Akuvutik kulankhul chichewayo ndi mchew oimbidwa mland mchew kom ndikumufun munthu win mchewanso kut azimasulir pal nzer yanj tsono kungonong nthawi
@ALLIEDAUDI2 ай бұрын
Neba neba neba mutu sukungwira ❤😂😂😂
@FatimanickisJaffer2 ай бұрын
Km iyi nd nkhan yen yen kapn sewelo pot abambowa ngt Tinawaonas week yatha pa nkhan yinas yokhuzanas za banja
@FragsonChimpanda-so4ft2 ай бұрын
Ndisewerotu ili
@CliveChikaphonya2 ай бұрын
Owooo Nd sewero et ndmadabwat
@eliaskachali-xn2ve2 ай бұрын
Aboma inu ndinu zisilu
@edgarmsofi5892 ай бұрын
Judgement: suspended sentence. A tengerepu phunziro basi.
@AREFRIEDNELSON2 ай бұрын
Nde ndimene lilidzikoli lathu li china chili chonse ndichovuta kupeza nde mumafuna kuti atani mmene dziko lilimu mfunso langa ndilakuti chomunjaJila mulandu Chifukwa chani
@jameskamanga6282 ай бұрын
Koma ziliko 🙌😋
@shayrafernandeslatif95562 ай бұрын
Kodi ana amasiye woynaglidwa ndi a ma bungwe,amafunika kuti azigwira ntchito yolima minda??? Kuno ku mudzikwarhu kuno tikuwona ana amasiye akulima Munda,zikumandimvesta chisoni
@Esther-r8c2 ай бұрын
Mmm iwe sunawathandize bwanji
@Esther-r8c2 ай бұрын
Neba uyu mesa ndi uja anamangitsa nkazi wake kuti wamupasira matenda
@ethelkamwendo7022 ай бұрын
Also me i think so
@AnnieKazembe-ic5vp2 ай бұрын
Boma limanga bwanji maiyu pomwe ana ake amavutika nawo okha opanda otengako mbali even bomalo siliwathandiza ,ine nde anaanga munthu wina sangandiuze zochitatu pokhapokha ngati amandithandiza atha kutengapo mbali
Kodi nkhani izi bwanji zumakhala za anthu amodzi modzi? Ndi drama mwina? Onsewa aliapawa amabwela ndi nkhani zosiyana siyana
@TakondwaSaidi2 ай бұрын
Eya
@egreymkumba-tj5ji2 ай бұрын
Anthu ake angokhala omwewo kodi ndi drama eti
@gladysmanthimba78512 ай бұрын
Bambo a mwana amangidwe
@mphatsomaluwa2 ай бұрын
Tiziyakhulanapo chichewa apa
@BillySaukani2 ай бұрын
Ku nzunza mwana kumpatsa udido pamene suli wake
@MalackPatrick-jt4hk2 ай бұрын
Koma maniwa atava anachitapo chani ndiompenga ameneyi
@CliveChikaphonya2 ай бұрын
Kd mboniyi ikupezeka bwanj pa nkhan zambir
@HalimuChisaka-o1tАй бұрын
😂
@wezzieneba92382 ай бұрын
She is so innocent, please, forgive her and tell her what is supposed to be done. She has said that she didn’t know. Even God will punish us on what we know. She doesn’t know what it means, the so called constitution. She is there to be forgiven and tell her what to doing. What she did or she was doing is just the consequence of poverty and neglect from her husband. Yes, it wasn’t right, but she needs to be guided and not penalized. My food for thought. Thank you.
@AUFIMADENGU2 ай бұрын
KHANI YAVEKA KOMA VUTO NDIMAVUTO BOMA LIKUYENERA KUKHARA NDI NDONDOMEKO YO PHUZISA MIZI KUTI KUTERO KULAKWILA MALAMURO IZI ZAPANGIKA CHIFUKWA CHOSAZIWA ZIKOMO
@AtupeleChitenje2 ай бұрын
Ma number ama athu oona zakhaza zanawo tipaseko 😢
@HarryChikandira2 ай бұрын
Ndi program yodziwitsa anthu za malamulo okhudza ana Komanso chilango chomwe chimaperekedwa Kwa olakwa.Program imatenga nkhani zenizeni zomwe zimachitika mmalo momwe tikukhalamu bwana wanga ndithu ACC mene munafunsa kuti ndi drama kodi nanga bwanji anthu ake as mangokhala Omwe omweomwewo.