NKHANI YA IMFA YA EDSON CHILEMBA

  Рет қаралды 6,846

Nkhalango Multimedia

Nkhalango Multimedia

Күн бұрын

Пікірлер: 47
@OlivaKambelembele
@OlivaKambelembele 4 ай бұрын
Eish chilungamo chikuyenera chiyende ngati madzi apa amqbungwe pls athandizeni nkhani yokhuza iyi😢😢
@JAMESSAIZI
@JAMESSAIZI 4 ай бұрын
Ndipo ndizooba 😢😢
@ThembiTrueway
@ThembiTrueway 4 ай бұрын
Mmmm shame 😢😢😢😢😢zovesa chisoni abale Mzimu wawo uwuse mu mtendele sure munthu anamfa imfa yowawa
@ShadreckMwija
@ShadreckMwija 3 ай бұрын
Ipakaso okupha kumachalenja ondandaula Malawi wakaka ndiuchi unja akupita kuti wasanduka wamangazi ndi misuzi? Zikomo Mulungu ndiamene akuziwa akuthandizani akumbanja sizinaenereke kutero ause mutndere chimwene waifeyo pooezaso amapita kukapanga zachalichi muyembekezere kuona zachilendo kwaoseo amen
@GladysChiwanga-vd9zp
@GladysChiwanga-vd9zp 5 ай бұрын
Mulungu oziwa chilulungamo akukhuzeni ndi dzanja lake pemphero langa ndi kuthekera kwachofuna chanu (justice)
@chrispahuwa
@chrispahuwa 5 ай бұрын
Mmm yandikhuza komanso kundililitsa Mulungu akukimbitseni mitima yanu nonse akubanja
@PangananiChikaoneka
@PangananiChikaoneka 4 ай бұрын
Limbani mtima chemwali. Mlandu sumaora. Mudzasuma boma likadzasintha. Yembekezerani pa Yeheva basi. Pepani 😢😢😢
@DroliiDongowa
@DroliiDongowa 5 ай бұрын
Achakwela mungotipha amalawi tonse mutchuke ndinu,,, pepani akubanja.
@joelkatembe9198
@joelkatembe9198 5 ай бұрын
ine ndingakaibwenze live imeneyo ndipo eish angamve kunyuunguunya
@PenjanNkhoma
@PenjanNkhoma 2 ай бұрын
Sorry sister Allah is grateful one day is one day
@LucyKasengwa
@LucyKasengwa 4 ай бұрын
Very sad 😭😭
@PaulKambuzi
@PaulKambuzi 2 ай бұрын
Mmmmmmmm sorry akubanja phepani phepani😭😭😭😭😭
@starlonJames-qr4xl
@starlonJames-qr4xl 5 ай бұрын
Aeee zosankhala bwino hey km dziko kd likupitakuti😭😭😭 pepani pepani akubanja
@LovethMhura
@LovethMhura 2 күн бұрын
Rest well Edson
@BensonChilundu
@BensonChilundu 2 ай бұрын
Ndiye wina mkumati chipani cha Malawi Chikangawa Party ndi chabwino simwaona ochitsatilawo momwe akuchitila kupha mzawo ngati nyama yet munthuyo amamudziwa,ayi ndithu sichilungamo ndipemphe kuti chilungamo chidzawoneke uyu ameneyu akadzachoka pa mpando.Ndi odala padakali pano komano popeza mlandu siwuola and mawumboni onse alipo ndizotheka ndipo omwe amapha nawowo adzakalowa limodzi pangachedwe pangafupike
@juliusnjerengo2610
@juliusnjerengo2610 5 ай бұрын
This is very bad, I hope people in authority can help this family. Mr Mgombe why?
@lingstonenagoli7729
@lingstonenagoli7729 5 ай бұрын
Koma dziko iliri limakonderad anthu alemera komanso andale omwe akulamula pa nthaw imeneyoyo,,kumupha munthu opanda chifukwa aaah
@robertkabade5011
@robertkabade5011 2 ай бұрын
Ayi mulungu ndi wabwino mudikile boma Lina rest in peace your brother
@MathpeterLemon-ls1ns
@MathpeterLemon-ls1ns 5 ай бұрын
Ineyo vuto ndi mm'ang'anja ingotumani munthu akatape phazi basi tilange
@CrossieTchauyah
@CrossieTchauyah Ай бұрын
Pepani mulungu akuthandizeni
@ThokoKamvuma
@ThokoKamvuma 4 ай бұрын
Zomvesa, chisoni pepani ndithu.
@HusseinMofatt
@HusseinMofatt 5 ай бұрын
Sizoona ulamulilo uwuwu siulibwinoayi guys chakwela atimaliza guys tiyenitimpephelelechakwela amwalile guys atiphatuuyu
@thokochilimba-bs2mm
@thokochilimba-bs2mm 3 ай бұрын
Koma dziko ili ndagoma nalo😢😢
@robenmatchilinga604
@robenmatchilinga604 5 ай бұрын
Ambuye akhururukre pepan akubanja
@EdwardPhiri-n1e
@EdwardPhiri-n1e 5 ай бұрын
Anthufe koma chikondi chimatisowa kwambiri ambuye yekha ndiamene akuziwa koma
@AlinafeZimba-d6h
@AlinafeZimba-d6h 2 ай бұрын
Zomvetsa chisoni
@EsnartMateuchi-bz7bo
@EsnartMateuchi-bz7bo 3 ай бұрын
Rest in peace
@TrishBanda
@TrishBanda 2 ай бұрын
Too bad
@LM-gz5pk
@LM-gz5pk 5 ай бұрын
Ku police kunalowa chinyengo pano... Kumwamba kuli Mulungu onse apanga izi komaso akubisa chilungamo Mulungu akukatheni
@AlasonPaulo-ht7zb
@AlasonPaulo-ht7zb 3 ай бұрын
Pepanpepan akubanja
@EstherKanjanga
@EstherKanjanga 3 ай бұрын
Pepani ambuye alowelele
@MathpeterLemon-ls1ns
@MathpeterLemon-ls1ns 5 ай бұрын
Kodi mulibe anyamata oti atha kungobwezera okha zachambazi inuyo musadandauleyi ingobwezerani basi
@MaliamuSikawa
@MaliamuSikawa 5 ай бұрын
Zovetsa chisoni ndithu
@angellahmuwowo9413
@angellahmuwowo9413 5 ай бұрын
Pepani akubanja very sad
@JamesPaul-rg6tj
@JamesPaul-rg6tj 5 ай бұрын
Farawo kkkkk mbambanfe
@ChrispinChikagwa
@ChrispinChikagwa 5 ай бұрын
Mulungu amabweretsa zinthu poyera ndipo choonadi chidziwika komanso munthu umakolora chomwe wabzala. Mu mtima mwanga mukuwawa ndipo mulungu chitani mukuweruza kwanu
@BlessingsMakalani
@BlessingsMakalani 4 ай бұрын
Pepani Mulungu atithangatire bas
@JAMESSAIZI
@JAMESSAIZI 4 ай бұрын
Zikomo
@nadiahPhiri
@nadiahPhiri 4 ай бұрын
Anthu kuyipa kuposa Satan 😭
@KavisikaMaria
@KavisikaMaria 4 ай бұрын
Sorry
@OmarSalim-jo4ne
@OmarSalim-jo4ne 4 ай бұрын
Chipani cha mcp
@OliverNkhoma
@OliverNkhoma 5 ай бұрын
Uyuyu kungomuphanso pogwiritsa ntchito gulu
@BentryThupa
@BentryThupa 4 ай бұрын
Pepani
@elias.m.chunga
@elias.m.chunga 5 ай бұрын
Very bad
@WorldSt-d5p
@WorldSt-d5p 2 ай бұрын
Very sad 💔
@hanneckkadyampaken2197
@hanneckkadyampaken2197 5 ай бұрын
Too bad
@ThokoKamvuma
@ThokoKamvuma 4 ай бұрын
Zomvesa, chisoni pepani ndithu.
TONDE WADULA DRAMA SERIES EPISODE 106
28:26
Nkhalango Multimedia
Рет қаралды 19 М.
UMBONI WA IMFA YA JOSSUA MZEMBE
14:24
Nkhalango Multimedia
Рет қаралды 53 М.
How I Turned a Lolipop Into A New One 🤯🍭
00:19
Wian
Рет қаралды 12 МЛН
ROSÉ & Bruno Mars - APT. (Official Music Video)
02:54
ROSÉ
Рет қаралды 151 МЛН
Fake watermelon by Secret Vlog
00:16
Secret Vlog
Рет қаралды 30 МЛН
Assista na íntegra o Cidade Alerta 26/10/2024
MIRAMAR
Рет қаралды 540
TONDE WADULA DRAMA SERIES EPISODE 107
28:29
Nkhalango Multimedia
Рет қаралды 18 М.
ZURAH- AYOGEDDE LWAKI BULI MUSAJJA GWAYAGALA ASIRAANA | Unveild Experience
53:47
MAYI AKE A EDSON CHILEMBA ALIRA MOKWEZA
5:52
Nkhalango Multimedia
Рет қаралды 1,5 М.
TONDE WADULA EPISODE 113
27:54
Nkhalango Multimedia
Рет қаралды 26 М.
CYCLONE FREDDY FUNDRAISING DRAMA #malawi
1:31:45
Kanema Online
Рет қаралды 507 М.
How I Turned a Lolipop Into A New One 🤯🍭
00:19
Wian
Рет қаралды 12 МЛН