KWANUNKHA MWAZI KU MCP.

  Рет қаралды 39,494

LIKI-LIKI TELEVISION

LIKI-LIKI TELEVISION

Ай бұрын

Пікірлер: 124
@user-un6qv6sj3h
@user-un6qv6sj3h Ай бұрын
❤❤❤iyiyi mwanena zogwila mtima lero mwaonetsa u independent wa times keep it up
@user-lw2yp1rf4n
@user-lw2yp1rf4n Ай бұрын
Iyiyi nde yandifikapo ndithu big up Hot current 💪💪
@rosekaliwo5547
@rosekaliwo5547 Ай бұрын
Ulamuliro wa nkhanza inde pano school fees anthu tikulephera kulipira ndiye Ana aphunzire motan mmmm ambuye atithandize
@user-zq3li3qw1m
@user-zq3li3qw1m Ай бұрын
Zoonadi
@rameckmauranagerald9783
@rameckmauranagerald9783 27 күн бұрын
Kuyakhula mopanda mantha. Komaso mwaphawi zofunikira kwaose amalawi pabwino mkuyamikirana. Poipapo dzuzurani, rangizani akapanda kumva arekeni!!!!🎉
@RobertCosmas-bo1uo
@RobertCosmas-bo1uo 29 күн бұрын
Massive analysis this is good idea and solution zoonad katangale akhoza kutha zkufunika azitsogoleri odana ndizopusa that's right guys.
@xinalungu9616
@xinalungu9616 29 күн бұрын
For the first time Malawi can see great roads not just miyala ya madziko. I pray that Malawi wakes up. We should wake up n balance our forums
@IshumaelMbewe-d4t
@IshumaelMbewe-d4t 29 күн бұрын
Tidakhala ndi atsogoleri ophunzira angapo koma sitidatukike pa cbuma ndi zitukuko ndiye tidzayese mtsogoleri wa form 4
@ElizabethMajiga
@ElizabethMajiga 29 күн бұрын
Apa ponkhapa mwawalakhulila amalawi🎉🎉🎉🎉🎉🎉
@PetersenjMwale
@PetersenjMwale Ай бұрын
Mumapanga ma demo abwino not like born kalindo, thanx TTV
@gracemkandawire8769
@gracemkandawire8769 Күн бұрын
Bravo guys,,mumaitha
@BwanaGD
@BwanaGD 29 күн бұрын
Tisinthe flag yanthu ilindi mintundu yoyipa ntunduwake mmm ndiwachabe mutundu ya bendera yanthu imagwilitsidwa nthawizabili ndizinthu zakumidima panayenela kuyisintha bas
@Lee-lee-w1r
@Lee-lee-w1r 29 күн бұрын
Koma ndipo Simukunama. Taonani flag ya Kenya 🇰🇪 ndi ya malawi 🇲🇼 sizisiyana kwenikweni koma mmene zinthu zilili ku Kenya ndi kuno nzonvetsa chisoni
@blessingsfalamenga4575
@blessingsfalamenga4575 27 күн бұрын
Anyamata inu get ready in 2025 boma lina likubwerari tikonze malawi you are good indeed.
@HastingsJonathan
@HastingsJonathan 29 күн бұрын
Nelson Nelson 🤣🤣ukumaika ma flash et
@user-mh7cc8up4i
@user-mh7cc8up4i 29 күн бұрын
Apankunku ndi ndevi zamwayi mwayamba bho next time muzapose apa apa ndakayika kuti mudadya chikondamoyo we love you lots ❤
@GiftNyirenda-q9d
@GiftNyirenda-q9d 27 күн бұрын
Koma ma decision makers particularly politicians amamva zimenezi? Uthenga nde ndikwabwino and straight forward. Vuto aliyense angofuna iye ndi abale ake akamachoka, zawo zikhale ziyenda. ie alibe chikondi kwa a malawi koma kuzikonda
@PetersenjMwale
@PetersenjMwale Ай бұрын
U guys u talking the really truth
@lastonmasoatenganji-bs5gf
@lastonmasoatenganji-bs5gf 28 күн бұрын
Tikadali njira, sindazione munthu wa zaka 60 akukakamira kuyamwa bere la amache. Mkakawo udakoma chotani.
@OssmanAbubaker-l5s
@OssmanAbubaker-l5s 26 күн бұрын
Zoonadi my brothers osaopa osapepesa zaka 4 palibe chanzeru olo chimodzi chimene achita awa a Tonse
@user-to5of3ks3g
@user-to5of3ks3g 29 күн бұрын
Nice message
@user-sw6rz4tz3z
@user-sw6rz4tz3z 26 күн бұрын
Musogoleri akawoneka wa good future kumapha basi
@user-sw6rz4tz3z
@user-sw6rz4tz3z 26 күн бұрын
Suzumilani mu MRA muwone zomwe zikuchitika especially in a hot activities eg boarders kkkk
@louisgolden
@louisgolden Ай бұрын
Mwauzeso kuti akugulileni track trauser kuti yikhale top and down
@FosterMatchano
@FosterMatchano 29 күн бұрын
I like the conversation
@dumisanimoyo3152
@dumisanimoyo3152 29 күн бұрын
Amati mwanapiye anawonera make kunyera munyumba nde tiphe mayi wakeyooooo
@user-un8yq1gg2i
@user-un8yq1gg2i 29 күн бұрын
Hahahaha koma iyiyi nde ndiyong'alura kuyipatu kkkkkkk
@ChettoSongeah
@ChettoSongeah 27 күн бұрын
impressive guys Ndevu za mwai umaitha ndi nzako yo 🤞
@MemoryKamanga-jv4jh
@MemoryKamanga-jv4jh 29 күн бұрын
Number one brothers
@user-pv9uk6sc3w
@user-pv9uk6sc3w Ай бұрын
Yeah! This is hot for sure.
@clintonhodda9830
@clintonhodda9830 Ай бұрын
Koma a Brown mpinganjira mpaka liti osavomeleza kuti Mulungu sanafune kuti akhale president iiiii
@user-no5eb7rp1o
@user-no5eb7rp1o 29 күн бұрын
Eeeeee anyamata relo mwatokota kkkkkk muli bho kwambiri mwaveka ❤❤❤
@GraceZumazuma
@GraceZumazuma 29 күн бұрын
Keep it up times musalore akupatseni ma banz mudzitiimilira chonchi
@nellybruhan5834
@nellybruhan5834 Ай бұрын
Ine nde kumalawi kwandikwana😭😭😭😭😭😭 thupi lonse likumachita kuwawa ndikuganiza
@user-ec3xh4pc6t
@user-ec3xh4pc6t Ай бұрын
Dear bwelani mbalikuno bas
@nellybruhan5834
@nellybruhan5834 Ай бұрын
@@user-ec3xh4pc6t kutiko kumeneko saka bag yanga ndapakililatu
@kotking-xg7pp
@kotking-xg7pp Ай бұрын
MWALANKHULATU MWAMPHAMVU RELO NDIYAMIKE KWAMBIRI.
@SolokingChimzy-yt7dj
@SolokingChimzy-yt7dj 26 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂..ati sitidya kwaaaanu eishhhh anyamata anakalowa mu studio ndi mkwiyoo awa...Iman moona mtima ndimopanda mantha ngat Mikaya wa mu Bible yemwe anasutsana ndi mafumu ochuluka pozindikila kut zoyankhula zake ndizo zinali zoona
@sulleahmnyimbili1362
@sulleahmnyimbili1362 29 күн бұрын
Well spoken
@user-em3xq2th4g
@user-em3xq2th4g 21 күн бұрын
❤😂😢 nkhani yagona pa utsogoleli, kwa anthu amene ukuvoteledwao, tinawavotela pachifukwa chiani?😢 Kd tinawavotela chifukwa choti mwaiwo tikuonamo muzimu wa utsogoleli? Kapena chifukwa choti tikumadyanawo? Apa tiwonepo apa, kwa Ife ngati ovota. Kwa iwo amene akhalapo atsogoleli, ndi iwo amene ali atsogoleli, Asanapange chiganizo chofuna kukhala mtsogoleli anayamba azifufuza okha kuti mwaiwo yilimo mphatso ya utsogoleli kapena ayi? Akulu akulu tisaname apa onse amene tawavotela awa ndi amene tikuwavotela awa akungogweramo chifukwa chokakamizidwa ndi anthu ane amene ali atidyenawo, chifukwa cha mzimu uwu uwu, woti tikamuona munthu ndikumuwuza kuti km inuyo kuti mukhale mtsogoleli anthu akhoza kukuvotelani zaziiii, mawa olira ndifetomwe, muMalawi alimo anthu anzelu ophunzira aliso ndi utsogoleli mkatimwao km chifukwa choti ndi osauka palibe munthu amene angawa votele, pano ndi izi zaka 60+ chifukwa chokonda kusankha bakawalala aba tilindicha zero chosangalasa ndichani kumuvotela munthu maba akukufiya pahoroh 😂 kpn kukumanga ndikukakusekera inside kirikiri😮
@Erickasonya-uw8yw
@Erickasonya-uw8yw 27 күн бұрын
Bravo guys mumakwana
@dysonmasiye5736
@dysonmasiye5736 28 күн бұрын
Hahahaha akuti 👇 "Sitidya kwanu!" 😅😅😅😅
@EugeneChiyenda
@EugeneChiyenda Ай бұрын
Kma iyiyi mwang'alula🥳
@amosmuluwane4182
@amosmuluwane4182 27 күн бұрын
Lelotu anyamata mwawalankhulila amalawi pitilizani
@user-em3xq2th4g
@user-em3xq2th4g 21 күн бұрын
😢 Apa palibezoti bola baja bandani ni same thing those bantu
@user-ux8bc6wy1i
@user-ux8bc6wy1i 29 күн бұрын
Iyi ndye hot current yen yen 🔥🔥🔥
@sparkdymon3429
@sparkdymon3429 29 күн бұрын
Iyi koma mwang,alulandi makosana abwana kutundako azizifusa makamaka achekwela ndimbava ndifukwa akopa ACB
@yamiecharles
@yamiecharles Ай бұрын
Mmmmm tiyeni ticheze bwino
@xinalungu9616
@xinalungu9616 29 күн бұрын
Malawi has suffered leaders who kept us in the dark for years. Without water. Leaders that store n cut all rail lines to replace it with mangochi based vehicles. The nation suffered from leaders without teeth who paralized universities for almost a year. If asked, they would go on holiday in the USA. Now, are we promoting such leaders to come back? This is an opposition forum. Not a program that talks reality. None bias reporting is what this nation needs.
@sungirenikampu8630
@sungirenikampu8630 29 күн бұрын
Guys mumatha keep it up
@jelsonmlowoka8611
@jelsonmlowoka8611 Ай бұрын
Zoti inali times television yooneledwa ndi anthu ambiri pano ndi history chabe hahaha ndaonela ma viewers ndi kuchuluka kwa ndemanga
@EdwinMakwangwala
@EdwinMakwangwala 29 күн бұрын
Ambiri amaonela but they reserve their comments but ndawakonda ma guys
@user-zo3bf3ec3g
@user-zo3bf3ec3g 28 күн бұрын
Nde mwati amagwila pati anyamata aja
@ShagaFologonya
@ShagaFologonya 29 күн бұрын
Mmakwana uzo ndi mzao
@dysonmasiye5736
@dysonmasiye5736 28 күн бұрын
Za katangalezi tinaluza munthu wofunikira kwambiri amene anali ndi masomphenya pa nkhani iyi....SKC 😢 tidzamlila mpaka kale...koma adaferanji?
@ThomsonmbiziGwazafupa-rr6zg
@ThomsonmbiziGwazafupa-rr6zg Ай бұрын
Brilliant idea 💡
@augrinngunga8031
@augrinngunga8031 28 күн бұрын
Mwalakhulako zazerutu, mukamadya ma bazi guys times izakhala Ngati MBC yoonera achakwera okha
@shephardlonex3371
@shephardlonex3371 Ай бұрын
Koma zikhale ng'omayo nde ayi aaaaa
@khwimamtonga954
@khwimamtonga954 Ай бұрын
Mmmm Zikhale Ng'oma nawoso akufuna u Vice President ku MCP? Mmmm awa ai body structure
@eliffagondewe8214
@eliffagondewe8214 29 күн бұрын
Kkkkkkk 🔥🔥
@mustafahassan9128
@mustafahassan9128 27 күн бұрын
Koma ndiye mwanena mosanyengeleratu
@lucianogeoffrey4275
@lucianogeoffrey4275 Ай бұрын
Vuto lolandililatu zanu tinkhope tanuto nditamanyaziii😢
@christophermukaka7403
@christophermukaka7403 27 күн бұрын
To say the fact ma guys awawa amayankhula zoona koma kumtunda ku mmm
@PrinceBlessings-bv5bs
@PrinceBlessings-bv5bs 28 күн бұрын
😂😂😂😂😂 apa mwatha manthatu
@obviouskedson6483
@obviouskedson6483 Ай бұрын
Ife timamva nanu kukoma chifukwa mumayankhula chilungamo ,ndipo nthawi ya program yanuyo muionjezele mabwana
@StevenFombe
@StevenFombe Ай бұрын
If yuo steal with sorrounded one day all will 😂😂
@francismungu7749
@francismungu7749 28 күн бұрын
Guys mwasiya kugawa ma sweet ulemu wanu. Timayesa nanuso akudyesani chibansi
@gracemkandawire8769
@gracemkandawire8769 29 күн бұрын
Brian alikuti Kodi? Amabebetsa
@raytavares2256
@raytavares2256 Ай бұрын
That's why they assassinated malemu mnyamata woganiza boo Adamupha KS and they think we have mastered the crime and they will not be able to be caught and arrested.
@stevephiri1043
@stevephiri1043 28 күн бұрын
Mmoziyi ndamene amalakwisa program amakonda kuwatchinga azinzakewo kuti asamasuke
@user-im7sc2my4w
@user-im7sc2my4w Ай бұрын
Komadi ma junior police akuvutika ,srs
@DalitsoulNchengah
@DalitsoulNchengah 28 күн бұрын
Ulemu
@JuuuKomba
@JuuuKomba Ай бұрын
China chake kuseliku nkumati ndikupeleza 7 kwa ten mfiti 😢
@user-si7po9sd5i
@user-si7po9sd5i Ай бұрын
The curtain in the temple is about to be torn, we are waiting eagerly
@EdwinMakwangwala
@EdwinMakwangwala 29 күн бұрын
The problem of you and us as Malawians we always celebrate when someone fail, this is very bad and ugly kkkkkk
@user-si7po9sd5i
@user-si7po9sd5i 29 күн бұрын
Sometimes it's good to understand the message properly,who is celebrating here? If someone is failing to run the affairs of the country,how does that concern me?,he has 23 advisors,What is their job?what are all the advisors doing, this is high level filth,Justice hurts.
@Lee-lee-w1r
@Lee-lee-w1r 29 күн бұрын
@@user-si7po9sd5iexactly tell this person the truth
@Lee-lee-w1r
@Lee-lee-w1r 29 күн бұрын
@@EdwinMakwangwalait’s not celebrating them. It’s celebration that the truth about them will be coming out
@fatimautilah5648
@fatimautilah5648 29 күн бұрын
Ati sitidya kwanu kmatu Mr wonder
@eliffagondewe8214
@eliffagondewe8214 29 күн бұрын
Watopera akanganya amenewa.
@Benson-cf6qd
@Benson-cf6qd 29 күн бұрын
Aaah koma ma boys inuyo mumakwana 😅
@DalisoulThom
@DalisoulThom Ай бұрын
Chanzelu apha chilima+anthu 8 kumphatizapo kasambala
@StevenFombe
@StevenFombe Ай бұрын
Why big people wear tinted sun glasses
@Yamikaniwalasi
@Yamikaniwalasi 29 күн бұрын
😂😂😂😂
@user-zq3li3qw1m
@user-zq3li3qw1m Ай бұрын
Every day kusokesa uniform ya police zovuta zedi
@user-qe3iu7jy4h
@user-qe3iu7jy4h 29 күн бұрын
Ayi palibe chabwino kulibwino undindo asiyile wena
@jamusnamwino-br2iz
@jamusnamwino-br2iz 29 күн бұрын
anyamata musamale muphedwatu mcp sifuna anthu oyankhula chilungamo
@EllenChione
@EllenChione Ай бұрын
Ndakutayilani kamtengo guys
@dumisanimoyo3152
@dumisanimoyo3152 29 күн бұрын
Iyayi bomali linaziyipisila kale
@mathewsmakina7845
@mathewsmakina7845 29 күн бұрын
Mukamatero tililimodzi pamenepo
@BlessingsSeleman
@BlessingsSeleman 29 күн бұрын
Zofunika osambisala munda wa mtedza timadabwatu koma apa mwabwera
@RuthMkangala
@RuthMkangala Ай бұрын
Koma kumeneko
@McstanleyChalema
@McstanleyChalema Ай бұрын
Mtsogoleri yekhayo adali ndi kuthekera koteroko adali Akamuna a Bingu seconded by Akamuna Dr Saulosi
@RitaKainga
@RitaKainga Ай бұрын
Exactly!
@madsondzintchira9831
@madsondzintchira9831 26 күн бұрын
Abodza awa sanena zoona komaso oopa kwabasi bwanji analephela kutuuza zoona nthawi ya maliro anyamata wanthu skc timakubukila zbs isakudziwa ndalama pa imfa ya bingu atolankhani amakwela mu tengo kuti anene zoona Koma pano mmmmmmmmmma radio ake cabbage oneka oliba koma mkati madzi okhaokha
@RitaKainga
@RitaKainga Ай бұрын
Thanks you 2 guys there,Komano kod mmesa achakwera anatiuza Kut adzamanga aliyense ochita katangale m'boma lawo? Ndy chilowele amenebanamuona mkumanga ndi achilima okha? Plz plz t mkwabwino kusangalatsa Mulungu than munthu mzako
@user-ce8ud5ed5y
@user-ce8ud5ed5y 29 күн бұрын
Mumakwana gayez
@ChiccoDzikolo
@ChiccoDzikolo 29 күн бұрын
More fire gentlemen, Malawi wathu ndiyemweyu,Osaopa kuzilangiza nkhutukumve ndi mbala zimenezi
@user-wi8xw9qh7n
@user-wi8xw9qh7n 29 күн бұрын
Chakwera must go before September pls God is looking for us
@RemaniNkhoma
@RemaniNkhoma Ай бұрын
bora bingu ndi ng'ono wake pta osati uyuyu chakwerayu ndimbzi
@abunaseem6866
@abunaseem6866 28 күн бұрын
Ku painter eti?
@ChifundoNinje
@ChifundoNinje 29 күн бұрын
Chilungamo chimamasula, azibambo inuyo mulungu azikudalisani ndikutetezani mukugwila tchito, from cape town
@JimmyGenda
@JimmyGenda Ай бұрын
Hello Guys. Please continue hitting the nail on the head.
@INNOCENTMOFOLO-io8tg
@INNOCENTMOFOLO-io8tg Ай бұрын
😂😂😂😂😂😂😂😂 ndemvu zamwayi apolice akumadula zikhadabo atavala nsapato kkkkkkkkkk
@CalvinThomson-ys5zf
@CalvinThomson-ys5zf 29 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂 uyu ndiwamwano ati kuwenga zikhadabo autavala nsapato
@INNOCENTMOFOLO-io8tg
@INNOCENTMOFOLO-io8tg 29 күн бұрын
@@CalvinThomson-ys5zf kkkkkkkkk akutero kuli kutha kwa nsapato kkkk
@EnockBwaila
@EnockBwaila 29 күн бұрын
Apapa ndiye mwabwera madolo ulemu wanu that is democracy
@juliochiwalo
@juliochiwalo 29 күн бұрын
Pamene apolisi akusowa nsapato nawo ma pensioners sakulandira ndalama zawo ena mpaka zaka panopa katangale mbona wa chulukadi
@DavieKalonga-y5j
@DavieKalonga-y5j 29 күн бұрын
Pitilizani kumatiyakhulira chilungamo pa hot current
@PetersenjMwale
@PetersenjMwale Ай бұрын
Mumapanga ma demo abwino not like born kalindo, thanx TTV❤
@PetersenjMwale
@PetersenjMwale Ай бұрын
Mumapanga ma demo abwino not like born kalindo, thanx TTV
@PetersenjMwale
@PetersenjMwale Ай бұрын
U guys u talking the really truth
@user-dc7qq9yz3v
@user-dc7qq9yz3v Ай бұрын
Matha
@RuthMkangala
@RuthMkangala Ай бұрын
Koma kumeneko
@PetersenjMwale
@PetersenjMwale Ай бұрын
Mumapanga ma demo abwino not like born kalindo, thanx TTV
@GiftNyirenda-q9d
@GiftNyirenda-q9d 27 күн бұрын
Vuto lanu lopanga compare anthu awiri osiya, zolinga zosiya, koma kulephela kusiyanitsa.
MALAWI COURT.... TAMVANI IZI ABALE 🤔
20:45
Jimmy
Рет қаралды 42 М.
MCP AING'ALURA NDIPO SANACHIOPE KUTI NDI CHIPANI CHOLAMULA |
21:53
لااا! هذه البرتقالة مزعجة جدًا #قصير
00:15
One More Arabic
Рет қаралды 20 МЛН
Schoolboy - Часть 2
00:12
⚡️КАН АНДРЕЙ⚡️
Рет қаралды 6 МЛН
Smart Sigma Kid #funny #sigma #memes
00:26
CRAZY GREAPA
Рет қаралды 7 МЛН
EXCLUSIVE INTERVIEW WITH ULADI MUSSA
1:01:29
Zodiak Malawi
Рет қаралды 21 М.
Olo Anthu A Ku Kasiya MCP Sakuyifuna - Comrade Ntanyiwa
21:24
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 24 М.
How Did JZU Feel When Chakuamba was Made MCP President instead of Him
3:19
Joab Frank Chakhaza
Рет қаралды 25 М.
ILOCO DRAMA / DAGITI TUGOT ITI DANA TI BIAG #402
43:01
Ferdz Caballero
Рет қаралды 10 М.
JOHN KAPITO WATOPA NAYE CHAKWERA. Ityoke ityoke Osabisa mau // PART 1
33:23
Famous Historian EXPOSES ISR*EL’S FACTS! | Isr*el’s Future In The Quran!
30:55
لااا! هذه البرتقالة مزعجة جدًا #قصير
00:15
One More Arabic
Рет қаралды 20 МЛН