The only wise and rational person who leaves a beautiful place where everything is going well and goes to live with the people who are suffering,will find favor in the presence of the almighty God.
@BrihippoАй бұрын
Komaso muthu akamwalila pamabeera wina basi
@JohnFrank-cg1yhАй бұрын
Tikuyenela kumapephela tsiku ndi tsiku, nthawi ndi nthawi chifukwa satana ndiwochenjela atha kutigwesa m'mayeseli
@user-sm6pr9cg2qАй бұрын
Zomwe adagwilizana chilima adanena pa press briefing kt ndi 5/5 ndy inu mukut anadziwana awili bwanji
@godfreyamos7452Ай бұрын
A Chawezi kunali amzathu , muzatha mosakhala bwino
Chawezi capaign director wa mcp banja likatha palibe za ulemu
@jameshuwanzuluАй бұрын
Or ndi dzina lomwelo likungosonyeza kut ndi wa MCP
@estonmnthali3719Ай бұрын
Chawezi ndi wa MCP
@idilissmuyer2914Ай бұрын
Pamtumbo panu inuyo mwasowa zokamba mamwapwala anu
@leonardmalirana7423Ай бұрын
Ngati, mgwirizano unali wa anthu awiri basi uthepo winayo anatisiya ndiye UTM isiyeni
@user-nf3ik3ff6yАй бұрын
Chawezi ndiwe Galu
@DysonUmaliАй бұрын
Whether the votes will be minus 20% we don't care . USI and the cabinet ministers can remain at MCP we don't care .The best Usi can do is to start his party and do the alliance with MCP . That will be his correct decision. He must not use UTM emblem because at UTM I don't see his impact achedwa kwambiri.
@user-qk2hw4ex3cАй бұрын
Chawedzi ndiwe osokonedza
@yotamumahomed1313Ай бұрын
Kod iweyo why ukukamira zimenezo ndiwe mbuzi et ?
@user-ck7eb7tb7vАй бұрын
Iwe apanga nthawi yoyenera, afufuza bwanji za ifa ali ku tonse komweko? Aasa!
Programe iyi kulibwino angoyithetsa chifukwa zimene zimakambidwa akumapanga back up mcp so palibe Amalawi yingatithandize Programe yanuyi ayi just suspend it
@SheenahMwalabu-iz3prАй бұрын
Kodi chawezi yu mumamutengelanji? Uyuyu adzandilakwitsa one day. Victor or abel, banda are the bes uyu ndiwa mcp. Sadzatheka Chawezi akupeza zabwino ku bomaku ndipo ativuta kulera 😅
@ChrissyluweАй бұрын
Chawez u hv no timing
@user-ml4bl2ll2gАй бұрын
Chawezi samalira ayise we know ukulimbana ndi azipani zotsutsa samalira ayise I know you are there for mcp
@DysonUmaliАй бұрын
Chaweza what you should know is we didn't do a hasty decision . It a fine a decision and you can't change it. We are not desperate rather and we as voters cannot take it Chawezi you are MCP and no body can listen to your views . Member wa nzeru cannot proceed to be in alliance with MCP .
@petroszgambo9949Ай бұрын
Useless program
@WisikiBlack-gj4guАй бұрын
Achilima anali odekha mtima, koma ku bwela kwawo ulendo wakunja uja koria,anali ndicholinga chotuluka mu tonse kale, koma tsoka asanaphume kubwela kwaku koria ,ndimene amapita kumarilo akusambala posadziwa kuti awusi chisisi anakamuuza kale chakwela, kodi zonsetu tikuzidziwa koma ndalama ndalama, koma mulungu simuthu
@leonardmalirana7423Ай бұрын
UTM IS NOT THE FIRST PARTY TO MOVE OUT OF THIS ALLIANCE , PEOPLE ARE TALKING ALOT BECAUSE IT HAS MANY YOUTH FOLLOWERS SO ZIKUBAYA ANTHU AMBIRI.
@user-si7po9sd5iАй бұрын
Where is victor
@Raph-kayRaph-kay-g5vАй бұрын
Chawezi uzafa ngati garu
@vincentkamangamr9062Ай бұрын
Chawezi umawoneselatu kuti ndiwe wa MCP all times on this program
@DysonUmaliАй бұрын
In life ngati mkazi wakukana olo mutalankhula motani it's helpless to the man. UTM is done with MCP
@WilfredChinkonoАй бұрын
DK simunthu wamba UTM ikutenga boma 2025
@UsumanLuwayoАй бұрын
Ngati Dewesi ali pa banja njofunika kumunyengera mkadzi wake nde kupanga dzoti anthu adzamugwire mkadziyo akuchita chigololo nde iyeyo adzamve, then tidzaone ngati adzadekhe osathetsa banja antil 3 months
@PaulChaleka-lb4vxАй бұрын
Chawezi ndi wa chakwera
@AliceChipeta-pc3nbАй бұрын
Chawezi chawezi chawezi
@ChikuMatembaАй бұрын
we don't like Chawezi on this Program
@BehindThecamera-xo1qgАй бұрын
Ulemu wa chani galu iwe chawezi, umamupasa ulemu munthu oipa
@BehindThecamera-xo1qgАй бұрын
Miyezi 4 inachuluka anthu ambiri akanasala ku mcp , achita bwino kutuluka fumbi la kuchikangawa lisanathe .
@DalitsoPhiri-sq5nlАй бұрын
Komatu chawedzi pena amayankhula ngati mbuli zedi kodi amene samadziwa kuti alliance ya utm ndi mcp inali yoti five yrs wina akhala president kenako wina azaimeso, ndi chifukwa ichi ndi chomwe chinabwelesa kusagwilizana cz ingakhale Dr late SKC ananena poyera kuti ngati Dr chakwera sakufuna kutula pansi udindo ndiye tiyenera tikavote. Utm kutuluka siinalakwise aii cz mcp siinalemekedze ingakhale imfa ya chilima mzinthu zambiri kumapanga msonkhano anthu akulilabe kenako uziti afulumira kutuluka ukhalike ndithu ngati akukunyemera tazingodya makobidiwo komano usaganize mombwambwana aiii
@user-lj7lm6ly7zАй бұрын
Ine anthu awa amandionekera mwa mcp cp eeee ndiye aaaa sinkonda kunvera zamenewa
@user-cs6zy3ix8dАй бұрын
Chawez ndi iwe mbuzi
@isaihmagani5697Ай бұрын
Chawezi wabodza iwe, sukuyenera kukhara analysis poti zuonekeratu ndiwe wa MCP
@PatrickDispleАй бұрын
He knows only how to speak but not to understand what he is speaking. Mr Chawezi 😅
@user-oc8nj3or6yАй бұрын
Ndi ntchito yawo,,,anali kuti? Nthawi yonseyi
@chimwemwechiundira6002Ай бұрын
Halayansi yabayatu
@tonnychimbiroАй бұрын
Zinthu zake
@PiusChawingaАй бұрын
Wabweza bwanji?
@user-my5jj5we5jАй бұрын
Unuso mukuziwa mugwilizano panalibe
@KestonNGUBOАй бұрын
Zoonad iwe
@user-gy8yn6qw2kАй бұрын
Ineyo i don't like this guy is not the best for me ........
@isaihmagani5697Ай бұрын
Chawezi ma comments ako ngooneseratu uli mbali yinayo uli against UTM