Moyo wa munthu pali thupi ndi nzimu choncho thupi ngati likumana ndi mavuto akuyenera kulankhulapo kumene ,nkhristu ngati ali ndi njala angamve bwanji mau zikufunika zonse ziyende limodzi
@GanieAlidih-gu7no3 ай бұрын
Palibe kunyoza apa km kunenachilungamo
@andyjames20503 ай бұрын
Pali kunyoza apa ichi ndi chilungamo cheni cheni
@festonphiri2 ай бұрын
Good message fr
@rhodrickmpumila18203 ай бұрын
Ndi cadet wa DPP uyu ndikumudziwa bwino
@shayrafernandeslatif95563 ай бұрын
Very true
@wilisonbornface42823 ай бұрын
Zoona kwambiri sikuwonapo cholakwika
@FavourKadzembe-sg1yf3 ай бұрын
another Dc
@clintonhodda98303 ай бұрын
Kwacha yagwa kumene ndipo akuti Chakwera ndi ophunzira koma akulephera kuyendetsa dziko
@sankhwe3 ай бұрын
Good one
@BeatGondwa3 ай бұрын
Good good
@kondwamlungu83842 ай бұрын
Amen
@uzaleuzale86033 ай бұрын
Ndiye kunyozako kuli pat
@actuarialscience22833 ай бұрын
MCPigs ndi ufiti
@AllanChabwela3 ай бұрын
Chilungamo kkkkk
@LangfordMabaso-z7u3 ай бұрын
True mssg
@PhilemonLloydGalawanda-tz2zb3 ай бұрын
Ulaliki wa kale uwu siwa pa 3 July 2024
@GraceMakoka-v2k3 ай бұрын
Koma akunena chilungamo
@RobertLuka-wy9cl3 ай бұрын
🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏
@WisdomMaseko-fi5sv3 ай бұрын
Andale ampingo
@PempheroMoleni3 ай бұрын
🤗🤗🤗🤗
@TrizaGeorge-q8w3 ай бұрын
Nanuso musamakokomeze kuti zonyoza boma cholinga amangedwe akunena zoona aliyese pamene zafikapa olo mwana akudziwa kuti dzikoli sili bwino athu akufa ndi njala mwezi uno Kodi nangytifikile January athu akhala motani dzikoli lafika powawa tayendani m,mizimu athu afika pongomupepha mulungu kuti angowatenga chokhalilaso ndi moyo sakuchiona chifukwa Cha mavuto
@MassPastor-bn8ck3 ай бұрын
Sindikuona chomwe Mkuluyu akuyankhula zonyoza boma koma kuti ambiri mwa ife timakondwa tikamalambalala chilungamo,koma chifukwa choti chilungamo chima pweteka ndichifukwa chake zikuveka ngati kunyoza kama ayi ndithu akukamba zona zake munthuyu. I wish if we can learn to stand for the truth like this Father..........
@HevenChiwaya3 ай бұрын
This is great massages to the Malawi government if they have knowledge they have to change the direction
@abdukarimmponda56983 ай бұрын
Zimakutuzo amalawi kumataegula..anakuuzan ndani kut kutimikira mulungu nde kut azionelera zopusa zikuchitika aba ndalama za anthu zamisonkho kubako siusatana? Nde ena akalankhula alakwitsa...munthu wachinyamata mmutu mukadali ndale za 1990 zachisoniiio,👺🤔
@MathewKalinkhu3 ай бұрын
Kuswa kuswa, Chakwera ndi boma lake la MCP kumene aliko mutu waima, zoona zokha zokha, ndipo latikwana boma limeneli.
@AlexNjanje3 ай бұрын
Ineyo sindikupeza vutoo and Chakwera alibenso mzotheka mchifukwa kumakhala cabinet members ntchito yawo kumuuza presedent pomwe sipakuyenda bwino ndipo amamva ndi munthu osamangoti presedent ali ndi vutoo vutoo ndaammbaliwa tere basi
Vuto anthu mumadana ndi chilungamo, wanyoza chiyani pamenepa?
@GreshamKadzembe-tn8cq3 ай бұрын
Kodi inu mesa ndi amene munalemba chikalata 1993 kuti mukufuna madipaty, ndiye mukuletsa chani zimenedzo ndiye ndarezo kuba basi onse akhara a kulowa aja ndi okuba ngakhare iweyo ukulankhula we kuti ukhare pampando utha kuba so
@DixonChimanya3 ай бұрын
Uthenga wabwino chifukwa anthu mukuwalikiralawo ali pamavuto mu dziko lawo
@MphatsoMhoney-xn2ft3 ай бұрын
Very good and short speech
@mtimatrading7903 ай бұрын
Ameneyu saopa anayamba kupalamula nthawi ya Bingu, anamupuputitsa mkulu wina wake magilasi a mmaso pa msonkhano.
@adammadi82483 ай бұрын
Kodi povhota mumasanga kuti awa ndi abusa asavhote? Yet kufnyika and them there are experiencing the heat.
Where is the politics in this speech?? Learn to accept when things went wrong.
@AllanaChiphazi3 ай бұрын
Ulaliki musamaphatikize ndizadziko pls
@simeonbanda42403 ай бұрын
Rad the Book of Prophet Isaiah! He denounced the oppression of the poor and the injustices of the government. So its the responsibility of the pastors to denounce the envils of the government. Moreover the church has contributed significantly to the development of the country so it has a say where things go wrong
@AllanaChiphazi3 ай бұрын
Ulaliki musamaphatikize ndizadziko pls
@FrancisDay-br7xb3 ай бұрын
Iwe kumeneko sikusaniza ndale ndi mpingo koma kuzuzula zoipa za boma
@EvanceLiphava3 ай бұрын
Lalikani wanu tiumvere
@GiftSnoxy3 ай бұрын
Nyani iwe wamva ukudziwa chan
@YamieManda3 ай бұрын
Kodi athu awa simadziwa,muve ndi toque yomweyo angakambe zabwino za mtundu wina?amafunana wokhawokha mtundu umeneu_
@Jfphiri-w7b3 ай бұрын
Rev....mwasokonela a Revrend yambani ndale...mwakanika inu kuthana ndi Santana Zaka zonsez....musatchukile pa ndale ..simudziwanso kulalika inu
@EvanceLiphava3 ай бұрын
Osamangosusa zilizonse akulu ngati inu mukumwa tea daily si onse amene akumwa tea ngati inu. Choncho ndi udindo wake ngati m'busa kulangiza nkhosa zake zammene dziko likuyendera. Palibepo za ndale apa nchirungamo chokhachokha
@Jfphiri-w7b3 ай бұрын
Its global...go to Zambia Kenya Haiti Amerika.....homeless...no tea r there....everyone must use his head to make things move urside
@RuthChilobwe3 ай бұрын
Kkkk koma politics yo sikuba. Sattargate @Cashgate @Achairs vashgate ..