Chizungu mukuwuza ndani simuzatheka dziko losauka koma vizungu kkkkk
@jafarilulanga6561 Жыл бұрын
muthu oti akudya bwinobwino sangarowe muchele ndikumadula mitengo? kod simukwaona amene akudula ndalama za malawi za misongo simumamanga? koma odula mitengo nde eeee☠️☠️💀💀💀💀😭
Á malawi mukufuna umukhale ngati nafni skúti tidzizungu izitu ndi zopusa með mukutizunzatu tikamasauka kukhala opanda chuma
@masterjailos3913 Жыл бұрын
Kupusa basi munaonapo mzungu akuyangura chichewa?
@zaidiealifualifu9989 Жыл бұрын
Nde mukuvutikilanji ndi chizungu chosecho alipamenepo ndi anthu ot amava chichewa cholinga winayo akhale ndi mantha muwine likubwela tsiku muzuzayankha zimenezi
@promise3693 Жыл бұрын
Kumamanga osauka kusia olemera popeza ndrama zao zuchitira umbon
@user-fg5iw1qy1k Жыл бұрын
Mzaziii basi mukusiya kulimbana ndimbamva zomwe zikuba ndalama za boma mmmmhh koma mulungu akulangeni ndithu
@trinitykalima1840 Жыл бұрын
Ena akuba ma billion mulibe nawo ntchto kma kulimbana ndi mphw chifkwa cha mtengo umoz,inuyo ndi amuyaya? Enawa mukuwaponya Pat?
@tomothybanda9070 Жыл бұрын
Mukumanga osawuka mukusiya akuba Gold ndi misonkho ya amalawi why amalawi? Ziwani chomwe chinapangisa kuti akalowe kunkhalango ndinu amu boma no jobs. And magesi amangoyaka 2 hours mukuganiza kuti amphawi iwe tiphirachani mumakomboni? Yambani kumanga akuba mubomawo ndi ena then pezani njira zabwino zathandizia amphawi.