CHACHITIKA NDI CHANI NDI BAKILI MULUZI TV PA FACEBOOK NKHANI YONSE ZAKHALA BWANJI KODI

  Рет қаралды 26,545

Malawi Trends TV

Malawi Trends TV

Күн бұрын

Пікірлер: 218
@ImranWyson-e9o
@ImranWyson-e9o 3 күн бұрын
Akung'alula ndithu😂😂😂 Best TV ever
@MandalaChaona
@MandalaChaona Сағат бұрын
🤣🤣🤣🤣🤣 Koma Ziliko liko komabe Utsogoleri usinthidwa. Anyway I love BAKILI MULUZI TV, History is the best teacher ✍️✍️
@DantonKaipa-v8i
@DantonKaipa-v8i 2 күн бұрын
Kutheka ndi yemweyu, pajatu chilungamo chimasakanikilana ndi mwana.l always proud with bmtv he is real the best teacher, now and forever.
@YusufAjida-t8r
@YusufAjida-t8r 3 күн бұрын
Zachamba izi akufuna kuononga Zina la bakili muluzi TV koma akunama kwambili Ana achepa timamukonda ❤❤❤❤ kwambili bakili muluzi TV
@PromiseSaidi
@PromiseSaidi 5 сағат бұрын
Mn akupanga post ekha bakili muluzi tv km chifukwa chachikulu ndichoti bakili muluzi tv amakonda DPP ndie dalitso kabambe wakana kupanga alliance ndi chipani cha DPP
@msatisi.reangfordphiri
@msatisi.reangfordphiri 3 сағат бұрын
​@@PromiseSaidinde moti a Kabambewo akuti ali nayo 50+1 yotchaira Chimwendo?
@LeonardEnock-e1t
@LeonardEnock-e1t 3 сағат бұрын
Bakili muluzi tv anayamba nkale kumung'alura chilima anangosiya apa atamwaliramu koma ndiyemweyu ndinthu BMT 😅😂
@SulaimanIssa-b2h
@SulaimanIssa-b2h 2 сағат бұрын
Ea ndima haka amene aja ineso ndavera nawo muli zofooka zambili zimene zikusonyeza kut siwa bakili muluz tv
@yusufu-g6e
@yusufu-g6e 3 күн бұрын
iyi Nd bakli muluz TV yaa mcp
@LinlyMathewe
@LinlyMathewe 6 сағат бұрын
Kaya ndi yemweyu Kaya zopeka but never give up UTM my vote ❤❤❤
@SulaimanIssa-b2h
@SulaimanIssa-b2h 2 сағат бұрын
Ayi sibakili muluz TV ndi mahaka amene aja. Muivele bhobho ndi fake voice. Page imene ija yapangidwa haki ndi athu a boma ndiofina kuononga chipani cha utm. Ndiye choyamba akuyenera kuipisa mbili ya chilima. N mu audio imene ija muli zofooka zambili zimene zikupeleka chikhulupililo kut siwa bakili muluz TV
@denndavie6041
@denndavie6041 3 күн бұрын
Ndipo ineyo chilima sindingamu bakile. He was indeed a bad guy with Lucius Banda.
@HOMEAWAY-h7t
@HOMEAWAY-h7t 3 күн бұрын
The ever best tv in mw we still love the people who are manengng this ❤❤❤
@ThokoMsonkho-hy4uc
@ThokoMsonkho-hy4uc 3 күн бұрын
Pamene page yomweyo ikawulutsa nkhani ya maliro a Chilima mumati ndiyabwino chifukwa akangofuna kukuthandizani kuti a UTM mumuziwe CHAKWERA pazomwe amapanga Chilima kufikira imfa yake. Koma kunena chilungamo inenso ndinamuona kuti Chilima uja anali wamwano ndiponso anali chitsilu pa ndale. Kuzichotsa yekha kwa PETER kenako kudzalumikizana ndi Chakwera pamene paja anapusa pa ndale potengera mbiri ya MCP mbuyomu. Munthu amapanga mistake koma pokhapa ndimamukonda kuti ndiwadyera komanso ndiwamwano ndinso alibe nzeru zautsogoleri. Mmene amamulankhulira BAKILI MULUZI purezideti wapuma uja ndinamuwona kuti tsogolo panalibepo mwa iye. Anali wa mwano kwa akuluakulu amayenera kumwalira basi
@Ayanali-cr4vy
@Ayanali-cr4vy 2 күн бұрын
UTM sichipani chomasapota Atupele Muluzi my Vote
@MathewKalinkhu
@MathewKalinkhu 3 күн бұрын
Kunena zoona, Bakili Muluzi tv alibe mbali, amayamikila pamene pali bwino, komanso amadzudzula polakwikapo.
@WilsonNedi-s6t
@WilsonNedi-s6t 3 күн бұрын
Siwa bakili muluzi ameneyo anthunu musakhulupilire
@petertengani
@petertengani 6 сағат бұрын
Zatembenuka, ng'ombe zayang'ana ku joko. Yomweyo... 😆😆🤦🏽‍♂️❤️.
@AlfredGanizani-v9f
@AlfredGanizani-v9f 3 сағат бұрын
😅😅 tingodikira kut give zambili my vote to my chakwera is number one
@wisdomlimbe9483
@wisdomlimbe9483 3 күн бұрын
Olo zitakhala zoona, who cares about DK's private life? All I know he can run the economy way better than the current situation. Malawi is not looking for munthu yemwe sananyengepo. Tikufuna munthu woti atsogolere kukonza chumachi kuti wolimbikira azidya thukuta lake. Enafe we don't care kaya akhala Chakwera yemweyi, kaya Enock Chihana, kaya APM, kaya Atupele kaya DK, kaya wa Bakili Muluzi
@usherjamson174
@usherjamson174 3 күн бұрын
Amene waja ndichi machine 😂🎉
@HenryNanthuwa
@HenryNanthuwa 3 күн бұрын
Nosense get lost bakili muluz zoputsatu izi
@NenaniMoyenda
@NenaniMoyenda 3 күн бұрын
Ma pulopaganda a MCP awa ndipo BMT akangotukila musambulidwa🤣
@GeoffreyMarko-v3s
@GeoffreyMarko-v3s 3 күн бұрын
Chilima anasocheresa dzikoli😢😢😢😢😢
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 3 күн бұрын
Akubweletsa nkhanizi siwa bakili muluzi tv, ndiena mwa afisi achikangawa kufuna kuipisa ndikuononga mbili ya utm , komabe tinene mosapsyatila pano , chilima ndamene anationongesela malawi wathuyu , after all anangoti duuuuu ngati akumetedwa osafuna kususa nkhanza zomwe zilimdziko , nayenso chikangawa kukapha mzake pambuyo poti amabela limodzi y?, y dd u do dat chikangawa?
@MorrisDzonzi
@MorrisDzonzi 2 сағат бұрын
Zazii kumudetserela Kabambe akumuopa awa,,Zonse nchabe koma Chakwera walephera achoke basi
@WilliamNhlane-fd9hi
@WilliamNhlane-fd9hi 3 күн бұрын
I don't think this is bakili muluzi , awa ndi mcp akufuna tisalankhule imfa yachilima .
@EmmanuelkpPraise
@EmmanuelkpPraise 3 күн бұрын
Aaa zazii uyu si wabakili muluxu tv
@SulaimanIssa-b2h
@SulaimanIssa-b2h 2 сағат бұрын
Ea ndima haka amene aja. Akayambileso. A mcp amaonatu ngat amalawi ngogona kwabasi kkkk
@harrymicah6140
@harrymicah6140 3 күн бұрын
😂😂😂😂 uyu nde ndakayika kut ndi Bakaili muludzi ukadusa wez history is the best teacher aa tabwali uyu
@AlexanderTraffick
@AlexanderTraffick 3 күн бұрын
Nkhani izi zokomera Kwa Anthu atambara wakuda.mcp
@RinosChilumpha-y2d
@RinosChilumpha-y2d Сағат бұрын
Zimachitika koma bakili muluzi TV sayimila mbali ai palipose amang'alula bass
@FrancisNyayi
@FrancisNyayi 4 сағат бұрын
Who said ahhhh Like me here when listening
@TaniaMphalumo
@TaniaMphalumo 2 күн бұрын
Ayi.izi akupanga ndi mayiko usi ngati simukuziwatu ndi manganya akupanga zosezi😊
@MathewKalinkhu
@MathewKalinkhu 3 күн бұрын
This is the best station
@GoodluckVithumbiko
@GoodluckVithumbiko 3 күн бұрын
Anthu woputsa inu asatana kupusa anachikangawa kufuna kutiwonongera utm yathu makape inu kupusa ndawononga bandle yanga panyo pani
@MetuseSelai
@MetuseSelai 3 күн бұрын
Bakili muluzi tv alibe Facebook account km Instagram basi
@ShoryenNgumuya
@ShoryenNgumuya 3 күн бұрын
Km yaaa ziliko kumalawi
@MuhammadAlie-b7v
@MuhammadAlie-b7v 2 сағат бұрын
Uyu si bakili muluzi tv
@SkevaMustapher
@SkevaMustapher 3 күн бұрын
Amene uja si bakili muluz tv tikumudziwa ife ayi akusiyanilatu kwambili
@PreciousBenes
@PreciousBenes 2 күн бұрын
Dk my vote
@ChrispineMuzungu-l8h
@ChrispineMuzungu-l8h 2 күн бұрын
History is the best teacher 🎉🎉
@EDSONMahamand-v2z
@EDSONMahamand-v2z 3 күн бұрын
Aise ulemu wako umalongosola moveka bwino zaveka bwino kwambili
@AbdulsharifulKalipinde-m6u
@AbdulsharifulKalipinde-m6u 2 күн бұрын
Uyuyu ndi munthu ong'alura basi Sayendela kuti uyu ndi ndani
@SaimonBanda-ez6km
@SaimonBanda-ez6km 12 сағат бұрын
Komano saknama bakili tvi 🎉❤
@abdulsalammkwepu3321
@abdulsalammkwepu3321 3 күн бұрын
History is the best teacher
@marryphili5419
@marryphili5419 3 күн бұрын
Ndiwe galu kwabasi sindiwe bakili muluzi TV mungofuna kungowononga mbiri zazipani zisiru inu
@bridgetmajor3646
@bridgetmajor3646 3 күн бұрын
Uyu siwa Bakili tv...zaboza izii mwayitani.....Bm tv za chamba basi
@DanMhone-iw6xg
@DanMhone-iw6xg 3 күн бұрын
Agalu a MCP awa
@SydneyMwale-u9w
@SydneyMwale-u9w 3 күн бұрын
Fake news
@HamdanMaleta
@HamdanMaleta 3 күн бұрын
Chilima anali opoila kwambiri
@AbdulsharifulKalipinde-m6u
@AbdulsharifulKalipinde-m6u 2 күн бұрын
Akabambe akuchepa kwambiri kuyelekedza ndi Bakili Muluzi tv
@LeyvanSamuel-pe5tc
@LeyvanSamuel-pe5tc 3 күн бұрын
I like to listening BMTV 🔥
@RoseThindwa
@RoseThindwa 3 күн бұрын
History is the best teacher
@StephanoMussa-q6d
@StephanoMussa-q6d 3 күн бұрын
Bakili muluzi guys wagudwa Inu simukudabwa ma videos ake for the past two weeks mmene akumvekela? Guys wake up everybody has price
@lastonmasoatenganji-bs5gf
@lastonmasoatenganji-bs5gf 3 күн бұрын
Si wa Bakili Muluzi uyu mpang'ono pomwe. Olo mdani atakuchimwira chotani ndipo kwa nthawinso yoyamba, ungayankhulirenji zonsezi ngati kulibe mawa?
@AngolaChinga
@AngolaChinga 3 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂 wakhaula uyu si wabakili muludzi tv
@SulaimanIssa-b2h
@SulaimanIssa-b2h 2 сағат бұрын
Kkķkkkk nane ndaivela so muli zofooka zambili
@ElizabethMulinde
@ElizabethMulinde 3 күн бұрын
Uyu sibakili muluzi tv
@LaynaAdam
@LaynaAdam 3 күн бұрын
Mmmmmmmmm siwa bakili tv ameneyo ndi munthu wina
@HarryMsudzula
@HarryMsudzula 3 күн бұрын
Bakili Muluzi tv is not God cancel him in your mind be careful ndiye sitikavota if it is that
@MathewKalinkhu
@MathewKalinkhu 3 күн бұрын
Chilima anawononganawo dziko la Malawi, kupupuluma Chilima, that's why anamupha.
@uzaleuzale8603
@uzaleuzale8603 3 күн бұрын
Chimashini chija chayamba kugwira ntchito mukatero😂
@GabrielMuziDlamini
@GabrielMuziDlamini 3 күн бұрын
Komabe sikudwisa big kuti ngati sanamuhaki😢
@Hdsagdf-t1n
@Hdsagdf-t1n 3 күн бұрын
Munamiza ana kodi kkkk mwanya
@AbdulsharifulKalipinde-m6u
@AbdulsharifulKalipinde-m6u 2 күн бұрын
Let's gathering here Iyiyi ndiye yeni yeni TV
@AllanChabwela
@AllanChabwela 2 күн бұрын
siyabakili muluzi
@AbelShaba
@AbelShaba Күн бұрын
Mmmm kwesi koma B TV wadya chibanzi
@ShukuraniTonex
@ShukuraniTonex 3 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂😂
@MiddayDeleza
@MiddayDeleza 3 күн бұрын
I don't think that this is Bakili Muluzi TV kaya mwina
@EmilyKanyika
@EmilyKanyika 3 күн бұрын
Machimo
@ChavuksFrancois
@ChavuksFrancois 3 күн бұрын
Nkhani zonsezo a Malawi akudzidziwa, kaya chilimayo, kaya Kabambe a Malawi akuwadziwa. Nkhani za personal sizingasinthe chilichonse kwa a Malawi zotsatira UTM
@Gwedeza-q3f
@Gwedeza-q3f 2 күн бұрын
Ndi bodza ili ndi propaganda ya mcp, uyu siwaBakili muluzi TV 😂😂😂😂😂 ndidzabodza ndi aganyu awa a mcp
@mbelengamavuto2517
@mbelengamavuto2517 3 күн бұрын
Zosamveka izi mukuyakhulazi
@KnowxySainet
@KnowxySainet 6 сағат бұрын
Uyuu c bakili TV weniweni anthu a mcp awa muone kumapeto kwake akukakamila mau oti history is best teacher nonsese
@ishaqyassin5001
@ishaqyassin5001 5 сағат бұрын
Ubwino wake Chisale ndi wa kuba Kabambe mbava ya munthu
@isaaczuze
@isaaczuze 3 күн бұрын
Koditu chilima sanali munthu wabwino ayi ngakhale chakwera anamupha
@GoodluckVithumbiko
@GoodluckVithumbiko 3 күн бұрын
murungu akunkhurukureni nthawi ndiyanu
@MosesMbale
@MosesMbale 3 күн бұрын
Bakili Muluzi ndi dolo ndamutayila kamtengo
@phillipchampoxychapola4165
@phillipchampoxychapola4165 3 күн бұрын
Kwamene akuvesesa sanganene kuti page yahakidwa koma vuto anthufe timafuna kuti munthu uja azikamba zambari imodzi
@ConsPempho
@ConsPempho 6 сағат бұрын
Ai I hanger😂
@GeorgePhiri-ub2of
@GeorgePhiri-ub2of 2 күн бұрын
Mwakhaula Uyutu si mtanyiwa ai oti tsiku ndi tsiku odzingolimbana ndi chakwela ai
@CharlesKaujole
@CharlesKaujole 3 күн бұрын
Dars
@AustinAllan-lh5ij
@AustinAllan-lh5ij 2 күн бұрын
Ku Chikangawa uku guys 😅😅😅
@AngolaChinga
@AngolaChinga 3 күн бұрын
Inu uyu si wabakili muludzi tv kapolo wa mcp uyu
@SolomonNjolomole
@SolomonNjolomole 3 күн бұрын
Doud Suleman ndi azizake kuyesera machine agula aja apa game mbola.
@SmartMailos
@SmartMailos 2 күн бұрын
Sizona siiye
@MimiKapito
@MimiKapito 3 күн бұрын
Zaboza uyu
@tasiyanakasalu6228
@tasiyanakasalu6228 3 күн бұрын
Ndiyomweyo kungot akangana bax kkk
@NoahPhiri-f7m
@NoahPhiri-f7m 3 күн бұрын
Sibakili tv ameney ndiwa mcp
@ErickCPatrick
@ErickCPatrick 2 күн бұрын
kabambe,wakuba
@KhirChisale
@KhirChisale 3 күн бұрын
Eeeeshiii koma ine
@KennedyPhiri-h9h
@KennedyPhiri-h9h 3 күн бұрын
Sibakili muluzi TV imeneyo ndi propaganda
@Mustapher-fb4qp
@Mustapher-fb4qp 3 күн бұрын
Chirima ineso sindingamuyikire kumbuyo
@NelesonchibwanaMandera
@NelesonchibwanaMandera 42 минут бұрын
Bakili muludzi TV imanena zoona ine ndimankhulupililad amankhala kut waziwona kale sogolo lake
@MikeLodzi
@MikeLodzi 3 күн бұрын
nkhani izizi siza bakili muluzi tv anjanjawidi angolowelelapo
@natashamathala8715
@natashamathala8715 2 күн бұрын
Yaaaaaah a mcp mwafika patali, koma mukunama naye wa bakiri muluzi simumukwanitsa ayi mwachepa dikilani akuyankhani nzanuyo akubwela ndithu chifukwa uyu si wathu wathu wa bakili muluzi ayi ine ndakana izi.
@EvanceSungani-cv9jk
@EvanceSungani-cv9jk 3 күн бұрын
MCP paja yakunga chiwembu kwa bakili muluzi TV this is plan ,,,,,
@ShamimuBisani
@ShamimuBisani 3 күн бұрын
Zaziiiii mwalephera kumusaka .mukhaula
@YounusWabullah
@YounusWabullah 3 күн бұрын
Ndi propaganda iyi zamkutu bas
@ChikondiMusaya-x6n
@ChikondiMusaya-x6n 3 күн бұрын
Sibakili muluz ameneyo
@greycianmbewe4573
@greycianmbewe4573 3 күн бұрын
Lankhulani koma timuvoterabe
@PatrickZinenanie
@PatrickZinenanie 2 күн бұрын
Si bakili muluzi ameneyo ndi zigawenga za chikangawa party mcp
@AlexanderTraffick
@AlexanderTraffick 3 күн бұрын
Komatu TV imeneyi imakhwefura munthu kkkk achina kamajekete Ali ziiii
@DonaldBanda-qi7yw
@DonaldBanda-qi7yw 3 күн бұрын
Ndale zaku Malawi ndi zosokoneza anthu
@DonaldBanda-qi7yw
@DonaldBanda-qi7yw 3 күн бұрын
Ndi kunena zoona Ana amasiku ano sakudziwa kuti Kodi Atsamunda amalamulira bwanji dziko lino. Chimene akudziwa ndi kulemba Nkhani ZOSOKONEZA A MALAWI pa SOCIAL MEDIA basi, komanso kuwapatsa Bomali popanda masankho sangathenso kulamulira dzikoli adzangokhala mavuto okhaokha basi.
@Extratremendouszeus
@Extratremendouszeus 3 күн бұрын
But you have to check because there are many bakili muluzi TVs...else you bakili muluzi never does this
@MCDAISONNKHWAZI
@MCDAISONNKHWAZI 3 күн бұрын
Mmm page is hacked history is the best teacher wa baliki TV wen wen amakhala in small letters ndipo kwambr amakonda ma audios not ma letters ndipo samapanga pafupi pafupi chonch
@KondwaniChaponga
@KondwaniChaponga 3 күн бұрын
Mkamalimbana ndi BMT mutha ngati makatani
@BrightLuciano
@BrightLuciano 2 күн бұрын
Zazi SI Bmtv uyu 😢😊
@AugrinNgunga
@AugrinNgunga 3 күн бұрын
Mayaz sibakili muluz tv uyu aaa timatha zimenezo kulemba pa page yamuthu
IL'HAN - Qalqam | Official Music Video
03:17
Ilhan Ihsanov
Рет қаралды 700 М.
99.9% IMPOSSIBLE
00:24
STORROR
Рет қаралды 31 МЛН
Quando eu quero Sushi (sem desperdiçar) 🍣
00:26
Los Wagners
Рет қаралды 15 МЛН
Кем был убитый в Москве Армен Саркисян
16:59
BBC News - Русская служба
Рет қаралды 96 М.
Kodi Baibulo limene timawerenga ku Malawi kuno linachokera dziko lanji?
15:34
Ben Longwe Kuyankhula Za Ku Chikangawa - Part 3
21:04
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 11 М.
Prophet Uyu Walosera Zoopsa Pa Zisankho Zikubwerazi ... Tanvani
27:34