Rev Alexander Kambiri preaching at Malawi Immigration Head Office -Lilongwe Malawi

  Рет қаралды 38,763

Rev. Alexander Kambiri

Rev. Alexander Kambiri

6 ай бұрын

It was morning devotion service which happens every Monday at Immigration' office

Пікірлер: 82
@blessingkamanga1781
@blessingkamanga1781 6 ай бұрын
Maybe they can stop corruption. The one who organized this program may God bless him or her abundantly.
@ceciliasibande7936
@ceciliasibande7936 6 ай бұрын
Kupezeka ku immigration ndi chisomo cha Mulungu zoonadi Mulungu adasankhadi inu kuti mupezeke pa maudindo muli nawowo. A big Amen
@user-fd6oh2vc1c
@user-fd6oh2vc1c 6 ай бұрын
Please continue organizing this program frequently as very helpful to such.God bless you Rev.Kambiri
@VictoriaWilliam-ms2ft
@VictoriaWilliam-ms2ft 4 ай бұрын
Amvekere Amen ngati za nzeru mbava zachabechabe izo ndipo alape anthu amenewo
@user-pf1xd3lp2u
@user-pf1xd3lp2u 3 ай бұрын
May God bless you pastor powerful message wakhutu wamva
@enipherphiri207
@enipherphiri207 5 ай бұрын
Wow! This is the divine definition of grace to individual staff at immigration. Review yourself and stop maladministration. The spirit has spoken. Thank you pastor Kambwiri
@MaggieKapalamula
@MaggieKapalamula 4 ай бұрын
This is beautiful may God bless immigration office for honoring God words
@marypatriciamakuru226
@marypatriciamakuru226 5 ай бұрын
Amen Amen Amen. Mwina asinthe mchitidwe wa corruption. Abusa mudziwayendera kawiri kawiri.
@user-xd5bp8wr1m
@user-xd5bp8wr1m 5 ай бұрын
Sipangakhale kusintha because pamwambapo pali mbava yeni-yeni Shakwera ndi afalisi azinzake
@user-qf4oc1xj8d
@user-qf4oc1xj8d 5 ай бұрын
God continue talking to us through the ones you have chosen So that we can know why we are in our positions Amen
@suzyomanda4359
@suzyomanda4359 6 ай бұрын
Amen, thank you for the word of encouragement Abusa. God bless you
@catherinechisale9567
@catherinechisale9567 4 ай бұрын
Good initiative by Immigration Department. May good Lord bless you. Zikungofunika kulapa basi, mgt Pampanga mbali yake.
@robertrichman9376
@robertrichman9376 6 ай бұрын
Best place to preach, next time to our Parliament
@mchipengule
@mchipengule 6 ай бұрын
Mau a Mulungu sasankha Malo. God is everywhere!!
@abdulrafiquekalembo469
@abdulrafiquekalembo469 5 ай бұрын
I always agree with this man.He knows how put sense into people mind.
@user-vi4ge5lq8t
@user-vi4ge5lq8t 5 ай бұрын
More blessings to you pastor
@LimbanChasasaThawi
@LimbanChasasaThawi 4 ай бұрын
Amen man of God
@user-lb6ek3ee6d
@user-lb6ek3ee6d 4 ай бұрын
Tadalitsika kwambiri Pastor
@user-ke7cd1et5k
@user-ke7cd1et5k 6 ай бұрын
Zinyengo ameneo zili mitu bibi
@funnychinsalu6198
@funnychinsalu6198 5 ай бұрын
😂
@user-cb2cv9fz7m
@user-cb2cv9fz7m 5 ай бұрын
Mbava za kuba MULUNGU awakanthe onse awa fire 🔥🔥🔥🔥 pano tilibe mtendere ndipo zoonadi akayamkhadi
@user-kv8fq6im3v
@user-kv8fq6im3v 6 ай бұрын
Anthu akatangale opondeleza ngati awa until they change that God has nothing to do with them
@bensonnkhatatonje6007
@bensonnkhatatonje6007 5 ай бұрын
Amen
@bensonnkhatatonje6007
@bensonnkhatatonje6007 5 ай бұрын
May I have it please
@user-uz7wp8mf6b
@user-uz7wp8mf6b 5 ай бұрын
To God be glory, ndadalitsika nawo uthengau ndipo wandikhudza
@abdulrafiquekalembo469
@abdulrafiquekalembo469 5 ай бұрын
Anthu amenewa uthenga aumve ndithu.Ma past port athu ali mmanja mwa ma Burundi,Ma Nigeria ndi Amwenye pomwe ife anuwake timavutika kuti tipeze passport.
@user-ps9nu6se9k
@user-ps9nu6se9k 6 ай бұрын
Amen man of GOD
@AminaPhiri-pp9tw
@AminaPhiri-pp9tw 6 ай бұрын
Amen Abusa awuzeni kwambili ave masozi ya anthu ili pamutu wawo
@user-wr7rm6yw3j
@user-wr7rm6yw3j 5 ай бұрын
Amen man of God 🙏🙏🙏🙏🙏
@LinesiKanzota-fw7sj
@LinesiKanzota-fw7sj Ай бұрын
Amen 🙏
@PaulMungoma-rs2st
@PaulMungoma-rs2st 5 ай бұрын
Amen tadalitsika nawo
@UchiziNyirenda
@UchiziNyirenda 6 ай бұрын
Preach on man of God
@quespeykatame2595
@quespeykatame2595 6 ай бұрын
Ma uthenga akumveka ndithu 😊
@e.r.mchanel1460
@e.r.mchanel1460 5 ай бұрын
Munasowatu a Rev
@user-ec3xh4pc6t
@user-ec3xh4pc6t 6 ай бұрын
Mrs luhanga ndakuonani number yanu bwanji
@user-zp6eq4br7t
@user-zp6eq4br7t 5 ай бұрын
Abusa zilingati mukulalika palibe coz muli pakati pa nkhosa zosochela😂😂😂
@mphatsojosephynyamatawakun3965
@mphatsojosephynyamatawakun3965 4 ай бұрын
amen
@Dan-Buleya
@Dan-Buleya 6 ай бұрын
Anthu awa eeeeeeh ambuye awayendere
@user-yt6ze8od9d
@user-yt6ze8od9d 6 ай бұрын
Amen Amen
@user-dx6jm4yx2e
@user-dx6jm4yx2e 5 ай бұрын
Ndizoonadi abusa amthu anenewa amati zuza ndi tauzika kudedza mulungu atithandize awakhululukike ambili akulila😢😢
@user-ec3xh4pc6t
@user-ec3xh4pc6t 6 ай бұрын
Amen 🙏 🙏
@alexbanda8463
@alexbanda8463 6 ай бұрын
Amen ❤
@PirtekDriver
@PirtekDriver 6 ай бұрын
Will the corruption stop????
@ruthnangwale
@ruthnangwale 5 ай бұрын
Powerful 🤝
@ChikondiLameckPhiri
@ChikondiLameckPhiri 5 ай бұрын
Thus Great
@user-sn4se3ul7i
@user-sn4se3ul7i 5 ай бұрын
Mulungu alemekezeke
@andrewchirwa2193
@andrewchirwa2193 5 ай бұрын
mwina angasiyeko chinyengo
@dumisanimoyo3152
@dumisanimoyo3152 6 ай бұрын
That is a very corrupt ministry in Malawi government plz from there kambiri go to traffic department
@mwale1154
@mwale1154 5 ай бұрын
Amen 🇿🇲🇿🇲🇿🇲
@mphatsojosephynyamatawakun3965
@mphatsojosephynyamatawakun3965 4 ай бұрын
lapan anyamata Inu aku immigration mukuba kwambiri tikamapangitsa ma passport
@adsonphiri6497
@adsonphiri6497 5 ай бұрын
Awa akufunikadi mapemphero,mbava zotheratu
@sweeneykamwendo6251
@sweeneykamwendo6251 6 ай бұрын
Ada awo anadya 100pin yanga...maofesara achinyengo😅
@AlliUsuman-mj1mr
@AlliUsuman-mj1mr 5 ай бұрын
Km musiye kuba anthu inuuu aku immigration
@masterkachingwe7448
@masterkachingwe7448 6 ай бұрын
Ma officers chinyengo awa alibzyoli anyenga okha okha mwina kumaalalikira Daily
@funnychinsalu6198
@funnychinsalu6198 5 ай бұрын
Kukonda ndalama a immigration
@khumbomkorongo4108
@khumbomkorongo4108 5 ай бұрын
Powerful
@josiahgarley3824
@josiahgarley3824 6 ай бұрын
Mpaka mmaoffesi?
@user-xk5se7ot8d
@user-xk5se7ot8d 6 ай бұрын
Kumapetoko munakawapemphelela
@AminaPhiri-pp9tw
@AminaPhiri-pp9tw 6 ай бұрын
Abusa nthuwa Alape kaye katangale amanyanyila kwambili alape ndithu
@amabhohlela.3492
@amabhohlela.3492 5 ай бұрын
Ingakhale mukuwalakhula choncho,sakumva kanthu ai ndithu"moti enawo angokutukwanani,angoti Galu iwe mumtimamo. tikakudyera kuti.
@user-ty6cs9ic5w
@user-ty6cs9ic5w 6 ай бұрын
Madalayo wosapanga retire bwanji akapume
@amabhohlela.3492
@amabhohlela.3492 5 ай бұрын
Abusa next week pitani ku STATE HOUSE,,kwaphulika zimimba kumeneko...
@numelimtenje5846
@numelimtenje5846 6 ай бұрын
Mwina angalapeko anthu ozunza awa
@user-vf1kt6fw7y
@user-vf1kt6fw7y 5 ай бұрын
Abusa musataye thawi ndi athu amenewo muchedwa nazo, zonsezo ndi mbamva zotheratu,funso nkumati mwasakha bwanji kulalikira office ya athu akubayo Bola munakapita kumamizi kulalikira km naizi Mmmmmm mbamva
@user-xs5mi3fr2y
@user-xs5mi3fr2y 5 ай бұрын
Please stop corruption
@funnychinsalu6198
@funnychinsalu6198 5 ай бұрын
Mukayankha pa maso ps mulungu ndalama mutazisiya pansi pano
@geoffreykalinda2672
@geoffreykalinda2672 5 ай бұрын
Apitekoso ku police (road traffic)
@amabhohlela.3492
@amabhohlela.3492 5 ай бұрын
Mukafikeso ku Ma Court...kuli mamafia kumeneko.
@amabhohlela.3492
@amabhohlela.3492 5 ай бұрын
Pomaliza chopereka abusa,,,
@NgomaRaheem
@NgomaRaheem 6 ай бұрын
Athokeni ngamo agalu amenewa akutilangadi passport ya 90pin kudisha 300,pin mulungu awaonedi
@gesinasutherland9241
@gesinasutherland9241 6 ай бұрын
komatu simukuwoneka abusa kapena Maliro achepa dera lanu..ulaliki wanu umatitsitsimutsa ndipo umatisintha..kapena 2024 Mwabwera ndi zina..😂😂
@rev.alexanderkambiri892
@rev.alexanderkambiri892 6 ай бұрын
uthenga si waku maliro okha, tili nawo ma videos ambiri koma sitimatha kutumiza kamba ka kuwonongeka kwa zipangizo zathu zogwiritsa ntchito. pang'ono ndi pang'ono tayambapo kuzitolera ndipo Ambuye atithandiza.
@fahadmilanzi
@fahadmilanzi 5 ай бұрын
Ulaliki wabwino aRev gulu lozuza limenelo
@user-tb6yh1kx3o
@user-tb6yh1kx3o 5 ай бұрын
Anthu awa amakhalangati anachoka direct kumwamba kuti azagwire ntchito ku immigration
@YasiduPemba
@YasiduPemba 5 ай бұрын
Immigration ya malawi ntchito ya NRB mumaidziwa koma chipangisireni chitupa changa sitinafunsidwepo mpaka pano from 2018 ndimafunsidwa ndikapita Zambia Mozambique Tanzania 😂😢😅😅
@damianokachingwe3531
@damianokachingwe3531 5 ай бұрын
Anthu opanda chisoni amenewa kuteroko lero lomwe lino amubera wina ndalama kulephera kugwira ntchito mwachilungamo too much corruption
@clintonhodda9830
@clintonhodda9830 6 ай бұрын
Anthu a corruption awa
@juliusnjerengo2610
@juliusnjerengo2610 5 ай бұрын
Pastor you are preaching to evil people. Ndinakanika ulendo wanga opita ku UK chifukwa cha asatana ameneo.
@AlexMwalec
@AlexMwalec 5 ай бұрын
Amen
@user-kd3lh4wy1m
@user-kd3lh4wy1m 5 ай бұрын
Amen
@gesinasutherland9241
@gesinasutherland9241 6 ай бұрын
Amen
@chisomonyerere7197
@chisomonyerere7197 6 ай бұрын
Amen
08 July 2024
25:46
Apostle Dinah Mabunda
Рет қаралды 3,2 М.
50 YouTubers Fight For $1,000,000
41:27
MrBeast
Рет қаралды 205 МЛН
Clown takes blame for missing candy 🍬🤣 #shorts
00:49
Yoeslan
Рет қаралды 43 МЛН
Mom's Unique Approach to Teaching Kids Hygiene #shorts
00:16
Fabiosa Stories
Рет қаралды 33 МЛН
Spot The Fake Animal For $10,000
00:40
MrBeast
Рет қаралды 176 МЛН
MR JOKES' LIVE PERFORMANCE IN FRONT OF VANGUARD INSURANCE.
24:38
MOSES KUNKUYU EXCLUSIVE INTERVIEW
56:13
Zodiak Malawi
Рет қаралды 27 М.
Revival  crusade at milamba prayer house preached by Rev Alexander kambiri
24:47
Katondo C.C.A.P Church-Dzenza Presbytery
Рет қаралды 19 М.
Mlaliki Shadreck Jonas Wame ( MASIKU A MOYO WANU NDI ANGATI?)
30:02
Hot Current Nduna Yoona Zachitetezo Cha Mdziko Wamukalipira Brian Banda
1:03:23
Rev Alexander Kambiri preaching at Kapaza CCAP- Mponera -Dowa
1:09:07
Rev. Alexander Kambiri
Рет қаралды 4,6 М.
50 YouTubers Fight For $1,000,000
41:27
MrBeast
Рет қаралды 205 МЛН