AMAYI OMWE ANALI CLOSE FRIEND WA CHILIMA ALIMBA MTIMA NDIPO ABWERA POYERA NDIKUMUSAMBWANZA CHAKWERA

  Рет қаралды 107,655

Makosana

Makosana

Күн бұрын

Пікірлер: 253
@LindaMalunjika
@LindaMalunjika 4 ай бұрын
U are right zimene wanena.....anakakhala kuti ndi iweoyo chimwendo unali mu ✈️ ndi anthu ena Chilima anakakhala okathandiza anakakhala SKC.....why coz anali ndi umunthu....ndeeee who did ever did tha to Chilima ili ndi dziko ndipo limatembenuka
@HalimaMussa-j6t
@HalimaMussa-j6t 2 ай бұрын
Mulungu sachedwa azawaika poyela dziko lizadziwa
@jameslifah7909
@jameslifah7909 4 ай бұрын
Strong woman ever,you stand by the truth. Let love lead❤
@MascotAnderson
@MascotAnderson 4 ай бұрын
Mulungu abwerese chilungamo pankhaniyi ndipo yehova musalore kt oipayo awine nkhondoyi
@BrightonNdalama-x2b
@BrightonNdalama-x2b 4 ай бұрын
Well spoken mama and we understand every single point of ur message and keep it up you're opening our brains
@Yungjoe786
@Yungjoe786 4 ай бұрын
I salute you aunt The TRUTH eish
@LukasBamus
@LukasBamus 4 ай бұрын
Always on my mind uncle God bless you wisely and continue to reviled more sicrets in this world
@WelemuSayizi
@WelemuSayizi 4 ай бұрын
Koma azimayi ngati amenewa ndi mwana wathu koma Malawi ndi yodala mayi uyu ngakhale azibambo 10 muli mu mcp simungafanane naye iron lady more fire!!!
@ROSELIKHWAKHWA-y7e
@ROSELIKHWAKHWA-y7e 4 ай бұрын
More 🔥❤
@SadrackTseka
@SadrackTseka 22 күн бұрын
Abusa okhumudwitsa okhumudwitsa dziko lonse lapansi ndiye ndi achakwera dyera khwidzi kuzikonda Dumbo zadzadza mwaiwowa kd ndikufuna udindo kokhakokhako mpaka pa menepo speech on mama God protect you
@AllanTamula
@AllanTamula 4 ай бұрын
Your comments towards Malawi politics is just great.
@LezinaBanda
@LezinaBanda 2 ай бұрын
Ulemu wanu mama,,, zimayi olimba mtima ngati inu nsinamuone
@HevenChiwaya
@HevenChiwaya 4 ай бұрын
Auzeni mai akuona ngati a Malawi ndi mbuli sitimaziwa kanthu never
@MercyChimaliro-fi6mv
@MercyChimaliro-fi6mv 4 ай бұрын
Well spoken Aunt ❤️ 💗
@ThomasBlessings-j8k
@ThomasBlessings-j8k 4 ай бұрын
Ineyo kwanga nkupempha amalawi ozindikila Kuti 2025 chikangawa asazakhale m'boma chifukwa kukhala NDI asogoleli ofanana ndi uyu ndekuti tonse tizaphedwa
@EllenKUMWENDA-b2z
@EllenKUMWENDA-b2z 4 ай бұрын
I kove the spirit u hv mamie.Malawi shld hv more ladies like u....💪💪💪
@ReyonAndrewBanda
@ReyonAndrewBanda 3 ай бұрын
She is not in malawi remember.
@howellbandah8211
@howellbandah8211 4 ай бұрын
Be protected ur a blessing mama not just to the Malawian but to whole world ❤
@JosephGama-v7r
@JosephGama-v7r 4 ай бұрын
Mama you are a true freedom fighter
@SpencerKadewere-cd5ok
@SpencerKadewere-cd5ok 3 ай бұрын
You deserve respect mumm continue fighting for the truth until these crocodiles🐊🐊🐊 repent there seens
@DuncanRashid
@DuncanRashid 4 ай бұрын
I respect you mom good words
@PatriciaTikhiwa
@PatriciaTikhiwa 4 ай бұрын
Ndipo zoona chilima eishiiii ngt zabodza ndege hooooo zosaveseseka😊
@0wenNkhambule
@0wenNkhambule 4 ай бұрын
Good message Mayi Chimwendo ndiwakupha ndi Chakwela
@BrightKuyaka
@BrightKuyaka 3 ай бұрын
Chemwali ndinkanyalanyaza zainu koma ndayamba kukumvetsani, more fire big woman
@alexjeremanuel2541
@alexjeremanuel2541 3 ай бұрын
Another example is Kondwani Nankumwa who was expelled from DPP but alive but MCP will never leave you alive
@JaneMhango-zl6pt
@JaneMhango-zl6pt 3 ай бұрын
Achakwera akudziwapo kanthu pa imfa ya a Biyeni. Mulungu alowelerepo ndithu. Komanso chilungamo chidzawonekele ndithiludi.
@Peter-yz8tm
@Peter-yz8tm 4 ай бұрын
Good lecture. Ine mkazi wanga anamwalira ku queens because anamicheka matumbo pomipanga operation. Bingu saulos pamodzi ndi mkazi wanga akukambirana konko. Kuwani mmene mungathere za olemera izi. Mkazi wanga anakambako palibe....
@LekelenSuwale
@LekelenSuwale 3 ай бұрын
Well spoken Mom, you deserve respect and I admire you more than ever teach us Mom
@PatumaCassimu
@PatumaCassimu 4 ай бұрын
Perfect said👍🔥🔥
@RoseChimbwefu
@RoseChimbwefu 4 ай бұрын
Well done mayi awuze chilungamo awa ave
@GerladMakayika-on5rt
@GerladMakayika-on5rt 4 ай бұрын
Just point of collection, that was not an accident it was planned for him to go sothat they'll rule again
@alexanderduncan9000
@alexanderduncan9000 3 ай бұрын
Reality talk
@LuwizaChika
@LuwizaChika 2 ай бұрын
Ndipo khaniyo ndiyona mamie sukunama ambuye akupasen moyo wautali mwayakhula chilungamo
@MussaChilembwe
@MussaChilembwe 4 ай бұрын
Chimwendo banda chakwera kunkuyu namajekete wankulu wa army manganya athu amenewa ndi amene anapha athu onse 9 aja koma thawi yawo yatha sopano mcp yamagazi crocodile 🐊
@BerthaMATUMBO
@BerthaMATUMBO 25 күн бұрын
Good speech mama may God be with you
@Sabina-hw4js
@Sabina-hw4js 4 ай бұрын
Oh yes a woman of truth
@Homeofpeace321
@Homeofpeace321 4 ай бұрын
Ku MCP amaphana polimbilana udindo. Chakwela anamupha chilima chifukwa amapingidwa kuti aimenso 2025
@MosesKamtndo
@MosesKamtndo 4 ай бұрын
People like this woman must be abandant, keep it up mama
@giftkanjuchi-qm8hf
@giftkanjuchi-qm8hf 4 ай бұрын
It is making sense mama ndinu di achipatala
@FelistasNkasalaMakumbo
@FelistasNkasalaMakumbo 4 ай бұрын
Love you mama mumatiyimirira❤❤❤❤❤
@atupelemposa4786
@atupelemposa4786 4 ай бұрын
Sanamukondepo chilima ,they just use him to remove DPP, Munthu woti ukumukonda or atadwala umathamangila nayo ku chipatala .
@GlynLumbe
@GlynLumbe 3 ай бұрын
Muti ineyo Ku Namwera Ndiye kwathu kumudzi kumachemba MOTi timatsikila galimoto pa chesailesi kumapita ku machemba tiyakhulileni Kwa Anthu wathu osowa chikondi wa kuno
@ErnestChansa
@ErnestChansa 4 ай бұрын
Point point anamumpha chakwela ndi fit anthuwa a MCP
@yassinn5634
@yassinn5634 3 ай бұрын
Point of Correction Sisy Mtambo sanachite kuchoka yekha mboma anachita kumuchotsa.
@Sabina-hw4js
@Sabina-hw4js 4 ай бұрын
Wise woman.
@CHAPITASINGINI
@CHAPITASINGINI 4 ай бұрын
Mwayakhula ndikwanga komwe cct eeeeh moyo kuwawa kwambiri
@geeman-p9d
@geeman-p9d 3 ай бұрын
Abiti mukunena zoona tonse tikudziwa zoti Saulos anaphedwa. Anali ndi ntchito yabwino osati ku chipiku. Tikulirabe ndipo tidzalira mpaka kalekale. Anali wa ndale nde tikukambanso za ndale apapa. Mwayankhula bwino abiti zikomo
@UfuluManondo
@UfuluManondo 4 ай бұрын
I silute you dear mommy mwaima pachilungamo,ambuye abise Moyo wanu pomwe a mcp isauone❤
@AginesWailes
@AginesWailes 4 ай бұрын
Ndipo pakhare misaaa yot ikachitikire pachikangawa pompooo
@pacharokoloviko1694
@pacharokoloviko1694 4 ай бұрын
Big up mama, please tayakhuleni madam Mary ngati nkotheka achitsogolere chipan i
@EliasManthenga
@EliasManthenga 4 ай бұрын
Mummy mukazafika ku South Africa zandizwsen tizadye kota limozi, kuima pa chilungamo amalawi aziwe ❤
@MchachaGoodson
@MchachaGoodson 4 ай бұрын
Keep doing good work yourselfless be blessed.
@ThomasNChinseu
@ThomasNChinseu 4 ай бұрын
Nice touching to u nurse in USA keep it up
@IvanRoux-vl8gu
@IvanRoux-vl8gu 3 ай бұрын
That's true negligence
@danielswaleyi9776
@danielswaleyi9776 3 ай бұрын
Well articulated, I have learned slot from you sis.
@Halima-i4x
@Halima-i4x 4 ай бұрын
MCP ndichiman chakupha chifukwa chilowelen MCP boma onan Malawi anthu mene akumwalilila eeeee chakwela akuononga dziko labwino bwino ndi 2 😢😢😢 koma one day is one day
@MaxwellMbesa
@MaxwellMbesa 13 күн бұрын
GOD Bless you
@amoschataika7440
@amoschataika7440 4 ай бұрын
Bravo Chemwali
@ChimwemweMuhelliwah
@ChimwemweMuhelliwah 4 ай бұрын
Anthuwa kupemphera kwawo mkwabodza...minbulu pakati pankhosa...olo nkhope zawo zimawoeka kt ndi anthu oipa ..fiti zopemphera...
@FRANKBEULA
@FRANKBEULA 4 ай бұрын
Mai iweo usazamfe umakwana ndipo ukunena zooona
@DamianoNombo
@DamianoNombo 4 ай бұрын
The only truth
@ChimwemweJoelKajawo
@ChimwemweJoelKajawo 3 ай бұрын
🤣🤣🤣🤣 Koma ndi osekesa kwambiri apa Pali cha nzeru chilichonse chomwe munthuyu wayankhula, even izizi sizikupeleka evidence or proof yoti munthu anaphedwa kapena Kuti inali movie
@YammsyZebron
@YammsyZebron 4 ай бұрын
Ndipo onse anapanga izi apenge
@AdizzMadizo
@AdizzMadizo 4 ай бұрын
MCP ndi anthu akupha zigawenga zakupha palibe kuchosera ayi
@FebbieNjewa-g3k
@FebbieNjewa-g3k 4 ай бұрын
Sure sure Abiti tell them ,,God bless yu more
@MussaChilembwe
@MussaChilembwe 4 ай бұрын
Komaso anachita kuphedwa athu onse aja ndege sinagwe ayi koma anachita kuphedwa basi straight point basi chakwera anachita kukonza kuti afe athu onse aja anapha basi chakwerayo
@RobertLuka-wy9cl
@RobertLuka-wy9cl 4 ай бұрын
Auzeni mayi achimwendo ndi chitsilu chopusa
@jameswajumpha6790
@jameswajumpha6790 4 ай бұрын
Dan Lu naye imukhuze nkhani iyi kulondola kosekose athu osakhazikika😂😂😂😂
@MukileNkhana
@MukileNkhana 24 күн бұрын
God should assist and respond us in this 2025
@ThomasBlessings-j8k
@ThomasBlessings-j8k 4 ай бұрын
Mayi munthu uyu siwopemphela anachita bwino kusiya ubusa Koma akanabwelapoyela nkumapanga nyanga uyu khulukunyinda zomvesa chisoni kwambiri munthu opanda manyazi uyu
@EmmanuelDanitsa
@EmmanuelDanitsa 4 ай бұрын
Great message Moom..
@GiftJulius-y6f
@GiftJulius-y6f 24 күн бұрын
I rember 2012 mwana wanga anali Al ndi 1year.anasowa koma mizionse unatuluka kufunafuna mwana ena kumalowela kupolisi ena kwa chairman.ena kulengeza ma video show mpaka mwana anapezeka ndiye vp akalekeze kufufuza Ati ayi kwada nyelo zamawo
@RidgieGondwe
@RidgieGondwe 2 ай бұрын
Well done mamie
@AlihIbrahim-s7v
@AlihIbrahim-s7v 4 ай бұрын
Athileni fire,,,,,,,,zitsilu za mcp plan yawo sanayitenge bwino amawona ngati nthawi ya kamuzu ino,,,,,this is new generation yopita ku school,,,,komaso Dr Muluzi anatimenyela nkhondo yolankhula pazomwe zikuchitika,,,,,,,,,,,,
@LawrenceBelson
@LawrenceBelson 4 ай бұрын
Amayi mulungu azikudalisani
@brendachirwa-u2q
@brendachirwa-u2q 3 ай бұрын
Zoona kwambr BN anali wochita zimthu moganizira anthu. Thanks
@HajiAslam-nd9xq
@HajiAslam-nd9xq 4 ай бұрын
Big up Mai mukhalise inuyo 💯💯💯💯
@MikeMtunduwatha
@MikeMtunduwatha 3 ай бұрын
Zoonazake zimenetikudziwa
@montfortwoka2896
@montfortwoka2896 4 ай бұрын
Ndipo osamaika mau akuti mwina akanakhala ali moyo akanapita mwachangu ayi answer ndiyakuti anachita kupha awa anthu oipa kwambili tichotsa oipa onse next year ino . SKC anali president wanga.
@solomonkasiya6904
@solomonkasiya6904 4 ай бұрын
Lankhulan Mai mumatiimilira❤
@ErnestChansa
@ErnestChansa 4 ай бұрын
Achemwa chakwela ndimbuli yamunthu nazikhale ng.oma saziwa kathu chomwe akuziwa kuba ndalama za malawi basi chizikhale ng.oma mutu ngati konyelela kwa vuwu
@CarolynBandA-bb6cn
@CarolynBandA-bb6cn 4 ай бұрын
True❤
@juliochiwalo
@juliochiwalo 4 ай бұрын
Mulungu alipo amaziwa ndi kuona chilichonse zoona ziziwika posachedwapa
@Halima-i4x
@Halima-i4x 4 ай бұрын
Zoona mama osaposa 🙏🙏🙏💪💪💪
@YusufGafa-s3j
@YusufGafa-s3j 2 ай бұрын
Black box inasowa bwanji mundenge ngati inali ngozi chabe eeeee koma a MCP inu mmmmm only God knows
@RachealHarawa-xc9gs
@RachealHarawa-xc9gs 4 ай бұрын
Ndipo Mulungu awakanthe anthu oipa awa kumupha mnzao ngati nkhuku chonchija mmmmmmm anthu oipa
@MiddayDeleza
@MiddayDeleza 4 ай бұрын
Yes timukamba kumene anafa imfa yowawa SKC ndi ena wonse aja ulemu wanu mama
@IvanRoux-vl8gu
@IvanRoux-vl8gu 4 ай бұрын
Thats true Mam
@JonathanMtambo-w6e
@JonathanMtambo-w6e 4 ай бұрын
Nkhani ya chilima sii, zatha pokapoka chilungamo chitabwera poyera
@AnniePetro
@AnniePetro 4 ай бұрын
Chilungamo mama
@KhumboNyerenda
@KhumboNyerenda 3 ай бұрын
Good message mum
@wonganimwase9881
@wonganimwase9881 3 ай бұрын
Even if a child is late coming from school, the parents don't wait for an hour to atart searching,, talk less of saying that the search will resume the next day. Every flight has a manifest and a whole pesident couldn't didnt have the correct list of passengers on the plane.
@NickUpoche
@NickUpoche 4 ай бұрын
Keep it up mm,proud of u
@dewasicmalunga3374
@dewasicmalunga3374 4 ай бұрын
I salute you kusyeto wakumangwetu
@PercyRoos
@PercyRoos 3 ай бұрын
That is true mamma
@QueenMoses-c1n
@QueenMoses-c1n 4 ай бұрын
Big up mama u really encourage us
@gladysmanthimba7851
@gladysmanthimba7851 4 ай бұрын
Abiti ndinu fire. Mau opanda chigamba. Zikomo kwambiri tili nanu limodzi
@DanielGeorge-l4h
@DanielGeorge-l4h 4 ай бұрын
May Allah bless you mom eish
@evangelistjacobmithi5061
@evangelistjacobmithi5061 3 ай бұрын
Ndinenese pano kuti aliyense okupha or opanga tchimo ngati sanalape sazapeza MTENDERE pokhapokha alapa.
@mabvutomichaelpanagona1949
@mabvutomichaelpanagona1949 3 ай бұрын
MCP inapitirira mfiti kuipa kwake mayi,
@EssauChimpango
@EssauChimpango 2 ай бұрын
Truth being told
@HendrixBrave
@HendrixBrave 3 ай бұрын
Eeeeeeeeeeeeh Koma yaaaaa ine ndili pheeeeee ena kuseliku akungosegura mmimba
@TITANIMATOLA
@TITANIMATOLA 3 ай бұрын
True mama osaopa osafooka
@ÑaloWemba
@ÑaloWemba 2 ай бұрын
Wow 😮 chilungamo ichi
@HolmanDazah
@HolmanDazah 4 ай бұрын
Anyani a MCP a mfiti, sanankonde spirit yao ndiyakupha basi ndipo ife a Ntcheu zikutiwawatu, DPP inamusula Bhiyeni mundale ndipo, you didn't know kuti end of the day 2025, chilima internally amaganiza alliance ndi DPP.
@gearardphiri6904
@gearardphiri6904 4 ай бұрын
Thanks my sister
Une nouvelle voiture pour Noël 🥹
00:28
Nicocapone
Рет қаралды 9 МЛН
Richard Mphopheya - Chi Wrong Turn (Official Video)
7:35
Nyimbo Zachimalawi
Рет қаралды 44 М.
TONDE WADULA DRAMA SERIES EPISODE 121
29:14
Nkhalango Multimedia
Рет қаралды 82 М.
Surviving the wind storm  at Mt.Saramati highest peak in Nagaland.
21:09
The Roving Naga
Рет қаралды 4,1 М.
Padziko LAPANSI PALIBE CHISISI. ZAWULULIKA ZA NGOZI. NTANYIWA
31:26
FRANCIS MTAWAYA TV
Рет қаралды 65 М.
Une nouvelle voiture pour Noël 🥹
00:28
Nicocapone
Рет қаралды 9 МЛН