Udf yatha basi ife tipita kwa adadi apm woyeeeeeeeeeee 💙💙💙💙💙
@HondaFredzoG5 күн бұрын
Ubwino wake udf tinaitsika kale kale
@TimeAbilu5 күн бұрын
Kabwezeni ndalama a UDF mukhala nokha nokha, from Mangochi south west, Mcp tilibe nayo mawu, maso ali pa Adadi inu muzipanga za ndalamazo(Adadi ali pa 89%)
ife tatuluka udf chipani chawusilu atupele ayiwale zawu president mpaka kale
@LafickDicksonКүн бұрын
Udf yata atupele patumbopanu
@PatumaCassim2 күн бұрын
UDF yatha bas mutu wawo sugwira sizalamuliraso
@BashielSalade6 күн бұрын
Udf ikhutikhumudwitsa
@rasheedjohn69562 күн бұрын
Kumango limbana ndi udf basi
@DumisaniMhango-e4i6 күн бұрын
Atha awa
@ChristmasChapeta6 күн бұрын
Udf kufuna kupusisidwa Ngati sakudziwa Kuti democrancy tinaimvera kuphweteka APA zafikapa sipakufunika dyera NDI ndalama kupanda app timalliza chipani
@Nelie-k4z5 күн бұрын
LL 😊
@PrinceBlessings-bv5bs6 күн бұрын
Mavuto alipo
@blessingssaiti5 күн бұрын
Wayamba manyiii
@TomatoKabichi-t1k2 күн бұрын
Koma sangalime ngat inu kumeneko muzikhalila kulila chocho lipopo munthu mutu juuu mukhala aphawi mpaka kalekale
@isaaczuze6 күн бұрын
Chipani cha udf chikutha chimenechi
@jameskachulu81414 күн бұрын
Kabwezeni ndalama 😂😂😂😂
@MlaziJames2 күн бұрын
Atupele ifa yanu ilipafupi mcp ikuphani mwaonesa uchisilu wanu
@EmilyKanyika5 күн бұрын
Machimo
@HerbartKaphamthengo2 күн бұрын
Zanyasa iweyo
@maidadyton26046 күн бұрын
Wabaza iwe
@MonalisaMwale-c5k5 күн бұрын
Wabodza ndani nanu munawaonako audf kumene kuja?
@SoundmasterElectronics5 күн бұрын
Uyu ndi galu ntchito kususa paja mumalipidwa
@ChristinaMdeza6 күн бұрын
inu musadandaule uyo kodi ngati amalepera kwawo kukhala mp. ndiye mukuganiza kuti akhale president ameneyo musiye wadya banzi uyu, musiyeni apita inu, akafike uko ku chikangawa. Ko
@ClementsKamanga2 күн бұрын
Ai kma mwagulitsa ndalama zingati
@SymonMwingitsa6 күн бұрын
Musamagwirirse mau a tonse alliance kuno tonse alliance inatha mwina yatsala ndi inuku limpopo ko poti kumeneko ndi kutali
@0wenNkhambule6 күн бұрын
Kkkķkk
@emmanuelchikowi87865 күн бұрын
Kodi a chair awathila doom mkamwa ndani ,a chair atani kutulika bwino bwino ku babulo ,azembela mtundu wa Malawi kubwelela okha mozembela a Malawi kukaphatikana ndi fano,maineeeeeee kuno ,a Charles kamphulusa, samu mpasu , a makhumula , a chair kuno zawaoneni
@RelaxCool-dp9jn2 күн бұрын
Boza ili Muluzi analemela kale guyz sangakabweleke ndalama ku mcp
@TomatoKabichi-t1k2 күн бұрын
Kuyakhula kumeneko big
@lyiemax5 күн бұрын
UDF inatha
@mayesojameskatete6 күн бұрын
UDF sitilola kukhala munkhwapa mwa MCP or DPP sitikuifuna tipita tokha kumasakho win or lose period
@UseniMailosi6 күн бұрын
Shupt
@ShamimuBisani6 күн бұрын
Ndpo nonsense yake yoooo@@UseniMailosi
@MzadziWanga6 күн бұрын
😂😂😂😂 ali mbuuu olo ku udf alibe udindo uliwose sakukudziwa mkomwe , takasamben uko msatichimwitsep apa tangothandiziran kudya ndalama zamagazizo uku mukusakaza kachipan kanuko
@EllenGomani-i4f6 күн бұрын
Atupele wayamba uchitsiru
@SaidSamuden2 күн бұрын
Uyu wadya Bazi olo za ifa ya chilima munavapo atupele kapena joyis Banda akukambapo kanthu
😂😂😂😂 Koma ziliko liko 2025. Koma Zipani zitatu ( 3 ) zapanga mgwirizanozo zili ndi kuthekera kutenga Boma DPP, AFFORD, UTM Gwiranani Manja ndikumanga Chimodzi ndipo mzotheka.
@MabushPaulo5 күн бұрын
Koma inuyo mumafuna udf ipange mugwirizano ndi chipani chiti?
@SandikondaIsaac5 күн бұрын
Kuononga chipani
@jaydee12366 күн бұрын
😂😂😂 simukudziwa inu this is politics
@RajaAlicky6 күн бұрын
Ife tmazwa kt atupele malingaliro ake Nd amenewo km ubwino wake ma members sakufuna kukhala pafupi Nd MCP so kumeneko aptako tuleleyo km ma members akuziwa kopta
@Sofi-p1v6 күн бұрын
Kutha kwa udf uku
@DamaliceWamalanguluko5 күн бұрын
Nanuso atupere mzafera ku chikangawa mzaona zizakuchitikirani khalani osamala kwambiri
Musaiwale kuti UDF Bakiri amakonda kupepha nde izi sizodabwisa
@NickUpoche6 күн бұрын
Udf/pp/ndi chinacho Kaya mukuti chipani cha nankhumwa ndi zofooka stikuopa
@ChifundoJohn-w3t5 күн бұрын
Tilibe nawonso ntchito basi
@IbrahimUseni-p8f5 күн бұрын
Atsogoleri. ndiomwe akufuna mgwrizano ndi MCP pomwe mamember akufuna mgwirizano ndi zipani zotsutsa ,,,eish! tiona
@SaidSamuden2 күн бұрын
Apitako okha
@DanielDoctor-t3p6 күн бұрын
Atupele ndi munthu oipa
@JamesIngeni-ku3qj5 күн бұрын
Anthu mukulimbana ndi udf chipani chot sichingawine ma elections or zitafutabwanji tafunani zina so zochita
@AcsonSaulos-d6s2 күн бұрын
Zitsiru inu a Limpopo mmangofuna kuyambanitsa mukutumikira satana aziwanda inu
@RodwellChisambo2 күн бұрын
Shame satanic iwe go away
@RobertLuka-wy9cl6 күн бұрын
Inu a udf olo mutayima pa nokha olo mutagwirizana ndi mcp inuyo a udf mwatha komanso simuzalamula dziko la malawi inu atupele abakili muluzi timakupasani ulemu koma apa machende anu nonse iwe bakili muluzi uli ndi uzimu mmene akuvutikila amalawi mungapange mgwirizano ndi chipani chija cha magazi kod magazi aja atha? Iwe bakili uzafa movutika mbuzi yamunthu
@FazackKambwiri-he8xe6 күн бұрын
UDF Inatha inu kuli ma mp angati kunyumba yamalamulo kut mpaka anthu azinjenjemela
@maidadyton26046 күн бұрын
Ukhalira maboza omwewo
@MzadziWanga6 күн бұрын
Iweso ukhalira yojiya yomwei kt akupase ya bundle 😅
@MalidadJaffalie6 күн бұрын
Km ngakhale zitakhala zipani 4 km ngat amalawi fe tikunva kuwawatu stinhavotele chipani chifukwa choti ilipo 4 mayazi
@RiteRoderick5 күн бұрын
Point boss
@Freedomchennl476 күн бұрын
amakili nd atupele akupanga za mabanja awo kma ngat ine sapota amene ndimachikonda chipanich kma pano bas znandipweteka pano or kumamuona atupele zot ndikonda ndkurumbila or pang'ono ndipo aziwe kut ine ndekha alipo ambri amene awtuluka a udf kwasiya agalu ameneo
@JamesAdmin-hx4ks4 күн бұрын
Atupele auze bambo wako kuti akalamba akusiye iweyo kuti uyendese ndale pa wekha ndi anthu ochikonda chipani cha UDF. Koma zokhazi mwapangazi zogwirizana ndi MCP mwalemba mmadzi vote ya masapota a UDF simuzaiona tinaziwa ife speech yomwe analankhura Bakili muluzi ku convention kuja