More 🔥 kweni ndimakunyadirani simusekelera zopepera ,aweee
@BentryChavinda2 ай бұрын
Koma a VP ,you cannot settle the dust within UTM on public meetings but through dialogue.
@Clement-vh5pf2 ай бұрын
The name of SKC is used now yet the same government did not honour him while alive and all his manifesto were not implemented.VP should ask himself why Chakwera was not listening to Chilima for 4 years yet had powerful suggestions that would develop Malawi.
@Okalekale2 ай бұрын
Corruption implication ija bwanji Chilima uja?,analidi serious zotukula dziko?.Andale ndi ma crooks,ndi mwa mwayi kuti anthu apeze munthu ngati Bingu. Amai Kaliati ndi ena azipani zinali mu tonse ndi anthu oyipa,akufuna ma political scores kuchokela pangozi ija kumati Chakwera anapha anthu aja (ngakhake akudziwa kuti alibe umboni kafukufuku sanachitike)ndipo Michael Usi is a sellout popitiliza kugwira ntchito m'boma.Patricia Kaliati ndi opportunist opanda manyazi komanso opanda chisoni pofuna kutenga uPresident wa UTM.In other words she's happy that Chilima died and Michael Usi remains in govt. with the alleged killers whom the electorate isn't happy with,so that she catapult herself to the presidency of UTM Andale ndi mbanda,hypocrites,Poona kuti anthu aja afa anaonelatu gap,gap yake ndi yoti,aMalawi akhuluilira kuti Chakwera or MCP yapha anthu aja chifukwa cha history ya Kamuzu,sinanga aMalawi ambiri school alibe, ndiye Chihana ndi aKaliatiwa akugwiritsa ntchito infa ya anthu aja kupezela support kuti mwina ndi m'gwirizano wawo or paokha paokha angadzawine.Ndiye amaiwa akumukankha VP mudzina la u sellout ndicholinga chofuna uPresident wa UTM,satan wa m'mai. Kutuluka m'boma sichifukwa cha imfa ya a Chilima ayi,anthuwa amakanika kuba m'boma chifukwa kunasintha,taonani Chilima weni weniyo anapezeka ndi mlandu waziphuphu.VP Usi ndi munthu was serious pa ntchito komanso okonda dziko lake,sali m'boma kukayang'ana mitaji yokuba koma kuyesa kusintha miyoyo ya aMalawi ndichifukwa sanachoke kukapanga ndale zombwambwana pamene aMalawi akudikila zitukuko ku madera awo.M'mayi uyu ndikale anayamba kusakasaka uPresident ndichifukwa amasinthasintha zipani kwambiri.Chihana ndi m'mai uyu ndi andale oyipa pa Malawi sangatithandize or pang'ono awonetselatu pano,koma ndale oyipa kwambiri. Mbuli komanso mfiti za a ndale zigwiritsa ntchito imfa ya anthu aja m'ma campaign kuti m'malawinso osazindikila adzawavotele.Malawi ak 13:37 upita kuphompho.
@nishanchiwaya45612 ай бұрын
Amanganya ndiwe chitsiru kwambiri
@zelliachamboto57442 ай бұрын
Koma Malawi sazatheka , zi anthu zamitu ngat nguli pasipasi zili zoona bwana 😂😂
Pobela makobidi pa manganya wawona kuti alowele popatsa anthu ngongole kuti naye adzichotsapo Kod amalawi munakhala bwanji inu kumangopusitsidwa, Ndalamazo osakapeleka kuma company bwanji akutsitsileni katundu
@AgnesLeonard-e2j2 ай бұрын
More 🔥kweni,susekelera zopusa,awe kaliyati
@CatherineDesire2 ай бұрын
Adzimai tsakusangalala povina sangavine ndi misozi mmaso yaku chikangawa,ine koma manganya tidzikutchula 🤸🤸🤸🤸
@andrewmazunda38462 ай бұрын
Rest well SKC. Your legacy will live forever 🙏
@PaulPoyah2 ай бұрын
Manganya wabalalika
@ChimwemweBottomani-hc5ju2 ай бұрын
Becareful usi u will regret on day ....and you need to think before you do things...Ahlomwe respect always
@0wenNkhambule2 ай бұрын
Mai number one kaliyati❤
@emmaculatemenzeiwa2 ай бұрын
Mangamanya's deliberate move to destroy the party
@emmammatsa12842 ай бұрын
Nanga tikawaona wodya zake alibe mlandu ndi abalenso amenewo?
@fredgabrielnyangulu2 ай бұрын
Hule uyu Manganya wagonana ndi ma Sikono mpaka mkazi uja banja lake linazasokonekera chifukwa cha ameneyi ndi makumbukiranso uyu Gradys ankamufuna mpaka zinathera ma penalty adamukana Usi simunthu ai
@StanleyChinsewu2 ай бұрын
Akweni ndi VP onse asiye ndale onse akubisala kumbuyo kwa chilima
@pacharokoloviko16942 ай бұрын
Ingoyambisani chipani chanu bwana mupange mgwirizano ndi MCP cz palibe supporter wa UTM weniweni akukondwa nawo mgwirizano ndi MCP
Manganya you went to school komano ulibe mzeru 😅 zamanyazi😢
@chesterphiri75232 ай бұрын
Amufunse Mkaka with that arrogance, what has happened now??
@IyshaBakali2 ай бұрын
Usi kuyesetsa kuthetsa chipani cha utm Koma team chikangawa mmmmmmm mupala
@MphatsoIshmaeladam2 ай бұрын
Ife tidaionera patali usi ndi wa MCP ndipo UTM mukachedwa kuchosa usi muononga chipani
@MaxWell-d7o2 ай бұрын
Zandalezi zikundidwalitsa mitu😮😮
@Lee-lee-w1r2 ай бұрын
Koma ndipo inu!! Andalewa ndizitsilu za anthu kwabasi. Mmalo moti azingokambilana amafuna kutipweteketsa mutu ndi za ziii
@dondamissonchdziwe39582 ай бұрын
Amalawi ena ndinu dzitsiru usavage kusaphunzira nkugona komwe mumadana nchiru ngamo, Ndipo Utsi ndichitsiru chamunthu Yudasi Mai kaliyati Ndi wa mzeru Ndi amene akumva kuwawa pophedwa Chilima pamodzi Ndi mamembala ena Chifukwa mzimai Ndi amene ama bereka manganya akulondola kudya Kwa Nkhumba imzakeyo Chakwerayo Kuma lawi kwanukooooo
Manganya lipoti la imfa ya skc likamazatuluka uzakhala pa nambala 2, ka predator iwe
@masterchitabwino8982 ай бұрын
Magalasi akula gulani asaizi yanu a Usi kkkk. Ngati president mukanaitana anzanuwo osati kuima pamenepo kuuza dziko
@JosephEmmanuel-nv5td2 ай бұрын
Manganya ndi kape kwabasi iyaa asatinyasepo
@billymhoni95272 ай бұрын
Ku utm kulibe mpungwepungwe as you say koma usi yoo nde si wa utm
@spargomw2 ай бұрын
Manganya ndiwa ma drama😂😂😂 u vice wangogweramo
@EffordKapichi2 ай бұрын
Manganya is a truelly dramatist he has just found himself in vp presidency flookly .
@EffordKapichi2 ай бұрын
Vera and manganya are not devoted to utm. They are after money .let them vacate .
@AlgentChilanga2 ай бұрын
Manganya ndi mthira kuwiri yudas sikalioti adampereka mzake chilima lero akupereka salute kwa madam Mary chilima fokofu usi tinakuzindikira kale kuti ndiwe wa MCP khala ndi Dr Chikangawa wakoyo .akweni kaliati samasekerera zopusa uyo ndiye mwadyiwanatu ngati sukuziwa uyo ndimwamuna mzako ndala anaymaba kalekale makona ose andale akuwaziwa .kape iwe usi magalasi nawoso si asayizi ako
@VictoriaKumwenda-k6o2 ай бұрын
Kaliyati akuwonga chipani msabakile nthawi yimene abingu atamwalila kaliyati anapangaso chomozi mozi ndipo mwakaliyati mlibe usogoleli yake ndi nsanje basi koma nanga malamulo achipani akuti chani kaliyati uli ndi vuto
@SherifaG.Mlelemba2 ай бұрын
Koma kumenekoo!!!!🙇🙇🙇
@FastCement-c7n2 ай бұрын
Malawi sazakonzekaso
@MuyaoComedies2 ай бұрын
I'm following Salam alaikum
@InnocentAssan-st3hb2 ай бұрын
Waleko m'musalamu
@ganizanimsowoya98432 ай бұрын
Ndale zaku Malawi 🇲🇼 zosekesa
@shayrafernandeslatif95562 ай бұрын
Akweni for President ❤❤❤a Micheal Usi sanawoneste khalidwe panthawi ya zabvuta ya chillima,mau awo oti vice amaeyenda ndi president,nanga SCK amaeyenda ndi a president???he was happy kutdziwa kuti atwnga mpando
@JimmyIsaac-xd4ef2 ай бұрын
Manganya ndi wa MCP asakupusitseni
@PortiaMhlambi-y4g2 ай бұрын
Zoona akweni osaopa osafooka,
@EmmanuelMpalagule2 ай бұрын
Manganyayi mzeru mulibe guys, coz these are sensitive issues that needs contact dialoque not in public life this, he was supposed to called Mrs kaliyat n others to sit down n discuss
@shapilchaponda99062 ай бұрын
I feel like he didn't show leadership after the accident. If he did , zonsezi kulibe .
@joyahmedjoma46152 ай бұрын
Ndiye unapanga zoti achilima azipita iwe unkhalepo pa pando gulu iwe kwambili
@0wenNkhambule2 ай бұрын
Usi ndi wa MCP
@zionekansinde28172 ай бұрын
How can a whole VP settle issues like these on a public podium? Pls guys be matured and act as matured people. How then can we trust you. Be matured!!!
@MaggieToneki2 ай бұрын
Ine makolo anga akugona ndinjala izizi za Anthu okhuta izi forseck zitafunanani
@ConlardNkhoma2 ай бұрын
Koma akweni pakamwa pawo popasula amafuna u VP Kaliati
@FWhite-w3l2 ай бұрын
Ulemu upereke lero kwa madam chilima cause walanda udindo Mmmm yudasi
@Extratremendouszeus2 ай бұрын
Palibe a UTM apa Propaganda UTM yeni yeni ili ndi Kaliati
@fredgabrielnyangulu2 ай бұрын
This is true Akweni ndie magazi a UTM
@Extratremendouszeus2 ай бұрын
@@fredgabrielnyangulu very good
@KondwaniLungu-x5l2 ай бұрын
Koma kwen kwa ine sandiwaza kwenkwen, ndi mmai owopsya kwambili sayankhula bwino some times, ndi mai ovuta kumfikila moti ndimakhulupilira kt even atolankhani ena amantha kwambili anasiya kumufusa mafuso kuli kuopa ishiii ai Mai asamakhale choncho chifukwa amapeleka picture yoyipa kuti ozindikila ndie kuposa onse and chilima anaziwa kuti apa si kuti tiendele 50 50 kuti vice akhale nkazi mayazi anaziwa kuti umu mwa kaliati muli moto wa lawilawi
Ati akakumana kuti komwe azikafusana mafuso ndi bwanawo😅
@KondwaniLungu-x5l2 ай бұрын
Ausi inuso dyela too much, aaah iwe usi ndi galu kwabasi ukunama MCP si abale amenewa asaukisa ziko amenewa moti ukumenya kampeni ya MCP aaah iwe enafe si ana kusekelera zofooila zakozo.
@Yungjoe7862 ай бұрын
This guy 💯% belongs to MCP n I guess even those supporters they're from the same crocodile party angobvala ma uniforms a UTM shame
@0wenNkhambule2 ай бұрын
Boza usi ndi wa MCP Galu usi❤
@loveshabani88342 ай бұрын
Manganya adali NDI cholimgadi chothetsa UTM koma akunama ameneyo atha ndi iyeyo
@MaxonKambazithe2 ай бұрын
Chitsiru iweyo tulukamo amene sia UTM uyu ndiye ulikuti iweyo ndiwe wa MCP uli ku chikangawa
@MARKODSOLOMON2 ай бұрын
If u really deserve to be a leader why not conduct top official meeting than coming on the platform and intimidating your own team.
@dondamissonchdziwe39582 ай бұрын
Nkhani ikuwawa Ndi yoti Amcp apha Chilima,koma Wanthu afuna aziwe chilungamo Ndiye uku lepheresa ndiwe Chitsiruu manganya mbuzi ya Munthu,chitsiru Ndi MCP yakoyo Ndi Galu mzako chakwerayo nkhope ngati kuphazi Kwa Njobvu
Usi sakunama apa SKC anali boma pamodzi ndi Usi yemweyo ndipo Usiyo anati bwato satsitsilana pakati panyanja akatathauza chiyani apa
@Itemsworld2 ай бұрын
He can't fire the secretary of utm, he don't know where he belong and who is with him
@ConlardNkhoma2 ай бұрын
Chipani Cha MCP ngati chimapezeka pa second pama general election nanga pano chili m'boma Ife a UTM tisamale 50+1 patokha without late SKC chathu palibe
Uyu manganya asapusise anthu ndi wamcp kuchokera kale uyu
@PaulPoyah2 ай бұрын
Manganya ndi galu kwabas ...fisi ndi chakwera wakoyo
@meditationmusic2932 ай бұрын
A manganya sangazikwanise zomwe akupangazi
@RuthMandawala2 ай бұрын
Likupitakwaod😢
@Musa1828-l5d2 ай бұрын
Manganya pamtumbo pako ndi Chakwera wakoyo munapha Chilima kuthako kwako ndithu siwe wa UTM mbolo yako wakhala ukuchinda ma Sikono mpaka banja lawo linatha galu iwe kunyinikwako
@williamhara18662 ай бұрын
Moto ukazima pamatsala utsi. If you know, you know!!
@JamesChaponda-em7op2 ай бұрын
Bwana vp fire the secretary General please
@YasinMusa-ym8lp2 ай бұрын
Unapa chilima kufuna udindo
@ForestElf-z1h2 ай бұрын
Please choose one position and follow hart ❤ which you are behaviors thanks,,,,
@bisweckchimphamba84972 ай бұрын
Yudasi wachabe chabe uyu,drama yaku Tikuferanji yeni yeni
@KondwaniLungu-x5l2 ай бұрын
Ndie guys utm-yi izatha ngati makatani anthu ake si achina kaliati-wa ndiwa ntima kwambili ngati si mai ndale zinamulowa ndi mmafupa momwe kwa ine kulibe chilimbikiso koma za ausi izi ndimachita kuonekelatu kuti ndi wa MCP
Manganya ndi amene akubweletsa zosakhala bwino chifukwa iyeyo ali.ndi chipani chake ndiye akufuna chani ku UTM moti iyeyo anachoka kale kale lero ali.ku MCP