Iweyo Timothy unali kale,Timothy pano unatha ngati katani,Watulukila chifukwa zisankho zayandikila ukufuna utiputsisenso ife amalawi,ndiwe dobadoba wozimenyera nkhondo kuti ukhutise mimba yako,You use the poor Malawians and dump them like Sheet and let them suffer,no one is going to follow you this time
Timothy Mtambo mapwala ako.inetu nditha kukuloza galu iwe
@user-rg5re6gh7e14 күн бұрын
Zigalu iwe mbuzi you got no point to convince anyone to vote for MCP nonsense
@OBETEDOS7 күн бұрын
Ife pano tilinayo kale otimenyera nkhondo ife tili pheeee Mr Bon Kaliiiiidoooooo!!!!! Inu chonde mkapume
@user-un6qv6sj3h15 күн бұрын
Shame on you mtambo your heavenly??? really
@PatsonChirwa-ks3rt12 күн бұрын
Mutambo zaziiiiii
@user-rg5re6gh7e14 күн бұрын
I don't see the point of voting for mcp he starved us since 2021💀
@chifundobuledi11 күн бұрын
🎉Bwana Mambo nobody I repeat nobody Wil never trust you Zisiyeni Bwana MALAWIAN ARE NOT ON YOUR SIDE Nthawi yanu Bwana inatha pano We poor People tatopa nanu. Kodi Alana panda kukuchotsani bodzali mukanakamba???????
@priscillamangata402316 күн бұрын
Ife pano tinakwela ya kalindo President wathu wosauka
@mishecksipolo715315 күн бұрын
Ndiwe galu kwabasi,4yrs against 1yrs which service delivery u expect from chakwera regime, my foot
@paulqualira536114 күн бұрын
Would you have come here if you were still a Minister? I smell activism driven by frustration (that renders followers as mere objects)
@user-kg1kb4rz9u15 күн бұрын
Mtambo you were working with this failing government so how can we trust you ....u r part of the failers u were quite becouse you had much benefits for your self .......try to have good strategy to convince us....don't be against the government just because u r out pliz mudakanika bwana mtambo
This guy thinks Malawians are stupid that he can play with us anyhow, people trusted this man so much mpaka kumakagona panseu iye mkuthawa kukalowa ndale ,
@HfamilyMw16 күн бұрын
Mbuzii iyi bola born kalindo
@SungananiBalaka-iw7kw14 күн бұрын
Timothy panyipako
@YassinHayatu16 күн бұрын
APM my vote
@bostonkhonje76937 күн бұрын
One of the most iconic nonsense to come out of Malawi
@afiyawilly3077 күн бұрын
Do your part but don't involve us again bro. We have opened our eyes sitiri mmene mukuganiziramo tatopa ndikukumenyerani nkhondo ndi banja anuwo
@tobiousmtenje13911 күн бұрын
If you saying that you didn't want to form a party why is it that upon fulfilling the mission of removing DPP in government why did you accept the ministrial position being an activist?
@user-rx4re9jv9i12 күн бұрын
The Problem I've seen here in Malawi our Country is that, we are just looking forward for our only own Benefits and we don't know the difference between politics and Leadership.
Timothy opusa iwe a Malawi akuvutika chifukwa cha munthu obwera ngati iwe
@isaackaluwa580416 күн бұрын
Apm my vote .... bolaso born kalindo....cft ur just so selfish
@user-op3nx5qt4q5 күн бұрын
My president is DC Kalido not you bwana munatichosa pabwino munatiyika pa moto ndi MCP Chakwera tonse pano tikulira lero mukubwera kuti mutisokonezeso eti brother Timothy aaaa kapumeni
@Omwale14 күн бұрын
dont expect large numbers at your demos again
@SteveMumba-gt1np12 күн бұрын
Apa ukuyankha chinzungu koma pamademo chichewa galu iwe
@saaddhumairah413 күн бұрын
Mbalame ya munthu tiye uko
@hamissimdoka966514 күн бұрын
Mapwala ako iwe ,uzazabwele ku South Africa watha galu
@user-my6sr7dq3k12 күн бұрын
Please please please Malawians do not listen to that one please I beg please have you forgotten already? Let him do other things and not mislead Malawians I repeat please
Mtambo shatup your mouth, Malawi now is on fire burning because of you. Mukuti vichi imwe Nobody is trusting you anymore. Munatha inu. Dpp my vote.
@user-ie5pc4ox8i10 күн бұрын
Bola ndifere kalindo not galu iwe
@BlessingsKachapa8 күн бұрын
Chisilu chamwana chimenecho chikagwer
@user-hq2hw7yc1u15 күн бұрын
Akhulupirira ndani awa aaaaaa
@MasiletiBilliat14 күн бұрын
First robot in Malawi
@user-uz6tr2db6g7 күн бұрын
Ntambo u r nothing ,u cheated people,u gave people hope while you are a helpless person where were you all this time stop saying such nonsense
@RuthChikanga16 күн бұрын
Iiii koma awaaa
@BUCHi26514 күн бұрын
uyu ndi kape kwambirir
@CRMTV-pw9jt14 күн бұрын
Anthu aku mpotoso ndinu ogunataso bwanji
@JamesChigaru-fg7tc4 күн бұрын
Zanzii
@AbuMussah-wi7gb16 күн бұрын
Iwe ndi mbava yene yene .mwatulukiranji ku mcp 😂you very sheet man you can see now malawi is very poor. Problem is you
@FanizoMatias-nh8gs8 күн бұрын
Kma this guy ndi m"malawi
@eliaskbanda82157 күн бұрын
Koma zilizose kumangoti God God mmmmmmhuuu, which God can bless someone Ndi phatso zotere?
@Wisdomjames95Mughogho12 күн бұрын
Aaaa pita uko wee
@PhillipAcquaron15 күн бұрын
Nthawi yomwe munali minister simunabwere buaj kumati muli nd press briefing lero zinavuta mwati ndli mbali ya Malawi amalawi ake ati opusawo omwe angamakuvere bro ulibe tiyiming kuwona maso ankhono kudekha ukanakhara wanzeru dzikoli mene lawonongekeramu ukanakhara modZi oliwombora ona azako ana achina faye atenge dziko Kamba ka nzeru
@Littlefair714 күн бұрын
Mistake yoyamba aMtambo munaovomera udindo wandale, mukanakana udindo uja panopa kungoyitanitsa press conference amalawi akanakhala ndi chidwi kumvetsera. Press briefing yanu cholinga chake chikanakhala kuzapepesa kwa amalawi zikanaonetsa kudzichepetsa kwanu, Julius Malema atachotsedwa mu ANC a anabwera ndi kupepesa poyera, panopa ali support kuposa kale. Apapatu legacy yanu man siyabwino.
@thomasky20849 күн бұрын
How can he start speaking after he has been laid off from the government Ministerial position and he has already endorsed AFORD? It's clear that everything he does is personal
@RashidKusum4 күн бұрын
Timotyhe ndiwe kape usaziyese doro ase
@samuelmayenda44645 күн бұрын
Odi ndisachimwe ine
@umalimaganga14 күн бұрын
JESUS IS COMING SOON
@user-vu5gy8wf8y13 күн бұрын
Nonsense... We've gone over 3 solid years since Malawi started suffering from this diseasters some caused by himself. All this time anali kuti.. And by the way, you want to work with Malawians on what matter? There was a time we needed you but you were nowhere to be found, so you need us now?Why coming this time... You can say whatever fallacy you feel is sensible to you, koma sudzawapusitsaso a Malawi... umusake omupusitsa... Malawi became clever and informed.
@AlexKazembe-qn5wk13 күн бұрын
Dyera dilimene lakura akuwa sizothadiza izii
@Felix-os3oq12 күн бұрын
Aleke Banda. Watchers kumwezi. Only your ancestors in heaven will listen to you. Shauri yako! Not this time bro! Nix.
@happykumbikano289710 күн бұрын
One useless creation
@user-op3nx5qt4q5 күн бұрын
Timothy iwe usandiyakhulise pabali pano ndinayithawa malawi kaba ka iwe ndili ku Mozambique ine unatiyika pa moto iwe MCP itakuyika pa mpando kwinaku ife tikumvutika chonde chonde bwelera kumene unali ife 2025 tikupita kwa a Dad Peter 🌽🌽🌽🌽💙💙💙💙💦
@EliasKodo-jf3mn14 күн бұрын
😮
@user-dj1zs3eo4f16 күн бұрын
Good but Truth, beautiful, remember Malawi are down everything God see, no more mcp please please please time to change Shure
@ThokozireSaikonda2 күн бұрын
Koma apa pavuta popanda comment yoyamikila kkkk Malawi wathu
@mishecksipolo715315 күн бұрын
He has been so selfish of late,bon kalindo took over for life
@user-rg5re6gh7e14 күн бұрын
Dpp my vote that devil is starving the Malawians it was much better in 2019 when peter munthalika analipampando
@HarrisonMwanga-xy4sc16 күн бұрын
Ku Malawi ufulu ochita zithu ulipo uyu osachita,matha,pa zomwe anachita uyu,koma apite pa khope za amalawi azikawaudza chani uyu,2025 tiona, zithu ngati satibulidwa,uyu,tiona.
@WysonMpatama-cv1mc4 күн бұрын
Atambo pano palibe zomukulupilira
@EmmanuelKapichi15 күн бұрын
Dyera a mtambo inu. Kalindo yemweyo basi only one standing till now