Bon Kalindo Ndi Guru lake la Malawi first ayankhura izi pamene anapangitsa press conference lero

  Рет қаралды 38,761

Makosana

Makosana

Күн бұрын

Пікірлер: 172
@user-mg5yy5hk9t
@user-mg5yy5hk9t Ай бұрын
Anganga Alula malawi fist member all the way from mangochi mamatiyimilira mr big man keept up mangochi yosaopayo
@user-eh1mg3ww6d
@user-eh1mg3ww6d Ай бұрын
Ndipo athu inuyo tchito mukuigwila mulungu azikusungani ndi moyo maka Mr boni kalindo simutopa mwamangidwa kambili mbili mukanakhala wina bwezi mutatisiya ife athu osauka sikuti ndinu Muthu ovutika ayi koma mumasiya pogona pabwino zakudya zabwino kukagona Malo onyasa chifukwa Cha ife aphawi kuzipeleka m,sembe pokhapo mulungu adzikudalitsani ❤❤
@RiyemaDomybusiness
@RiyemaDomybusiness Ай бұрын
Exactly 💯💯 bon amatiyimirila ampwawi
@user-eh1mg3ww6d
@user-eh1mg3ww6d Ай бұрын
@@RiyemaDomybusiness sure tidziwapephelela ndithu athu amenewa
@VungaQueen
@VungaQueen Ай бұрын
Boni Kalindo munthu wotiyimilira 🔥🔥🔥
@Moses51
@Moses51 Ай бұрын
The Dc bon kalindo keep up update 💪💪🇲🇼🇲🇼💯 osawopa
@user-ez8uk7py8n
@user-ez8uk7py8n Ай бұрын
That is true it needs all Malawian to vote as long as he/ she is Malawian Mr president keep continue loving your poor people abd our country Malawi proud of you thanks
@esaMoha-dm4kj
@esaMoha-dm4kj Ай бұрын
I respect your Mr nkalindo together with Malawian fest and the cautrry everyone DC is so powerful as well and you are always welcome to our team of Malawi wholld my Allah bless you always about the what happened with Malawian
@esaMoha-dm4kj
@esaMoha-dm4kj Ай бұрын
I am a Malawi but now I'm in the sauth Africa estan about working on
@WysonJalamu
@WysonJalamu Ай бұрын
Big up the DC osatopa, osafowoka, osawopa malawi ndi wathu uyu, tili limodzi pa nsewu basi.
@user-ml4bl2ll2g
@user-ml4bl2ll2g Ай бұрын
Please please ife TIKUFUNA ufulu wathu wovota a MCP asauchotse ponamizira ma id, aliyense akuyenera kukavota popanda id
@Franklifo2217
@Franklifo2217 Ай бұрын
Nzelu mulibe enanu! Anthu omwe mumalephelesa malawi kutukuka🙌
@hudycorex1893
@hudycorex1893 Ай бұрын
Inu amzeru kwambiri?​@@Franklifo2217
@SamKaposa-i5c
@SamKaposa-i5c Ай бұрын
Anzeru ndinuyo? ​@@Franklifo2217
@MussaHassani-zg1hm
@MussaHassani-zg1hm Ай бұрын
This is our president kalindo thanks so much for your help Malawias
@DavieBinzih
@DavieBinzih Ай бұрын
More fire mr kalindo we proudly of you keept up we love you
@YousufMpunga
@YousufMpunga Ай бұрын
Ndine Yusuf wakumangochi kmnso amalawi amene Ali kumaiko akunja apasidwe mwai wovota kuchokera kunja konko kumene ali
@patrickmacheso5062
@patrickmacheso5062 Ай бұрын
That's true, we need to vote and choose the President that we want not this Manyaka Government, but the problem is Akazembe athu sathandiza or kuwapempha kuti atipatse mwayi ovota.
@WezzieChimuzi-ek7bk
@WezzieChimuzi-ek7bk Ай бұрын
Good job my people Ambuye azikutetezelani ndi mwanzi wawo nthawi zonse ..
@user-uf4db7im7d
@user-uf4db7im7d Ай бұрын
This government must go
@user-gs7wc3nx3q
@user-gs7wc3nx3q Ай бұрын
yaa wa mcp ngati akunyasidwa ni boni karindo asavere khani zake ayi chonde ife anthu osauka tiyeni tizimuvera boni koma uzayime iwe boni tizakuvotere
@user-uf4db7im7d
@user-uf4db7im7d Ай бұрын
Every malawian should be in a possession of ID, If the NRB is failing to reach all malawians for ID registration, you should expect Malawi to be on fire, because voting results will not be accepted, People have rights to vote for who they want not rigging.
@FrankSpison-o7o
@FrankSpison-o7o Ай бұрын
The Dccccccc Booooooooon kalindo inu nde anthu oti mzika zamalawi tizikupemphererani kwambili 🙏
@NellieKabvina
@NellieKabvina Ай бұрын
Pa ziphatsopo ndie zikudabwitsa zikupezeka kuti anthu ambiri akumadziwa tsiku lokuti akumaliza kupanga ma ID,,,sakulengeza tsiku loyamba anthu ambiri akudandaula
@harrisonlowheat6569
@harrisonlowheat6569 Ай бұрын
My president
@RemaniNkhoma
@RemaniNkhoma Ай бұрын
boni karindo tingopita mawa bwanji pa sewu kuti agaru awa tiwakhawurise
@chippakaribafox2865
@chippakaribafox2865 Ай бұрын
Lets presure dem evo!....aluta continua!
@user-wi9pe2hz7e
@user-wi9pe2hz7e Ай бұрын
Good move Malawi First ❤
@esaMoha-dm4kj
@esaMoha-dm4kj Ай бұрын
I respect your nkalindo bisid ashankwela and everyone else has been in the path of mcp I don't respect anyone anymore because the people who keep and keeling Malawian people 2025 mashall Allah bless you nkalindo 😮😮😮
@ChristopherMadulira
@ChristopherMadulira Ай бұрын
Congugulations Mr DC ntchito mukugwila anthu inu only God bless you ❤❤❤❤❤
@AnussaAlli
@AnussaAlli Ай бұрын
Big up the DC Bon kalindo continue timakunyadlan❤❤❤❤❤❤🎉🎉
@jogechawa6192
@jogechawa6192 Ай бұрын
Bon Kalindo and malawi first our hope basi
@dawsonwaya4722
@dawsonwaya4722 Ай бұрын
Za ziiiiiiiii munthu unalephera kuimirira constituency ndiye ukati amalawi osauka aaaa zangokuvutani Moya, .
@robenallie6985
@robenallie6985 Ай бұрын
Ndizako zimenezo dc number 1
@FatimaAyami
@FatimaAyami Ай бұрын
Vuto ndi bomalo iyeyo amangopanga imprement
@OdettaLowrence
@OdettaLowrence Ай бұрын
Ulemu wanu Mr Born 🙏🙏🙏🙏
@Samu-q3z
@Samu-q3z Ай бұрын
Boni karido ndikatundu
@SamKaposa-i5c
@SamKaposa-i5c Ай бұрын
Viva malawi first Richard mphepo umadziwa kuyankhula more fire dc
@Okalekale
@Okalekale 25 күн бұрын
Tikufuna tidziwe kuti ndi ndani amapanga sponsor gulu lanuli Mr.Kalindo?.The nation should know if you claim to advocate for transparence.
@BacklinebwanaliBwanali
@BacklinebwanaliBwanali Ай бұрын
Akupatsen moyo was utali
@user-dq9oe8sp8k
@user-dq9oe8sp8k Ай бұрын
Ifetu though tilibe ma ID kma tikazavota Angoona kuzinamidza agwapewa Fireeee the DC❤
@KeftonChimaliro
@KeftonChimaliro Ай бұрын
Iyayi zonsezitu akupangazi akufuna ndalama mtambo samachitaso chocho anango kuwapatsa zochita ndikungokhala duuu osayakhulaso amalawi anthuwo ndi amodzi Lucia's. Anayimba kale
@FatimanickisJaffer
@FatimanickisJaffer Ай бұрын
Wa mcp ngt born kalindo amakunyasa usamaver nkhan Zak iwey ndy opanda zelu ife tikufuna dziko libwerer ngt kal osat mukumakambo shem on you 😢😢😢😢
@KhalidwePentani-c6q
@KhalidwePentani-c6q Ай бұрын
Iwe ndamene ukava ngat ine mbuz izi za duuu
@amoschataika7440
@amoschataika7440 Ай бұрын
Well done guys kpt up
@YohaneChitapini
@YohaneChitapini Ай бұрын
Mumakwana ndipo ndinu nokha boss ndagwada ndikumvesela
@MikeKoloko
@MikeKoloko Ай бұрын
Mumatiimilira, big up
@usherjamson174
@usherjamson174 Ай бұрын
Mulungu azikhala namu guy's 💪💪
@MercyJohnsonkanchure
@MercyJohnsonkanchure Ай бұрын
Mr Kalindo Mulungu azikupansani zeru zakuya ngati Solomon ❤
@HusseinAdamLidezo
@HusseinAdamLidezo Ай бұрын
Never give up guys let's see what happens
@ShariffAbdul-m9t
@ShariffAbdul-m9t Ай бұрын
I salute you
@TiyamikeMakande
@TiyamikeMakande 28 күн бұрын
Mumatiuankhulira ndinu bwana ,mutiyankhulireso za ndrama za masiye ku Capital hill Chaka chino nchachitatu ndrama sakutipatsa tikuvutika ndi ana
@RanaQari-py4bd
@RanaQari-py4bd Ай бұрын
Mumakwana guys we love you all the time 🙏🙏🙏🔥🔥🔥🔥
@user-uv5rf4zt5q
@user-uv5rf4zt5q Ай бұрын
Malawi first all the best u are representing poor people. To be honest Malawi is the poorest country in the world our leaders are selfish we are going backwards.
@AlidWidon
@AlidWidon Ай бұрын
Wosawopa bon kalindo tili limodxi 💪💪💪🔥🔥🔥👆👆
@AndrewNyondo-ut3gk
@AndrewNyondo-ut3gk Ай бұрын
King David bon kalindo the DC❤
@lastonkandiyado4526
@lastonkandiyado4526 Ай бұрын
Respect 🎉🎉🎉
@HarrisonMangani
@HarrisonMangani Ай бұрын
They need to address those issues other wise Mmmmm panunkha mphira
@nelsonmhango7515
@nelsonmhango7515 Ай бұрын
Inu ndi king
@Lazarus-qo1sl
@Lazarus-qo1sl Ай бұрын
Pick up guys chilungamo ndimwano
@patrickmacheso5062
@patrickmacheso5062 Ай бұрын
Ndimayesa ngati mukhala kumbuyo kwa a name anu kkkkkkkk let's fight together, this country is belongs to all Malawians not MCP only.
@RanaQari-py4bd
@RanaQari-py4bd Ай бұрын
🙏🙏🙏🙏🙏 Thnx good work
@isabelmartin7567
@isabelmartin7567 Ай бұрын
The DC ❤
@KhalidwePentani-c6q
@KhalidwePentani-c6q Ай бұрын
Zopanda ntchito izo akalindo mumangofuna udindo ngat mungakwanitse kutumikila dziko aaaa zawumbuli
@Mervic-vm8eo
@Mervic-vm8eo Ай бұрын
Wa MCP pamtu...
@ImanRashidi-so4oo
@ImanRashidi-so4oo Ай бұрын
Congratulations mr DC
@GodisoneNoel
@GodisoneNoel Ай бұрын
Asirikali achirendo muzikorathu zichepe mr DC
@GetrudeBanda-sd1yf
@GetrudeBanda-sd1yf Ай бұрын
Only GOd Bless you DC
@MuhammedNtaba
@MuhammedNtaba Ай бұрын
❤❤❤ The DC
@user-bd5kw8oq1r
@user-bd5kw8oq1r Ай бұрын
Akumangeni ngati mwaphwanya malamulo dala mbuli
@kenmasta
@kenmasta Ай бұрын
Ndiye mmene akumamumangamo ndiye akumamupeza ndi milandu yanji,,,,..ndaletu zisakusokonezeni mchimwene andale amabwera amapita koma Malawi adzakhala yemweyu ndiye let's love Malawi.
@user-bd5kw8oq1r
@user-bd5kw8oq1r Ай бұрын
@@kenmasta mwanena nokha awa asiyeni koma akanalankhula zinthu zambili ndi za against popeza ine ndinapanga nawo compain ndiye sanandipatse udindo awona, zimenezo ndi zabodza,chikuwawe sichimanga dziko amwe awa ndi a ndale musokonekera sayamika ndi ankhwidzi amafuna zawo ziwayendere kalindo akudya makobidi inu mukudya nawo 🤗🤗 ayi so bola yesu
@user-dy5bj9ck5e
@user-dy5bj9ck5e Ай бұрын
The DCCC
@CostanceLalli
@CostanceLalli Ай бұрын
Good move bafethu salute you
@frankiechasokoneza5802
@frankiechasokoneza5802 Ай бұрын
Point of correction not guru lake koma Born kalindo ndi guru la Malawi 🇲🇼 first
@YohaneChitapini
@YohaneChitapini Ай бұрын
Guys inu musazafe mulungu azikudalisani
@PempheroMoleni
@PempheroMoleni Ай бұрын
Firr the DC
@EliasMcray
@EliasMcray Ай бұрын
Go go ahead
@AnockyDavidd
@AnockyDavidd Ай бұрын
Congratulations to all
@gracetjomane-jj3ib
@gracetjomane-jj3ib Ай бұрын
Kutundu uyu the DC❤❤❤❤❤❤
@SueWahna
@SueWahna Ай бұрын
Big up Malawi first 💪💪
@Fridayasani
@Fridayasani Ай бұрын
Osawopha Bon kalindo tikukupembela kwamulungu Kuti anzikala nawe kwina kulikonse komwe udziyenda
@ambeweburton
@ambeweburton Ай бұрын
Timenyeleni nkhondo please mulungu imvani kulira kwathu
@user-tw2zf7bj3e
@user-tw2zf7bj3e Ай бұрын
❤❤❤❤ guys
@PetroMatias
@PetroMatias Ай бұрын
Amarawig fct muri nbi mfunbo zabwini timakuyamikirani
@InnocentKavalo
@InnocentKavalo Ай бұрын
Zoona big umakwana dc
@Malambia
@Malambia Ай бұрын
Mr kalindo ulemu wanu
@ritchardchakuma5725
@ritchardchakuma5725 Ай бұрын
Apomwayikwanisa maiko enasaziwa Chichewa pakufunika ayaluke mbavazi 💯🔥🔥🔥🔥🔥
@kurhikhoza8298
@kurhikhoza8298 Ай бұрын
Tipiya pa sewu akapanda kuyakha
@Samu-q3z
@Samu-q3z Ай бұрын
Zikomo boni karindo umatiyimilila big Kom amalawi sitimayamika
@user-dy4gc2hr5e
@user-dy4gc2hr5e Ай бұрын
Good move
@AgnessChiwalo
@AgnessChiwalo Ай бұрын
Your good man bon
@LukaJaulanchirwa
@LukaJaulanchirwa Ай бұрын
You people you thinking harder that is good Diction thank chakwera is not thinking
@chikoko-uj2tt
@chikoko-uj2tt Ай бұрын
Salute 🫡 The DC
@ntandokazindzwana3083
@ntandokazindzwana3083 Ай бұрын
Fire fire tili pa mbuso pa malawi oyambirira
@JafaliAjusa-zg2xi
@JafaliAjusa-zg2xi Ай бұрын
Respect Mr
@DavidJackson-ox4xm
@DavidJackson-ox4xm Ай бұрын
The DC'S mwana woooopsa kwambiri chilungamo chiyende ngat madzi.
@AgnessChiwalo
@AgnessChiwalo Ай бұрын
❤❤❤ good news
@shephardlonex3371
@shephardlonex3371 Ай бұрын
Booooooooni kalindo
@Mervic-vm8eo
@Mervic-vm8eo Ай бұрын
Go konko bwana DC❤
@HajaSande
@HajaSande Ай бұрын
Zikomo kwambiri umawona patali
@PreciousKARINGANIZA
@PreciousKARINGANIZA Ай бұрын
Tilikomweko
@SolokingChimzy-yt7dj
@SolokingChimzy-yt7dj Ай бұрын
Following with all my chidwi
@sarahmphande6108
@sarahmphande6108 Ай бұрын
I'm sure, the government you will grant our request
@MaryNgola
@MaryNgola Ай бұрын
Mmene wafikira Malawi alipodi amene akumamuona uyu kt akupanga zolakwika? Iweyotu wa MCP nkana akukubowa
@shephardlonex3371
@shephardlonex3371 Ай бұрын
Munene kuti ife ngati A Dpp
@user-mh7cc8up4i
@user-mh7cc8up4i Ай бұрын
❤❤❤💯💯🔥🔥🔥
@RitaKainga
@RitaKainga Ай бұрын
Auzen anthu adyerawo amve ndithu
@JoshuaNyirongo
@JoshuaNyirongo Ай бұрын
Go konko..
@user-hr6dj4xc8l
@user-hr6dj4xc8l Ай бұрын
Koma mukuvutikatu kwambiri, munayambilira muja
@user-ru6fc3qy5n
@user-ru6fc3qy5n Ай бұрын
Zilibwino kwambili osaopa
@kashmirmohakashmirmoha8659
@kashmirmohakashmirmoha8659 Ай бұрын
Ulemu wanu DC😊😊
@ShadreckChimaimba-l9y
@ShadreckChimaimba-l9y Ай бұрын
Kunoso kwachitika zodabwitsa kunkhoma
@ShadreckChimaimba-l9y
@ShadreckChimaimba-l9y Ай бұрын
Osatopa big
The Joker kisses Harley Quinn underwater!#Harley Quinn #joker
00:49
Harley Quinn with the Joker
Рет қаралды 12 МЛН
Bony Just Wants To Take A Shower #animation
00:10
GREEN MAX
Рет қаралды 7 МЛН
КТО ЛЮБИТ ГРИБЫ?? #shorts
00:24
Паша Осадчий
Рет қаралды 3,6 МЛН
Malema addresses Gauteng EFF members
1:25:51
SABC News
Рет қаралды 264 М.
Jomo wamukana Bon Kalindo
4:20
Nkhalango Multimedia
Рет қаралды 63 М.