Chimwendo wamanyi sadickmia Ali Kuti munamupanga chipongwe asenanu amanyinso
@isaackinod12563 сағат бұрын
A Malawi don't make mistake kuvotelanso anthu awa!
@GiftKumbwezaСағат бұрын
Komanso osadzavoteranso DPP
@JacklineNiwahereza-ni3pm2 сағат бұрын
Achimwendo mukufuna mutchuke koma chilungamo mukuchiziwa kuti boma lanu lalephela
@JonesChingaya-yf4gg4 сағат бұрын
What a stupid government is this??? Chimwendo kodi Muthalika kuima nawo pa u president 2025 walakwa??? Always kumunyoza, koma sumachita manyazi kumatukwana munthu yemwe samakuyankha???
@GiftChilanga-u3c2 сағат бұрын
ine busy kuwerenga ma sms komaso ndiri kuseriku kuonera Bakili muluzi tv history is a best teacher mwamusakasaka mwalephera panopa mkuyamba kumuwawaza msekula naye mmimba kkkkk
@dalisoulphiri30942 сағат бұрын
Awa anakakhala anzeru sibwenziso akumatchula za infa ya Chilima 😢
@ellenMakoloma2 сағат бұрын
Akufuna kuima u president ndi DPP yokha? Mukuwaopa inu hiyaaa
@FelixMapemba3 сағат бұрын
Achimwendo osamatha mau You never know what comes tomorrow Samalani ndi mulomo wanu
@BlestoneJonas3 сағат бұрын
Chimwendo udzakhumudwa kwambiri ukumunamiza chikangawa wakoyo iwe galu kwabasi
@JonesChingaya-yf4gg3 сағат бұрын
MCP muzimuthokoza late SKC, without him ife sitikanakuvoterani.
@ThandiShandu-l6w3 сағат бұрын
Zachamba mesa naye amalandila zaboma as wachiwiri or iye akanawina yekha bring another point not that nonsense check 2025 another way of kicking DPP will be there
Chipan cha anthu opanda mfundo ndondomeko zawo zopoira
@NtchindiChirwa-l8o3 сағат бұрын
Kkkkkk 😂 chimwendo usasiye kumunyoza muthalika ndi chinsiru kwabasi
@JamesBrown-gx8my3 сағат бұрын
Thanks Tatchena ma T_shirt a MCP lero...APM My vote
@RosinaPatel2 сағат бұрын
Kkkkkkk...adyeleni
@RebeccaChikalenda2 сағат бұрын
Khani kumangonyoza Peter basi kusowa fundo galu lwe apm my vote❤❤
@DalitsoMatope3 сағат бұрын
Akufunika kuzamugenda miyala pa stage kuti asiye zopusa,,,,iwe Chimwendo uzafela kundende watch out
@EdahAlick-gq2qx3 сағат бұрын
Zomwe ukuyakhula chimwendo ndizamisala ndiwe garu kwabasi
@GabrielThomas-ij1fo33 минут бұрын
Koma anthu tupembedza madano a Malawi let's work hard nd pray hard KUT Mulungu azitipatsa zosowa zathu otherwise a ndale amangofuna kutipeperetsa!
@Jacksonmuhackeya2 сағат бұрын
Ulibe nzeru bambo. Iwe asilamuo siomweo mwapangila upo kuti aziphedwa ndi chikangawa opanda nzeru ukakhala pa nsonkhano usamachulepo galu iwe
@DalitsoPhiri-sq5nl2 сағат бұрын
A Banda ma press briefing simunayankhetu pano koma mzayankha chaka chamawa malume cz kukana kufufuza imfa ya chilima it shows munachita kumupha so amalawi Ali maso ndipo akudzimvera okha zoti inuyo mlibe nadzo ntchito
@RafickAlissah2 сағат бұрын
Awa zomwe anamuphera chilima ndi chani kdi😢😢😢
@MacleansKatungwe4 сағат бұрын
😂😂😂😂😂, Mfundoless, Ndalama zaphwekadi eti? Anthu akufa ndi njala, inu muli busy kugawa Ndalama from our own misonkho. Time will tell tell soon
Achitsilu inu Chibvumbulutso 3 vs 17 bible lake ndi la Mulungu kapena la Satana?😢😢
@GiftMeatine3 сағат бұрын
Kandalama muperekako tapita naoni ku machinga anthu akudya chitedze mwatani achimwendo banda mtima wanji uwu opanda chison a Richard eeeee koma tkapuma kumwambaaa eeeee ai
@AndrewAsanChipangaya2 сағат бұрын
kma apo ndizonad mulungu anangomutenga chakwera ndi chimwendoyi kma nanga achimwendo aba ndalama za mbili za boma kma tamuoneni sakuoneka ngati ali ndi ndalama kukhwima ngati maungu ana amenewa kmaso utsazinamize ife sitingavotele agalu awa ayi
Please tanenani fundo zoti anthu azakuvotereniso not kunyoza Peter, nsonkhano uliwonse tisamangonva za Dpp and Peter, uwuzeni anthu muzawapangira chani popeza 4 years zakukanikani what is your dream for next term mbuzi inu
@FaysonChimbalanga2 сағат бұрын
Kkkkk makadeti mukufuna kutiuza kuti chomwe mumadziwa mkutukwana basi nde mwagwa nayo, yotukwanayo sikuthandizani mwina kapena mchilakhulo chanu (sanje basi ndinu buzi zamano kusi
@hassanfaizadaffer242146 минут бұрын
Kaya chinapangisa ndichani osakwera dege ija eshhhh bola ukanafa iweyo
Ndalama musiranfira kom wo sa votera chakwera akumvunika UDF and dpp utm aford
@MbeedaJames3 сағат бұрын
I hate this chimwendo alot than chakwera himself chimutu kukula🙄
@MisheckAselo3 сағат бұрын
Chimwendo ndale za chimidzi zonyozanazi talekani
@ChingaChibambaСағат бұрын
Koma tiva ziti lelo kuyankhula zina mawa kuyankhara zina eich koma ziko lathu zochitika kuchuluka
@swadikimbwana76803 сағат бұрын
Pls don't use money distribution as campaign
@GoodsonLevison-r1r41 минут бұрын
Ukulimbana ndi dpp iwe chimwendo uzafa ndi mwala umox kut thiiii
@LastonChamila3 сағат бұрын
Zose tisiye mmanja mwamulungu a M CP muziwe kut de sky is limit mukamaika achipan ku MEC transparency and acounterbility tiwona bwanji koma muziwe kut msembe iliyose ilindimalile mulungu akuona
Kodi ndalamazo akugawira ndani ,mesa ndi a Malawi.Ganizani guys polankhula
@Lushaka2 сағат бұрын
Guys Malawi people we lost way this is not politics bt talking shirt without plans just think 🤔 what kind of this people always busy about Peter Peter problem our people who like to follow every way why Malawi people u don't teach how to respect one another every day Peter just build our country we tried kind of this things amalawi we must wake up this people taking advantage with our youth why Guys check South Africa youth or Kenya youth never allow kind of this readers no respect nothing we can see ourself 😢
@TedzaniIVPowerStation2 сағат бұрын
😂😂😂😂nde za maudindo ansenawo chikuwakhudza mchan?😂
Iwe njanji unyadila ya ku Mozambique pajaso umanyadila magreda a ku India chimanga chikunena iwecho ndalama wagulila iwe chimangacho wazitenga kwa amako
@JoãoChirwa-n3l17 минут бұрын
Mcp likuopa dpp bas mbona khumbai ali busy ndi dpp pakunya pamako ndithu
@MaxonKambazitheСағат бұрын
Chipani chokupha nizomwe amaziwa
@MfipaKapweraСағат бұрын
Kukula mutu koma fundo mulibe.
@RosinaPatel2 сағат бұрын
Usalimbane ndi Sameer suleman..
@simonpaul65673 сағат бұрын
Chitsilu owe zomwe ukudziwa ndizimenozo just answer the question who told you that plan is full?
@BrianMuleke3 сағат бұрын
Ma president onsewa kma peter bas kkkkk kupanda mfundo