INTERVIEW YOMWE YADODOMETSA OPPOSITION YA PRO PETER MUTHALIKA YOMWE NDAPELEKA COMMENT YA CHICHEWA|

  Рет қаралды 32,775

DZIWE TV

DZIWE TV

Күн бұрын

Пікірлер: 102
@augustMag
@augustMag Ай бұрын
Even Mr Chakwera sangayakhe kwamphamvu chotere akanayankha zopanda pake ndichifukwa akuluakulu amati Munthu wachikulire akankhala pamudzi mumakapemphako nzeru amatinso munthu wachikulire ndi m dambo modzimila moto mmmm momwe ayankhulira a APM dziko la Malawi likudikira Inu adad 2025 🔥🔥💃💃💃💃 Malawi ikuyembekeza munthu ngati inu❤❤🥳🥳🥳🥳
@MuhireDominic-rw4vf
@MuhireDominic-rw4vf Ай бұрын
Funso la nepotism 😂 brian kungot zii atakwapulidwa
@user-eu1cx9gp5w
@user-eu1cx9gp5w Ай бұрын
❤ awa ndiye machine a dziko I love the speech it makes sense that this is good to me and Malawians who love the country
@StanleyKusakala
@StanleyKusakala Ай бұрын
Q
@RodgersPhiri-ju1eo
@RodgersPhiri-ju1eo 15 күн бұрын
Mukunama inu nanga munamchoselanji bozabasi ingonenani kuti ndinu a DPP palibe angakonze Malawi
@DalitsoTanganyika-gw9qi
@DalitsoTanganyika-gw9qi Ай бұрын
We are praying for you
@user-xs2xc1nl5r
@user-xs2xc1nl5r Ай бұрын
Munthuyu mmmm sikuti wakalamba mmene ife tuganizira ,mmutu Mwake muli mnzerube kobasi,angomusiya Ngati kuli kumbwita akambwite yekha koma amusiye ayese mwayi basi.
@user-wr1km2gh4g
@user-wr1km2gh4g Ай бұрын
Sawe are on your side, keep well, wishing you all the best
@FosterChilumba
@FosterChilumba Ай бұрын
Nzerutu izi from the leader simwantere mwantere coz he speaks his English from the nose English is a language even pple who did not go to school can speak English A Malawi anabesa posankha Lazaro
@ophlexmkondowe8107
@ophlexmkondowe8107 Ай бұрын
Welcome back APM,I didn't see anything bad with you.
@lindiwematanya9716
@lindiwematanya9716 Ай бұрын
That is very true Sir APM global problems are there in world everytime
@lindiwematanya9716
@lindiwematanya9716 Ай бұрын
Bwana APM mukunena zoona zoti zikalata zokavotera zitakhalanso monga: chauzika, passport, kalata ya kwa Mfumu ndi driving license zingathandizetu kuti a Malawi akhale ndi mwayi woka vota
@user-lz6lr8bv9t
@user-lz6lr8bv9t Ай бұрын
A p m kuyankhula mwanzelu komaso mwamphavu kuposa, mbuzi chakwera
@user-do2cs8nf4b
@user-do2cs8nf4b Ай бұрын
I silute you ADAD may the almighty God give you a long life❤
@olivemalomboza9010
@olivemalomboza9010 Ай бұрын
I also sit on chair because of my back pain Is there anything wrong with that??
@mashallahleonard2793
@mashallahleonard2793 Ай бұрын
Adad osaopa ndpo osayang'ana mbuyo maso patsogolo Boma mwalitenga ilii🔥🔥🔥
@kazembewailesi
@kazembewailesi Ай бұрын
Powerful interview, APM my vote.
@HarryChizengo
@HarryChizengo Ай бұрын
Ngati sunapite ku xool sukuyenera kumakamba nawo za anthu ozindikira ase DPP ❤
@user-vo7cb4cv5d
@user-vo7cb4cv5d 24 күн бұрын
1 Billion imeneyo aimaliza agaru ali panowa
@DamianoKapachika-ft1ye
@DamianoKapachika-ft1ye Ай бұрын
Big man
@YusufuKaifa-fr4wt
@YusufuKaifa-fr4wt Ай бұрын
❤ ❤❤ my vote to adadi long life
@thomasyohane987
@thomasyohane987 Ай бұрын
My vote ❤❤❤
@InnocentMtakulamusi
@InnocentMtakulamusi 27 күн бұрын
The best person to rescue this country
@user-eu1cx9gp5w
@user-eu1cx9gp5w Ай бұрын
Brian Banda wakumana ndi machine a boma, Peter Mutharika,adadi ndi katundu
@user-fr4gb4bq6q
@user-fr4gb4bq6q Ай бұрын
❤❤❤❤ you Mr APM God bless you and protect you
@shayrafernandeslatif9556
@shayrafernandeslatif9556 Ай бұрын
I agree wt APM we are a failed state n worse
@mollymasangano473
@mollymasangano473 Ай бұрын
It was abig mistake for my fellow MALAWI 🇲🇼 today the COUNTRY is in the HOT SUPU 🔥 🥵 ADADI receive my VOTES ❤🎉❤🎉❤🎉❤
@WilsonLimited-os1xd
@WilsonLimited-os1xd Ай бұрын
Tikavota opanda ID nrb ikutiputsitsa kwambili
@SandraBanda-hd1li
@SandraBanda-hd1li Ай бұрын
Adad. aaaa. ndagoma. nanu. njala. anthu. Kumafa nayo. chifukwa. chosowa ndalama. yogulira. Chakudya koma. President. a kuona..., what. nonsense. Chakwera
@user-uc1pd1tc2x
@user-uc1pd1tc2x Ай бұрын
Our only Dad, my vote❤❤❤❤❤❤❤
@LusunguMkandawire-fh5eq
@LusunguMkandawire-fh5eq Ай бұрын
Long life dad 🥰
@user-vh9uk1jy7w
@user-vh9uk1jy7w Ай бұрын
Long life dad
@user-wd9yd1bg9n
@user-wd9yd1bg9n Ай бұрын
Man in action
@YamzyAmos
@YamzyAmos 10 күн бұрын
Ndife ana ADADIIIII❤
@jamesphillipo9952
@jamesphillipo9952 Ай бұрын
He is a genius
@LukaThawe
@LukaThawe Ай бұрын
Mbuziiii Peter aliyese amapita kumanda samakhala pampando kumeneko ndikupusa. Iye angonena Kuti sangayime nthawi yayitali wakalamba iyaaa
@JaneJames-rb6js
@JaneJames-rb6js Ай бұрын
We really want u Adad
@DalitsoTanganyika-gw9qi
@DalitsoTanganyika-gw9qi Ай бұрын
Mafumu komanso abusa amakhala pa mpamdo Ku maliro,akanakhala mpasi ndiye omwalirayo akadadzuka?
@SteveriaChakalamba
@SteveriaChakalamba 28 күн бұрын
Adad woyeeee❤
@andrewkalukho
@andrewkalukho Ай бұрын
Boma 💙💙💙2025
@user-oq5rg5mz7q
@user-oq5rg5mz7q Ай бұрын
Mbavu💪 chimakhala chibadwa, sakuwelenga pepala koma akuyankhula zambavu, akanakhala chakwela ndi peplalake zaziiiiiii 😢 AMP my vote
@user-wx1jt5fd2j
@user-wx1jt5fd2j Ай бұрын
Tikukumvesesani adadi liphuleni ziko lamalawi pa moto amalawi tisazachitenso mistake awiri komanso zakhaleni ndi ma adivaiza okonda kuthandiza anthu awo osati adyera opanda chisoni opanda chifundo ongoona Bola zawo zikuyenda mafuno a bwino no kwa adadi God be on your side
@MackenzieChipeta
@MackenzieChipeta Ай бұрын
Koma kuimba atakuima koma kampeni akwanitsa kuyenda paliponse ndithandauza kuti a former president ndi akulu
@AhmadumkomaTambala-lr9gp
@AhmadumkomaTambala-lr9gp Ай бұрын
❤❤❤❤❤❤🎉🎉🎉
@marryphili5419
@marryphili5419 Ай бұрын
We're waiting for you adadi mwina mungazatichotse ku bagamoyo kuli mavuto wochuluka
@HendersonNkhoma
@HendersonNkhoma Ай бұрын
Big boss AMP more fire🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉
@georgemponda
@georgemponda Ай бұрын
A leader with skill never condemn other than find solution to solve matters thats Peter Munthalika... I think Malawians have learnt a lesson from mcp government.....
@YusufuUsumani
@YusufuUsumani Ай бұрын
@JonesChingaya-yf4gg
@JonesChingaya-yf4gg Ай бұрын
Thus the voice of the President to be, God is keeping you for a reason. Good answers from APM,
@user-po6ir6eh4z
@user-po6ir6eh4z Ай бұрын
Apm more fire its my vote
@dusterelias6805
@dusterelias6805 21 күн бұрын
A malawi amaiwalakwambili mukuziwa Congress party inalienable ya chabe mukuziwa zimenezo inu mmalawi munabvotelanso yomweyo simunaganize bwino
@FractionSyless
@FractionSyless Ай бұрын
❤❤❤
@aarondickson70
@aarondickson70 Ай бұрын
APM put all things to almighty God to pull back Malawian who are now going to Bagamoyo
@RodgersPhiri-ju1eo
@RodgersPhiri-ju1eo 15 күн бұрын
This is just campaigning issue if fuel is getting up here in South Africa almost every month what about Malawi
@YasinAdam-pn4bh
@YasinAdam-pn4bh Ай бұрын
❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
@atusayeMtalama
@atusayeMtalama Ай бұрын
Ndezodabwisa pamenepo poti anakhala pampando ku maliro?
@YusufuUsumani
@YusufuUsumani Ай бұрын
adadi❤
@gladysbonongwe1038
@gladysbonongwe1038 Ай бұрын
Timakunyadirani dad
@IbrahimSquare
@IbrahimSquare 27 күн бұрын
Zochitisa manyazi presdent wosasata chikhalidwe cha ziko lache kumanda sitikhala pa mpando shame
@chifundopetro422
@chifundopetro422 Ай бұрын
Micaso socasa
@samdiverson9733
@samdiverson9733 Ай бұрын
APM machine machine kwamtele out
@williamsalexmbonga
@williamsalexmbonga Ай бұрын
Ndi nthawi yandani ija munkati anthu azidya ziwala ija?
@user-nx7yz4qo8f
@user-nx7yz4qo8f Ай бұрын
Mabodzatu ammenewo,mpandowo unapitaki bwanji kumaliroko? Ndiposo anthu amakhaliratu mpando kumaliro
@DANIELLUCKY-wc4ny
@DANIELLUCKY-wc4ny Ай бұрын
Our last hope APM my vote
@HedgensChisale
@HedgensChisale Ай бұрын
Adadi omwewo
@GloriousPhiri-tv3rw
@GloriousPhiri-tv3rw 20 күн бұрын
He is going to lose miserably and that's when he will understand that Malawi is not the same
@LuteSynos
@LuteSynos Ай бұрын
Vote andandi❤❤❤❤
@mollymasangano473
@mollymasangano473 Ай бұрын
Kikikiikiki koma anakwapulidwadi Brain Banda Hahaha didn't employee his Children he didn't send his children to embassy 😂😂❤
@beinhardkausiwa7107
@beinhardkausiwa7107 Ай бұрын
My president APM❤
@user-ve4yl1gq8e
@user-ve4yl1gq8e Ай бұрын
Interview inali bwino kwambiri koma bambo Brian muchepetse zizunguzo ambilife ku xool sitinapite 🤔🤔🤔🤔🤔🤔
@user-ph2dw9qt1l
@user-ph2dw9qt1l Ай бұрын
APM was sleeping on his job NEVER vote him again
@user-dd4mn3yk4f
@user-dd4mn3yk4f Ай бұрын
APM my vote❤❤❤❤
@user-ux9ik4zr5x
@user-ux9ik4zr5x Ай бұрын
Apm is just selfish & greedy, he didn't born a politician but because of our stupidity after his brothers death we gim him power,There's no permanent enemy in politics but this man still keeps anger between Joyce Banda.Muluzi is the one who could have be angry with Mutharikas family of what they did with UDF but he shows that he's a real politician.
@user-eh1mg3ww6d
@user-eh1mg3ww6d Ай бұрын
Adad omweo kuti wawaa❤❤❤
@samdiverson9733
@samdiverson9733 Ай бұрын
only hope for malawians APM back in 2025
@user-eh1mg3ww6d
@user-eh1mg3ww6d Ай бұрын
@@samdiverson9733 sure
@user-bi6pb5gc8t
@user-bi6pb5gc8t Ай бұрын
Enterview iye kwaine sinandisangalasi chifukwa yakampindwa mchizungu enafe kuaukulu sitinapiteko nkhani ili APA ndiyamalawi vuto ndichani kulankhula cyichewa Kuti nafenso timveko mwina kapena enterview imeneyi mumapangila kuamerika
@patrickmacheso5062
@patrickmacheso5062 Ай бұрын
Mutseke Dambwe mutsekula sukulu.
@GloriousPhiri-tv3rw
@GloriousPhiri-tv3rw 20 күн бұрын
This gogo will learn the hard way. He thinks he knows everything. Remember in his time he use to tell the hunger-stricken people to go and eat grasshoppers . And also told government workers to go for private sectors or work outside Malawi if they want to prosper
@yusufsadic2930
@yusufsadic2930 Ай бұрын
Amagomeranso kt mukwanamiz ndan
@user-eh1mg3ww6d
@user-eh1mg3ww6d Ай бұрын
Ndipo mulungu akupatseni moyo wathazi kuti Satana achite manyazi
@user-vl5on2lj8b
@user-vl5on2lj8b Ай бұрын
Kutanthaudziraku mukuchita bwino chifukwa sitonse timamva chizungu
@tisuhmakhwah7085
@tisuhmakhwah7085 Ай бұрын
APM NDI DEAL
@user-uc1pd1tc2x
@user-uc1pd1tc2x Ай бұрын
DPP❤❤❤❤
@user-bg7ur1gw1q
@user-bg7ur1gw1q Ай бұрын
Apm pampando
@SaidiMbawa-st6bj
@SaidiMbawa-st6bj Ай бұрын
Interview yonse ya chizungu ngati amalawi ndi amzungu izi ndi zausilu ndiye kumamasulila gogo iyiso ngati kwerekwele
@patrickmacheso5062
@patrickmacheso5062 Ай бұрын
Paja mumapita ku Dambwe mmalo mopita ku sukulu that's why.
@SaidiMbawa-st6bj
@SaidiMbawa-st6bj Ай бұрын
@@patrickmacheso5062 Uziwuza azako akumangochi osati ine ndilibe nazo ntchito
@patrickmacheso5062
@patrickmacheso5062 Ай бұрын
@@SaidiMbawa-st6bj Anzanga akumangochi??? Ine si Mulawo aise ngati ukufuna kudziwa za ine undipeza ku page house kwa APM.
@user-oe1lg4xo7w
@user-oe1lg4xo7w Ай бұрын
M C P imati APM wakalamba , funso ndirakuti munthu Okalamba angamayankhe mafunso mwamphamvu ndi mwadongosolo moteromu? Adad ndimphaso yochokera kwa Mulungu palibenso angamake pa APM
@kingsleyhopematchaya5184
@kingsleyhopematchaya5184 Ай бұрын
Ndi mnyamata apm iwe sudziwa
@eliffagondewe8214
@eliffagondewe8214 Ай бұрын
Mcp ndi olephera ndipo apm akuwapatsa theng'enenge 🔥🔥
@williamsalexmbonga
@williamsalexmbonga Ай бұрын
So this guy is claiming that He will do better the things he failed to do in his 10 years of leadership? What a joke in Malawi 😂😂😂
@samungwira6927
@samungwira6927 Ай бұрын
Imwe mwatuka apa nkhalo mulije God should punish you
@user-nc4vi1jt5g
@user-nc4vi1jt5g Ай бұрын
Boloyako apm kuno sikuamereca
@user-qv4ko6ps4j
@user-qv4ko6ps4j Ай бұрын
Bambo onso yawo
@mashallahleonard2793
@mashallahleonard2793 Ай бұрын
Iweso chitsiru Makolo ako akuvutika ndnjala abale akowo ali president
@user-pt8wb4vw6r
@user-pt8wb4vw6r Ай бұрын
Dyela agogo nkhamba zoona kuddp kulibe wanzelu kuposa gogoyu moti ndimbuli zokha zokha malawi yonse wanzelu ndi gogo nkhalambayi tizivele chifundo
@YusufChikweo
@YusufChikweo Ай бұрын
Anyamata omwe mukufunawo ndamene akukulamulani panowa, ziko limaendetsedwa ndi nzeru zakuya noti mphavu zonyamulira njerwa even akanakhala kuti Ali ndi Zakaria 100 tikanamuvoterabe
@beinhardkausiwa7107
@beinhardkausiwa7107 Ай бұрын
Nzeru ulibe ndaonera zolemba zakozi
@PaulLuka-hz3hd
@PaulLuka-hz3hd Ай бұрын
Talembani modekha phone ndiyanu
@EllenLuwanika-tl5ck
@EllenLuwanika-tl5ck 21 күн бұрын
Osandau tiku Ku pephereni nthawi zone mulungu ndiwakulu
Beyond The Last Mile   - The Story of Rose Magayi #Film4Health
8:01
Eccentric clown jack #short #angel #clown
00:33
Super Beauty team
Рет қаралды 19 МЛН
ONE MORE SUBSCRIBER FOR 6 MILLION!
00:38
Horror Skunx
Рет қаралды 11 МЛН
100❤️ #shorts #construction #mizumayuuki
00:18
MY💝No War🤝
Рет қаралды 20 МЛН
Cute Barbie gadgets 🩷💛
01:00
TheSoul Music Family
Рет қаралды 71 МЛН
Misomali Ya Six Inches Yothana Ndi Zipani Zotsutsa - Bon Kalindo
17:18
Times Exclusive featuring Bon Kalindo - 6 January 2024
1:03:20
Times 360 Malawi
Рет қаралды 200 М.
Su cosa è costruita la nostra SOCIETÀ?
19:16
Will Media
Рет қаралды 18 М.
Какой смысл худеть к лету? / Редакция
49:15
Редакция
Рет қаралды 705 М.
CRUISE 5 WITH MLAKA MALIRO PART  1
42:04
Zodiak Malawi
Рет қаралды 29 М.
Napoleon Dzombe speaks on Standard Bank Africa China Agent Proposition
2:35
Standard Bank Malawi
Рет қаралды 23 М.
CRUISE 5 WITH REV ALEXANDER KAMBIRI
46:48
Joab Frank Chakhaza
Рет қаралды 176 М.
Times Exclusive featuring Peter Mutharika - 20 April 2024
1:05:34
Times 360 Malawi
Рет қаралды 165 М.
KWAVUTA LERO NDE WATOKOTA PA 30 MAY 2024 |
15:08
DZIWE TV
Рет қаралды 10 М.
Eccentric clown jack #short #angel #clown
00:33
Super Beauty team
Рет қаралды 19 МЛН