Koma muthu wadwala, akanapanga address the nationa ,kutiuza za well being ya muthuyo, a spokesperson awo, kuli akubanja, kuli ma minster, cabinet, we need to be up dated on our pastor
@HarryKandani2 сағат бұрын
Lets wait till mawalo tiwaona ku limbe komenya golf
Ngat apule ali moyo abwele atìlankhule kuntundu wamalawi athetse phekeselazi
@PeterChimbayoСағат бұрын
Koma akaona antha kudzinvera chisoni..
@BostonMalack57 минут бұрын
Kodi ngati ndizowana nde chimanga chizingowa pa madenga ammanyumba mwathumu or fertilizer atsika mitengo komaso kuti umphawi tilinawo kumalawi kunowu ukutha akamalowa mmanda
@giftkayome3568Сағат бұрын
Ndinakakhala ine ndikanangotula pansi udindo apa zikuwoseratu kuti sakufunidwa
@DanielDoctor-t3p3 сағат бұрын
Tiva zonse madzulo ano kuti ndizoonadi wapita mulungu adalitse chakwela ngakhale ali ndikhalidwe loipa koma ndikumufunila zabwino komwe aliko
@BrightZionga56 минут бұрын
Afe basi akudikila chani ngati pali achita iye kupatula kuba iyaaa
@JeanBanda-zy6wu32 минут бұрын
Abale anthu kumasangalala chonchi kungomva kuti wina wamwalira? Which means something is wrong ngati asanamwaliredi a chakwelawo aganizepo bwino something somewhere is wrong
@EsnartGirivinСағат бұрын
HAHA pajatu amatelo president akamwalila amatha kulengeza kuti akachititsa msonkhano kwakuti Koma akudziwa kuti wafa, Inu dzikoli simunalisziwebe??
@JohnConar-kq4hi21 минут бұрын
🤔🤔🤔🤔🤔🤔🤔🤔🤔
@Belinda-c6e2 сағат бұрын
Kusonyeza kuti manganya akhala president????????
@KennedyPhiri-h9hСағат бұрын
Chakwela watisiya basi amalawi onse sanganame Okay ngati ndizabodza abwele atiyankhule chakwela apa
@HaroonAlibarara3 сағат бұрын
Dan lu zikuvuta iwe ngat wamwalira sunanjoye kkk
@FelistusEmmanuel-f1oСағат бұрын
Waiting official results ndabuka kale nkhuku yachikuda 😅😅😅
Chakwera watisiya bas, uthenga ndi umwewu bas don't wait for another report. Paja amati boma ndilomweli ifeso lero tikuti uthenga ndi omwewu bas
@EffitaKandiwo2 сағат бұрын
Hahahaha
@BeatriceLameck-x2oСағат бұрын
Hahahah kma
@ShamimuBisani2 сағат бұрын
Chakwera komwe uliko ngt ukufuna kukhal moyo zako zimenezo kaya ukufuna kufa zako zimenezo ihave no business with u REST IN PIECESSSSSS
@benjaminmvuma-rk6muСағат бұрын
Leave him alone ,chakwera has along life
@ArronBenson-g6d3 минут бұрын
😂😂
@NoelChalunda-j2g2 сағат бұрын
Kuweruza ndikwake Yehova
@EsnartGirivinСағат бұрын
Chiweluzo chilipamsi pompano inu 😂😂😂😂
@TrizaGeorge-q8w2 сағат бұрын
Koma tipephe chilima ndi athu ena anawaphela. Kuchikangawa aja amukokele komweko asakhaleso ndi moyo sitikumufuna afe afe muthu oipa kwambili
@RaffickAllie2 сағат бұрын
Zikapsa mutiudza nafe makombora tilidze
@fannyzimba1492 сағат бұрын
😂😂😂😂😂😂😂
@Stretor2 сағат бұрын
Ngakhale kufunira nzako kulowa manda ndi tchimo koma na apa pokha bola zikhale zoona munthu yu watizunsa kwambili
@MuhireDominic-rw4vfСағат бұрын
Totholan ndevu zonsezo baba😂
@ShamimuBisani2 сағат бұрын
Or atakhal kuti alimoyo palib Malawi angachite manyazi apa tamtuma ndfe kuti kumwalirako kulephereke apita dzikol alingati chakwera akampeza mzake Idi Amini
@usherjamson174Сағат бұрын
😂😂 😂😂
@danielmagwaya10742 сағат бұрын
Rest in peace Chikangawa Chakwera
@moureenmolesiСағат бұрын
iwe khala cheteeee boma likubisa izi wafa ameneyo
@Aubreysekeyah2 сағат бұрын
Koma nde atangolengexa kungavute
@JonerdandhamuzMisokwe2 сағат бұрын
😂😂😂😂koma ndizonadi izi
@IqrahSikweya-wm5mn2 сағат бұрын
Kod nanunso zot Chakwera wafa ndindan angatsimikize... Angabwere mkulemba kuti wafa mwa easy?.... ka wafa or Ali ndi moyo we don't care.................. Ma research anuo sangagwire ntchito so far
Mene MCP inasangalarira mene Bingu atafa .. this life is what goes around comes around.
@CharityMhone-uk9ym2 сағат бұрын
Zikisiyan pati atafa bingu, Joyce Banda ndi Lucius ndi anthu Ake Anali pa chimphwando ku hotel nde asiyen anthu asangalala ntchito zake zimutsata 😮😮😮😮😮 ngati anali wabwino bwenz anthu akulira ndepoti chinali chigawenga basi😮😮😮😮 chipite
@KentWilliam-r2v2 сағат бұрын
Eya Kaya chifukwa ndi munthu oyipa
@SteveNkhambule2 сағат бұрын
Nde what's funny
@RACHEALKanyenda-b8f3 сағат бұрын
Koma Malawi kokoma
@MaxwellChiwaya-i8q3 сағат бұрын
Koma anthu ndiye achita manyazitu akamuona Ali ku golf club sartaday lo
@WisdomChimalizeniСағат бұрын
😂😂😂 Kaya apita sizikutikhuza tudikira Kumkuyu amalengeza za dongosolo la maliro kuti a Blantyre tikasonkhane ku Sanjika Palace