Agree or not...there are some grains of biasness here..
@DimakatsoMolaba2 ай бұрын
Achisiru achaweziwa.
@TRUSTDAVID-yt5um2 ай бұрын
Chawezi amalakhula ma wise okhaokha more 💥💥💥💥
@user-ux3ed3ni1p2 ай бұрын
Onse DPP and MCP had no opposition to leadership. No Democracy.
@DanMhone-iw6xg2 ай бұрын
Program ya makape sadic miya mesa munaphaso ndye mukulubwalubwa chan apa ana agalu inu
@ThomJohn-e6v2 ай бұрын
Ngati Pali program ndia zisilu ziwili zimenezi
@edsonnyasulu53942 ай бұрын
Kuphunzila kwa kuno ku Africa ndi memory chabe saziwa kupanga zinthu koma amasungila zomwe anaphunzisidwa kuchoka ku America
@FocusPanje-nd2pr2 ай бұрын
Chawez ukufuna mp ku blantyre city east uzitenge bwino coz anthu aku bt akukumva ukudzipanga wekha de campaign,,, uzibaya mmaso wamva uzitenge bwino kuno sikwa mcp,,, deusi nawenso ukufuna mbali yomweyo play ur cards well OK??? Museseleka muona
@samsonmtumbati48552 ай бұрын
Kodi program imeneyi amene amapanga sponsor ndi chipani cha mcp eti mukutinyasa kwambiri
Kodi iwe ukulimbana ndi muthalika bwanji chakwela bwanji kunalibe ofuna kupikisana naye
@benjaminmvuma-rk6mu2 ай бұрын
Chawezi 2030 uzagwila ntcĥito mu state house ntchito ija Brian banda analepherà
@BENSONRANGWANI2 ай бұрын
Chakwela wamupha chilima zasala zosatila Zach
@GiftChitsulo2 ай бұрын
Chawez iwe sukuziwa kuti ku MCP kulibe ufulu waiwala kuti ku MCP ukangoyakhula kuti mundisiyile nane ndiyimileko anafa ndichikangawa waiwala iwe bolani ku dipipiko anthu sakufa amasiyana bwinobwino
@lacksonkim96222 ай бұрын
Chawezi iwe umalandila ndalama Za MCP kape iwe
@Littlefair72 ай бұрын
Koma buns imene wadya Chawezi kodi yellow buns kapena chani? Achakwera analephera kumusoyira mnyamata Chilima, ma buns akuwononga atolankhani.
@GraciousBilly2 ай бұрын
Akulu nkhani ndi usogoleri osat zanuzo
@crytoniegrantliffa24312 ай бұрын
Chawezi mukulakhulira izi chifukwa cha kwiyo yoti anakuchotsa ntchito ku mbc............zako izoo
@CharityChirwa-t1e2 ай бұрын
Chakwela alindizaka 65 wapangachani chothandiza amalawi chawezi uzingonyopola ndalama zaku MCP ufune usafune APM akulamula next year
@alecahkaluza95572 ай бұрын
Chawezi wa MCP
@michaelcharles-p9v2 ай бұрын
Chawezi wa Mcp galu uyu
@RemitterFlik11302 ай бұрын
Ndipo ine amandinyasa ndale zake amafuna kampando kena kake
@ShukuraniTonex2 ай бұрын
Ndalama za MCP zikukoma Achawez 😢
@GeshoMwakitwile2 ай бұрын
Nanga peter akachezera sakagona uku anthu akanva mikonono ya munthu wamkulu
mutharika atupele muluzi adatiuza ife amalawi kuti mukasanga mcp mavuto siizi kodi amalawi manyi akutinyela achakwera palibe chimodzi akudziwa pangani yoyendetsa dziko ndiye chifukwa chake chinachilichonse mmalawi muno chili upset down because we choose arearner to drive along distance that was abig mistake we have done
@MikeArthur-jd2ij2 ай бұрын
What is MCP then 🤷
@BenBanda-q9j2 ай бұрын
Mutharika ndi wamtendere
@ThokozaniAlfred-w2u2 ай бұрын
Programm yonse kunthera nkhani yofoira ngt imene ah or kuika nkhani zoti zitukule dziko ah
@WanangwaSokochikwete2 ай бұрын
Inu simunaphe chilima chifukwa champando wa president
@ayamichaponda11132 ай бұрын
Chawezi tikudziwa zonse kuti ndiwe wa MCP, ndipo mmutumwako munazadza mwazi nde palibe ungatiuze .zaku DPP zisakukhudze iwe ndi mbuzi .zoti APM analengeza kuti wapuma pa ndale ,npomwe enawo ankaonesa chidwi sudziwa? Koma anthu atamupempha APM kuti awaphule pa moto wa MCP nde enawoso akanakaimila chifukwa chani? Munya muyankhatu milandu mukuopayo tikakuchotsani pampando
@Spaw-BTheGogoBoy2 ай бұрын
Chomwe achawez mmawaikira pama problem sindimachidziwa chifukwa amayankhula zofoira always
@PeterPhiri-di1ux2 ай бұрын
achawezi bambo anu atakalamba ana siya kukusamalani ndinu achitsiru