Zachipani ndiye kuchezera president uja, koma vice president atasowa kuimitsa operation yofufuza😢
@marthachakoma45582 ай бұрын
Papàappppaapaďpp,źxd'ź,,,,
@retirementtoafrica2 ай бұрын
Thank you mr pankuku for not being bias
@NchebeMilliyano2 ай бұрын
Chikangawa sadzawinaso ,Mr chikangawa where is Mr chilima kafana koganiza bho Kali kuti ?
@EnockChembe2 ай бұрын
Moti aukufziwa komwe adapita chilima
@mazumabekumwenda38762 ай бұрын
I support, the idea Mumba to be considered in the cabinet. I believe he can deliver
@AnnaPhiri-b8t2 ай бұрын
Tinavota chifukwa Cha chilima osati iyeyo Mr chikangawa
@imraanJafal2 ай бұрын
Koma bwanji sanapite ku chikangawa kod kuonetsa utsongoleli PA bwino pokha pamavuto ai
@DumisanMkandawre2 ай бұрын
Good message to Mr President
@MsondaBanda2 ай бұрын
And it's good a leader must show a strong leadership not to keep quiet where things are not going well, he must talk where things are not ok
@MOGAMW2 ай бұрын
Chikangawa era ija bwanj sanachezele nawo instead anaimisa operation rescuë
@violetkamvanthupi24432 ай бұрын
Watching from nsipe
@GodfreyWhayo-hh1dm2 ай бұрын
Ndikadakhala a Chakwera , anyamata akalewa ndikadaganizira mozama chifukwa anagwira ntchito yayikulu kuima nawo limodzi pa nkhani ya ngozi ya ndege yaku Chikangawa .
@TopoTopo-bm4vw2 ай бұрын
Kuchezela ku vote zikungowoneselati kuti MCP kulibe m'gwilizano ,,,,a peter or asachezele zilibe ntchito bola ngati anthuwo akugwiliza ngati chilungamo chilipo,,,,,, komaso kodi achilima atasowa munangona kusonyeza kuti mcp yose inali ndi plan yokupha chilima
@DeeHMugonya2 ай бұрын
Too later..kumanena za CHAKWERA lero tizimuyamikira munthu chifukwa sanagone!! MALAWI tachangamukani chabwino sanagone, koma ziganizo zake ndi zogona ndiye chabwino nchani?.
@JustinWBanda2 ай бұрын
Koma chakwela kungomupasaso mpatu olamulila chaka chamawa tili mmazi
Kodi Makosana, zoti voice ya intro yo siimveka zimenezo simudziwabe mpaka pano?
@FRANCISKAMPIRA2 ай бұрын
Good news
@MercyKatongo-p9b2 ай бұрын
😂😂😂 guys you always make my day
@masterchitabwino8982 ай бұрын
He can talk but no will to make it. Corruption now is beyond measure which was one of the songs be4. We have seen people playing around with public funds and he even backed up Chithyola no action was taken. Words vs Actions
@MitchChanza2 ай бұрын
Khala ngati Unifrom Ya Lunzu Secondary tu 😂
@GodfreyWhayo-hh1dm2 ай бұрын
MCP is a divided party .From the women's dressing you can tell that some are continuously loyal to the first founder of the Party than the current leadership .
@AlexKaunda-ny2eg2 ай бұрын
Joyce Banda tamuwudze kuti adzikango peleka yakumbuyo kwa banda iya sangakhaleso president
@tamalangoma27652 ай бұрын
🤣🤣🤣🤣 She's is too old and fat to manage that kkkkkk
@Vascomw2 ай бұрын
🔥🔥🔥
@PatrickSomanje2 ай бұрын
2 late chikangawa we never forget Malawians waiting for report and we know who is chakwela
@juliochiwalo2 ай бұрын
Is chifundo zimba in Malawi or abroad
@haroldchirombo79182 ай бұрын
Background music mwina itasikako bwana ikumazasokoneza pomvesela koma timakunyadilani
Ada kanikilanji kugona itasowa ndege ya chilima koma uko paka kuchezela osaopa osafowoka osagonja ndizafela ndembela UT ikuwina mzimu wachilima uuse mtendele
@vussoh002 ай бұрын
With the new alliance if they fall out they should vote again if the fall out is less than 50%+1
@PatrickSomanje2 ай бұрын
Kodi chakwela anapha dala chilima ndipo Malawi waiting for u chakwela
@sylvesteralfred83552 ай бұрын
Achunga mukuti democracy ikuyenda just because Chakwera anangoti aloleni akumpotonso avote basi aaaah aMalawinso timaiwala mwachangu bwanji
@user-ux3ed3ni1p2 ай бұрын
Palibe kulekanitsa mphamvu pakati pa Executive ndi nyumba yamalamulo Gotani Hara is compromised.
@kadijachilwan9672 ай бұрын
😂😂 mpaka mutharika angachezere😂😂😂😂
@burnetkalembere45282 ай бұрын
Anyamata mumakhazula osanyengerela koma kamajekete asamupatseso unduna
@retirementtoafrica2 ай бұрын
Bring back obanda to chair awa amapereka ma restrictions
@MosesNkumaniza2 ай бұрын
Awa sangalongosole zinthuchifukwa Cha anthu womwe amati chipani ndi Cha makolo kunyoza tsongoleri
Awa nchifukwa chake Peter Mutharika amafuna kuwamanga nkhani ya Cashgate kkkkkk.
@AlickChikaonda2 ай бұрын
Kuchedzera kin covension sizikutanthaudz kuwina
@FractionMailosi-p3n2 ай бұрын
DPP zivele mtolo
@GeorgeNamonde-sy5ue2 ай бұрын
Anachedwa
@raymondchilimba70102 ай бұрын
President Chakwera not just A Chakwera, mwatani Kodi?
@MzadziWanga2 ай бұрын
😂😂😂. Nde chomwe chingasinthe nchani mweteremu , mwadya nyama??
@MaryNyirenda-nq3mh2 ай бұрын
Kod chakwera ndindan Mr chikangawa not president President amakhara ndichifundo ndi anthu ena koma upule wakubanja kwake kokha chifukwa chake anthu amangot chakwera chikangawa