Hee bwanji pamaliro achilima munalephela kusegula mlomo chochi bwanji simunena kuti chakwera ali ndi dyela loipa mpaka kupha munthu sure chifukwa cha 5years😢😢😢 machende ake
@user-lb6ek3ee6d8 күн бұрын
Malawi ndi chitsazo chabwino cha kusauka koma zikukhala zovetsa choni kwambiri mpaka pano ma President adakalibelabe a Malawi ndi President yekhayo yemwe amandisangalatsa Professor Dingu wa Muthalika zimu wawo ukuse mu ntendere adasitha zithu kwambiri osati izi tikuziona panozi manyaka enieni the must go out stupid Government
@stevenchirwa50288 күн бұрын
Don't just talk we need action to change Malawi 🇲🇼
@yusufbakali8 күн бұрын
Nduna zaboma zosezakuba zimangidwe it only one way katangale akhoza kuta akamangidwa no belo ndende basi akagwire
@RobertLuka-wy9cl8 күн бұрын
🙏🙏🙏🙏🙏🙏Anyamata lero muli bwino kwambili 🙏🙏🙏🙏🙏🙏
@JustinChiwale8 күн бұрын
Khoswe akakhala pakhate sapheka Malawi we can't fight against corruption
@user-un6qv6sj3h8 күн бұрын
Kkkkkk anyamata inu leroli ndakupatsani 100 pa 100 ❤❤❤ guys iyiyi ndiye hot current
@SamukLungu-zg7fl8 күн бұрын
Talk guys we are together but don't eat baz from chakwera
@ahmedmsume14898 күн бұрын
Akuonesana zikwanje inu lero mwatasa 😂😂😂😂
@RaymondKaumba8 күн бұрын
Vuto ndale zanthu zimapatsa mphanvu president.koma democracy parliament ndiyomwe imakhala ndi mphanvu yolemba ACB director azipanganso report Ku parliament basi
@g_forcemusician42428 күн бұрын
2025 we choose wisely
@AlexKaunda-ny2eg8 күн бұрын
Abida mia wapelekera bwino kwachakwera😂tiona dzinthu yakumbuyo😂😂
@AlexKaunda-ny2eg8 күн бұрын
Kuti katangale kuti athe muphe chakwera ndi chimbava choipa kuchokela kumpingo that's why he kill chilima
Kumalawi tili ndivuto katangale sangathe. Chifukwa ndi culture. Katangale ngati mukufuna kuti athe choyamba president akhale oopa Mulungu komaso akhale osanama chachiwiri azikhala ndinthawi yotendera ma office mwazizuzi osawawuza anthu ogwira ntchito. Chachitatu a police a traffic army ikhale yachilungamo ndipo asavere boma pankhani za katangale. Simungathane ndikatamgale pamene oteteza ziko ndi amene akuchita katangale ndiye mukugani anthu angasiye katangale
@thulanimpphiri68738 күн бұрын
Nkhani ya police kuti alibe uniform sapata zili bwino ngati akuvutika choncho chifukwa apolice wo ndi amene akumanga anthu akamazuzula boma so azivutika motero
@Moses518 күн бұрын
Chakwela ndigalu kwabasi
@SaukaniMbiliyawanda-ur7zb8 күн бұрын
Amene sanachimweko ayambe kumugenda miyala
@TarPoor-ye9jx7 күн бұрын
Lero ndaziwa kut anthu chilungamo akuchziwa koma mantha mcp ndi chakwera anthu atopa nawo kkkk 😂😂anthu amaba koma tonse yalepera pazonse kuba kuli pa high too much
@user-cf9yz3ei5o8 күн бұрын
we shall be singing like this for how long
@StevenMjMbama8 күн бұрын
Guys big up kwinako muzitchulako mayina aaaanthu amene akumapanga katangale
Anthu ena anagontha ku makhutu chifukwa cha matemberero
@peterchikwakwa84768 күн бұрын
Kikikikiki
@MusaManati-ho4zf8 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂
@SandramKambalame8 күн бұрын
Boma ilili ili ndi manyaka
@augustinechibbalazi88978 күн бұрын
In Malawi we consider corruption as a problem.It is not a problem but the result of something.Therefore,to end corruption in Malawi we must list down main causes of corruption and get rid of them.
@giftmwango32148 күн бұрын
You don't know what you are talking about
@IssacMateyo8 күн бұрын
Chakwela akufunika kuti achoke ndimuthu wakuba komaso dzikoli linalo bwino koma chakwela waononga kwambili zedi koma 2025 aona nyekhwe
@IssacMateyo8 күн бұрын
Chakwela akufunika kuti achoke ndimuthu wakuba komaso dzikoli linalo bwino koma chakwela waononga kwambili zedi koma 2025 aona nyekhwe