Anybody joining UTM should go to the branch and area and constituency. Nobody should enter at Central executive level. Ngati uli umphawi ndi wanu. UTM youth should not accept corruption, mediocrity and rubbish.. The UTM youth should protect the party for greedy leaders.
@Georgechimfuti2 ай бұрын
Amalawi tidatani Kabambe wakhalapo Reserve Bank Governor osathandiza zeruzo zaoneka Lero Amalawi ndi otemberedwa Kaliyati yemweyu wanyoza akulu enandiena lero akuchuluka zeru. U T M Ndiya olemekezeka a vice president a Dr Usi komanso olemekezeka Akambala omwe mophatikizana ndi okondedwa athu Dr SKC mzimuwawo uuse muntendere ana panga United Transformation Movement (UTM ) asakunamizeni a Kabambe abwera Kuti DPP isavutike kupanga mgwirizano NDI UTM. Kuba mbava izo a Malawi osanamizidwa.
@MpogoroMwikoko2 ай бұрын
Exactly 💯💯💯💯💯💯💯💯💯💯
@Mary-lb4ce2 ай бұрын
You r welcome bwana Kabambe.
@danmbuzi2 ай бұрын
Umakwana katswiri engineer bk tv
@ChimmsRichardOrden2 ай бұрын
Achimwene anga ndasangalala kwambiri chifukwa cha chisankho chanu choyenera nanenso ndili m, mbuyomo ndikupezani
@dicksoncassim19542 ай бұрын
My vote
@PollyLysonLutepo2 ай бұрын
Dzikomo a Kabambe chifukwa chokumbutsa bodza lomwe tinalandira pomwe UTM inali limodzi ndi Mcp. Anthu azadya katatu pa tsiku Koma anthu kusowa ndi phara lomwe. Kulemba anthu 1.000.000 pa Chaka, Koma anthu amaphunziro awo kukharira maganyu m'ma Town ndi m'minda ya anthu. Chonde Manfestar amenewo chotsaniponi angationongele Chipani chathuchi. Amenewo ndi amene alepheleka kale. Bodza limenelo tiyeni tiwasiyile Eni ake a Mcp
@williamsalexmbonga2 ай бұрын
Man inu simukudziwa kuti zimenezo angalonjeza ndi kathyali wa Miyambi uja zonsezo
@joyceellis90452 ай бұрын
Koditu manifesto mwanenadi idali yathu ife a Utm . Koma tiziti siidatheke chifukwa kum'phika sikudali ife. 😂