Ayi a Manganya mukuoneka okondwa, chasala nchiweruzo basi pa imfa ya nzanu, continue rest in peace SKC, tizakulira mpaka kale kale Biyeni
@bristonmwenga5286Ай бұрын
Mmmmmmm,,,koma Malawi,,,,z
@petroszgambo9949Ай бұрын
Manganya is a happy man nowadays, he is exactly where he wanted to be all along. RIP CHILIMA.
@user-lj7lm6ly7zАй бұрын
Ndiposoo
@stephancommercial580Ай бұрын
He is more than happy
@user-cs3lq5mr9tАй бұрын
He is just a puppet wa apule uyu😅😅 kd anthu simukuona what's going on... 😅😅 8:35
@user-ep7gu2td6yАй бұрын
He got opportunity he was looking for 😢😢
@vukanifracksonchinkonde7324Ай бұрын
You guys are unrealistic,you expect him to always morn....remember you can not keep crying for a workmate as if it's your mam and Dad. Why shouldn't he be VP ?
Koma anthu aku Balaka congratulations mumatha anthu amenewa tisawaoase mpata please.
@StevenMjMbamaАй бұрын
Good job Mr president and vis wanu limbikitsa ndinthu ulimi umenewuu
@user-rz8qp8tj8eАй бұрын
Koma guys sindikufuna kuseka ati monica imeneyi wig yanji 😂😂😂😂😂😂😂😂😂ndakomoka ❤Dr chikangawa woyeee and mr short chakwera ndi manganya mukuvala mochititse manyazi bwanji Kwachema ndi ku Balaka no people 🙌🙌🙌
@user-mv1ho9pp7oАй бұрын
Mamie ndiye mumangolondora kuli konse mulibe zochita zanu ndiyekut eti achakwerawo ndiye ayamba kuondatu chonsecho akudya misokho ya malawi or mutero chaka cha mawa muchoka mudyeretu misokho ya malawiyo paja dzina lina ndi chikangawa 😂😂😂😂😂😂
@chrisschikozera7271Ай бұрын
😂😂😂😂😂😂😂 koma akuliziwa dzinali LA chikagawali
@user-cs3lq5mr9tАй бұрын
Ndipo pansana pawo ndithu😅😅😅
@prettytambala5687Ай бұрын
Kumaka, dad asayende okha angayambe kukodwa ndi ana anjoka😅
@chitanibenito1109Ай бұрын
Ka msanje bwa???? Mix ti atsikana tosezenzedwa ma unduna tili ku mcp kkkk kuopa kulandidwa
@cynthiakananji1608Ай бұрын
Ulibe manyazi manganya kuchenjera konsekuja kumupha nzanu ngat galu ndi chikangawa nzakoyo,anthu akakuona akumakumvera chison chifukwa mawa ndiwe.utm yake itiyo yomwe uli iweyo,popeza chilima ali Moyo sunasapotepo utm.anthu amagazi mmanja
@anthonynkhoma4265Ай бұрын
With or without anthu program yachitika basi. Zomwe amakapanga president ndizothandiza anthu omwewo. Kupanda nzeru eti. Ndale zanji zimenezi. Nsanje paMalawi
Kunganakhala ku maliro tikanati angokhala po ananfedwa okha
@ThokoGomezaАй бұрын
Kuononga ndala kukayendera nyemba basi ndi matumba angat achimanga mukanagura kupasa anthu akusowa chakudya 😢😢😢😢😢
@user-gd6zb2bv8fАй бұрын
Watching from Johannesburg
@yusufbakaliАй бұрын
❤ Maiko usi a chakwela pano a kuyendela nzeru za Maiko usi
@yusufbakaliАй бұрын
Akugofuna kumugwilitsa ntchito then asamuphe mcp plan
@chitanibenito1109Ай бұрын
Bolanso kukanapita anduna okha mwinako kukanakhala anthu not as it is manyazi bwanji koma!!
@CleverJosafatАй бұрын
Ai zikomo anthu aku Baraka ❤❤❤❤❤
@MalitaKapesiАй бұрын
Km ndie kuli chinamtindi cha anthu!!! Kkkkkkk
@inessmsiyambiri8517Ай бұрын
Fanz mphwanga
@marryphili5419Ай бұрын
Keep it up balaka people mupitilize wosapitako achikangawa akamabwera kumeneko
@user-gd6zb2bv8fАй бұрын
My district ,keep it up
@user-io2uw2me9fАй бұрын
Manganya or utavala zofafana ndi chilima sungamake 😂😂😂kod apule mwachedwa nazotu nthawi yonseyi munalikut
@joyahmedjoma4615Ай бұрын
Ndipo live ife tikufuna chilima basi
@JeanKambala-gm1zrАй бұрын
Ndipo inu galu manganya Kwa basi ufiti basi kulakwa Koma chomumohela munthu ndichani mmmmmmmmm takaoneni kufupika
@stevezulu2108Ай бұрын
African countries need different type of Democracy designed by Africans them self. The one we follow now has a lot of European influence, control, and interest. It contains ideas whose goals are to control and pin down developing. countries. China has its own type, and Russia has its own. Many European countries have what fit them better. While in Africa, we are controlled by the West. People who shared our continent among themselves in 1884 without involving any African representative. So, let's not blame our leaders so much. But let's fix come up with our own type of Democracy.
@LindaKestonАй бұрын
Sapato ya madam yo eeh😅
@AleksaWilliams-qc6cnАй бұрын
Ku Balakatu anthu anafika kukenani mkona mwapeza kulibeko😂😂😂
@HannahBandah-ks1uhАй бұрын
😂😂😂
@SteveriaNyalugweАй бұрын
😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
@GanieAlidih-gu7noАй бұрын
Athu kod alikuti zukhala bwanji kumeneko😂😂😂😂
@GospelSoldiers-sr7npАй бұрын
Kaya alikutiko kkkkkk
@CleverJosafatАй бұрын
Inu simukuwona noka akuwopa kuti akawagesa
@RhodrickBandaАй бұрын
🤣🤣🤣🤣🤣 koma Malawi penapake zimaoneka ngat ena tidakali muzaka zamma 1980 nanga tikamunene munthu chifukwa choti wavala mofanana ndiwina wake kkkkkkk 🛌🛌🛌🛌🛌🛌🛌
@Lee-lee-w1rАй бұрын
😂😂😂😂😂😂😂
@RachelNkhoma-vn2joАй бұрын
Kkkkkkkkkk koma kuli anthu kapena kuli achina yudasi okhaokha?😂😂😂😂😂😂😂mbali yakuno chikangawa yomweyo msonkhano wa Mr chikangawa.Balaka number one pitilizani mtima umenewu❤❤❤❤❤❤ ndakukondani ndife abanja limodzi zigawengazo mutalikile Nazi zingakupheni zili ndi poison
@MonyaNtchonaАй бұрын
A Malawi chenjerani chakwerayo ali ndi asilikali akulwan
@MonyaNtchonaАй бұрын
A Malawi chenjerani chakwerayo ali ndi asilikali akulwan
Kodi ndiye mwati ku farm ya Demeter ku amakataniko. This farm has been there b4 iyeyu kulowa m'boma.
@user-mw8dq4is6kАй бұрын
Mr chikangawa ndi VP nde akuyendatu ngat campaign yayambika kale😮
@thomasbotha9790Ай бұрын
Sikulina anthu azapanga transfer ena Azapita ku Zambia ena ku Tanzania 🇹🇿 chifukwa cha mavuto boma silibwino ndalama zimabedwa kwambiri chithandizo palibe
@prettytambala5687Ай бұрын
Koma mpaka kukayendera nyemba like seriously apule?
@user-jn9tz3li3vАй бұрын
Kusowa chochita
@AREFRIEDNELSONАй бұрын
Mukufuna kumangoba zitukuko chamuthu chabe osati ndi boma linalima zimenezo mabodza basi 😅😅😅😅😅😅😅😅 koma azitsogoleri Enawa eeeti
@AREFRIEDNELSONАй бұрын
Sazidziwa zawulimi mukungo tha mawu palibe chomwe chikulowa mmakutumo. Koma zomwe akuganiza akachoka kumeneko ndi kukaba mitsonkho ya thu avutika ba mutamuwuza zamitsokho nde nde eeeeeee sngajowejowetu Tsinzina mntole mr Raza 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
@muhammadisaid3968Ай бұрын
Zachita bwino osapita anthu, chipani chokupha chimenecho, chondee ma boma ena mutengelepo phudzilo osawasekelera akanganya amenewa , I'm White Willison from machinga T/A chamba , Lulindi villege
@DavisonKambiaАй бұрын
Bomaloooooo!¡!!
@user-wi9pe2hz7eАй бұрын
Utsi watengekatu nawenso ukwela ndege pompano nd zigawenga zimenez😅
@PatriciaMbewe-xn7keАй бұрын
Kubalaka kuno tinali busy kusaka ya thumba lachimanga mpata opita Kwa apulesidenti sitinaupese😂
@MarvellousTech-kz6noАй бұрын
Abale azanga musiyen manganya ,usamunyoze zakutsogolo sizidziwika , adzatero Ali ana anu Ali pa mpando wa up resident
@joyahmedjoma4615Ай бұрын
Ife tidya masambao za ziii munali kuti nthawi yoseyi aaaaa ife si zisilu
@user-nv3rf7bl7rАй бұрын
Ulimu wanu ma pulezdent athu ❤❤❤❤❤❤
@bristonmwenga5286Ай бұрын
Wow!what a good initiative
@NellieMaulidiChimanda-p5tАй бұрын
Tiyeni titenge ngongole za Neef kuti titukule Business zathu ndi magulu a business Ndalama zimene akhazikitsa a President
@user-im8bv2el9bАй бұрын
Kodi Michael usi wavala kut afanane ndi big akunamatu uyu komanso iye kuzavula chipewa. Manganya iwe ndiwa map to see tikuziwa
@chrisschikozera7271Ай бұрын
Mr chikagawa akuondatu mzimu wachilima ukuzuguza
@FrankKambwaniАй бұрын
Idzidzi sidzingapangitse kutsitsa katundu ndi kukweza mphavu Kwacha