NAMIWA WAULURA ZINSISI ZODABWISA ZOMWE ANTHU SAMADZIWA ZA KAFUKUFUKU WA IMFA YA CHILIMA PA INTERVIEW

  Рет қаралды 160,246

Makosana

Makosana

Күн бұрын

Пікірлер: 702
@AdamBwanali-kr5fw
@AdamBwanali-kr5fw 3 ай бұрын
Namiwa ....you are so brave ...zikuonetseratu kuti chakwera anamupha Chilima .....uyuyu wachita bwino kuchokamo akanaphedwa
@hamiltonsolomon3756
@hamiltonsolomon3756 3 ай бұрын
Mbambande,namateture weni weni.....Kulankhula kokhakokha..kwa chilungamo...Bravo Comrade Namiwa❤❤❤❤❤❤
@UncleShopRite
@UncleShopRite 3 ай бұрын
Anakubelekayo sanaluze I never see I faithful and trusted person like you
@chrisboyce2
@chrisboyce2 3 ай бұрын
Uyuyu akufunika award (2024 the best political activist Ndi Comrade NAMIWA 💪🔥) 2024 the best Tv ndi Bakili Muluzi Tv 🔥 Kalindo ndiye pangolin wathu 💪
@RiteRoderick
@RiteRoderick 3 ай бұрын
Ndipo zoonad zed brother
@Belinda-c6e
@Belinda-c6e 3 ай бұрын
Ndipo bro sukunamai ma guyz awawa amatiimilira
@patrickmacheso5062
@patrickmacheso5062 3 ай бұрын
Really agree with you my brother.
@HajraTar
@HajraTar 3 ай бұрын
Ndipo tikanakhala ndi anthu okwana ngat 10 okhala ngt uyu malawi sakanafika apa ayi I really like his speach ,mulungu amuteteze ndithu
@PraiseShongwe
@PraiseShongwe 3 ай бұрын
Please Brian Banda pezani nthawi mukamupangeso interview Namiwa the most powerful and brilliant guy in this country. God protect these men Namiwa and Brian from devils.
@patrickmacheso5062
@patrickmacheso5062 3 ай бұрын
I really agree with you my brother
@MkuwaCharles
@MkuwaCharles 3 ай бұрын
Namiwa ndli pa mbuyo pako
@montfortGhobede
@montfortGhobede 3 ай бұрын
Surely Mr Namiwa needs a lot of support from all of us Malawians.
@johngrem2838
@johngrem2838 3 ай бұрын
A Man of great knowledge and ideas, Namiwa knows what he is saying and he is a true son of Malawi osati zinazi, this guys Namiwa deserve a great respect and security chifukwa Chakwera ndi Crook akhodza kumupangila chiwembu munthu oyipa ameneuja anapha Chilima ndi anthu ena 8. Pa Chakuti pake Chakwera and Big Up! Mr Namiwa ndipo Osatopa, Osafooka komanso osaopa❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
@McshonWilliam
@McshonWilliam 3 ай бұрын
Mr namiwa anakubelekani wo sanaluze ai ndipo komwe aliko alandile maulemu and isaid may god continued kuwapasa zosowa zawo 🙏🙏🙏🙏
@TendaiGwiriza
@TendaiGwiriza 3 ай бұрын
A Namiwa mumakwana heavy
@DicksonLingsonmulauzi
@DicksonLingsonmulauzi 3 ай бұрын
Ndipo pakanapezeka anthu oterewa malawi muno okwana 10 dzikoli bwnzi lili lolemera kwambiri
@FrancoKaunga-rq2ki
@FrancoKaunga-rq2ki 3 ай бұрын
Bravo Mr namiwa you are a man of integrity indeed God almighty keep blessing you.
@BonifaceBanda-s5l
@BonifaceBanda-s5l 3 ай бұрын
Ndip inu
@InnocentHassan-m3r
@InnocentHassan-m3r 3 ай бұрын
May ALLAH protect you Mr Namiwa you're true fighter
@JamesALLi-m8i
@JamesALLi-m8i 3 ай бұрын
More fire 👦 🔥 mr Namiwa 🔥 we trust you 🙏 💯 God bless you and give you more years 🙏 ❤️ 🙌 💙 powerful message 😀 tipangadi mademo anyoooo
@Cammie921
@Cammie921 3 ай бұрын
Thank you Mr Namiwa for standing up and being HONEST, You are BRAVE Man 🙏🏽🙏🏽🙏🏽🙏🏽
@imraanJafal
@imraanJafal 3 ай бұрын
Mr inutu ndi boooon kalindo ntchito yanu imanditsangalatsa kwambili simuopa simutopa❤
@DickieDulamanja
@DickieDulamanja 3 ай бұрын
Big up Mr Namiwa, dzikoli likufunika people like you
@WisikiBlack-gj4gu
@WisikiBlack-gj4gu 3 ай бұрын
Ndakumvetsela Mr namiwa ndiwe big man more fire 🔥 ipulumutse malawi 🇲🇼 malawi 🇲🇼 akufuna athu onena chilungamo ndimopanda matha ndimomasula more fire 🔥
@mohamedriazshreef8697
@mohamedriazshreef8697 3 ай бұрын
Mai amene anabeleka namiwa my god bless them always
@pastorjamesseyama3147
@pastorjamesseyama3147 3 ай бұрын
Keep up the good work sir Mr Namiwa and whole CDEDI team. God bless you for representing Malawians 🎉🎉❤
@MiddayDeleza
@MiddayDeleza 3 ай бұрын
Well done, your a great man indeed, I silute you, God bless and protect you wherever you shall go in Jesus name ❤
@montfortGhobede
@montfortGhobede 3 ай бұрын
I didn't know that Mr Namiwa is like this. Very brave! Malawi needs many Namiwas for it to transform. May the good Lord bless Mr Namiwa.
@cynthiakananji1608
@cynthiakananji1608 3 ай бұрын
May the good Lord continue to give you strength 💪 eeee your the best fighter,ndiwe mamuna olimba mtima.mai ako anakubeleka ndipo she is blessed 💞
@NelsonNyirenda-m5q
@NelsonNyirenda-m5q 2 ай бұрын
Namiwa you are doing a great job please we are behind and praying for you God bless 🙏
@mohamedriazshreef8697
@mohamedriazshreef8697 3 ай бұрын
Malawi akukufunika akunikafa ngati inuyo mr namiwa my god bless you All the time ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
@thatgirrroskrr3570
@thatgirrroskrr3570 3 ай бұрын
Mtolakhaniyi nde ayi. Namiwa akumane ndi Byani Banda interview izakoma
@MaggieBanda-ft5tu
@MaggieBanda-ft5tu 3 ай бұрын
Tolakhani wachinyengo eeee shame
@OmarManjawira-up3ns
@OmarManjawira-up3ns 3 ай бұрын
Following dude ,,,, very soft and clear ❤
@DarlingtonChaura
@DarlingtonChaura 3 ай бұрын
Mtolankhani yu alibe mfundo, Namiwa is on the right track.
@Russell-sq9rm
@Russell-sq9rm 3 ай бұрын
Mtolankhaniyu nd kape Ali nd mafunso ofoila ngat mwana
@umalibudala9121
@umalibudala9121 3 ай бұрын
Ndichitsiru mtolankhani uyu. Ndikanamutukwana koma ndimapemphera
@GeoffreyKaluwa-em7eb
@GeoffreyKaluwa-em7eb 3 ай бұрын
This a man of confidence! Mr Namiwa we need more of you.
@EmmanuelNgambi-y6h
@EmmanuelNgambi-y6h 3 ай бұрын
Umakwana Namiwa,,,,may God bless and protect you
@ManfredNakhuba
@ManfredNakhuba 3 ай бұрын
Mtolankhani uyu akhalangat wasyetsedwa banzi akufunsa zoti wafotojoza kale aaaaa
@chikondisatchipa7676
@chikondisatchipa7676 3 ай бұрын
Ndiposo ndiwobhowa bwanj
@bennihope3272
@bennihope3272 3 ай бұрын
A very patriotic gentleman. The country needs immensely. Take your fight to a bigger level. In short just 2 Biyeni. I rest my case
@patrickmacheso5062
@patrickmacheso5062 3 ай бұрын
Exactly
@PaulMapala
@PaulMapala 3 ай бұрын
May the almighty God protect you mr namiwa the true reflection of trustworthy,passionate and freedom fighter 🔥🔥🔥 with God's hand we wu sing a victory song
@graciouskamwendo1873
@graciouskamwendo1873 3 ай бұрын
Mtola nkhani uyuyu ntchito yake ikuoneka ngati amangofuna kupeza vuto mwa a Namiwa. Sakuoneka ngati akupanga zosaka chilungamo ayi
@bobkatas1974
@bobkatas1974 3 ай бұрын
Exactly my point,,,,,akukhala ngati sintola nkhani,,, chifuwa zoti commission of inquiry imeneyi anthu anaikaikilla ndi zoona and iyeyu ngati ntola nkhani anamva zimenezo
@SheenahMwalabu-iz3pr
@SheenahMwalabu-iz3pr 3 ай бұрын
Pajatu zodiac ikuyendetsedwa ndi mcp gospel kazako. pano radio station yanzeru ndi times television and radio and mibawa TV ilikonse bhoo
@MoosaSame
@MoosaSame 3 ай бұрын
Congrats mr Namiwa atolakhaniwa ndi ogudwa onse musalimbane nawo
@YaseenJohn-l5y
@YaseenJohn-l5y 3 ай бұрын
I like the way u have spoken for us. Namiwa brave mn
@SamKaposa-i5c
@SamKaposa-i5c 3 ай бұрын
And me too
@ThomuChiwanga
@ThomuChiwanga 3 ай бұрын
Mr your number one In my country thanks mr namiwa keep up malawi
@JoelTchuma-g3s
@JoelTchuma-g3s 3 ай бұрын
Mr S.Namiwa you are a man of Kafanikhale,Smartmatic must go out of MEC,please!
@DONNEXKhama-bk1gy
@DONNEXKhama-bk1gy 3 ай бұрын
God bless you Mulungu akupase Moyo wautali
@ElizaOsman-y5r
@ElizaOsman-y5r 3 ай бұрын
Munadalitsidwa mwene and i support you i ll always support you ndinu munthu wanzelu mumaziwa kuongala ndinu munthu ofunikila mdziko muno ndili pambuyo panu and i ll always be there for you ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤ well said and i love it i support it i appreciate it thanks
@believersanddeciplesofjesu8602
@believersanddeciplesofjesu8602 3 ай бұрын
Tolakhani uyundi chisiru kwambiri koyamba kuona tolakhani opanda zeru osaziwa tchito ngati uyu buluzi weniweni
@graciouskamwendo1873
@graciouskamwendo1873 3 ай бұрын
Ntchito amatha koma vuto watumidwa
@Russell-sq9rm
@Russell-sq9rm 3 ай бұрын
Ineso ndkudabwatu kd anapitadi kusulu uyu😢
@Russell-sq9rm
@Russell-sq9rm 3 ай бұрын
Sukulu
@lucksonmoonga4426
@lucksonmoonga4426 3 ай бұрын
Keep it up sir.may God continue protect u and bless u.
@CollinsChimsendenji
@CollinsChimsendenji 3 ай бұрын
Host akanakhala Joab Frank Chakhadza
@InnohPhili
@InnohPhili 2 ай бұрын
❤mumayitha brother mulungu akudaliseni
@DeliphDevi
@DeliphDevi 3 ай бұрын
Tola khaniyi ndopusa kwambili alibeso nzelu akufusa mafuso ngati sanapite ku school
@KondwaniBMnyontho
@KondwaniBMnyontho 3 ай бұрын
Zoona ndikape kwambili
@AlexGomani-ss5nj
@AlexGomani-ss5nj 3 ай бұрын
The great man of our country, continue fighting for the truth
@GraceShaibu-i9d
@GraceShaibu-i9d 3 ай бұрын
god bless you namiwa ndiwe muthu wachilungamo kwambili ambuye akudalitse manja mwanu mulibe mwaziiii
@lorainemponela
@lorainemponela 2 ай бұрын
✊🏿✊🏿✊🏿As a far left activist I agree with Namiwa. He didn't go there to be a tick box. ✊🏿✊🏿✊🏿
@MagretNsopera
@MagretNsopera 3 ай бұрын
God bless Mr namiwa mukutiimilila
@frankwilliam9844
@frankwilliam9844 3 ай бұрын
Mr namiwa is so genius and brave,big hand to him!!!!
@Mobilot2android
@Mobilot2android 3 ай бұрын
Mr Namiwa ambuye azikudalisani u r more than the millions people and it's our prayer for you long live🎉
@YamikaniWitness-vw3jl
@YamikaniWitness-vw3jl 3 ай бұрын
Namiwa ndakamuna mmmm! Iwe umabwera ndithu. Big up bro.
@JimmyMaster-l1x
@JimmyMaster-l1x 3 ай бұрын
Mr Namiwa your a the greatifull Man kuyionera patali Game ndinali ndinkhawa nditambva kt mwapita nokha koma pokumbva kuti mwatuluka moyo wanga uli osangalala kooopya 🎉🎉🎉🎉🎉
@MakesoMjuma
@MakesoMjuma 3 ай бұрын
Anamiwa amai anu anamvadi kuwawa chifukwa chainu mulungu anamiwa adzadalitsa Mai anu bambo anu chifukwa anabala mwana muombori WA dziko la pansi❤❤❤
@RodneyTomato
@RodneyTomato 3 ай бұрын
We need people like anamiwa in malawi 🇲🇼
@RiteRoderick
@RiteRoderick 3 ай бұрын
Koma uyuyu mmmm ndimupasa sister wanga sure ❤❤❤❤❤ Namiwa katundu guys owopsa
@abangaabanga4677
@abangaabanga4677 3 ай бұрын
Bwana Namiwa I applaud u sir, u do stand for the people and what u r saying is fact, keep it up sir, Malawi will rise again.....!
@FishaniNgulube
@FishaniNgulube 2 ай бұрын
It's a Shame that we still let these politicians play with our sanity, this guy is wise and strong, opanda dyera. May God protect u Mr namiwa
@Edwardchimenya
@Edwardchimenya 3 ай бұрын
This guy's so brave,respect💯
@MoosaMwanyali
@MoosaMwanyali 3 ай бұрын
Wachilungamo samafa agogo anga anandiuza kale more fire 🔥 brother
@JosephIsaac-s1c
@JosephIsaac-s1c 3 ай бұрын
Comrade Namiwa inu mulungu adzikudalitsani you are special ❤❤❤❤❤❤
@AustinNangwale
@AustinNangwale 3 ай бұрын
Bravo boss kuwala ndi M'dima siziyendela limozi
@ChimwemweZuze
@ChimwemweZuze 3 ай бұрын
May the almighty Lord Jesus Christ keep you safe legend ( Maso a Malawi alunjika painu bwana 💪💪💪💪🙏🙏🙏🙏🙏)
@TalazanGamah
@TalazanGamah 3 ай бұрын
We need people like u namiwa. If u was A president tikanati we have power Mn l very interested on u.
@KalongaWhy
@KalongaWhy 3 ай бұрын
Namiwa Amakwana ❤❤❤ I love your voice
@FREZERMICHAELBANDA
@FREZERMICHAELBANDA 3 ай бұрын
Namiwa, kamangila, BM TV, mnyanyiwa, times hot current etc excellent 👍👍
@patrickmacheso5062
@patrickmacheso5062 3 ай бұрын
Mtanyiwa and not forget Bon Kalindo the DC.
@katalamajames4947
@katalamajames4947 3 ай бұрын
Well done mr namiwa ur very interesting to malawian people we need people like you,,,
@AishaJafali-h3b
@AishaJafali-h3b 3 ай бұрын
bwana namiwa bwanji mutakhala pamozi achina bon kalindo mtanyiwa mthambo mumatikwanila ❤❤❤❤❤❤❤❤
@BenjaminMtima
@BenjaminMtima 3 ай бұрын
Zodiak uyo sintola nkhani sadziwa ntchito ngobowa
@PamderaInvestment
@PamderaInvestment 3 ай бұрын
Keep fire burning Mr Namiwa,,,inu nd machine🔥👌👌
@kakachimtengo7340
@kakachimtengo7340 3 ай бұрын
Wow what a guy ❤we love you sir
@Sally-n3t
@Sally-n3t 2 ай бұрын
God bless you sir ,umuthu wavuta ku malawi athu akusowekera umuthu ngati wanuwo sir
@mikebernabechimundi3472
@mikebernabechimundi3472 3 ай бұрын
Salute Namiwa, you are a commission of enquiry at your own
@cynthiakananji1608
@cynthiakananji1608 3 ай бұрын
Eeee Koma Namiwa ndiwanzeru ndipo ndimutu,EEE anabadwa munthu uyu,anthu akaikila kale ndipo takaikila,chimene munthu uyuyu wagunitsitsa nkuchotsa kuyeletsa dzina lake,munthu uyuyu amaimiladi anthu,and akanangokhalapo uyuyu ma millions akanadana naye he is very clever,he is 💯 perfect munzeru.
@JohnFrank-cg1yh
@JohnFrank-cg1yh 3 ай бұрын
Yes am agreed with namiwa, president ananena kut dege inafika ku mzuzu, kumkuyu ananena kut black box ilipo ndipo yasungidwa Malo abwino, chimwendo Banda anati adauzidwa kut dege idazaza,so palibe zomaononga ndrama kungowakoka akuluakuluwa kupita nawo ku court akazengedwe milandu
@stevendemanje
@stevendemanje 3 ай бұрын
Yehovah akutetezeni kwa mikango ya mcp mr namiwa
@BrotherLester
@BrotherLester 2 ай бұрын
This is very sensible he force the president to set the commission of inquiry and he would not be surprised to seat for the meeting but to follow after finalize
@JasonMailos
@JasonMailos 3 ай бұрын
Namiwa number one, Koma MCP isaonengati ikuchenjela
@AlexNjovu-j4z
@AlexNjovu-j4z 3 ай бұрын
Ifetikuwavesa anamiwa🙏🙏
@KondwaniLingisoni
@KondwaniLingisoni 3 ай бұрын
Uyu ndie munthu anamiwa
@bridgetmajor3646
@bridgetmajor3646 3 ай бұрын
Heavy
@vitumbikomunthali8185
@vitumbikomunthali8185 3 ай бұрын
Namiwa for presidency. I would vote for this guy if he could be one of the contenders.
@andrewnkhoma3566
@andrewnkhoma3566 3 ай бұрын
Namiwa he is wonderful man and he is real man of god!!!!!
@hopesonmathafu2346
@hopesonmathafu2346 2 ай бұрын
Truth Carrie's waight and heavy to handle.... The truth is a sin not a liar' in this world....
@dysonmasiye5736
@dysonmasiye5736 3 ай бұрын
Brovo to Mr. Namiwa....mwapangazo nzofunikira kwambiri...izi za majority rule izi nzopoila kwambiri. I remember nnakhalapo elder wa mpingo wina ndipo anakhadzikitsa lamulo loti zomwe mwakambirana ku council ko ngati sukugwirizana nazo koma anthu onse agwirizana nazo iweyo ulibe say and umakhala m'kati mwa zomwe enawo agwirizana zomwe nzopoila kwambiri. Now mwapanga bwino kutuluka and chomvetsa chisoni ndi chakuti kuli amipingo kumeneko koma mwatiuza kuti anali mbali inayo 🤔🤔🤔 chipulumutso ndithu ngati sitisamala
@kadijachilwan967
@kadijachilwan967 3 ай бұрын
I was misunderstood Namiwa ndimamuongati ndiwa dpp bt the way he spoke here ndayamba kumukonda ndi real freedom fighter
@FebbieNjewa-g3k
@FebbieNjewa-g3k 3 ай бұрын
God bless yu more sir,,God has a final say
@HannifordWitness
@HannifordWitness 3 ай бұрын
This is one of the reason zodiak inatsika value atolankhani anzeru ngochepa better times
@rangersonngirazi6741
@rangersonngirazi6741 3 ай бұрын
Satha ntchito uyu, Namiwa amafunikira Chakhaza or achina Brian Banda
@patrickmacheso5062
@patrickmacheso5062 3 ай бұрын
Eya Zodiac ndiya MCP paja mwini wake ndi Gospel Kazako emwe anali spokesperson wa MCP Government and President.
@mohamedriazshreef8697
@mohamedriazshreef8697 3 ай бұрын
God bless you mr namiwa my god be with you always
@HassanChibwana-m8j
@HassanChibwana-m8j 3 ай бұрын
We love you Sir Keep it up.we trust you
@PeterGrant-ih1sr
@PeterGrant-ih1sr 3 ай бұрын
Nzimu wamuthu ndi nkhan zina chaka Chino ziliko
@MavutomandaMandamavuto
@MavutomandaMandamavuto 2 ай бұрын
Mr namiwa big up don,t big up we trust coded 🎉🎉🎉🎉
@ChristinaStambuli-q3e
@ChristinaStambuli-q3e 3 ай бұрын
Commission of inquiry izakhalapo 2025 just after a new elected president ..Mcp ndi Caikwera waoyo ali pa bench anzao akuvinamo ngat momwe akuvinra Chikangawa ndi kunkuyu,Chimwendo Banda..,iyiyi com of inquiry ndiya mcp anthu aja akochedwa kale palibepo phindu amalawi sitipezamo mayankho.Rip Skc and all the victims
@wisdombwanali7956
@wisdombwanali7956 3 ай бұрын
We are for this movement Mr Namiwa
@PraiseShongwe
@PraiseShongwe 3 ай бұрын
Silvester Namiwa you are really different character. I wish you were Malawi's president. Hopefully god will touch your mind to one day contest for presidency and Malawi will vote for you so that you are given room to change Malawi for the best.
@InnocentMtafya
@InnocentMtafya 3 ай бұрын
Hopefully your are ................
@MisheckChinjala
@MisheckChinjala 2 ай бұрын
Mulungu Ali payinu Mr Namiwa,ndipo musaseweletse Mzimu Wa Mulungu ulipayi please please please 🙏 in Jesus name
@JonesBenNgaiyaye
@JonesBenNgaiyaye 3 ай бұрын
Mmmmmmmm Namiwa bravo bravo,lets join hands and support each other for the truth to prevail and make Malawi should be freed from all these nonsense leadership
@ALICESHEKI
@ALICESHEKI 15 күн бұрын
Namiwa you are right ndipo iweyo Moyo Wautali chifukwa Mantha amaononga zithu
@JudithMaida-ug4oi
@JudithMaida-ug4oi 3 ай бұрын
Big up Mr Namiwa amfumu aku tcheu wo aza seva ndende ya chikumbu mtima afta mzimu wa chilima ukuwasautsa
@HamiltonwaNamuwah
@HamiltonwaNamuwah 3 ай бұрын
Keep it up Mr. Namiwa. Kupanda kuwuwawuwa andalewa ndioyipa kwambiri
@indiAisha-q2o
@indiAisha-q2o 3 ай бұрын
❤❤❤❤ndizoonadi namiwa ndinu wachilungamo❤❤❤❤❤mulunguakudaliseni zikomo
@CharityshantieMwenda
@CharityshantieMwenda 3 ай бұрын
Ine dzulo sinagone, kuwamvetselela bwino bwino bwana namiwa,,,,,, GOD bless you
@MosesDicostar
@MosesDicostar 3 ай бұрын
Namiwa bravo man
@RichardNkumbira
@RichardNkumbira 3 ай бұрын
May God bless you Mr Namiwa
@WITTNESSMBOBADINHONJOLOM-bv4un
@WITTNESSMBOBADINHONJOLOM-bv4un 3 ай бұрын
Dziko likufunika anthu ngt awa mr NAMIWA VS BON KALINDO tikusowekera anthu onga awa osati mbava zili ku mcp en chikangawa
@BrightNthendelo
@BrightNthendelo Ай бұрын
Big leader chakwera anapha chilima ndipo nayo timupha ndi vote
@DominicNantowa-t4d
@DominicNantowa-t4d 3 ай бұрын
Kodi mbuzi ya ntolakhani ameneyi ndiye iti? Sakumunvesa pati Namiwayi?
@PeaceNkhoma
@PeaceNkhoma 3 ай бұрын
Eee 😂 anthu mulindiukali😂😂
@DominicNantowa-t4d
@DominicNantowa-t4d 3 ай бұрын
@PeaceNkhoma aa man akundipetekesa ntima ngati akundifunsa ine bwanji.
@PeaceNkhoma
@PeaceNkhoma 3 ай бұрын
@DominicNantowa-t4d Ndamumvano apa kut zikumuvutadi kumvesera....
@DominicNantowa-t4d
@DominicNantowa-t4d 3 ай бұрын
@PeaceNkhoma nanga man Anamiwa ayakhula monveka bwino kuti anakumana ndi kunkuyu amafuna amupase chibanzi Namiwayi anachikana. Zachiziwikile anthuwa akufuna zikhale zonama be bas.
Beat Ronaldo, Win $1,000,000
22:45
MrBeast
Рет қаралды 158 МЛН
人是不能做到吗?#火影忍者 #家人  #佐助
00:20
火影忍者一家
Рет қаралды 20 МЛН
A Simbi Phiri Akhuza Imfa ya Dr. Saulos Klaus Chilima
22:44
Zodiak Malawi
Рет қаралды 87 М.
GOtv Malawi Izeki ndi Jakobo Kukhala Awiri Simantha
19:56
Queen Melz
Рет қаралды 1,5 МЛН
Prophet Uyu Walosera Zoopsa Pa Zisankho Zikubwerazi ... Tanvani
27:34
Padziko LAPANSI PALIBE CHISISI. ZAWULULIKA ZA NGOZI. NTANYIWA
31:26
FRANCIS MTAWAYA TV
Рет қаралды 64 М.
CRUISE 5 WITH ENIFA CHIWAYA   ANANYONI 27 MARCH 2022
1:13:40
Joab Frank Chakhaza
Рет қаралды 150 М.