To be honest Hot current iyiyi yaonetseratu kuti Brian and Jona, you guys are truly investigative Journalists... I like your courageous presentation because you have hitted a nail by head. Ya Kabwira komanso ya Extended Credit Facility ndiye mwaing'aluladi... Kuswa Kuswa, kugaza kugaza, kubandula kubandula. Kkkk kkkk kufotokoza nkhani osati based on speculations but facts on ground. The media has a very important role towards politics, rule of law and good governance. Guys you are a leading analysts in Malawi, so far😊😊😊😊😊😊
@HesfordMathemba15 күн бұрын
Brian aise Mulungu azingokudalitsa. You represent us the poor and voiceless people.
@user-rn7wv8ze3v18 күн бұрын
Koma Boma la Chakwera latipweteka amalawi
@ChejaliChirwa18 күн бұрын
My vote 2025 DPP 💙💙
@ConfusedClam-ov4mx18 күн бұрын
Opakuku akudya bwino ku times eee Masaya amenewo?
@GeorgeChitapapata17 күн бұрын
Ulemu wanu brain .kuima pachilungamo kuzukuta kosekose .I'm really happy with this program
Jona is right I feel the same let's no t brame ma ministers president yu ndi is incompetent he has no sense of direction hence his appointment s are also poor... Good example is bingu He was sharp upstairs as results he had ma Ministers oziwaso chomwe akuchita
@swadikimbwana768018 күн бұрын
She is completely confused and mad pls MCP instruct her to stop she is denouncing your party mcp
@YughozMw18 күн бұрын
Inuo guys mumandiwaza heavy🔥
@user-xd1cm7tm7t18 күн бұрын
Brian ndikatund osat andevu zamway😅😅
@KendrickLuckyc18 күн бұрын
Ndevu zamwai kape
@josephmunthali252615 күн бұрын
Chifukwa choti awa akukwela DPP mwati ndiabwino, koma wonder poti amayi balancer mwati ngoyipa mxieeeeew
@PatrickSomanje17 күн бұрын
Next year must think nice when we going to vote pls everyone knows now mcp not helping Malawians
@user-jk8sh7fh2d18 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂! Koma apankuku mwati pomaliza mwati who is a better devil kapena sinamve bwino kkkkk
@HassanHussein-x6o17 күн бұрын
I really appreciate your speech guys mumatha inuyo
@LytonMatola17 күн бұрын
Nice and lovely conversation guys keep it up.
@IssaJohn-cb8vn18 күн бұрын
Sizingatheke kukonza nthawi alibe kwachuluka komwe awononga mazi Ada basi
@henryphiri610018 күн бұрын
Osanamizira Nduna,vuto ndi President Chakwera amasankha dala incompetent ministers ndicholinga choti adziba.Bwanji Nancy Tembo alibe mbiri yonunkha ngati akapolo enawa
@user-eq8hr8li8h18 күн бұрын
Yesu akubwera mavuto onsewa adzatha amen
@GracianJames18 күн бұрын
Amen and amen God bless you brother or sister
@LuckyChsi18 күн бұрын
Atetezi a mkaka😂😂
@joegibsonzulu259917 күн бұрын
Program yosangulutsa iyi. Keep it up guys
@IssaJohn-cb8vn18 күн бұрын
Anyamata awa akulu akulu akugwila chinchito chachikulu pa redio iyi tikukunyadilani achina brain banda
@user-jk8sh7fh2d18 күн бұрын
Bola asazasinthe ena akazabwela
@christopherkuseli619017 күн бұрын
Hot current at its on best ,Sponsors should consider a bottles of water.
@macnellnamanja669817 күн бұрын
Koma pa Chilima pokha paja anatilakwila
@JustinMpunga-c8b17 күн бұрын
Plz connect your line properly coz breakdown communication
@Costance-nf7ue16 күн бұрын
Watching from johansburg
@ALEXAlli-ck8lj17 күн бұрын
Times ndi katundu auzen anthu zoona tatopa
@jameslweya-eo1uj16 күн бұрын
Azidandaula Ma americans about our malawian welfare…pomwe akumipandowo they cant see
@HenryChiwaya-u8l18 күн бұрын
The trueth free
@ishmaelsiffah990018 күн бұрын
I remember tsiku lina pa Sana mu Lilongwe kunabwera Richard kungokhala mgalimoto akuti akatero amwenye amangotuluka kuzapeleka ndalama n day imeneyo anachedwa,komatu mzibambo anaulephera mtima watsika kukathira fire mkati muja,mungangondikhanzika panjapa ine,do u knw whom i am ine shaaaa🤔🤔🤔
@veronicamustafa30518 күн бұрын
Amakatani mu Sannah mo
@wisdomsadyalunda200118 күн бұрын
Chithyola wa community development kumpasa unduna wa za chuma how do you expect him engenier the economy? Jona hold that vuto wankulu ndi empty tin.
@FrancisNyayi18 күн бұрын
Dennis mahata the new party basi though sitikumiziwa ahhh we know bingu coz of bakili and ahh
APM ndikuvotela chifukwa ukawina umusiila Kabambe as president utm boma.
@knoxymaulidimaloya417416 күн бұрын
Ine kwanga ndikuyamika chifukwa cha Tv imeneyi ya Times ndi Tv yokhayo imene imatithanndiza kuunikila zambuyo komanso zakusogolo, Pitilizanikutisegula mmaso ife achinyamata. vote UTM
Boma ndi lomweli ofunika kungosintha chipani ndi mtsogoleri
@user-ju9lg5pg5g18 күн бұрын
Awa ndi azungu akufuna tingwesetso kwacha
@user-jk8sh7fh2d18 күн бұрын
Vuto la usogoleri opusa opemphapempha basi azibusa ndi kukhala kwao ndie ndikukhalaso nsogoleri wa ziko aah basi m'mitu mwake ndizopempha basi kuendeza church ndi ziko nzosiyana system yake so asakaniza ati ndi yofanana to be honest kwa chakwelayu zativuta kwambili more problems
@UchizieFMtemela16 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂Mai kabwira azitengeratu zinthu pa mngong'o
@AkimuKindsonchirwa-j7l18 күн бұрын
Ngati a DPP akufuna kuwinaso must follow your advice and guidance another thing vice President must be Enock Chihana and Atupele Muluzi finance minister and next President agreement
@MercyHassan-p4e17 күн бұрын
Keep it up 🎉❤
@josephmunthali252615 күн бұрын
Mesa a Dpp, amayimba Kuti lozani zanu, nde a MCP asalodze zawo, a Brian ndi Jonah pena pake mmakondela DPP iyaaaah, Simufunila Dziko lino zabwino, koma Mufuna DPP yanu yokupha Ma Albino, Ma black outs aja, Miseu yogumuka ija Aaaah, inu nga DPP basi komanso mwatatsa poti Wonder ndi Bayana Chunga palibe. Aaaah inunso mumakondwela ndi DPP yanu ija iyaaa ndipo simunati, Chakwera ndi Mpakana 2030 wooooo!!!!
@GraceLakatika14 күн бұрын
Tiyeni nazoni 🙆
@thomasmcbanda979415 күн бұрын
Inu ndimadoro koma number 1
@chisomokotamu756312 күн бұрын
Koma mwaziziwa kuti kuseliku aneba anu akukukambilanani???
@LysonMkomadzinja17 күн бұрын
12:45
@HaloonChikoko18 күн бұрын
Atsukuluzi mukambazo ndizowona APLE wa alindi ndivuto
@JoiceNkhoma-s1m18 күн бұрын
Brian hot current ipatseni 3hrs sure olo even do it everyday. Please
@RodrickMwakatundu-gl6yo17 күн бұрын
Ufa sakandira ndi madzi owira,mcp nthawi yatha
@StiveneChikafa18 күн бұрын
Brian ndi anzanu awuzeni atsogoleri azipani zonse kuti asamati anthu akutifuna koma aziti ndikufuna kulamula kuti zofuna zanga zitheke
@MexcoJepter-p5f17 күн бұрын
Mai kabwira polani moto,Boma silomwelo inde
@FatimaAyami16 күн бұрын
😂😂ndinachoka ku south africa kupita ku bluenfornteen ,,,,k kkkk mesa bluenfornteen ndiye south africayo,,,ok koma abusa mumatinvetsa kukoma lets go!!!!
@DanMhone-iw6xg18 күн бұрын
Boma silomweli zona zake
@constancemkandawire737818 күн бұрын
Ndalamazo nde zikumapezeka ku zambia,no one to be held accountable No arrest no nothing ......aaaaaaaash why malawi every thing looks like is falling apart instead of fixing the economy ali besy kutukwanana mumisonkhano aaaaaaaaaa fwiti iyo ili kulowa malawi i think njanakazi iwenge yanalume nthe yagowoka Lord come rescue us
@eliffagondewe821418 күн бұрын
So sad 💔
@paulphalandwa313312 күн бұрын
Apankuku ndi Abanda musadzafe mudzangosowa
@yusufbakali17 күн бұрын
Imf must must go out of Malawi
@corretabanda768518 күн бұрын
MCP must go for Malawians to survive. Ambuye tsegulani maso ndi mitima ya ma sapota a mcp onse kuti adziwe choonadi.
Eti nkumati boma ndi lomweli? Mutikakamiz bwanji?😂😂. Mwatitolatu a malawife😂
@LightonNdala17 күн бұрын
Apa ndiye hot current yasukuluzadi. Wokumva wamva.
@freddyndzukuma135718 күн бұрын
To times .check what dpp says kumisonkhano yowo .amaloza zinthu anapanga ndi iwowo yet ndimitsonkho ya amalawi. Don't look one side here I think she is answer the dpp party. Onsewa angosiya zoloza zomwe zikuchitika zonkhudza boma. Or dpp isiye nyimbo ya lozani zanu
@SolomonNjolomole18 күн бұрын
Palibe chanzeru mwakamba apa nanu nkhani ndi kagwilitsidwe ntchito ka misonkho yathuyo coz sangatenge zamuthumba mwao amaloza zomwe apanga pamene enaso apatsidwa mpata omweo km zikuwakanika tsono kumaganiza kmso kumazindikira zinthu.
@MarthaBango18 күн бұрын
Bwanji?mwadwala?
@YohaneKaluzi18 күн бұрын
Brian usachoke pa hot current ,a ndevu za mwai akabwela mwapase mpando mbali inao coz amasisititsa kwambiri.