Wansembe wamkulu wa katolika anayankhula zonyoza boma zayambaso kuzungulira dzina ndi Fr Tamani

  Рет қаралды 19,522

Malawi Trends TV

Malawi Trends TV

Күн бұрын

Пікірлер: 75
@augustMag
@augustMag 3 ай бұрын
He is saying truth message he is advice the Government sananyoze kapena kutukwana ai❤
@DanMhone-iw6xg
@DanMhone-iw6xg 3 ай бұрын
Sananyoze koma amalakhula zona zokha zokha komasotu wanenelatu kuti zochezatu sono chomusakila nchani ndye akunama
@scoobymatola8314
@scoobymatola8314 3 ай бұрын
Sakunyoza You can't run a government without knowing economics
@WinerdShadreck
@WinerdShadreck 3 ай бұрын
This is good massage
@adammadi8248
@adammadi8248 3 ай бұрын
To speak the truth sikunyoza ,therefore tisiye mukalidwe woyika anzatu pamoto.
@ChembeWaimba
@ChembeWaimba 2 ай бұрын
Mwalalikazi mwatenga book liti lamulungu, kusochera ndikusocheresa uku, aneneri onyenga
@PeterRabson-z3w
@PeterRabson-z3w 3 ай бұрын
Wakamba zoona wansembe amenei chakwera n boma lake sakuzaununkhanso mpando 2025 muzandivoera✋
@paulmanyamba5437
@paulmanyamba5437 3 ай бұрын
Osati kuti wayankhula zonyoza anayankhula chilungamo osamadana ndikuuzidwa chilungamo ayi
@erasmopedrombewe8842
@erasmopedrombewe8842 2 ай бұрын
Esse padre falou a verdade, não é desprezo
@FrancoKaunga-rq2ki
@FrancoKaunga-rq2ki 3 ай бұрын
Father you are number one! Chakwera is a big failure. Indeed we made big mistake to put chakwera as a president.
@corretabanda7685
@corretabanda7685 3 ай бұрын
Kunyoza boma ndie kuti chaani? Kudana ndichilungamo kapena?
@Maliko-bp1xn
@Maliko-bp1xn 3 ай бұрын
Moyo wa munthu pali thupi ndi nzimu choncho thupi ngati likumana ndi mavuto akuyenera kulankhulapo kumene ,nkhristu ngati ali ndi njala angamve bwanji mau zikufunika zonse ziyende limodzi
@GanieAlidih-gu7no
@GanieAlidih-gu7no 3 ай бұрын
Palibe kunyoza apa km kunenachilungamo
@andyjames2050
@andyjames2050 3 ай бұрын
Pali kunyoza apa ichi ndi chilungamo cheni cheni
@festonphiri
@festonphiri 2 ай бұрын
Good message fr
@rhodrickmpumila1820
@rhodrickmpumila1820 3 ай бұрын
Ndi cadet wa DPP uyu ndikumudziwa bwino
@shayrafernandeslatif9556
@shayrafernandeslatif9556 3 ай бұрын
Very true
@wilisonbornface4282
@wilisonbornface4282 3 ай бұрын
Zoona kwambiri sikuwonapo cholakwika
@FavourKadzembe-sg1yf
@FavourKadzembe-sg1yf 3 ай бұрын
another Dc
@clintonhodda9830
@clintonhodda9830 3 ай бұрын
Kwacha yagwa kumene ndipo akuti Chakwera ndi ophunzira koma akulephera kuyendetsa dziko
@sankhwe
@sankhwe 3 ай бұрын
Good one
@BeatGondwa
@BeatGondwa 3 ай бұрын
Good good
@kondwamlungu8384
@kondwamlungu8384 2 ай бұрын
Amen
@uzaleuzale8603
@uzaleuzale8603 3 ай бұрын
Ndiye kunyozako kuli pat
@actuarialscience2283
@actuarialscience2283 3 ай бұрын
MCPigs ndi ufiti
@AllanChabwela
@AllanChabwela 3 ай бұрын
Chilungamo kkkkk
@LangfordMabaso-z7u
@LangfordMabaso-z7u 3 ай бұрын
True mssg
@PhilemonLloydGalawanda-tz2zb
@PhilemonLloydGalawanda-tz2zb 3 ай бұрын
Ulaliki wa kale uwu siwa pa 3 July 2024
@GraceMakoka-v2k
@GraceMakoka-v2k 3 ай бұрын
Koma akunena chilungamo
@RobertLuka-wy9cl
@RobertLuka-wy9cl 3 ай бұрын
🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏
@WisdomMaseko-fi5sv
@WisdomMaseko-fi5sv 3 ай бұрын
Andale ampingo
@PempheroMoleni
@PempheroMoleni 3 ай бұрын
🤗🤗🤗🤗
@TrizaGeorge-q8w
@TrizaGeorge-q8w 3 ай бұрын
Nanuso musamakokomeze kuti zonyoza boma cholinga amangedwe akunena zoona aliyese pamene zafikapa olo mwana akudziwa kuti dzikoli sili bwino athu akufa ndi njala mwezi uno Kodi nangytifikile January athu akhala motani dzikoli lafika powawa tayendani m,mizimu athu afika pongomupepha mulungu kuti angowatenga chokhalilaso ndi moyo sakuchiona chifukwa Cha mavuto
@MassPastor-bn8ck
@MassPastor-bn8ck 3 ай бұрын
Sindikuona chomwe Mkuluyu akuyankhula zonyoza boma koma kuti ambiri mwa ife timakondwa tikamalambalala chilungamo,koma chifukwa choti chilungamo chima pweteka ndichifukwa chake zikuveka ngati kunyoza kama ayi ndithu akukamba zona zake munthuyu. I wish if we can learn to stand for the truth like this Father..........
@HevenChiwaya
@HevenChiwaya 3 ай бұрын
This is great massages to the Malawi government if they have knowledge they have to change the direction
@abdukarimmponda5698
@abdukarimmponda5698 3 ай бұрын
Zimakutuzo amalawi kumataegula..anakuuzan ndani kut kutimikira mulungu nde kut azionelera zopusa zikuchitika aba ndalama za anthu zamisonkho kubako siusatana? Nde ena akalankhula alakwitsa...munthu wachinyamata mmutu mukadali ndale za 1990 zachisoniiio,👺🤔
@MathewKalinkhu
@MathewKalinkhu 3 ай бұрын
Kuswa kuswa, Chakwera ndi boma lake la MCP kumene aliko mutu waima, zoona zokha zokha, ndipo latikwana boma limeneli.
@AlexNjanje
@AlexNjanje 3 ай бұрын
Ineyo sindikupeza vutoo and Chakwera alibenso mzotheka mchifukwa kumakhala cabinet members ntchito yawo kumuuza presedent pomwe sipakuyenda bwino ndipo amamva ndi munthu osamangoti presedent ali ndi vutoo vutoo ndaammbaliwa tere basi
@MabvutoMichaelPanagona
@MabvutoMichaelPanagona 3 ай бұрын
Kunena zoona munthu wa mulungu sanafotokoze monyoza ayi ngati mukufuna kumutapa mkamwa mungomutapa mkamwa sindikuona chifukwa ayi.
@jameschibwana2751
@jameschibwana2751 3 ай бұрын
Vuto anthu mumadana ndi chilungamo, wanyoza chiyani pamenepa?
@GreshamKadzembe-tn8cq
@GreshamKadzembe-tn8cq 3 ай бұрын
Kodi inu mesa ndi amene munalemba chikalata 1993 kuti mukufuna madipaty, ndiye mukuletsa chani zimenedzo ndiye ndarezo kuba basi onse akhara a kulowa aja ndi okuba ngakhare iweyo ukulankhula we kuti ukhare pampando utha kuba so
@DixonChimanya
@DixonChimanya 3 ай бұрын
Uthenga wabwino chifukwa anthu mukuwalikiralawo ali pamavuto mu dziko lawo
@MphatsoMhoney-xn2ft
@MphatsoMhoney-xn2ft 3 ай бұрын
Very good and short speech
@mtimatrading790
@mtimatrading790 3 ай бұрын
Ameneyu saopa anayamba kupalamula nthawi ya Bingu, anamupuputitsa mkulu wina wake magilasi a mmaso pa msonkhano.
@adammadi8248
@adammadi8248 3 ай бұрын
Kodi povhota mumasanga kuti awa ndi abusa asavhote? Yet kufnyika and them there are experiencing the heat.
@owenmoses9434
@owenmoses9434 3 ай бұрын
Zonyoza??? In what way??? Nananuso mwayambae???
@samuelazumah1050
@samuelazumah1050 3 ай бұрын
Sananyoze koma chilungamo
@chrismezalumo5698
@chrismezalumo5698 3 ай бұрын
Very profound 🔥🔥🔥
@ThomsonNyirenda-df9io
@ThomsonNyirenda-df9io 3 ай бұрын
Nothing wrong good
@PatricMwadzera
@PatricMwadzera 3 ай бұрын
Kaya ndizaliti koma he is saying the truth
@0wenNkhambule
@0wenNkhambule 3 ай бұрын
Good Messnge Chakwela walephela you mast go
@isaacpaulrabson2099
@isaacpaulrabson2099 3 ай бұрын
Good point farther
@viennasamuel2976
@viennasamuel2976 3 ай бұрын
Pali kunyoza apa? Chilungamo ich
@MelvinVanRooyen
@MelvinVanRooyen 3 ай бұрын
aaaa kunyoza kwake..kulipati pamenepo akuyakhula chilungamo
@comradechimbayo3167
@comradechimbayo3167 3 ай бұрын
Powerful
@lazaruschitsamba8394
@lazaruschitsamba8394 3 ай бұрын
koma bwanji kunyoza wosatandiza maganizo
@MabvutoMichaelPanagona
@MabvutoMichaelPanagona 3 ай бұрын
Uthenga wa bwino zikomo
@AnaffSayamika-uh6vg
@AnaffSayamika-uh6vg 3 ай бұрын
Sananyoz akunena chilungam uyu
@RaphaelKweve
@RaphaelKweve 3 ай бұрын
Palibe kunyoza apa ,,,,
@MussaNgoma-r2k
@MussaNgoma-r2k 3 ай бұрын
Stop politics, mwayiwara ntchito yanu
@EvanceLiphava
@EvanceLiphava 3 ай бұрын
Where is the politics in this speech?? Learn to accept when things went wrong.
@AllanaChiphazi
@AllanaChiphazi 3 ай бұрын
Ulaliki musamaphatikize ndizadziko pls
@simeonbanda4240
@simeonbanda4240 3 ай бұрын
Rad the Book of Prophet Isaiah! He denounced the oppression of the poor and the injustices of the government. So its the responsibility of the pastors to denounce the envils of the government. Moreover the church has contributed significantly to the development of the country so it has a say where things go wrong
@AllanaChiphazi
@AllanaChiphazi 3 ай бұрын
Ulaliki musamaphatikize ndizadziko pls
@FrancisDay-br7xb
@FrancisDay-br7xb 3 ай бұрын
Iwe kumeneko sikusaniza ndale ndi mpingo koma kuzuzula zoipa za boma
@EvanceLiphava
@EvanceLiphava 3 ай бұрын
Lalikani wanu tiumvere
@GiftSnoxy
@GiftSnoxy 3 ай бұрын
Nyani iwe wamva ukudziwa chan
@YamieManda
@YamieManda 3 ай бұрын
Kodi athu awa simadziwa,muve ndi toque yomweyo angakambe zabwino za mtundu wina?amafunana wokhawokha mtundu umeneu_
@Jfphiri-w7b
@Jfphiri-w7b 3 ай бұрын
Rev....mwasokonela a Revrend yambani ndale...mwakanika inu kuthana ndi Santana Zaka zonsez....musatchukile pa ndale ..simudziwanso kulalika inu
@EvanceLiphava
@EvanceLiphava 3 ай бұрын
Osamangosusa zilizonse akulu ngati inu mukumwa tea daily si onse amene akumwa tea ngati inu. Choncho ndi udindo wake ngati m'busa kulangiza nkhosa zake zammene dziko likuyendera. Palibepo za ndale apa nchirungamo chokhachokha
@Jfphiri-w7b
@Jfphiri-w7b 3 ай бұрын
Its global...go to Zambia Kenya Haiti Amerika.....homeless...no tea r there....everyone must use his head to make things move urside
@RuthChilobwe
@RuthChilobwe 3 ай бұрын
Kkkk koma politics yo sikuba. Sattargate @Cashgate @Achairs vashgate ..
@AllanaChiphazi
@AllanaChiphazi 3 ай бұрын
Tidzangomvotera iyeyo, amalekeranji kukawadzudzula pamaso pa abomawo, lilipo boma lomwe linayamikiridwa ndi anthu amenewa? Popeza bolili lonse amalipezera zifukwa, zilalikani zoti anthu asiye kupanga ntchimo tiziopa tsiku lachimaliziro. Zamavote munayambitsa ndinu nomwe
Do you choose Inside Out 2 or The Amazing World of Gumball? 🤔
00:19
Как подписать? 😂 #shorts
00:10
Денис Кукояка
Рет қаралды 8 МЛН
小路飞嫁祸姐姐搞破坏 #路飞#海贼王
00:45
路飞与唐舞桐
Рет қаралды 9 МЛН
Mfumukazi - 2 October 2024
29:00
Times 360 Malawi
Рет қаралды 503
JOHN KAPITO WATOPA NAYE CHAKWERA. Ityoke ityoke// PART 2
27:18
MALAWI TODAY
Рет қаралды 51 М.
Mkangano wa Lucius Banda ndi Bingu
13:20
Sam Malvitha
Рет қаралды 172 М.
The War in Yemen, Mapped
22:09
Johnny Harris
Рет қаралды 2,1 МЛН
NDINKAKUUZANI KUTI UYU MUSAMUVOTERE
8:03
josephy kwendah
Рет қаралды 52 М.
AKAMUNA PA RADIO KUTULUKILA NDI NKHANI ZIJA ATOLERA PAJA SAMABISA MAU
22:10