwiitsa anthu ochuluka nthawi yatha kale iyi musanvere MCP kukunyengeleleni ndi ndalama misozi ili manso ndithu mutenga tsoka
@MathewsChitambe
@MathewsChitambe 2 ай бұрын
Zoona mb'ale
@FrankAndsen
@FrankAndsen 2 ай бұрын
Khan nd yoona
@LucyMasiku
@LucyMasiku 2 ай бұрын
Mr Kalindo mukutitsegula mmaso kwabasi keep it up
@JamesChiphwanya-m4v
@JamesChiphwanya-m4v 2 ай бұрын
Komatu bon kalindo amayakhula ngati wamisa koma ndizoonadi zimene amayakhula anhtu inu muzichenjera
@PempheroAlufandika
@PempheroAlufandika 2 ай бұрын
Mumatiimilira a bon
@AhmadShariff-bk3rr
@AhmadShariff-bk3rr 2 ай бұрын
Tiyeni tiyeni tiyeni Mr DC
@Mussa-qs7km
@Mussa-qs7km 2 ай бұрын
Good Good news
@fahadmilanzi
@fahadmilanzi 2 ай бұрын
Kalindo amalankhula zoona uyu ndi mpulutsi.
@MarvGerald
@MarvGerald 2 ай бұрын
A UTM uthenga ndiumeneo zili ndiinu kunyalanyaza kapena kutengapo kanthu km mawa pangatalike muzawakumbukira mau a Bon sadutsa pachabe
@AgnessMzengo
@AgnessMzengo 2 ай бұрын
Wise man
@ChristopherChimbalanga-ez5he
@ChristopherChimbalanga-ez5he 2 ай бұрын
Kmat uyu tiyen Tzimuvela zimene amayankhulaz
@priscillamangata4023
@priscillamangata4023 2 ай бұрын
The DC agogo anga akufuna azakuoneni
@MaxwellMakoka
@MaxwellMakoka 2 ай бұрын
Mr DC 2025 woyyeee.
@TamalaMwamlima-gk5im
@TamalaMwamlima-gk5im 2 ай бұрын
Chilungamo chimamasula go ahead the DC
@SaidiMbawa-st6bj
@SaidiMbawa-st6bj 2 ай бұрын
Utm siingatuluke mugwilizano ngakhaleso atatuluka palibe chazelu chomwe angapeze
@AndrewMbewe-yp7kg
@AndrewMbewe-yp7kg 2 ай бұрын
Usazafe kalindo uzangotsowa ngati eliya
@MartinMajola
@MartinMajola 2 ай бұрын
DC Huma kwana
@sydemsamude190
@sydemsamude190 2 ай бұрын
the dc
@alexmkolongo3089
@alexmkolongo3089 2 ай бұрын
Koma manganya asamuwelengele ndiwa MCP kuyambila kale
@InnocentMatemba-y1k
@InnocentMatemba-y1k 2 ай бұрын
Big up de DC our pool p
@PeterMalizan
@PeterMalizan 2 ай бұрын
The DC mulomwe wathuwathu odziwa zinsinsi
@greymasha838
@greymasha838 2 ай бұрын
Bwana DC mumatiimilira
@MussaAmadu-o9f
@MussaAmadu-o9f 2 ай бұрын
Very true
@OwamiSimeon
@OwamiSimeon 2 ай бұрын
Kalindo more 🔥 ❤
@MaxwellumbiriLumbiri
@MaxwellumbiriLumbiri 2 ай бұрын
Bon kalindo umakamba zoona
@KelvinNamowa
@KelvinNamowa 2 ай бұрын
The DC😊
@chifundobuledi
@chifundobuledi 2 ай бұрын
🎉More fire!!!!!!!!!!!
@AndreaSignala-hk2yg
@AndreaSignala-hk2yg 2 ай бұрын
It's true bwana president woyamba wa anthu osauka muno Malawi
@Martha-m6e
@Martha-m6e 2 ай бұрын
Mzimu wa bwana Chilima uwavuta.mukaone maruwa ngati akukanika kufa .musamale kwambilitu.
@WestonGawaza
@WestonGawaza 2 ай бұрын
Bon kalindo akunena zowona lelo muchoke ku mcp mukapitiliza ndiye kuti mukusangalala ndi ife ya chilima chipani chimene chingawine ndi UTM kampeni wake zikolose lapasi lipanga saport
@LenoMvula
@LenoMvula 2 ай бұрын
My vote kalindo umatha umatiimirila
@GeorgePhiri-ub2of
@GeorgePhiri-ub2of 2 ай бұрын
Mbuzi iwe takudziwa akutuma adpp chitsilu chamunthu DPP UDF aford zonse izo palibe ndimakampani amabanja
@BlessingsMaheya
@BlessingsMaheya 2 ай бұрын
Sanena boza uyu
@WestonGawaza
@WestonGawaza 2 ай бұрын
Mayi chilima to be president, braund banda,mwana wachilima awa kaliyati, awa musankhemo mumozi ankhale president mwana wa chilima anyamata ose ankhala ndi chidwi
@PachaloShaba-pf5vw
@PachaloShaba-pf5vw 2 ай бұрын
Umakwana winiko
@CaptainNyenga
@CaptainNyenga 2 ай бұрын
UTM ithetse ngwilizano kut zawo zikhakebe oabwino
@LottiAffati
@LottiAffati 2 ай бұрын
kalindo umakwana ase
@BensonChakalamba-db7uf
@BensonChakalamba-db7uf 2 ай бұрын
The problem is anthu akumudz unthengawu suwapeza cz of social media
@TrizaGeorge-q8w
@TrizaGeorge-q8w 2 ай бұрын
Ndipo a mcp ndi athu ochenjela ndi kuipa komwe ndipo chilima amusasa lelo akuyanja otsalao mukapusa akumezani
@khuzenigunya
@khuzenigunya 2 ай бұрын
Kalindo good advice
@Homeofpeace321
@Homeofpeace321 2 ай бұрын
Gibo Pearson wachita misala, is zikumveka kuti zadza kamba kangozi ija
@OscarChizula-qr4bi
@OscarChizula-qr4bi 2 ай бұрын
Iwe ulongosoke
@MartinMajola
@MartinMajola 2 ай бұрын
Manganya yunda sikalioti
@YasinMusa-ym8lp
@YasinMusa-ym8lp 2 ай бұрын
Dc 🎉🎉🎉🎉
@willardkajalika-m8g
@willardkajalika-m8g 2 ай бұрын
😹😹😹 iwe umakwana aaa nilinje mau
@AnnieMuliya-n5s
@AnnieMuliya-n5s 2 ай бұрын
Mumatha
@PeterRabson-z3w
@PeterRabson-z3w 2 ай бұрын
Kalindo your a king and good adviser i salute you always ,many thanks to you and may god protect you
@josephphiri564
@josephphiri564 2 ай бұрын
Ah b
@OsumaniJaffali
@OsumaniJaffali 2 ай бұрын
Amakwana koma ❤
@MerryWayson
@MerryWayson 2 ай бұрын
Na pa Bone Kalindo palibeso same same Mtanyiwa anthu awa amanena chilungamo chokhachokha
@MaryPanje
@MaryPanje 2 ай бұрын
Makwana mr keep it up
@WestonGawaza
@WestonGawaza 2 ай бұрын
Brayani Banda ndimunthu wa chikondi ndi ziko Lake mayi cilima tiwona ngati chilimayo alipo anthu tivota ambiri mwana wachilima anakonda achinyamata ndiye achinyamata ose ali ndi ife
@IshallahMwanyali
@IshallahMwanyali 2 ай бұрын
The DC kkkk konda u ife
@Moses51
@Moses51 2 ай бұрын
The Dc bon kalindo 🎉🎉🎉
@WisikiBlack-gj4gu
@WisikiBlack-gj4gu 2 ай бұрын
Musapusisidwe a utm mcp sichipani .muzifunse kuti kodi chilima chamupha ndichani kodi mukugona a utm, tsegulani mumaso
@Shelifibraheem
@Shelifibraheem 2 ай бұрын
Our freedom fighter ndiwe kawawa ndithu
@MuhammadSamson-yz1kl
@MuhammadSamson-yz1kl 2 ай бұрын
A UTM mukapanda unvera za bon kalindo muzalira moyo wanu onse
@antiepogba1534
@antiepogba1534 2 ай бұрын
The DC mwana ohopya kwambili
@ChrifordBiziel
@ChrifordBiziel 2 ай бұрын
Palibepo zomwe mukulusapo zazelu zimodz modzi zosavekaso mkomwe
This mother's baby is too unreliable.
00:13
FUNNY XIAOTING 666
Рет қаралды 29 МЛН
Life hack 😂 Watermelon magic box! #shorts by Leisi Crazy
00:17
Leisi Crazy
Рет қаралды 76 МЛН
Kluster Duo #настольныеигры #boardgames #игры #games #настолки #настольные_игры
00:47
A DPP Ku Parliament Mupite Okonzeka  - Bon Kalindo
17:57
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 16 М.
Chimwendo amafuna kulepheletsa mwambo wa Mulakho wa Alomwe
4:39
Bakili Muluzi TV
Рет қаралды 57 М.
Maloto A Bon Kalindo (Part 2) - Bon Kalindo
14:17
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 120 М.
Watondeka; Chitukuko kulibe ku Malawi; Fetereza wadura kwambiri
15:19
Bakili Muluzi TV
Рет қаралды 43 М.
This mother's baby is too unreliable.
00:13
FUNNY XIAOTING 666
Рет қаралды 29 МЛН