A Michael Usi Inu Si A UTM - Lyton Mangochi

  Рет қаралды 34,847

Nyasa VoiceBox

Nyasa VoiceBox

Күн бұрын

Пікірлер: 268
@user-un6qv6sj3h
@user-un6qv6sj3h Ай бұрын
Iwe mangochi umandibowa pazambiri koma leroli wakamba chilungamo ❤❤ the spirit
@tinigo-k8e
@tinigo-k8e Ай бұрын
😂😂😂
@shadreckphiri1799
@shadreckphiri1799 Ай бұрын
This is straight forward talk and advice
@MEGANABIGAILMNTHALI
@MEGANABIGAILMNTHALI Ай бұрын
Munthuyu nthawi zina amalankhula zoduka mutu koma lelo walankhula chilungamo ndakukonda Mr mango hi for this audio.
@mayesojameskatete
@mayesojameskatete Ай бұрын
Galu ndi gula manganya siwa utm komaso anamupeleka chilima
@peternashyo9850
@peternashyo9850 Ай бұрын
Uthenga opanda chigamba, apa ndiye chilungamo.
@user-bn8hh2wb5b
@user-bn8hh2wb5b Ай бұрын
Bwana Lyton mangochi lero mwakambako mfundo zomveka bwino ulemu wanu
@user-cy4pg1bo5o
@user-cy4pg1bo5o Ай бұрын
Apapa ndiri mbariyako or mntaniwa atanva audio yakoyi akunva kukoma mot utamatero anthu akukonda kwambiri the fact u hv say to day congrats Mr Layton big up tufuna chirungamo choncho
@alexsumani6823
@alexsumani6823 Ай бұрын
Ndipo bwana Mangochi mwang'alula ulemu wanu akulu awa eeeish atipepelesa sure
@TheresaNtodwa
@TheresaNtodwa Ай бұрын
Mr. Mangochi awuxeni abambo amenewa chifukwa ndiye akupanga. Zinthu zobowa kwabasi.kasatana kachabe chabe kauzeni kamvetsese
@DysonUmali
@DysonUmali Ай бұрын
@@TheresaNtodwa exactly
@DONNEXKhama-bk1gy
@DONNEXKhama-bk1gy Ай бұрын
Ine umandinyasa heavy kma lero Mutu wako wayamba kugwila ntchito ❤zanzeru Someone hit Like for me
@AiwaMedia-sh6vx
@AiwaMedia-sh6vx Ай бұрын
Iwe Lyton Mangochi apa wanena mfundo osati yamasewera. Ndamvera each and every sentence looking for a mistake koma mwalankhula zaufumu weniweni. I love you
@JuvenileDebwe-bv8ow
@JuvenileDebwe-bv8ow Ай бұрын
Apa pokha Usi avomereza chilungamo kuti anthu alindi maso ndipo amaona ndithu iiiii
@PollyLysonLutepo
@PollyLysonLutepo Ай бұрын
100%. Usi si wa UTM. Angofuna kusokoneza UTM yo. Tilitonse mau olawura asiye. Ngati zolankhura alibe angosiya. zamadirama ife sitikufuna. Ine ndili wakwanu. Kumwitu koku Karonga. Komam'sasiye kudziwitsa anthu choonadi, monga m'nachitira pakatipa. Tinali kuganiza kuti nanutso mwagudwa.
@SolomonMbewe
@SolomonMbewe Ай бұрын
I think you are coming back to your senses Mr Mangochi.... Keep it up.
@user-un6qv6sj3h
@user-un6qv6sj3h Ай бұрын
Ndakuombela mmanja mangochi apa pokha chilungamo chimamasula usi ndi wa MCP
@laurentbutao4084
@laurentbutao4084 Ай бұрын
Chilungamo chimawawa koma izizi ndi zoona..Malumewa SI a UTM
@user-tb6yh1kx3o
@user-tb6yh1kx3o Ай бұрын
Apa nde wang'alula zeni zeni momveka bwino dziko akulitengela chibwana
@zulubeats1071
@zulubeats1071 Ай бұрын
Bwanji osakayendera ma office a NRB ku southern, eastern and northern regions kuti anthu alandire za unzika mu nthawi yabwino?
@MEGANABIGAILMNTHALI
@MEGANABIGAILMNTHALI Ай бұрын
Akanangopanga za tikufzlanji asamasokoneze anthu
@user-bs8nk1si4e
@user-bs8nk1si4e Ай бұрын
AMangochi,apatu mwaonesa umunthu.ndipo mukukhala ngati siinu a Mangochi,koma zikomo. coonadi ncofunika
@FatimaSande-lb1hd
@FatimaSande-lb1hd Ай бұрын
Uku tu nde kuyankhula kopanda chigamba mau mau. pena nso atipeperetsa a Usi wa Aaaaa inu
@user-db3mh9wr9v
@user-db3mh9wr9v Ай бұрын
Mr Lyton Mangochi ulemu wanu mwayankhula chilungamo God bless you Mr Mangochi
@user-cv3zw9ic6d
@user-cv3zw9ic6d Ай бұрын
Lyton Mangochi apa walankhulatu ngati munthumuuzeni usi akutitenga ngati ife zitsilu hule wamunthu
@lastonmasoatenganji-bs5gf
@lastonmasoatenganji-bs5gf Ай бұрын
Madala madala tsopano, munasowatu😁💗💗
@masterchitabwino898
@masterchitabwino898 Ай бұрын
Well composed speech keep it up Mr Mangochi. Teach him a lesson
@FelexMisolo
@FelexMisolo Ай бұрын
Apa ndiye wayanbapo kumeneko zanzeru
@RitaKainga
@RitaKainga Ай бұрын
Mwayankhula chilungamo malumee,May God bless you!!! Ameneyu adzazunzika nao mzimu wa Chilima
@user-ih7li3im4s
@user-ih7li3im4s Ай бұрын
Apa wayankhulatu za nzelu even BON Kalindo ajuyamikila
@ClementbWatches
@ClementbWatches Ай бұрын
Lerotu Mr Mangochi mwakambatu mfundo zomveka bwino. Ulemu wanu manganya komwe aliko amve. Chipan chathiko Ife ayi.
@user-ck7eb7tb7v
@user-ck7eb7tb7v Ай бұрын
Ife UTM sangatigulitse .... UTM yachilima ija ilipobe ija yachina Kaliati
@user-mw8dq4is6k
@user-mw8dq4is6k Ай бұрын
Koma apapa zikumveka bwino kwabas Mangochi walankhula mwanzeru chifukwa Manganya samamukonda Chilima .
@ZebronTembo-u6p
@ZebronTembo-u6p Ай бұрын
Mqngochi your right ukunena zenizeni congratulations bro
@petertaulo8014
@petertaulo8014 Ай бұрын
Mwanena zoona Mr Mangochi. Manganya akufuna Kuba Chipani!
@Geraldmkwewu
@Geraldmkwewu Ай бұрын
Iweso ukuti musiyeni usi ndwe Galu team ya Mr chikangawa fiti agalu lnu
@InnocentnMbale-zq8pk
@InnocentnMbale-zq8pk Ай бұрын
Mangochi apa nde wandilankhulila ndithu angofusa kutisokoneza ife a UTM
@CharlesChamveka
@CharlesChamveka Ай бұрын
Ay Mr mangochi apa pokha mwayesesa kulakhula kwa nzeru
@CharlesKanuni
@CharlesKanuni Ай бұрын
Mr mangochi took his time to recharge and came back stronger 💪
@PartLupiya
@PartLupiya Ай бұрын
Lero wayankhula mwanzelutu a bro, more fire 🔥
@user-is5zi5rw8w
@user-is5zi5rw8w Ай бұрын
Today it's ur best audio mr mangoch best audio ever muuzenidi achose kachiwanda ka ma drama kkkk
@mphatsosadiki4983
@mphatsosadiki4983 Ай бұрын
Well spoken.....
@paulpaseli6310
@paulpaseli6310 Ай бұрын
Amangochi mukafuna mudye za ausi .
@DaveMakondetsa
@DaveMakondetsa Ай бұрын
mwayankhula bwino kwambili ngati zikadi wa Malawi❤❤❤❤
@CtvnMpina
@CtvnMpina Ай бұрын
Well said big man,thumb up🔥
@masterchitabwino898
@masterchitabwino898 Ай бұрын
Anali ngati Petro yemwe amamuonera Yesu patali ali pakati pa adani kumfunsa uyunso anali waiwo amvereke akunama sindikumudziwa ine ameneyo.
@LamieTiger
@LamieTiger Ай бұрын
Apo Nde wanena zoona a usi Sia UTM
@EmmanuelGasiten-fo5dr
@EmmanuelGasiten-fo5dr Ай бұрын
Bravo, wayamba kuyankhula mfundo zenizeni, zamphamvu.
@AlexKamowa-u7m
@AlexKamowa-u7m Ай бұрын
Good speaking mr Lyton mangochi
@eliffagondewe8214
@eliffagondewe8214 Ай бұрын
Well spoken 🔥🔥
@DaudKYSilindu
@DaudKYSilindu Ай бұрын
Mr Lyton excellent spoken keepitup
@asahelmachila3026
@asahelmachila3026 Ай бұрын
Long live Impi Biyeni
@user-nf3ik3ff6y
@user-nf3ik3ff6y Ай бұрын
Good Message Mr mangochi
@DicksonMacheso-lr7oy
@DicksonMacheso-lr7oy Ай бұрын
Fundo zinazo za mangochi ndi zopoila, amalawi tikuyenera kudziwa kuti tonse ndi amalawi koma zinkhulupiro ndi zotsiyana,kutsapedzaeka a Micheal usi ku candle 🕯️ light sichifukwa choti anene kuti si wa utm koma anene zifukwa zina
@tobiasshalla
@tobiasshalla Ай бұрын
Let the Vice President be please !!!
@ThokozaniBilliat-im7lf
@ThokozaniBilliat-im7lf Ай бұрын
Manganya palibe akulakwitsa and zomamena kut sanali wa UTM kapena kut si wa UTM ndikulakwa chabe.Mvuto lomwe Malawi tili nalo ndi nsanje.Chilima anamutenga chifukwa chani Micheal usi ngat sanali ofunikila?.Amene akudzimva UTM kwambiriwo bwanj Chilima sanawaike pa vice president?.Nsanje kusavomeleza phunzirani makape inu
@dunstankgombezi2911
@dunstankgombezi2911 Ай бұрын
Apa mwayankhula big. Osaka asowa poyambira.
@ewn-mc6jv
@ewn-mc6jv Ай бұрын
Amanganya ayenela kugwetsedwa mmpingo chifukwa ana phwanya limodzi la malamulo khumi. (Bodza)Ndinamva akukamba bodza mu zoyankhula zao pa zokhuzana ndi UTM. Mwanyozetsa mmpingo.
@ChimwemweKondowe-nj4lx
@ChimwemweKondowe-nj4lx Ай бұрын
For the first time I am happy with you Mr Mangochi pa zanzeru zomwe mwalankhula apa. I'm sure kuti we're expecting more from you
@HamzaMkwanda-bh8dc
@HamzaMkwanda-bh8dc Ай бұрын
Respect
@slow-kkamanga4906
@slow-kkamanga4906 Ай бұрын
very true mangochi
@user-cf9yz3ei5o
@user-cf9yz3ei5o Ай бұрын
You. have said. the truth utsi. is not for utm
@user-ds6zj9um6g
@user-ds6zj9um6g Ай бұрын
Powerful message
@BensonMoyo-pf2ci
@BensonMoyo-pf2ci Ай бұрын
Mwayakhura fundo ❤
@AchinaKellz
@AchinaKellz Ай бұрын
Apo wabaya
@VictorCustom-my1nv
@VictorCustom-my1nv Ай бұрын
Powerful advice from Mr Mangochi.
@chimwemwemorris6827
@chimwemwemorris6827 Ай бұрын
Zangongore zakezo tilibenazotchito koma asamatinamizekuti ndi wa UTM ai sitikumudziwaife
@williamsalexmbonga
@williamsalexmbonga Ай бұрын
Michael Usi the big man
@mrcool531
@mrcool531 Ай бұрын
Amangochi mwalankhula zanzeru kwambiri mu audio iyi
@GladysBanda-h2w
@GladysBanda-h2w Ай бұрын
manganya watikwana kale.Mr Mangochi mwabwera
@blessingsnyalo-rp9ko
@blessingsnyalo-rp9ko Ай бұрын
Manganya ndichisilu galu ndi mozi mwa anthu ogwesa ndege ameneyo😮😮
@AishaChipande
@AishaChipande Ай бұрын
Ndinalutuluka kale koma yapa pokha wayankhula zazelu ngati siukufunaso kupepha kwa manganyayo
@user-hx6ly3cl8m
@user-hx6ly3cl8m Ай бұрын
aLyton APO mwalankhu zoona avaice si a UTM ayi
@user-nj5vu8cd5l
@user-nj5vu8cd5l Ай бұрын
Paja amalawi pomwe munthu akupadula muwombela mumanja. But utm be careful once a party is divided into two no matter mbali yona ndi yochepa the conclusion will be a big space. Believe me utm usi and kaliyati please just sit down together and agree united and peace and friendly....utm yitha kutha mosavuta pa dziko lathu ndi into Three no matter what. Ya Papa kumwera yikhala usi utm pakati chilima UTM kupoto ndidela lovutitsisa don't relax with people from north they are chameleons... You can't trust northern region
@RabeccaMkandawire-i9j
@RabeccaMkandawire-i9j Ай бұрын
Walankhula zoona Lyton
@JonesChingaya-yf4gg
@JonesChingaya-yf4gg Ай бұрын
Kodi Usi akamayenda m'mene akuyenderamu ndie kut ntchito ya nduna ndi chani? Akungofuna kupeza credit koma akutionongeranso misomkho yathu.
@user-ck7eb7tb7v
@user-ck7eb7tb7v Ай бұрын
Mwayamkhula bwino sure
@StoneckJali
@StoneckJali Ай бұрын
Mumafuna muzidya naye ngati achipani muziyenda naye mwauponda. Musiyeni zanu agwire ntchito ya boma mufune musafune president wa UTM ndi Usi
@user-cf9yz3ei5o
@user-cf9yz3ei5o Ай бұрын
Lyton. mwalankhula zan,zelu. Kwambiri kwambjri. takuyamikila kunokuchitipa
@DysonUmali
@DysonUmali Ай бұрын
Mangochi wandigwira mtima koopsa
@GabrielMzich
@GabrielMzich Ай бұрын
Manga NDI Yudas weni weni munthu opanda manyazi opanda chifundo ngati uyu mizimu ya Chikangawa Ili pa mutu pake fiti iyi
@milliambandah1939
@milliambandah1939 Ай бұрын
Yudasi sikaliyoti Manganya siwa UTM angotaya nthawi yache pachabe munthu oipa
@SoldierWilison
@SoldierWilison Ай бұрын
Leroditu alangula zaseru
@doreenkaliati3166
@doreenkaliati3166 Ай бұрын
Nkhani iyi ya Straight forward 🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌 ulemu wanu uku kulakhura mwabnzeru manganya or tsiku limodzi lopedzeka pa mwambo oyasa ma candle yoooo or tsiku loyakhulapo zokhudza imfa ya chilimba mmmmm Ambuye akukhululukireni iwe ndi mpeni othwa konse konse iiiih Chilima Rest well tidzakulirani mpaka kale 😭😭😭😭😭😭
@user-nf3ik3ff6y
@user-nf3ik3ff6y Ай бұрын
Very good Mr Mangochi good Message ❤
@Gwedeza-oz3jv
@Gwedeza-oz3jv Ай бұрын
Zanzeru ndizochepa umu kuti mumumvele bwinobwino statement yakeyi yachoka kwa iye manganya mwini kuti awuze mtundu wa anthu kuti akazamati ndine wa mcp anthu asazazizimuke kwambili, Ndipo chakwera ali mommu this is propaganda of mcp
@user-qh5jo5qh3b
@user-qh5jo5qh3b Ай бұрын
Layton magochi lero wayesetsa utamatero mwina anthu ayamba kukukonda
@mphatsomalenga
@mphatsomalenga Ай бұрын
Anatha awa 😂😂😂😂😂😂😂😂😂 boma ili silikufuna kukhala ndi opposition ai,kusafuna kukhala ndi opposition zimasonyeza kuti ndiwe otayilira and sufunaso kudzudzulidwa.
@user-gu3sp8ci6v
@user-gu3sp8ci6v Ай бұрын
Wayankhula za nzeru koma awa itha kukhala njira yopemphera ndalama kuti awapatse kenakake akhale chete
@robertrichman9376
@robertrichman9376 Ай бұрын
Apatu Mangochi walankhula zanzeru, tikumudziwa Manganya kuti ndi betrayer wankulu ndipo ndi mthira kuwiri
@masterchitabwino898
@masterchitabwino898 Ай бұрын
Listening Keenly .....kambani ndithu
@JanetJamesMachila
@JanetJamesMachila Ай бұрын
Kumva kumakuvutani amalawi manganya si wa utm anali ndi chipani chake anapanga ngwilizano ndi chilima amalawi mwatani kodi
@giftedmshan6779
@giftedmshan6779 Ай бұрын
Ngakhale Mangochi ndiwamisala koma apa ayankhulako zanzeru
@anusahjenala1063
@anusahjenala1063 Ай бұрын
Ndende ndende ndipaseni acount yanu mukatenge sweat muike mkamwa mwalankhula zoona zeni zeni ndipo inuyo mulungu alowele pa nzeru zanu
@ibrahimdyman4356
@ibrahimdyman4356 Ай бұрын
Wayakhula ndithu za zeru
@PatrickMbenje
@PatrickMbenje Ай бұрын
Well spoken
@JamesKamtedza
@JamesKamtedza Ай бұрын
Lelo mwayakhulana zazeru Mr mangochi ndalam zathano et
@user-lu6nq9bs6w
@user-lu6nq9bs6w Ай бұрын
Nsokhano uliwonse ine nali wakut nali wakuti Inu anthu ambili anasinthika kuchoka ku umphawi kumene koma sikut ukachita bwino basi history yokha yokha pa nsokhano.
@user-jn9tz3li3v
@user-jn9tz3li3v Ай бұрын
Akulipira zingati amene akutuma? Koma wayankhula mfundo zabwino. Zikuomeka ngati MCP yikufuna kuti Usi angopanga declare kuti walowa MCP osati zakabisalira ayi. Lyton Mangochi wapeza profession yabwino nawenso, yamalipiro abwino koma a temporary.
@OsmanYassin-co9ye
@OsmanYassin-co9ye Ай бұрын
mangochi ulemu wanu
@user-wi9pe2hz7e
@user-wi9pe2hz7e Ай бұрын
Mangoch wabwelanso ukufuna akupase ndalama zina mwatitola et😂
@EllahChikwatu
@EllahChikwatu Ай бұрын
Colinga chake usi amuitane mwapadera apase ndalama kt asamu kambe
@thomasphiri7799
@thomasphiri7799 Ай бұрын
😂😂😂
@JonaZimpita
@JonaZimpita Ай бұрын
UTM inatha guzy lero uyipa uja wasanduka wabwino lyton
@KingsleySomanje
@KingsleySomanje Ай бұрын
Ndipo zoona zenizeni mzimu wa chilima uwakathe amanganya pazomwe akuchita posokoneza chipani cha UTM
@ChikondiChauma-ib9pg
@ChikondiChauma-ib9pg Ай бұрын
Akatelo mangochi ndalama zamuthera akufuna Zina kuchokera kwa manganya koma wanena pakati aise
Mafuso Oti Tidzifunse Tikamawelenga Report la ndege - NVB Original
7:27
Will A Guitar Boat Hold My Weight?
00:20
MrBeast
Рет қаралды 61 МЛН
Running With Bigger And Bigger Feastables
00:17
MrBeast
Рет қаралды 201 МЛН
Akufuna Kugulitsa Kampani Ya Salima Sugar Kwa Azungu - Bon Kalindo
3:31
MICHAEL USI WAYANKHA ZOMWE ANANENA A FELIX NJAWALA KU MZUZU.
8:04
Nkhalango Multimedia
Рет қаралды 23 М.
Report La Ndege Ndi Manyaka - Pastor G Shumba
11:53
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 13 М.
A Chakwera Opanda Anthu Mukhala Mfumu? - Pastor G Tembo
15:01
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 4,3 М.
Will A Guitar Boat Hold My Weight?
00:20
MrBeast
Рет қаралды 61 МЛН