Utumiki wa a Twaibu - kufotokoza za IMFA YA OYIMBA M'malawi...

  Рет қаралды 50,275

Living for Christ - Malawi

Living for Christ - Malawi

9 ай бұрын

Mverani kufotokoza kwa a Twaibu pa imfa ya oyimba nyimbo m'Malawi...

Пікірлер: 67
@princedetbozsmallboy1749
@princedetbozsmallboy1749 9 ай бұрын
100% agree, ndimakangana ndi ena pa imfa ya martin nkhana, ndimanena zimenezi kuti anyamata akwathu atha chifukwa chofuna kutchuka, Iiiiiiiiiii Ndinayipalamula kwa ena Amalawi, lero ndi izi apululukabe kukonda kutchuka. thank you brother Twaibu. Zimene akuyimba zaziiiiiiii
@user-up5wp2hp3f
@user-up5wp2hp3f 2 ай бұрын
Liwu la ofuula mchipululu kuyesesa mtumiki kulira achinyamata km ayi ndithu vuto kukana kutchipa,ngati kut kugahenako tizikanjoyaso ngat tikuchitiramu.God have mercy
@RyleChole
@RyleChole 18 күн бұрын
Kuchita chilugamo ndidongosolo la Mulungu m'bale
@user-en8bk1hm7z
@user-en8bk1hm7z 9 ай бұрын
Mr Twaibu maso auzimu mulungu apirize zivumbuluso zake pa inu. Ambuye akudalitseni
@PetroKachingwe-jf7dh
@PetroKachingwe-jf7dh 9 ай бұрын
Amen mtumiki Twaibu Yehova Mulungu wamphavu zonse apitilize kutisamalira Amen
@melaku6264
@melaku6264 9 ай бұрын
Mr twaibu mulungu apitilize kukudalitsani ndikukusungilani moyo wautali mukutitsegula maso amen
@binalidjeyshabahzombamalawi
@binalidjeyshabahzombamalawi 9 ай бұрын
Zikomo kwambiri shek twaibu ndipo mwafotokoza modekha komanso momveka bwino Mulungu aonjezere mpweya womwe mumagwilisa ntchito polondoloza anthu muchifuniro chake
@user-xh4bu5he9r
@user-xh4bu5he9r 9 ай бұрын
From Zambia,pitirizani osaleka mpaka kumapeto
@user-xh4bu5he9r
@user-xh4bu5he9r 9 ай бұрын
Keep on posting more plz, we are being blessed with your massages😂. from Zambia
@albertkambuwa1329
@albertkambuwa1329 9 ай бұрын
Sakubakila bushiri koma akuti imfa iyi sikumukhudza koma naye ana peleka mwana wake
@Phinifolo-mm4hh
@Phinifolo-mm4hh 9 ай бұрын
Yes
@kennethnkosi55
@kennethnkosi55 9 ай бұрын
Eshiiii.Mulungu alowererepo
@markbanda7434
@markbanda7434 9 ай бұрын
Amen abusa zikomo potiziwisa komaso potiphuzisa my God continue to protect you
@gracemotta7818
@gracemotta7818 9 ай бұрын
Thanks now tadziwa
@successngoma
@successngoma 9 ай бұрын
Mulungu akudise kwambiri man of God
@isaackinod1256
@isaackinod1256 9 ай бұрын
Amen mtumik tiyen tithawile Kwa Ambuye 🙏
@fwasanishaba
@fwasanishaba 9 ай бұрын
Izi ndithu ndi zinthu zomwe anthu tikamamvetsera zimakhala ngati nkhambakamwa koma kuno kudziko kuli zambiri zomwe zimachitika. Zikutengera mzimu woyera ndi Yesu atalowererapo. Yesu atichitire chifundo. Zikomo chifukwa cha mau amenewo
@user-hy1kl8bj8b
@user-hy1kl8bj8b 9 ай бұрын
mulungu atilanditse kwa oyipayo
@user-cm3pl3pb9u
@user-cm3pl3pb9u 9 ай бұрын
😢😢 zovuta kwambuli. Pastor Twaibu mulungu akuyang'anileni
@dennismwenifumno994
@dennismwenifumno994 9 ай бұрын
I know you man of God and all what you say I believe because is what you went through and you was doing it before.. may God help us in this end time as you continue telling us the truth....
@user-lc3dk9jc4x
@user-lc3dk9jc4x 9 ай бұрын
Muzidalisidwa mtumiki
@KeffasSimion
@KeffasSimion 9 ай бұрын
Ameeen zoona Mr Twaibu mwasitha moyo wanga Mulungu thandizani moyo wanga
@Phinifolo-mm4hh
@Phinifolo-mm4hh 9 ай бұрын
Atwaibu mulungu nafe atikhudze
@FrankChikhadzu
@FrankChikhadzu 9 ай бұрын
Oimbaw ufit
@romanmanjolo1991
@romanmanjolo1991 9 ай бұрын
So blessed by these messages Keep doing this great work And almighty God of the most high be with you always to protect.
@user-ez1dt2zh1m
@user-ez1dt2zh1m 9 ай бұрын
Amen mwatusegula maso
@user-mc8gk4xv3f
@user-mc8gk4xv3f 9 ай бұрын
Chemwali ake ndani abale atisiyawonso?
@MemoryLanga-eb4vm
@MemoryLanga-eb4vm 9 ай бұрын
Amen powerful message
@user-oz3sj7yc9y
@user-oz3sj7yc9y 9 ай бұрын
Ambuye atitsogolele
@AlfredStingMw
@AlfredStingMw 6 ай бұрын
Help us Lord
@Crysis25
@Crysis25 5 ай бұрын
Amangotchula anthu aliphe 😂😂😂
@user-ph3zy9ox7d
@user-ph3zy9ox7d 9 ай бұрын
Mwainu ndikondwera maso anga akutsekuka muuzimu ambuye akudalitseni
@user-jw5rx9ze8k
@user-jw5rx9ze8k 9 ай бұрын
May almighty God, help us in Jesus name, Amen.
@user-mi3sf7it8n
@user-mi3sf7it8n 9 ай бұрын
Amen
@KenethJohn-bf1gz
@KenethJohn-bf1gz 8 ай бұрын
Amen
@ashikalam8616
@ashikalam8616 9 ай бұрын
Zomvesa chisoni
@shakiraameen8001
@shakiraameen8001 9 ай бұрын
May our living God continue blessing you
@Crysis25
@Crysis25 5 ай бұрын
😂😂😂so fun
@user-md5uv2cg6i
@user-md5uv2cg6i 9 ай бұрын
Asiyeni azipita vuto ndi kuchulukidwa
@user-jo6kw4ni2x
@user-jo6kw4ni2x 9 ай бұрын
@lightwelljamugondwe4213
@lightwelljamugondwe4213 9 ай бұрын
Amen 🙏
@maclearjass8389
@maclearjass8389 9 ай бұрын
Uthenga wa mphamvu tikasowa chowilingula ambuye akudalitseni bale
@user-ib6wr7pw6n
@user-ib6wr7pw6n 9 ай бұрын
God have mercy upon us😢😢😢😢
@SurprisedKomodoDragon-jb5yb
@SurprisedKomodoDragon-jb5yb 6 ай бұрын
Ndinthu munthu samavetsa anena kuti malo amene amaveka sound mulungu samakondwera nawo
@alicechinyama4155
@alicechinyama4155 9 ай бұрын
Atsogo,anthu akungogwa ENA kufa kumene tinene kuti ndi mipweya yoyipa yomwe yatumizidwa kapena ma side effects a vivid vaccines?
@user-zh2jq8tu1w
@user-zh2jq8tu1w 8 ай бұрын
Powerful
@KinziwindassoniKinzi
@KinziwindassoniKinzi 9 ай бұрын
Apa ndiye mwakamba mwa tchutchu .....wakumva wamva osamva adzakhalabe osamva .sitikukana tonse tidzafa koma izi zokha zawonjeza ....satanic is too much
@EmmanuelBatumeyo-pn7bc
@EmmanuelBatumeyo-pn7bc 9 ай бұрын
Mulungu wamoyo atimenyere nkhondo ndikutitsogolera
@AlfredStingMw
@AlfredStingMw 6 ай бұрын
Mulungu atithandize
@FostinaPhiri-yb7bb
@FostinaPhiri-yb7bb 9 ай бұрын
Zoonadi mulungu atithandizile.
@DanielKaliati
@DanielKaliati 9 ай бұрын
Eeee end time we need to repent
@jorohbee8750
@jorohbee8750 9 ай бұрын
Mulungu azikiludalitsa ndikukusamaliran maka potipasira zobisikadzi
@YusufuMaundala-
@YusufuMaundala- 8 ай бұрын
Chisilamu ndi chikatolika chidapanga ubale kod nanga tingatsatire bwanji njira yolondola kapempheredwe, komanso mavuto akubwerawo kuchojera kwa satana tizazemba bwanji kuti chakudyacho tisadye?
@moseschiphaliwari3598
@moseschiphaliwari3598 9 ай бұрын
Cent
@Phinifolo-mm4hh
@Phinifolo-mm4hh 9 ай бұрын
Zovuta
@WanangwaShammah
@WanangwaShammah 7 ай бұрын
Ndiliko ndi funso koma kodi kulibe oimba onse omwe akutchuka amapita kwa Satana? Mufotokoze bwino chifukwa tikhodza kumachita mantha kumaimba....komano Ambuye anatipatsa utumiki enafe oimba kuti tutembenuzire anthu kwa Mulungu...tutani nanga kuti tikhoze,?
@user-sz2lv3xm9q
@user-sz2lv3xm9q 9 ай бұрын
Koma akumalowa bwanji illuminat poti ndi ya anthu aku america
@malumbonyirenda2486
@malumbonyirenda2486 9 ай бұрын
Mmmmm nanu
@user-pe7pd8bg7j
@user-pe7pd8bg7j 9 ай бұрын
Thank you 🙏
@enelessdimba8122
@enelessdimba8122 9 ай бұрын
😢😢😢😢😢
@tasiyanakasalu6228
@tasiyanakasalu6228 9 ай бұрын
Mr twaibu mulungu azikudalitsan
@tasiyanakasalu6228
@tasiyanakasalu6228 9 ай бұрын
Mumakwana
@mozykavalo7352
@mozykavalo7352 9 ай бұрын
Ine ndamvela audio bwino bwino koma pali pomwe mwaonesa kuti mubakila bushiri and bushiri si munthu oti mkumu bakila he is the one who is giving money to young artist i have all the evidence he is the devil himsef
@livingforchrist-malawi9476
@livingforchrist-malawi9476 9 ай бұрын
Zikomo chifukwa cha comment yanu. Mu audio imeneyi, mfundo ya a Twaibu ndiyakuti mapangano omwe oyimba akumalowamo okha kudzera m'magulu osiyanasiyana, ndi amene akupangitsa oyimbawo kukodwa mu zinthu za satana zomwe pamapeto pake akutaya nazo miyoyo. Mukamvera bwinobwino mupezanso kuti a Twaibu akunena kuti munthu yemwe mukuti akumubakilayo osati ndiwabwino ayi; iyeyo ali kale mu mapangano otumikira satana. Mwachidule, a Twaibu akuti: chomwe chikupititsa oyimba kumanda ndi mapangano a zomwe oyimbawo amalowamo, osati kwenikweni munthu yemwe akutchulidwayo.
@user-fg4dp9zc7h
@user-fg4dp9zc7h 9 ай бұрын
Gud explanation
@stevenfrancism3638
@stevenfrancism3638 9 ай бұрын
Amen
A Michael Usi Inu Si A UTM - Lyton Mangochi
23:13
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 13 М.
MANGANYA VS AKWENI - KWAPHULIKASO INA KU UTM
13:37
Makosana
Рет қаралды 3,2 М.
БАБУШКИН КОМПОТ В СОЛО
00:23
⚡️КАН АНДРЕЙ⚡️
Рет қаралды 16 МЛН
Looks realistic #tiktok
00:22
Анастасия Тарасова
Рет қаралды 106 МЛН
DAD LEFT HIS OLD SOCKS ON THE COUCH…😱😂
00:24
JULI_PROETO
Рет қаралды 16 МЛН
KU CHIKANGAWA NDIYE KWACHEMA UKU / ZINTHU ZAKE ZOVUTA🙌🙌
17:19
CRUISE 5   ELIYA NZERU WILLIAM
1:20:13
Joab Frank Chakhaza
Рет қаралды 384 М.
zinaukamva , N'sing'anga agwira ntchito ndi Apolisi
57:13
Blessings Cheleuka
Рет қаралды 45 М.
Utumiki wa a Twaibu - kufotokoza za kuopsya kwa malonda ogula ndalama zakale za siliva
27:03
UMBONI wa a Twaibu - ZA SATANA SI ZAULERE
1:06:55
Living for Christ - Malawi
Рет қаралды 13 М.
Utumiki wa a Twaibu - kufotokoza za chikhristu cha mphamvu
37:16
Living for Christ - Malawi
Рет қаралды 4,7 М.
БАБУШКИН КОМПОТ В СОЛО
00:23
⚡️КАН АНДРЕЙ⚡️
Рет қаралды 16 МЛН