KU HOT CURRENT KWATENTHERATU

  Рет қаралды 15,987

HOT 265

HOT 265

10 күн бұрын

Пікірлер: 45
@AlexKaunda-ny2eg
@AlexKaunda-ny2eg 8 күн бұрын
Hee bwanji pamaliro achilima munalephela kusegula mlomo chochi bwanji simunena kuti chakwera ali ndi dyela loipa mpaka kupha munthu sure chifukwa cha 5years😢😢😢 machende ake
@user-lb6ek3ee6d
@user-lb6ek3ee6d 8 күн бұрын
Malawi ndi chitsazo chabwino cha kusauka koma zikukhala zovetsa choni kwambiri mpaka pano ma President adakalibelabe a Malawi ndi President yekhayo yemwe amandisangalatsa Professor Dingu wa Muthalika zimu wawo ukuse mu ntendere adasitha zithu kwambiri osati izi tikuziona panozi manyaka enieni the must go out stupid Government
@stevenchirwa5028
@stevenchirwa5028 8 күн бұрын
Don't just talk we need action to change Malawi 🇲🇼
@yusufbakali
@yusufbakali 8 күн бұрын
Nduna zaboma zosezakuba zimangidwe it only one way katangale akhoza kuta akamangidwa no belo ndende basi akagwire
@RobertLuka-wy9cl
@RobertLuka-wy9cl 8 күн бұрын
🙏🙏🙏🙏🙏🙏Anyamata lero muli bwino kwambili 🙏🙏🙏🙏🙏🙏
@JustinChiwale
@JustinChiwale 8 күн бұрын
Khoswe akakhala pakhate sapheka Malawi we can't fight against corruption
@user-un6qv6sj3h
@user-un6qv6sj3h 8 күн бұрын
Kkkkkk anyamata inu leroli ndakupatsani 100 pa 100 ❤❤❤ guys iyiyi ndiye hot current
@SamukLungu-zg7fl
@SamukLungu-zg7fl 8 күн бұрын
Talk guys we are together but don't eat baz from chakwera
@ahmedmsume1489
@ahmedmsume1489 8 күн бұрын
Akuonesana zikwanje inu lero mwatasa 😂😂😂😂
@RaymondKaumba
@RaymondKaumba 8 күн бұрын
Vuto ndale zanthu zimapatsa mphanvu president.koma democracy parliament ndiyomwe imakhala ndi mphanvu yolemba ACB director azipanganso report Ku parliament basi
@g_forcemusician4242
@g_forcemusician4242 8 күн бұрын
2025 we choose wisely
@AlexKaunda-ny2eg
@AlexKaunda-ny2eg 8 күн бұрын
Abida mia wapelekera bwino kwachakwera😂tiona dzinthu yakumbuyo😂😂
@AlexKaunda-ny2eg
@AlexKaunda-ny2eg 8 күн бұрын
Kuti katangale kuti athe muphe chakwera ndi chimbava choipa kuchokela kumpingo that's why he kill chilima
@paulpaseli6310
@paulpaseli6310 8 күн бұрын
Lelo mwayakhula zokomela athu osaukano. Osati zachamba zanu zinja.
@williamdaka79
@williamdaka79 6 күн бұрын
Apo mwanena ndithu omva amva
@user-wx1jt5fd2j
@user-wx1jt5fd2j 8 күн бұрын
We need to change this leadership
@SheenahMwalabu-iz3pr
@SheenahMwalabu-iz3pr 8 күн бұрын
Ajona mwamvatu malango anga kkk cz ndeumabowa bolako lero ❤
@thulanimpphiri6873
@thulanimpphiri6873 8 күн бұрын
Kumalawi tili ndivuto katangale sangathe. Chifukwa ndi culture. Katangale ngati mukufuna kuti athe choyamba president akhale oopa Mulungu komaso akhale osanama chachiwiri azikhala ndinthawi yotendera ma office mwazizuzi osawawuza anthu ogwira ntchito. Chachitatu a police a traffic army ikhale yachilungamo ndipo asavere boma pankhani za katangale. Simungathane ndikatamgale pamene oteteza ziko ndi amene akuchita katangale ndiye mukugani anthu angasiye katangale
@thulanimpphiri6873
@thulanimpphiri6873 8 күн бұрын
Nkhani ya police kuti alibe uniform sapata zili bwino ngati akuvutika choncho chifukwa apolice wo ndi amene akumanga anthu akamazuzula boma so azivutika motero
@Moses51
@Moses51 8 күн бұрын
Chakwela ndigalu kwabasi
@SaukaniMbiliyawanda-ur7zb
@SaukaniMbiliyawanda-ur7zb 8 күн бұрын
Amene sanachimweko ayambe kumugenda miyala
@TarPoor-ye9jx
@TarPoor-ye9jx 7 күн бұрын
Lero ndaziwa kut anthu chilungamo akuchziwa koma mantha mcp ndi chakwera anthu atopa nawo kkkk 😂😂anthu amaba koma tonse yalepera pazonse kuba kuli pa high too much
@user-cf9yz3ei5o
@user-cf9yz3ei5o 8 күн бұрын
we shall be singing like this for how long
@StevenMjMbama
@StevenMjMbama 8 күн бұрын
Guys big up kwinako muzitchulako mayina aaaanthu amene akumapanga katangale
@AustinNkhula-j6y
@AustinNkhula-j6y 8 күн бұрын
Ttv awunikileni anthu aziwe zenizeni tatopa ife ndianyapapiwa
@IssacMateyo
@IssacMateyo 8 күн бұрын
Chakwela akufunika kuti achoke ndimuthu wakuba komaso dzikoli linalo bwino koma chakwela waononga kwambili zedi koma 2025 aona nyekhwe
@paulpaseli6310
@paulpaseli6310 8 күн бұрын
Bon kalindo anayakhula kt aku prison akudandaula kt iwo palibe amapita muziwaganizila km mukati wamisala
@Austinyonah
@Austinyonah 8 күн бұрын
Kuyankhula kwabwino
@Trancy-xt4py
@Trancy-xt4py 8 күн бұрын
Ambuye mulungu wanga mudapereka mwana wanu modzi yekha yemweyo kufera ifeyo ochimwa kudzuzika yesu chifukwa chaife , kodi ngat mudalora mwana wanu modzi yekha kufera ife ,simungalore yehova wina osakhala mwana wanu kuti angofa yekha kutulo osadwara ai kuti afere ifeyo amalawi tatopa naye ndiy skhale Chakwerayu ambuye ndimvereni mbuye wanga Chakwerayi atifere ife chifukwa wanyañya tikumvutika musadzuze ndimatenda ai akangogona apitilirekonko kuti tipume mbuye wanga ndimvereni yehova chskwerat akutidxuza musakhare chete yehova akhoza kumayesa ngat mulibe phamvu ngat safera kutola koma afeeee chakwera kuti nduna zake ziziwe kuti inuyo mdinu owopsa yehova
@AustinNkhula-j6y
@AustinNkhula-j6y 8 күн бұрын
@@Trancy-xt4py eee koma yaa
@HarryMsudzula
@HarryMsudzula 8 күн бұрын
Sinanga ntchito zina akanatha kugwira aprison like kugadira mayeso ameneb anaipereka ku mdf omwe sizimayenera kutero malinga ndi nature yantchito yawo
@Moses51
@Moses51 8 күн бұрын
Aphana 🤣🤣🤣🤣
@IssacMateyo
@IssacMateyo 8 күн бұрын
Aona nyekhwe 2025
@WisikiBlack-gj4gu
@WisikiBlack-gj4gu 8 күн бұрын
Lelo maimatu pachilungamotu kunenachoona chomwe ngakhale ife akumudzi tikuziona masomu boma ili linangolowelamo Kuba basi, chifukwa chilima anangomunamizila kuti apeze mphata Obama bwino, after kuona kuti bodza anapangila chilima kunamizila Kuba, anaona kuti kubako otsogolela anali chakwela chifukwa anatetsa mulandu cholinga amuphe chifukwa anadziwa kuti chilima amadziwa zonse. Chakwela chakwela iweyo mulungu azikupangila za bwino
@KanjoIsaac-u1w
@KanjoIsaac-u1w 8 күн бұрын
Kkkkkkkkkkkk
@DalitsoulNchengah
@DalitsoulNchengah 8 күн бұрын
Ulemu wanu
@user-wx1jt5fd2j
@user-wx1jt5fd2j 8 күн бұрын
Anthu ena anagontha ku makhutu chifukwa cha matemberero
@peterchikwakwa8476
@peterchikwakwa8476 8 күн бұрын
Kikikikiki
@MusaManati-ho4zf
@MusaManati-ho4zf 8 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂
@SandramKambalame
@SandramKambalame 8 күн бұрын
Boma ilili ili ndi manyaka
@augustinechibbalazi8897
@augustinechibbalazi8897 8 күн бұрын
In Malawi we consider corruption as a problem.It is not a problem but the result of something.Therefore,to end corruption in Malawi we must list down main causes of corruption and get rid of them.
@giftmwango3214
@giftmwango3214 8 күн бұрын
You don't know what you are talking about
@IssacMateyo
@IssacMateyo 8 күн бұрын
Chakwela akufunika kuti achoke ndimuthu wakuba komaso dzikoli linalo bwino koma chakwela waononga kwambili zedi koma 2025 aona nyekhwe
@IssacMateyo
@IssacMateyo 8 күн бұрын
Chakwela akufunika kuti achoke ndimuthu wakuba komaso dzikoli linalo bwino koma chakwela waononga kwambili zedi koma 2025 aona nyekhwe
BON KALINDO LERO PA 16 JULY 2024 |
14:25
DZIWE TV
Рет қаралды 6 М.
DEFINITELY NOT HAPPENING ON MY WATCH! 😒
00:12
Laro Benz
Рет қаралды 49 МЛН
1 or 2?🐄
00:12
Kan Andrey
Рет қаралды 56 МЛН
- А что в креме? - Это кАкАооо! #КондитерДети
00:24
Телеканал ПЯТНИЦА
Рет қаралды 6 МЛН
MAU AMENE LUCIUS BANDA WASIYILA OYIMBA
12:48
Factory265 Media
Рет қаралды 9 М.
Lero mwamuona Yudas Skariyot Yemwe adampereka Yesu (Born Kalindo)!!
15:21
Malawian Cameras
Рет қаралды 25 М.
WAING'ALULA BON KALINDO LERO PA 16 July 2024
13:28
HOT 265
Рет қаралды 1,3 М.
"OCCUPY EVERYWHERE": WHY THE REVOLUTION WILL NOT END SOON!
22:54
Herman Manyora
Рет қаралды 35 М.
Louis Liebenberg || Facebook Live || 2024/07/14
1:39:16
Louis Liebenberg
Рет қаралды 4,6 М.