Big up mr ntanyiwa, ndipo pitilidzani kuigwira ntcito to.🤝🤝🤝🤝🤝🤝🇲🇼🇲🇼🇲🇼
@LYDIANYAKATUКүн бұрын
Ambuye azikutetezerani a ntanyiwa ,amene akulimbana ndi Inu akulimbana ndi Mulungu kumene amene akulimbana ndi a rwara akulimbana ndi Mulungu kumene anthu a Mcp opanda nzeru mmalo mopangira chitukuko ndarama akupangira kuti achotse mutiti ya anthu heeedee tawaonani eti anthu opanda manyazi ngati awo timakhnyadirani a ntanyiwa may God bless you all the time
@NastonVicktaКүн бұрын
Tili ngaaaaaa pa Limpopo fm, mpaka agaru oyamwitsa Inu mawere auma
@harrisbanda5891Күн бұрын
Mumakwana ma Freedom fighters athu athu akumalawi, timakukondani guys❤, MULUNGU azikutetezani ndikukupasani zosowa za pa umoyo wanu, inudi ndima HEROES adziko lamalawi ❤❤❤😢
@user-ul1fb4yn5oКүн бұрын
I love limpopo fm with Comrade ntanyiwa
@esaMoha-dm4kjКүн бұрын
Lipopo tiutseni soona shonde lipopo is my favorite shoiss ever from 6pm to 12am osawopha osavowonka ndive amalawi mtanyiwwa osawopha bakili muluzi TV osawopha mulungu adalise inuyyo nosse nkumene mulinko my must brress you orrowyess 💪💪💪💪👀
@jamesmulangalimatemba5351Күн бұрын
May God protect you my brother tikufuna anthu olimba mtima ngati inu
@BlessigsChabzolaКүн бұрын
Nanga Iwo a Mcp sakulira nawo nanga bwanji 21days isanathe Iwo akupanga program ya convention. Ndizona zimezi,
@meganabigail-ye7fwКүн бұрын
We Love you our junior pangolin no matter what they can't find you chifukwa inuyo Muli mumapapiko a mwini moyo wanu Chauta, Namalenga chisumphi. Ndeno angotaya nthawi azingodya basi
@Blessings-td4crКүн бұрын
Andale ndi athu oipa ndizoona ,,koma ndale za tonse alliance ulendo una akutionjeza,,,zinazi this current government akuyenera afufuze nkhope yamulungu,,,azidziwatu pena kuti izi ndizachabechabe Iwo eni adzafasotu!!!
@clairelewis5309Күн бұрын
Mwadzuka bwa Comrade Ntanyiwa from Nottingham.ndakunvani ,very clear
@harrisonkalimbakatha5339Күн бұрын
Comrade ntanyiwa umatiyimirira MCP ndi chipani chakupha ndipo sichizasintha mpaka kalekale ndipo atikwana anthu amenewa tikuona kuchedwa 2025
@user-ky4ce9gb6jКүн бұрын
Ndipo kwambiri tu mmm
@MadalitsoTamayenda-ez5pjКүн бұрын
Stay safe doctor ntayiwa ,, God protect yu whereever yu go kept up💯🔥💥
MCP yonse ikupenga pano ?? Keep Resting well Klaus Chilima
@user-dq9oe8sp8kКүн бұрын
Long live bwana Ntanyiwa
@MerryWaysonКүн бұрын
Mr Mtanyiwa End Mr Kalindo , mulungu sakutayani tikukuikizani m,mmanja mwa mulungu azikutetezani nthawi ndinthawi mukutiimilira ambuye akusungeni maka kukutetezani Kwa adani a MSP
@VirginiaPaulino-xc8phКүн бұрын
What either like or not ife nganganga pa Limpopo aziona agalu amenewa
@RuiJemusse-om7po20 сағат бұрын
Mulungu akhale Nanu amina Inu, wina asakutsekeni pakamaa, Mr Ntanyiwa and Mr Kalido go ahead
@mariamahamadu8402Күн бұрын
Nawoso amanganya ali kwangwalala njekate kuno olo ndimantha omwe alibe adzikale ng'oma mudzazafe mukale amuyaya ku MCP pamosi ndichimimba chanucho pamosi ndi chakwela chigawenga chakumpa chilombo chigawenga chakumpa
@mcsellahntv6896Күн бұрын
Mungoti pheeee muone !!!! 🎉🎉
@SymonZemben-gd3neКүн бұрын
Much love to you Limpopo FM with your team,Mr Born kalindo and Bakili TV we love you all keep it up leave long with 🐐🐐🐐
@user-ky4ce9gb6jКүн бұрын
Ndipo tikuziwa zinthu ndi BAKILI MULUZI TV bg up brothers
@frankdiyele7467Күн бұрын
Truth shall prevail we have suffered enough abale
@Sabina-hw4jsКүн бұрын
People are sleeping literally without food yet they can spend all this huge amounts of monies just to protect themselves.May God honestly judge them.God bless you in and may he always protect you
Zakhali n'goma panyopako wava ukuwasakilanji azako galu iwe osongomadya ndalamazo bwanji mimbayo ngati nyini yamako zakhali n'goma
@user-xk9vs9qc2sКүн бұрын
Fighting for the nation god never leave you like that freedom fighter mtanyiwa God protect you
@EdwardMathuwaКүн бұрын
Kodi a zikhale ng'ona mvuto lawo ndi chani?
@harrisbanda5891Күн бұрын
Mumuwuze Cilil Ramaphosa President wa South Africa kuti chakwela and his useless government ndi zigawenga
@LeonardMhone-cg1tkКүн бұрын
May God protect you 2 Bakili tv and MR Ntanyiwa 🙏🙏
@memoryedwin19 сағат бұрын
Mulungi azikudalitsani mr mtanyiwa
@user-xf8xb2iq9iКүн бұрын
Usi ndamuda bas tilire bwanji ifa ya chilima😢😢😢😢
@aligrayjeo1071Күн бұрын
Kodi nzotheka kuti tikhale ndi silent special forces Ku Malawi kuno tingopanga za MCP iyi basi chifukwa campaign nde sapangatu akapangila ground yake iti yoti akhale ndi chikhulupiliro kuti a Malawi akawamvetsera nyasi zawo mapeto Ake akachoka ataphwanyidwa ndi miyala ngati sakudziwa savage people
@TwalikiWisikiКүн бұрын
M'busa wa ntundu wanji opanda chifundo,opanda chisoni,, kukanika ku khululukila Chilima ngati adawalakwira
@jafalimussa5146Күн бұрын
Wawa ma boss muwuze avesese azazolowela
@shadreckphiri1799Күн бұрын
Malawi army and police will side with the civilians on 10th July. You will see.
@user-yc3ik9dq3xКүн бұрын
Hopefully 🤞
@patrickndojime1632Күн бұрын
Sizayiwalika ifa ya Chilima mpakana kale kale tizakhala tikukumbukira misozi yosantha
@leviouslongwe2950Күн бұрын
Angoni akulira zoona a Malawi, averwni zadutsa malire. Kunaphedwa ANTHU odziwika ndiponso amene amafunira Boma lathu zoyenerara. Kuphedwa Kwa: Mr.Albert Muwalo Mr. Focus Gwede Mr. Dick Matenje Mr. Sam Mpasu Mr..Saulosi Chilima ANTHU asanuwa anafa imfa zowawa a Malawi muli apa. Zowawa kwambiri.
@hudycorex1893Күн бұрын
More moto Ntanyiwa!!!
@Yungjoe786Күн бұрын
142 million for what?they're very stupidity instead of helping the needy with that cash.....mitu ngati zidebe
Iwe Zikhale ng'oma udzathera mmanja tsiku lina😂😂😂😂😅😅😅😅mimba yako
@harrisbanda5891Күн бұрын
Ndipo ndewalasa mtantiwa, fans yonse yokonda limpopo FM and bakili muluzi tv alongside Bon Kalindo, sitimagona and daily timakhala tikusakasaka ma audio anu and popanda kutulusa ma audio anu, amalawi sitimamva bwino mmitima mwathu . Tinasiya kumvera times , zodiac , mbc, mtv, luntha, nzeru, too many to mention
@StiveKantikiКүн бұрын
Timakunyadilani bigy🎉🎉 km ndipemphe Nyimbo mwaika kumapetoyi yemwe anaimba tikuifuna ikuti matembelelo agwele pamutu pako kkk
@sarahlukongolo4901Күн бұрын
Tinaona kale ife a usi kuti aliku mcp mmene amkayankhira pa Times nawo akolola akuona ngati chilima anali opusa eti
@AlexManuelMisomali-sv1vnКүн бұрын
Zoonadi penapake Chilima anali osamva komanso osakhwima pa ndale chifukwa Michael Usi ankaonekeratu kuti ndiwa MCP and why Chilima bravery told Usi kuti akufuna kuthetsa m'gwilidzano, that's why he's died
@AnaffSayamika-uh6vgКүн бұрын
Nkhan nd pa 10 July tikalile malilo achilima ku Lilongwe 🥺🥺
@chimwemwenkute3839Күн бұрын
May God bless and protect you wherever you are comred
@cynthiataulo5211Күн бұрын
Usi amaoneka maso mwa mwa mwa kuchenjelesa. Ka snake kenikeni. Blood in their hands, angobwelesa matemberero to their generations to come. Anawo zizukulu zawo mapemphero awo azakhala abomination before God. Peace will be their enemy.
@lottiempata2487Күн бұрын
Don't be afraid 😨 for anyone else
@ElasonAimonКүн бұрын
Mukuti imilira a Limpopo mulungu azikusamalirani nthawi zose
@dedzafranchiseКүн бұрын
much love to you comrade musadzamwalire
@Sammy-vb1edКүн бұрын
Mmmmm ay koma mcp yaonjeza nkhanza ndipo sitikuifuna.
@Jamesmwale-iz4riКүн бұрын
Ntanyiwa mukumatimvetsa kukoma za IFA chilima
@NgongireMwakasungulaКүн бұрын
Ine ntanyiwa tikungodikila 10 July kuti zalire bwino marilo achilima from kalonga
@user-wq9ex2sf3bКүн бұрын
God bless you
@user-do2cs8nf4bКүн бұрын
Mmmmmm koma ndalamazi zimenrzi zokumachokera kuti? Chifukwa nde zikumadabwitsatu
@ChimwemweKondowe-nj4lxКүн бұрын
Amenewo tikumana pa 10 pano
@ImanRashidi-so4ooКүн бұрын
Dziko lanthu la Malawi likamati lizilakhula chilungamo ngat Limpopo FM tikadalemela kwambiri koma eeeeeh
Nsiku lina mlungu azakwiya nanu ndipo muzayaluka masana sanaa
@NelliekaiyaКүн бұрын
Ingoing'alulani azidzakugwilani atayaluka kale
@Sabina-hw4jsКүн бұрын
God fights the battles
@INNOCENTMOFOLO-io8tgКүн бұрын
❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤ mtanyiwa iweyo usazafeyi😂😂😂😂 kusiteti hausiko wina akungonyeratu magazi uku 😂😂 mwazi wanthu amene aja ena akungosanza gamazi kkk
@TwalikiWisikiКүн бұрын
Mayi Yolamu Mulungu akudalitseni,akuyang'anileni,,akusunge moyo wanu,, chonnde chonde musavomele kuti a MCP akupakeni magazi a chilima chonde mayi, a MCP panopa ali so desperate thay can do anything as long as it can keep them from being exposed,, may yolamu a MCP akufuna opita naye,,akufuna akupakeni manyi,,,zikomo mayi inu ndi nakubaladi osati joyce Banda
@EllahEllah-hu7hiКүн бұрын
God have mercy
@SteveMamani-nv3mo19 сағат бұрын
Nice work brother
@Uncle_B265Күн бұрын
Ndalama mmalao mothandiza a malawi Ali buzy kupanga hayala kuti azipha anthu osalakwa why koma
@AlinafeChimoto-pp7wpКүн бұрын
Power message
@user-fi7ko7bl6fКүн бұрын
Morning Mr Ntanyiwa
@OweniMalokooweni-es9qxКүн бұрын
Kwacha bwenji if kuno ku khonjeni kwa bhobho 🎉🎉🎉🎉
@StanzioDymonКүн бұрын
Alekeni ana a agaluwa
@AbdulsartalSartalКүн бұрын
Khani imeneyo mumuuzenso Leyton mangochi chifukwa ndi kangaude amagothengeka ndindalama