Mverani kufotokoza kwa a Twaibu pa imfa ya oyimba nyimbo m'Malawi...
Пікірлер: 67
@princedetbozsmallboy17499 ай бұрын
100% agree, ndimakangana ndi ena pa imfa ya martin nkhana, ndimanena zimenezi kuti anyamata akwathu atha chifukwa chofuna kutchuka, Iiiiiiiiiii Ndinayipalamula kwa ena Amalawi, lero ndi izi apululukabe kukonda kutchuka. thank you brother Twaibu. Zimene akuyimba zaziiiiiiii
@user-up5wp2hp3f2 ай бұрын
Liwu la ofuula mchipululu kuyesesa mtumiki kulira achinyamata km ayi ndithu vuto kukana kutchipa,ngati kut kugahenako tizikanjoyaso ngat tikuchitiramu.God have mercy
@RyleChole18 күн бұрын
Kuchita chilugamo ndidongosolo la Mulungu m'bale
@user-en8bk1hm7z9 ай бұрын
Mr Twaibu maso auzimu mulungu apirize zivumbuluso zake pa inu. Ambuye akudalitseni
Keep on posting more plz, we are being blessed with your massages😂. from Zambia
@albertkambuwa13299 ай бұрын
Sakubakila bushiri koma akuti imfa iyi sikumukhudza koma naye ana peleka mwana wake
@Phinifolo-mm4hh9 ай бұрын
Yes
@kennethnkosi559 ай бұрын
Eshiiii.Mulungu alowererepo
@markbanda74349 ай бұрын
Amen abusa zikomo potiziwisa komaso potiphuzisa my God continue to protect you
@gracemotta78189 ай бұрын
Thanks now tadziwa
@successngoma9 ай бұрын
Mulungu akudise kwambiri man of God
@isaackinod12569 ай бұрын
Amen mtumik tiyen tithawile Kwa Ambuye 🙏
@fwasanishaba9 ай бұрын
Izi ndithu ndi zinthu zomwe anthu tikamamvetsera zimakhala ngati nkhambakamwa koma kuno kudziko kuli zambiri zomwe zimachitika. Zikutengera mzimu woyera ndi Yesu atalowererapo. Yesu atichitire chifundo. Zikomo chifukwa cha mau amenewo
@user-hy1kl8bj8b9 ай бұрын
mulungu atilanditse kwa oyipayo
@user-cm3pl3pb9u9 ай бұрын
😢😢 zovuta kwambuli. Pastor Twaibu mulungu akuyang'anileni
@dennismwenifumno9949 ай бұрын
I know you man of God and all what you say I believe because is what you went through and you was doing it before.. may God help us in this end time as you continue telling us the truth....
Atsogo,anthu akungogwa ENA kufa kumene tinene kuti ndi mipweya yoyipa yomwe yatumizidwa kapena ma side effects a vivid vaccines?
@user-zh2jq8tu1w8 ай бұрын
Powerful
@KinziwindassoniKinzi9 ай бұрын
Apa ndiye mwakamba mwa tchutchu .....wakumva wamva osamva adzakhalabe osamva .sitikukana tonse tidzafa koma izi zokha zawonjeza ....satanic is too much
Mulungu azikiludalitsa ndikukusamaliran maka potipasira zobisikadzi
@YusufuMaundala-8 ай бұрын
Chisilamu ndi chikatolika chidapanga ubale kod nanga tingatsatire bwanji njira yolondola kapempheredwe, komanso mavuto akubwerawo kuchojera kwa satana tizazemba bwanji kuti chakudyacho tisadye?
@moseschiphaliwari35989 ай бұрын
Cent
@Phinifolo-mm4hh9 ай бұрын
Zovuta
@WanangwaShammah7 ай бұрын
Ndiliko ndi funso koma kodi kulibe oimba onse omwe akutchuka amapita kwa Satana? Mufotokoze bwino chifukwa tikhodza kumachita mantha kumaimba....komano Ambuye anatipatsa utumiki enafe oimba kuti tutembenuzire anthu kwa Mulungu...tutani nanga kuti tikhoze,?
@user-sz2lv3xm9q9 ай бұрын
Koma akumalowa bwanji illuminat poti ndi ya anthu aku america
@malumbonyirenda24869 ай бұрын
Mmmmm nanu
@user-pe7pd8bg7j9 ай бұрын
Thank you 🙏
@enelessdimba81229 ай бұрын
😢😢😢😢😢
@tasiyanakasalu62289 ай бұрын
Mr twaibu mulungu azikudalitsan
@tasiyanakasalu62289 ай бұрын
Mumakwana
@mozykavalo73529 ай бұрын
Ine ndamvela audio bwino bwino koma pali pomwe mwaonesa kuti mubakila bushiri and bushiri si munthu oti mkumu bakila he is the one who is giving money to young artist i have all the evidence he is the devil himsef
@livingforchrist-malawi94769 ай бұрын
Zikomo chifukwa cha comment yanu. Mu audio imeneyi, mfundo ya a Twaibu ndiyakuti mapangano omwe oyimba akumalowamo okha kudzera m'magulu osiyanasiyana, ndi amene akupangitsa oyimbawo kukodwa mu zinthu za satana zomwe pamapeto pake akutaya nazo miyoyo. Mukamvera bwinobwino mupezanso kuti a Twaibu akunena kuti munthu yemwe mukuti akumubakilayo osati ndiwabwino ayi; iyeyo ali kale mu mapangano otumikira satana. Mwachidule, a Twaibu akuti: chomwe chikupititsa oyimba kumanda ndi mapangano a zomwe oyimbawo amalowamo, osati kwenikweni munthu yemwe akutchulidwayo.