Chifunga singasowetse ndege pa Radar. President Chakwera walephera

  Рет қаралды 74,032

Bakili Muluzi TV

Bakili Muluzi TV

14 күн бұрын

Пікірлер: 584
@user-ir8dd8lm1c
@user-ir8dd8lm1c 12 күн бұрын
Odana bakili muluzi TV ndimfiti🔥🔥🔥
@blessingsmzeka8153
@blessingsmzeka8153 6 күн бұрын
Replied
@DavidJackson-ox4xm
@DavidJackson-ox4xm 12 күн бұрын
The best TV in southern Africa.
@FrankSimfukwe-w1s
@FrankSimfukwe-w1s 12 күн бұрын
Kunena mosafisa inu ndi wariya wachilungamo Inu nde mamuna weniweni mulungu apitilize kuonjezela chitetezo chako l love you brother ❤
@kingwaltermdezo
@kingwaltermdezo 12 күн бұрын
Best KZbin channel ku malawi, ntchito mukuyigwira kunena chilungamo❤
@dalitson3558
@dalitson3558 12 күн бұрын
We always here for you our own brother
@petertaulo8014
@petertaulo8014 12 күн бұрын
We love you Big and Chakwera will pay for this!
@elishamael-shadai
@elishamael-shadai 12 күн бұрын
Chakwera mkhumba kwambiri
@JackNagoli
@JackNagoli 12 күн бұрын
Eeee inuyo boss ndi number one keep going bwana N may God bless you 🙏
@lottiempata2487
@lottiempata2487 12 күн бұрын
MCP will never change and I told people that MCP will finished us but God's good always Amen
@user-be5fc3ed1i
@user-be5fc3ed1i 12 күн бұрын
Kp it up Bakili muluzi tv chakwera asanamize anthu iye ndi Amen adapha chilima.zodabwisa mnthu adavara suit koma kukapezeka ngati adali ndizovala zamanyaka zomvesa chisoni amalawi.chakwera awona chaka chamawa 2025 uchoka ndi ndi nduna zakozo achina kamajekete
@DalitsoPhiri-sq5nl
@DalitsoPhiri-sq5nl 12 күн бұрын
Chakwera knows every single move yomwe ikuchitika ku malawiko asakunamizeni he's a master mind pa chilichonse zamisala akunenazo zoti palibe akudziwa iye akunamiza Ana.
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 12 күн бұрын
Ada inuyi mumatha with comrade mtanyiwa alongside bon Kalindo ❤
@JeanBanda-zy6wu
@JeanBanda-zy6wu 12 күн бұрын
You're blessed brother with knowledge, keep on fighting we are behind you ❤
@johnkambala692
@johnkambala692 12 күн бұрын
There is God in heaven.
@zynmf9086
@zynmf9086 12 күн бұрын
Chilimas death ndiyowawa😢
@RabeccaMkandawire-i9j
@RabeccaMkandawire-i9j 12 күн бұрын
Kwambiri
@Homeofpeace321
@Homeofpeace321 12 күн бұрын
Mumapha Anzanu Kufuna Maudindo Achakwela ndi MCP Yanu, Chilima Munamupha Kuti Anthu Akuvoteleni 2025 Koma Manyazi Akugwilani.
@user-sk1wj9bw6l
@user-sk1wj9bw6l 12 күн бұрын
Siyani mau otu achewa musagawqnitse mitundu nafeso tikuvutika ndi garu ameneyu wa nyawuyu
@Homeofpeace321
@Homeofpeace321 12 күн бұрын
@@user-sk1wj9bw6l Takumvani, Pepani kwambili Timaona ngati Nonse Ndichimodzimodzi Tikayangana nthawi Yakamuzu Tinaluzanso Abale Nthawi Ya MCP
@AiameAdamo-su1nt
@AiameAdamo-su1nt 12 күн бұрын
You are saying the truth big. It's clear and very loud from Mozambique.
@fraserbereck2269
@fraserbereck2269 12 күн бұрын
Best tv ever in Malawi 🇲🇼 keep it up brother
@ManzyMassa
@ManzyMassa 12 күн бұрын
Ur knowledge is beyond ❤
@user-zx1zs8el7q
@user-zx1zs8el7q 12 күн бұрын
Chilima anachita kuphedwa 😢😢
@SamKaposa-i5c
@SamKaposa-i5c 12 күн бұрын
Straight zosachita kufunsa
@MisheckAselo
@MisheckAselo 12 күн бұрын
Ing'aluleni big man, zodziwikiratu kuti mission inali ya chakwera ndi Boma Lao loipali, chakwera, mulungu akukuona ndipo mzimu wa chilima uziusa mumtendere 🙏😭
@ChifundoChiwanda-ru3pg
@ChifundoChiwanda-ru3pg 12 күн бұрын
Sambi! ndenge kugwa mma 10 koloko mmamawa osatekeseka mpaka Chilima kugona muchikangawa as if he was nobody. Pokhapa apa pamasonyeza ufiti woopsa. And zinaonetseratu kuti Chilima samamufunadi
@user-be5fc3ed1i
@user-be5fc3ed1i 12 күн бұрын
Ndinthawi yomweyo amafuna kuti Chilima mpaka athane nayo ngati chilima Adali moyo iye Chakwera ndikutimiza anthu oyipa mtima kuti akawamalize zomvesa chisoni ndithu amalawi.
@MasausoMsiska-rz3id
@MasausoMsiska-rz3id 10 күн бұрын
We want justice for chilima and everyone who died in that plane. Ambuye musowetse mtendele wina aliyense anatengapo mbali pa infa izi mpaka chilungamo chidazadziwke no matter how long it takes. Rise from your throne heavenly father and show justice on your people
@JonesChingaya-yf4gg
@JonesChingaya-yf4gg 12 күн бұрын
APM once said, " One day Malawi will be ruled by evil"and now i agree the evil is rulling under Chakwera leadership.
@MemoryKilofasi-e5b
@MemoryKilofasi-e5b 9 күн бұрын
God bless you my brother 🎉
@mayesojameskatete
@mayesojameskatete 12 күн бұрын
Chakwera killed chilima we all knows about that
@FatimaMsusa
@FatimaMsusa 12 күн бұрын
Koma inuyo mulungu adzikudalitsani ntchito mukuyigwila kwambili... ❤
@LoyedEhemmah
@LoyedEhemmah 12 күн бұрын
Keep fire burning, we love you Bakili tv
@Creslevison-vj2sl
@Creslevison-vj2sl 11 күн бұрын
U r in the has of God fully protected and long live sir iniyo munatha ntchito and the best jornalist ever
@FredrickPhiri-vc6we
@FredrickPhiri-vc6we 10 күн бұрын
Keep it up man, till now tikulira SKC 😭😭
@ZaxTembo-v3w
@ZaxTembo-v3w 4 күн бұрын
I like this man go ahead
@georgesmart3791
@georgesmart3791 12 күн бұрын
More fire Bakili muluzi tv❤❤
@user-oc8nj3or6y
@user-oc8nj3or6y 12 күн бұрын
History cannot be hidden anymore en Will never be hidden anymore 😢😢😢
@user-ug9zn8nu8y
@user-ug9zn8nu8y 12 күн бұрын
Imfa yachilima mpaka pano ikumandiwawa ndisaname😢😢😢😢😢😢😢😢😢
@user-xx4jb9se3z
@user-xx4jb9se3z 12 күн бұрын
Bakili tv my best may GOD bless you. Koma imfa ya chilima ine ikundiwawa
@manualrapheal6048
@manualrapheal6048 12 күн бұрын
😂😂😂😂 koma ndiye kamajekekedi. My desire is, God continue save you bakili muluzi tv comrade thanyiwa bon kalindo and many more but only who come to telling us the trueth what happening at MALAWI through zomwe zikuchita zigawenga 💓🙏🙏🙏🙏🙏 i remember 2016 Grace chinga said, chipani cha mwazi chikubwera takumukira amalawi😢?
@alicegama8138
@alicegama8138 12 күн бұрын
Zikhale mwamupasa zina lina kama jacket 😂😂😂😂
@webstermbewe8395
@webstermbewe8395 12 күн бұрын
Thanks very much we have been waiting for you to come with this one Continue to do this
@EmmanuelNgambi-y6h
@EmmanuelNgambi-y6h 12 күн бұрын
Mulungu akudalitseni bg keep it up
@user-cd4df3vg4y
@user-cd4df3vg4y 12 күн бұрын
God protect you broo.Chakwera is a killer
@DanielMbewe-jo9vv
@DanielMbewe-jo9vv 9 күн бұрын
Bakili muluzi tv ndi mbambande 🇿🇲🇿🇲🇿🇲🇿🇲
@ChippieChikaonda
@ChippieChikaonda 8 күн бұрын
Respect to you brother
@Aubreychiso
@Aubreychiso 12 күн бұрын
More apdates We learn more through here Big up
@RiannahKaliat
@RiannahKaliat 12 күн бұрын
Zimandiwawa sanamei 10 am ndikumayang,ana chama 6 zoona then ndikumat ai tipitiliza mawa aaaaaaaa
@kellsonOfficial
@kellsonOfficial 12 күн бұрын
the best Tv in Malawi Zikachika timvela pano
@ChiccoJelly-wp5wj
@ChiccoJelly-wp5wj 12 күн бұрын
Am stand with you and l will always stand for you, truth is your behavior
@user-Grant260
@user-Grant260 12 күн бұрын
Always you stand for us ❤
@ThokoMaggie
@ThokoMaggie 12 күн бұрын
😂😂😂😂 pano nduna ndi a pre mitu yao sikugwila chifukwa Cha inu boss💪💪
@RabiaOsman-wy1ud
@RabiaOsman-wy1ud 12 күн бұрын
Well documented, keep up ❤
@DaudiRose
@DaudiRose 12 күн бұрын
Always love you big man keep it up
@user-do2cs8nf4b
@user-do2cs8nf4b 12 күн бұрын
Amakhala akudziwa sizingatheke kupanga chinthu kumbali president osadziwa
@YasinMusa-ym8lp
@YasinMusa-ym8lp 12 күн бұрын
Inuyo abwana mumata❤
@AnthonyMhango-e9q
@AnthonyMhango-e9q 12 күн бұрын
Umakwana iweyo bro ur the best enawa ndi makape
@isaiahsensekaunda5036
@isaiahsensekaunda5036 12 күн бұрын
❤❤❤❤❤❤❤❤ we love you brother
@lyiemanganjira9708
@lyiemanganjira9708 12 күн бұрын
God will always be on your side, cos you're truly God's sender to us, so can see and know what is happening outside there
@mayamalango7820
@mayamalango7820 11 күн бұрын
U too good fada
@BrianHZolo
@BrianHZolo 12 күн бұрын
History is a best teacher umakwanila BT
@edwinrobert5346
@edwinrobert5346 12 күн бұрын
Chakwera chimwendo kamajekete chizamba mkaka ndi athu akupha Ku mcp congratulations bakili tv
@premtalawe
@premtalawe 12 күн бұрын
Good job mr muluz tv❤❤❤
@ChimwemweStima-ht5ty
@ChimwemweStima-ht5ty 11 күн бұрын
Long live BMTv❤
@letsonpansipayenda7706
@letsonpansipayenda7706 12 күн бұрын
History is the best teacher!
@winamlaston4688
@winamlaston4688 11 күн бұрын
Your the best broh keep it up bakili muluzi tv👌🔥🔥
@user-no2sn1fo1h
@user-no2sn1fo1h 11 күн бұрын
Thanks big man ntchto mukuigwila kwambili
@felixmbama3999
@felixmbama3999 12 күн бұрын
Keep it up big bro,we need such kind of you pipo for Malawians to know the truth,chilima anaphedwa basiii.lets wait and see next year ngati MCP izatengaso boma
@alliemuhammad7534
@alliemuhammad7534 12 күн бұрын
Bakili muluzi tv we love you otsapowoka thili kumbuyo Kwanu chakwera must go. 🤞
@ulongwearomakawanga2318
@ulongwearomakawanga2318 12 күн бұрын
Kamajekete why 😅😅😅😅
@EllinaBitto
@EllinaBitto 10 күн бұрын
Timenyereni nkhondo😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭
@LouisAndrew-jr1yj
@LouisAndrew-jr1yj 12 күн бұрын
The best TV ever ✌️
@user-eh1mg3ww6d
@user-eh1mg3ww6d 12 күн бұрын
Koditu chakwela adzalipila tsiku ndilimodzi iyeyo si opambana kuti adztisautsa ife Muthu watundu wanji tchito zake za usatana
@sharifujoe7633
@sharifujoe7633 12 күн бұрын
Kwake kwata big uyu chakwera nkhani ndiyamademo bansi ngati tikufuna dziko lathu libwerere kwa amalawi
@EleniJames-rc3ot
@EleniJames-rc3ot 11 күн бұрын
Ndipo mfiti chakwelayo akamuvotela achewa omweyo osati mitundu lnayi ayi akutisala kwambili nyani ameneyu
@cadlymondoma2911
@cadlymondoma2911 12 күн бұрын
Stay blessed broh, let's work together to kick out this foolish party
@jamesgama5489
@jamesgama5489 12 күн бұрын
The is no secret under the sun
@Hellenistic109
@Hellenistic109 12 күн бұрын
On Chilima's death,I hate the Malawian President for the Negligence that he deliberately did...MCP must Go..The death of the innocent Young Souls on the Chilima plane has left my heart bleeding to date😢😢😢
@ImranDaud-ir8jj
@ImranDaud-ir8jj 11 күн бұрын
May almighty protect you brother
@patrickkusailemp3769
@patrickkusailemp3769 12 күн бұрын
Osaopa bgyyy,,chakwera ndi mbudzi ,galu ,wakuba ,,wakupha,, chigawenga
@ManganiStanley
@ManganiStanley 12 күн бұрын
Ndipo chakwera sindikufuna ndipo akundinyansa kwbiri
@PaulMulomo
@PaulMulomo 12 күн бұрын
Ngati iwe uli ndi umboni pita ku court ukanene zoduka mutu ay
@Isaac-ok4ev
@Isaac-ok4ev 12 күн бұрын
Mpaka kama jakete😂😂😂😂
@user-mh7cc8up4i
@user-mh7cc8up4i 12 күн бұрын
God bless you always Mr mumativesa sugar 🔥
@ElonBlack1999
@ElonBlack1999 12 күн бұрын
Kodi sanamalizebe kufufuza a UTM MEMBERS
@user-oe1lg4xo7w
@user-oe1lg4xo7w 12 күн бұрын
Timakunyadirani big. Onondaga kudya maliro anayaluka ndi mwana wangobadwakumene . Achakwera kupha anKuyambira kale Ali kumpingo lero ayaluka ndi infant ya Skc
@AbdhakeemDoisi-lw6tq
@AbdhakeemDoisi-lw6tq 12 күн бұрын
Still can't believe this shame😭😭😭😭😭💔💔💔💔💔💔💔💔💔💔💔💔💔💔💔💔💔💔💔
@user-vl8uw8mc3u
@user-vl8uw8mc3u 12 күн бұрын
Zoona zokhazokha.ufumu wa chakwela chikangawa ndi mcp watha basi
@petertukula1649
@petertukula1649 12 күн бұрын
biggie musamasowe
@AnaffSayamika-uh6vg
@AnaffSayamika-uh6vg 12 күн бұрын
Chakwela, zikhale ng'oma and nkukuyu zisilu kwabasi
@Yonayolamu
@Yonayolamu 12 күн бұрын
Mukwana tikudziwa zambiri Kwa inu
@EstherShaba-fh8ib
@EstherShaba-fh8ib 12 күн бұрын
Anthu akupha awa , days are numbered tikumana 2025
@user-px1rq6sj9t
@user-px1rq6sj9t 12 күн бұрын
Best TV ever
@RachealHarawa-xc9gs
@RachealHarawa-xc9gs 12 күн бұрын
You are the best keep it up ,mmatiimilira
@usherjamson174
@usherjamson174 12 күн бұрын
I really like you bro you like true and wise💪💪
@user-xd1cm7tm7t
@user-xd1cm7tm7t 12 күн бұрын
King of history in malawi
@ahhobebamw7365
@ahhobebamw7365 12 күн бұрын
Bakili muluzi Tv
@HassanSinoya-wl3vl
@HassanSinoya-wl3vl 12 күн бұрын
Ndimomwemo bg man afusen atiwudze anyan amenewa chakwela ndifiti ndithu 😢😢
@maskinmsungeni8763
@maskinmsungeni8763 12 күн бұрын
Ine ngakhale ndili mbuli koma chakwers sangandinamize , za ngozi imene ija. Chakwera ukazaluza chisankho uzapezeretu kokakhala not Mmalawimo tingoyanganatu.
@WinesiAkatundu
@WinesiAkatundu 12 күн бұрын
❤❤❤❤❤ Tinakusowa
@user-ee1ci2ku6o
@user-ee1ci2ku6o 12 күн бұрын
History is the best teacher
@preciousstambuli
@preciousstambuli 9 күн бұрын
Still following ❤
@Sabina-hw4js
@Sabina-hw4js 12 күн бұрын
Let God expose them
@user-pt1fy3qg4u
@user-pt1fy3qg4u 12 күн бұрын
Never give up bro ❤
@MosesKalenge
@MosesKalenge 12 күн бұрын
Koma anthu awa mmmmmmmh mwamupha SKC 💔😢 Cholinga 2025. Mlamurileso 🚮🚮🚮 👀😭😭😭😭😭😭😭😭
Зачем он туда залез?
00:25
Vlad Samokatchik
Рет қаралды 2,7 МЛН
🤔Какой Орган самый длинный ? #shorts
00:42
Mom's Unique Approach to Teaching Kids Hygiene #shorts
00:16
Fabiosa Stories
Рет қаралды 6 МЛН
Was ist im Eis versteckt? 🧊 Coole Winter-Gadgets von Amazon
00:37
SMOL German
Рет қаралды 40 МЛН
Minyama yathu ngati amalawi ikuchokera pati?
16:31
Bakili Muluzi TV
Рет қаралды 54 М.
Atikumbutsa Samora Machel wa ku Mozambique
10:23
Bakili Muluzi TV
Рет қаралды 45 М.
Trump Accepts Nomination | News on The 700 Club - July 19, 2024
15:29
Donald Trump waomberedwa; Anthu atatu akufuna kusokoneza UTM
6:38
Bakili Muluzi TV
Рет қаралды 62 М.
EXCLUSIVE INTERVIEW - 28 JULY 2018 - VICE PRESIDENT SAULOS CHILIMA
1:00:00
Times 360 Malawi
Рет қаралды 86 М.
Зачем он туда залез?
00:25
Vlad Samokatchik
Рет қаралды 2,7 МЛН