Akuwapanga anthu khaza kuwangwaditsa pa Road block osawakwapula bwanji just Mlulanjeko tapitani pa Road blockhouse anthu akuwanzuzatu don't allow this.
@MuhammadBAKILI-kl2mj2 ай бұрын
Mbambande Limpopo fm best radio station
@GeorgePatels-go7wj2 ай бұрын
Very true but the opposition is too wick
@LastonMmanga-r2u2 ай бұрын
Chakwera ndi wakuba, kusawukitsa dziko kuti anthu a m'dziko akhale ngati opempha polandira zithandizo zake pomwe Ali wakuba, wakupha, Mizimu igone ku malawi congress pate and tiyeni tiwonelere chisangalaro cha satana kunamiza anthu ku Balaka pomwe akudyetsa Kasiya yokha, Shame to u Mr Lazaro😢
@RitaKainga2 ай бұрын
Endless salute kwanonse pa Limpopo
@FisherAction2 ай бұрын
It will happens bcz the wickness of opposition leaders bcz they just need to be leading the country why they keep quite like this
@AlexManuelMisomali-sv1vn2 ай бұрын
You deliberately forgot that you are the same people who remove DPP and UDF and you said APM failed to govern you and now you want APM and Atupele to do what ?
@EfeloYovita2 ай бұрын
kodi ndingaijoine bwanji Radio imeneyo
@EfeloYovita2 ай бұрын
tiuzeni zochita chonde ndijoine Radio station
@MohammedMajiga2 ай бұрын
Koma ine ndandadaula kwa athu akwathu kumangochi ayiwalandi
Tayu votani pai please choonde ndaphata manyalo ako pai javoten pakujabulusa nyantongiii nibulutu maningi
@JohnAsendi2 ай бұрын
Uthenga umenewo ndi oona koma osati muzinena kuti mupite kwaovota okha ayi upitenso Kwa atsogoleri omwe kupanga tizipani tating'onoting'ono chifukwa ameneyo ndi omwe angapangise kuti MCP ioloke apange n'gwilizano ndi zipani zazikulu monga momwe anapangira 2019. MCP inde imwaza ndipo idzativinya mpaka tidzabiba matumbo komanso MCP siliyo Abuchili Ali momwemo potengera zomwe anayankhula zulo tichenjele amalawi ndithu MCP khaya
@samanthamuller76432 ай бұрын
Koma akunama awa olo angawe chimanga chawocho anthu olo ali osamva koma apa amva kuti akubwera ndikunamaso komanso mr tanyiwa mumanena nthawi ndi nthawi
@wilfredkazembe6762 ай бұрын
Big mmalawi sazatheka sitichedwa kuyiwala ife wolo muthayakhula motani koma mukutimasula ndi kutiwonetsa koma chimanga chimenecho chikangopelekedwa ayamba yemweyo
@OweniMolokooweni2 ай бұрын
Ndipo kwambili Malawi ndi mbunzi
@PatrickMailos2 ай бұрын
Allah yaalam 😢
@SimonBanda-b1f2 ай бұрын
Azapanga KU Lilongwe konko zimenezo
@JohnAsendi2 ай бұрын
Chimanga chibwere bola chikhale Kenya guys voti ndi muntima
@ronaldordinga65372 ай бұрын
Inu manyaka osewa ndi opposition party palibe yemwe akuwoneka pa ground pano opposition yose ya makape sakusiyanaso ndi MCP amandinyasa a opposition nawo
@petertaulo80142 ай бұрын
Zoona Don't Trust 😅
@IbrahimWezely-qd4vj2 ай бұрын
Aaaas propaganda iyi ya dpp . Mcp ili busy kumanga malawi osati zopusa zaumbuli ukukambazi
@jameskachulu81412 ай бұрын
Koma chakwela ngati amavela ladio iyi eeeeeee
@VeronicaChirwa-ct4os2 ай бұрын
Ine ndikuganiza kuti samamvera
@MiddayDeleza2 ай бұрын
Nde chimanga cho adzagawe mpakana liti, nthawi yonseyi anali kuti anthu akhala akufa ndi njala chimanga mutachibisa
Iweeee panyopako sopano watikwan nda akazi ako omwe ndi ana ako omwe
@EstherBonga2 ай бұрын
😂😂😂😂Iwenso watikwana ndi chikangawa wakoyo watuma ndani unvele pachiphisi pako ifeyo we love them anayankhula ndi ife ndipo sanatikwane
@petertaulo80142 ай бұрын
Iwe ndiye ukutukwana ndani?
@daltonjafali38562 ай бұрын
Ndiwe savage kwambiri kutukwanako wapindula chiyani
@MaritaBanda-p4z2 ай бұрын
𝕜𝕠𝕞𝕒 𝕟𝕕𝕚𝕪 𝕫𝕚𝕞𝕒𝕜𝕦𝕨𝕒𝕨𝕒
@GeorgePatels-go7wj2 ай бұрын
Very true but the opposition is too wick
@AlexManuelMisomali-sv1vn2 ай бұрын
Just you go and be the opposition so that things will be working according to how you like because you're the same people who voted for Chakwera and now what you want opposition to do for you ??