Politicians In Malawi Learn to Tell the Truth Mukalephela - Samuel Lwara

  Рет қаралды 5,676

Nyasa VoiceBox

Nyasa VoiceBox

4 күн бұрын

In his latest audio Samuel Lwara pleads with Malawi politicians to learn to tell the truth when they have failed to lead the country.
M'mawu ake aposachedwa a Samuel Lwara apempha andale ku Malawi kuti aphunzire kunena zoona pomwe alephera kutsogolera dziko.
#malawi

Пікірлер: 31
@JamesMalango
@JamesMalango 2 күн бұрын
You're a great man with an idea
@LumbaniNeba
@LumbaniNeba 2 күн бұрын
Powerful Mr Lwara
@user-fp5qn5ci2v
@user-fp5qn5ci2v 2 күн бұрын
Zikomo munthu wanzeruwe Samuel Lwara I salute you bwana
@LysonMtalika-tb6fk
@LysonMtalika-tb6fk 2 күн бұрын
Powerful talking
@alexsumani6823
@alexsumani6823 2 күн бұрын
Powerful,Lwara ,you deserve respect
@DavieMaloya
@DavieMaloya 2 күн бұрын
Powerful massage
@victormaluwa6710
@victormaluwa6710 2 күн бұрын
Powerful indeed 💪
@blessingmanda
@blessingmanda 3 сағат бұрын
namuwongani dada chiuta wamutumbikani
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 2 күн бұрын
Obwelesa mvula si azibusa ayu maan inuu, mvula amabwelesa ndi MULUNGU
@josephinemisomali6840
@josephinemisomali6840 2 күн бұрын
Eish imfa ya Dr Chilima I kupweteka tsiku ndi tsiku mutu kumachitakupweteka Rlp
@ruthchikhoswe6028
@ruthchikhoswe6028 2 күн бұрын
Powerful
@petertaulo8014
@petertaulo8014 2 күн бұрын
Ndege inali yabwino bwino koma inali plan yoti aphe Chilima thats all!
@user-qq3ip1od6i
@user-qq3ip1od6i 2 күн бұрын
Where is osward jumani
@user-un6qv6sj3h
@user-un6qv6sj3h 2 күн бұрын
Adanena kale kuti mudalibe black box
@MartinMsimuko
@MartinMsimuko 2 күн бұрын
Tikamanena wisdom ndi izi munthu uzivomereza zikavuta or uli pa position yotani accept ngati walephera
@user-pt8wb4vw6r
@user-pt8wb4vw6r 2 күн бұрын
Ndikudabwa adada wachitumbuka uyu akutukwana mafumu anthu komaso zimene akuyankhula onse amene akutukwana pano ali ndi zifikwa zawo iwe ukukakamila kukhala mnyumba yaboma undamange nyumba yako kumzimba uko nyumba zikuntchipa basi mpaka nalelo nyumba mlibe mkatukwane mafumu chikwa cha ndale mbusa uyu nyo ngwakutangwanika chomene ndicho chifukwa wakakangama na mamembazi ake siwosankhidwa ndi mulungu ayi .
@user-pt8wb4vw6r
@user-pt8wb4vw6r 2 күн бұрын
Akatolika ndiwozindila not enanu
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 2 күн бұрын
Anthu ena owona patali akusungila serial number ya black box yomwe inali mundege yomwe inapha chilima, nde iwe ukuti munalibe black box, stop confusing the pple
@chiefmalindi4070
@chiefmalindi4070 2 күн бұрын
Another Born Kalindo's brother from another mom
@Elvin-dr8tv
@Elvin-dr8tv 2 күн бұрын
Mtitole Makola 😂😅
@ebenezerkamanga6016
@ebenezerkamanga6016 2 күн бұрын
Iwe lwara wabwera tsopano tikufuna anthu ngat inu
@sydneyngoma2356
@sydneyngoma2356 2 күн бұрын
Where is Lyton Mangochi we miss him for his commitment to democracy
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 2 күн бұрын
Don't talk about laytin men!, we don't need to hear anything about dat stupid crocodile, I'm saying dis coz dat guy is a hypocrite and he don't deserve to be a freedom fighter
@meganabigail-ye7fw
@meganabigail-ye7fw 2 күн бұрын
Lyton mangochi zakudya Kaye ndalama ndi azikhale, chambiko nda chikuni anatelo oyimba Ena
@emmanuelsoko87
@emmanuelsoko87 2 күн бұрын
Malawi in not a lawless country,if you break the law,u will face the music.mukati asamange anthu nde likhala dziko? mkwiyo ochotsedwa mnyumba ya housing uwu😂
@petertaulo8014
@petertaulo8014 2 күн бұрын
Yes is not lawless country but Mcp take law in their hands ✋. This is also democratic country Mcp must respect this too and we can not accept this nonsense of arrest innocent people!
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 2 күн бұрын
Akulu inu, wat's ur point?, ngat munalibe blackbox, chimayeza temperature mumlengalenga mchiyani?, nanga mafon awanthu anafa mundege aja munalibenso?, nanga chilima anakapezeka 200 metres away from the place were the plane wer crushed y?, why chilima anapezeka alibe zovala chikhalirecho anali mu suit, and y anapezeka ndi mabala akuluakulu azikwanje mumiyendo yake😢? , eish!,
@LeendaDeborah2005
@LeendaDeborah2005 2 күн бұрын
Hmmm mulungu athandize ndithu. Kuyankhula yankhulaku kukubwera chifukwa cha mabodza omwe president amatiuza zokhudza za ndegezi. He knows the truth but God will expose him
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 2 күн бұрын
@@LeendaDeborah2005 data true , and they know wat they dd on dat day and the truth will review
@alickkachepa3801
@alickkachepa3801 2 күн бұрын
Ngamo yonkha yonkha
@GoodsonLindani-gf8pn
@GoodsonLindani-gf8pn 2 күн бұрын
Inuso ndiachitsilu papitapo zaka 4 chakwera akukwela yomweyo, bwanji ndege simagwa.lurwa nanuso point yanu siikuziwika mukuikila kumbuyo boma pena ayi,nde ndinu opepela kwambiri, bola kalindo amanena zomveka.
Maloto A Bon Kalindo (Part 2) - Bon Kalindo
14:17
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 73 М.
1❤️#thankyou #shorts
00:21
あみか部
Рет қаралды 88 МЛН
THEY WANTED TO TAKE ALL HIS GOODIES 🍫🥤🍟😂
00:17
OKUNJATA
Рет қаралды 5 МЛН
3 wheeler new bike fitting
00:19
Ruhul Shorts
Рет қаралды 51 МЛН
Ine Sindingasiye U Akitivizimu - Bon Kalindo
11:12
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 14 М.
EXCLUSIVE INTERVIEW WITH SAMUEL LWARA
51:08
Zodiak Malawi
Рет қаралды 29 М.
Wina Ndinamuthyola Khosi - Samuel Lwara
14:15
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 41 М.
Chimtengera - Iwe Malawi (Stool Session)
8:42
Nyimbo Zachimalawi
Рет қаралды 3,1 М.
BON KALINDO LERO PA 28 JUNE NDETU KULI NKHANI |
17:01
DZIWE TV
Рет қаралды 49 М.
KUMUYANKHA BILLY MALATA 29 JUNE 2024(MALCOLM)
8:42
Club Junta
Рет қаралды 13 М.
1❤️#thankyou #shorts
00:21
あみか部
Рет қаралды 88 МЛН