Asiyeni mbuzi ikakodwa amalonda ali pafupi kalindo akawina u plesdent adzawalanga ose
@smt70363 ай бұрын
we are tired of talking shit we need kenya vibe
@ChikumbutsoJohn-rs4tt3 ай бұрын
Chilima was future for Malawi 😭😭😭😭
@ChikumbutsoJohn-rs4tt3 ай бұрын
😂😂😂😂😂 iweyo umakwana
@EdwardMwale-p2j3 ай бұрын
Mene adalowela m boma chitukuko chawo ndi ndi kuba
@BashielSalade3 ай бұрын
Chakwera sitikwafuna achoke
@philonampha3 ай бұрын
Awaphweteke kumene, aone polekera
@YellowmanMalawi-qe8zh3 ай бұрын
Auze lwara
@Amgwagwa3 ай бұрын
Kkkkkkk
@TheboZilinde-tq1gf3 ай бұрын
Ma facts 😂😂
@DaveSitolo3 ай бұрын
Yeah for sure zimu wa chilima uwatikite anthu amenewa and kanakondwa ofufuza Za Ngozi ya ndege atazabweraso 2025 chakwera atachoka pampando not now because patha kulowa katangare
@Mussa-qs7km3 ай бұрын
Good Good Good Good Good
@MusaDickson-tn5yq3 ай бұрын
Hello how are you that one long story that president third president is a very stupid 2025 you must you must change you can choose me anyone
Boma iri lilibe dzelu chimene akudziwa kupha Kuba bass
@innocentkalako78143 ай бұрын
Mwaiwalanso nkhani ya ma passport ndi ma license
@GospelSoldiers-sr7np3 ай бұрын
Boma ili silikudziwa chomwe likuchita, Mulungu wachotsa chisomo basi palibe chomwe akudziwa,Ambuye athandize Malawi.
@EdwardMwale-p2j3 ай бұрын
Agalu amenewa achoke basi achoke alenphela boma yawo inadzadza ndimburi
@elishakalungwe68993 ай бұрын
Aphalile chakwela palije icho akumanya,,,watondeka he should just pack and go
@WalkerElick3 ай бұрын
Vuto anthu amene ali ku tsogolo la MCP onse ndi mbuli zokha zokha sanapite ku school mokwanila angotiuza kuti amagwiritsira tchito kunthwima ufiti basi.
@Rose-wu5ef3 ай бұрын
Chakwela ndi amene wapha chilima
@ajasikalonga32103 ай бұрын
Do not hesitate yes
@TrizaGeorge-q8w3 ай бұрын
Baga Moyo plesdent 😂😂😂
@EllinaMasimo3 ай бұрын
Kulira kwabwino uku Comrade good evening too
@AliAli.aliheassim3 ай бұрын
❤❤❤❤more fire bigman
@leviefeston76263 ай бұрын
Ndi vipuwa va MCP
@EdwardMwale-p2j3 ай бұрын
Tipita Kuma demo
@GraceLimani-zw7dx3 ай бұрын
Inu so ndinu amene mapanga campaign kuti anthu tavotere achakwera
@vinceynyone66933 ай бұрын
Pakamupeni azanena chani kaya, mwina azatiuza zachiwelengero cha anthu omwe apha in 5yrs 😢😢
@DanielMbingwani3 ай бұрын
MCP government ndi ma vampire!
@spargomw3 ай бұрын
😂😂😂😂😂😂 Mbunde za MCP zikavera Audio iyi zichezera kukanyera
@vinceynyone66933 ай бұрын
Wanthu opita ku canani akumana nd ciberclam 😂😂😂😂😂😂😂