Bola Inu amzathu kukumangani potuluka ndiye kuti zanu zalowa
@alexandermeke69942 сағат бұрын
Anthu opanda nzeru ngati inu munthu ngati waganizilidwa kuti walakwa aamamangidwa then court limanena kuti munthuyi ndiwolakwa kapena ayi koma basi poti muli kunja kwa boma ndiye mutase kulankhula zazii zopanda umboni omwe ngati mukufuna mpando wa u president awuzeni anthu zomwe mudzachite ngati boma mukutsutsana nalolo silikupanga koma basi polankhula bweeee ndi zamkhutu zomwe,fundo mulibe koma malilo a chilima ikhala fundo mayi uyu anyanya kulalata plus bodza eeeee zachuluka mbuli ku malawi zophunzila ina ndi kaliyati zaziiii popeza ndi mkazi ndiye samangidwa kagwereni oko musatinyase apa bola vice president 😂😂😂
@CholohLungu43 минут бұрын
Zapantumbo zomwe ukuyakhulazi anakudyesa chibanzi eti