Massive analysis this is good idea and solution zoonad katangale akhoza kutha zkufunika azitsogoleri odana ndizopusa that's right guys.
@xinalungu961629 күн бұрын
For the first time Malawi can see great roads not just miyala ya madziko. I pray that Malawi wakes up. We should wake up n balance our forums
@IshumaelMbewe-d4t29 күн бұрын
Tidakhala ndi atsogoleri ophunzira angapo koma sitidatukike pa cbuma ndi zitukuko ndiye tidzayese mtsogoleri wa form 4
@ElizabethMajiga29 күн бұрын
Apa ponkhapa mwawalakhulila amalawi🎉🎉🎉🎉🎉🎉
@PetersenjMwaleАй бұрын
Mumapanga ma demo abwino not like born kalindo, thanx TTV
@gracemkandawire8769Күн бұрын
Bravo guys,,mumaitha
@BwanaGD29 күн бұрын
Tisinthe flag yanthu ilindi mintundu yoyipa ntunduwake mmm ndiwachabe mutundu ya bendera yanthu imagwilitsidwa nthawizabili ndizinthu zakumidima panayenela kuyisintha bas
@Lee-lee-w1r29 күн бұрын
Koma ndipo Simukunama. Taonani flag ya Kenya 🇰🇪 ndi ya malawi 🇲🇼 sizisiyana kwenikweni koma mmene zinthu zilili ku Kenya ndi kuno nzonvetsa chisoni
@blessingsfalamenga457527 күн бұрын
Anyamata inu get ready in 2025 boma lina likubwerari tikonze malawi you are good indeed.
@HastingsJonathan29 күн бұрын
Nelson Nelson 🤣🤣ukumaika ma flash et
@user-mh7cc8up4i29 күн бұрын
Apankunku ndi ndevi zamwayi mwayamba bho next time muzapose apa apa ndakayika kuti mudadya chikondamoyo we love you lots ❤
@GiftNyirenda-q9d27 күн бұрын
Koma ma decision makers particularly politicians amamva zimenezi? Uthenga nde ndikwabwino and straight forward. Vuto aliyense angofuna iye ndi abale ake akamachoka, zawo zikhale ziyenda. ie alibe chikondi kwa a malawi koma kuzikonda
@PetersenjMwaleАй бұрын
U guys u talking the really truth
@lastonmasoatenganji-bs5gf28 күн бұрын
Tikadali njira, sindazione munthu wa zaka 60 akukakamira kuyamwa bere la amache. Mkakawo udakoma chotani.
@OssmanAbubaker-l5s26 күн бұрын
Zoonadi my brothers osaopa osapepesa zaka 4 palibe chanzeru olo chimodzi chimene achita awa a Tonse
@user-to5of3ks3g29 күн бұрын
Nice message
@user-sw6rz4tz3z26 күн бұрын
Musogoleri akawoneka wa good future kumapha basi
@user-sw6rz4tz3z26 күн бұрын
Suzumilani mu MRA muwone zomwe zikuchitika especially in a hot activities eg boarders kkkk
@louisgoldenАй бұрын
Mwauzeso kuti akugulileni track trauser kuti yikhale top and down
@FosterMatchano29 күн бұрын
I like the conversation
@dumisanimoyo315229 күн бұрын
Amati mwanapiye anawonera make kunyera munyumba nde tiphe mayi wakeyooooo
@user-un8yq1gg2i29 күн бұрын
Hahahaha koma iyiyi nde ndiyong'alura kuyipatu kkkkkkk
@ChettoSongeah27 күн бұрын
impressive guys Ndevu za mwai umaitha ndi nzako yo 🤞
@MemoryKamanga-jv4jh29 күн бұрын
Number one brothers
@user-pv9uk6sc3wАй бұрын
Yeah! This is hot for sure.
@clintonhodda9830Ай бұрын
Koma a Brown mpinganjira mpaka liti osavomeleza kuti Mulungu sanafune kuti akhale president iiiii
Keep it up times musalore akupatseni ma banz mudzitiimilira chonchi
@nellybruhan5834Ай бұрын
Ine nde kumalawi kwandikwana😭😭😭😭😭😭 thupi lonse likumachita kuwawa ndikuganiza
@user-ec3xh4pc6tАй бұрын
Dear bwelani mbalikuno bas
@nellybruhan5834Ай бұрын
@@user-ec3xh4pc6t kutiko kumeneko saka bag yanga ndapakililatu
@kotking-xg7ppАй бұрын
MWALANKHULATU MWAMPHAMVU RELO NDIYAMIKE KWAMBIRI.
@SolokingChimzy-yt7dj26 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂..ati sitidya kwaaaanu eishhhh anyamata anakalowa mu studio ndi mkwiyoo awa...Iman moona mtima ndimopanda mantha ngat Mikaya wa mu Bible yemwe anasutsana ndi mafumu ochuluka pozindikila kut zoyankhula zake ndizo zinali zoona
@sulleahmnyimbili136229 күн бұрын
Well spoken
@user-em3xq2th4g21 күн бұрын
❤😂😢 nkhani yagona pa utsogoleli, kwa anthu amene ukuvoteledwao, tinawavotela pachifukwa chiani?😢 Kd tinawavotela chifukwa choti mwaiwo tikuonamo muzimu wa utsogoleli? Kapena chifukwa choti tikumadyanawo? Apa tiwonepo apa, kwa Ife ngati ovota. Kwa iwo amene akhalapo atsogoleli, ndi iwo amene ali atsogoleli, Asanapange chiganizo chofuna kukhala mtsogoleli anayamba azifufuza okha kuti mwaiwo yilimo mphatso ya utsogoleli kapena ayi? Akulu akulu tisaname apa onse amene tawavotela awa ndi amene tikuwavotela awa akungogweramo chifukwa chokakamizidwa ndi anthu ane amene ali atidyenawo, chifukwa cha mzimu uwu uwu, woti tikamuona munthu ndikumuwuza kuti km inuyo kuti mukhale mtsogoleli anthu akhoza kukuvotelani zaziiii, mawa olira ndifetomwe, muMalawi alimo anthu anzelu ophunzira aliso ndi utsogoleli mkatimwao km chifukwa choti ndi osauka palibe munthu amene angawa votele, pano ndi izi zaka 60+ chifukwa chokonda kusankha bakawalala aba tilindicha zero chosangalasa ndichani kumuvotela munthu maba akukufiya pahoroh 😂 kpn kukumanga ndikukakusekera inside kirikiri😮
😢 Apa palibezoti bola baja bandani ni same thing those bantu
@user-ux8bc6wy1i29 күн бұрын
Iyi ndye hot current yen yen 🔥🔥🔥
@sparkdymon342929 күн бұрын
Iyi koma mwang,alulandi makosana abwana kutundako azizifusa makamaka achekwela ndimbava ndifukwa akopa ACB
@yamiecharlesАй бұрын
Mmmmm tiyeni ticheze bwino
@xinalungu961629 күн бұрын
Malawi has suffered leaders who kept us in the dark for years. Without water. Leaders that store n cut all rail lines to replace it with mangochi based vehicles. The nation suffered from leaders without teeth who paralized universities for almost a year. If asked, they would go on holiday in the USA. Now, are we promoting such leaders to come back? This is an opposition forum. Not a program that talks reality. None bias reporting is what this nation needs.
@sungirenikampu863029 күн бұрын
Guys mumatha keep it up
@jelsonmlowoka8611Ай бұрын
Zoti inali times television yooneledwa ndi anthu ambiri pano ndi history chabe hahaha ndaonela ma viewers ndi kuchuluka kwa ndemanga
@EdwinMakwangwala29 күн бұрын
Ambiri amaonela but they reserve their comments but ndawakonda ma guys
@user-zo3bf3ec3g28 күн бұрын
Nde mwati amagwila pati anyamata aja
@ShagaFologonya29 күн бұрын
Mmakwana uzo ndi mzao
@dysonmasiye573628 күн бұрын
Za katangalezi tinaluza munthu wofunikira kwambiri amene anali ndi masomphenya pa nkhani iyi....SKC 😢 tidzamlila mpaka kale...koma adaferanji?
@ThomsonmbiziGwazafupa-rr6zgАй бұрын
Brilliant idea 💡
@augrinngunga803128 күн бұрын
Mwalakhulako zazerutu, mukamadya ma bazi guys times izakhala Ngati MBC yoonera achakwera okha
@shephardlonex3371Ай бұрын
Koma zikhale ng'omayo nde ayi aaaaa
@khwimamtonga954Ай бұрын
Mmmm Zikhale Ng'oma nawoso akufuna u Vice President ku MCP? Mmmm awa ai body structure
That's why they assassinated malemu mnyamata woganiza boo Adamupha KS and they think we have mastered the crime and they will not be able to be caught and arrested.
@stevephiri104328 күн бұрын
Mmoziyi ndamene amalakwisa program amakonda kuwatchinga azinzakewo kuti asamasuke
@user-im7sc2my4wАй бұрын
Komadi ma junior police akuvutika ,srs
@DalitsoulNchengah28 күн бұрын
Ulemu
@JuuuKombaАй бұрын
China chake kuseliku nkumati ndikupeleza 7 kwa ten mfiti 😢
@user-si7po9sd5iАй бұрын
The curtain in the temple is about to be torn, we are waiting eagerly
@EdwinMakwangwala29 күн бұрын
The problem of you and us as Malawians we always celebrate when someone fail, this is very bad and ugly kkkkkk
@user-si7po9sd5i29 күн бұрын
Sometimes it's good to understand the message properly,who is celebrating here? If someone is failing to run the affairs of the country,how does that concern me?,he has 23 advisors,What is their job?what are all the advisors doing, this is high level filth,Justice hurts.
@Lee-lee-w1r29 күн бұрын
@@user-si7po9sd5iexactly tell this person the truth
@Lee-lee-w1r29 күн бұрын
@@EdwinMakwangwalait’s not celebrating them. It’s celebration that the truth about them will be coming out