That's good l dea God be with you we love you pangani gwilidzano Ife tili pa mbuyo Pano
@GiftJulius-gx2kb29 күн бұрын
Utm udf my vote
@chrispinechirwa2655Ай бұрын
Vyakuyoghoya vya mtambo ni boza lekha😢😢
@marthaphiri3600Ай бұрын
Join hands with all the opposition parties, gawani mipando molingana campaign wisely win 2025.
@chrisboyce2Ай бұрын
UTM ikuyenera ibwerele ku DPP ndipo Ife angoni a ku Ntcheu tili ready kudzawavotera DPP Pamodzi ndi UTM ngati alliance
@KikaImranАй бұрын
You re very right. Sindinavoteko and if DPP coraborate with UTM i ll vote for them though am 100% sure that andale ndi oipa onse, they re there for their empty bellies
Mtambo NDI MBUZI...mavuto alipo panowa,anyani akulamulira panowa..mesa anawathandizila kukhala pampando ndi iyeyo😂😂
@PeterPhiri-u7hАй бұрын
MuKufuna alliance mukuopa chani
@user-im7sc2my4wАй бұрын
I don't trust NTAMBO ,NTambo vuto nngosamudalila Komanso nkovuta kumukhulupilila uyu . Ife aMalawi mukanakhala Ngati Bingu ,mmali ndi munthu wosavuta ,kungomupangila njira ya chakudya basi ,President ameneyo adzakhala WA muyaya. Ngati dziko Lili ndi chakudya ,ma business amayenda BWINO .Koma aaaaa uyuyu ayi mwina
@actuarialscience2283Ай бұрын
Ngakhale banja limayenda bwino ngati chakudya chikupezeka. Zovala ndi zina zimaphweka kugula.
@user-qp8kh2hj9oАй бұрын
Utm & UDF Boma 2025 ❤❤❤❤❤❤❤❤
@user-bv8wo2fn4eАй бұрын
I hope if all mupoto must vote for AFORD
@yassinn5634Ай бұрын
Mtamboyu akunena zoona nthawi Chihana Senior UDF imamunyengerera chifukwa Chihana anali ndi MP ambiri anali ndi mphamvu koma chifukwa chakugawanikana alibenso mphamvu
@BestonChagalaАй бұрын
Regionalism inamkanika chihana ,you can't win the national presidency without people from other regions.Nthawi zina musanayankhula mudzikhala Kaye pansi nkuuzana kuti kodi izi ndizoyenera kudziyankhula pagulu?Mukuti unduna simukuufuna chonsecho mukudziwa kale kuti simungadzawine u president wa 2025.Ngqkhale iwe mtambo pa ticket ya AFORD sungawine kuchitipa u mp ,nthawi imene munali nduna palibe chomwe munawathandidza anthu aku chitipa
Koma a Enock muchenjere ndi mtambo,mugawana zida 2025 isanafike chifukwa aliyense akuyankhula ngati ndi president payekha.Nanga mmene akuyankhulira mtambomo akuyankhula ngati vice president wa chipani ngati?Akudziwa kuti kupatula Ku hrdc sangayambitsenso gulu lina lotchuka paokha,nchifukwa chake asankha AFORD.Akuti safuna mpando chonsecho amayankhula ndi zodiak kuti afuna Udindo ngati platform yoti adzikhala influential
@WanangwaMfuneАй бұрын
Join
@Donnex-gn2sfАй бұрын
Aford akuwona kuti ku UTM kulibe utsogoleri komabe sizingatheke chifukwa a Aford akufuna mpando and UTM nayo yikufina mpando 🤣🤣🤣🤣
@user-qp8kh2hj9oАй бұрын
Ife tapanga kale ndi UDF musavutike 😂😂😂😂😂
@yassinn5634Ай бұрын
Chipani cha UTM chija ayamba kuchikanganirana. Chizungu chake SCRAMBLE FOR UTM. Ena apita kwa Aford, DPP ndipo ena atsala ku MCP. Thats my opinion. You got yours take it or leave it.
@ntombiunice8637Ай бұрын
Mtambo ndikhuluku...u minister unamurephera
@ChrifordBizielАй бұрын
Zimenezo2 zithera konko mwene
@user-rg9zc6eo2qАй бұрын
My vote afod
@SyakinongwaАй бұрын
Team up and cartel leadership positions within your team. Otherwise forget individual-party leadership as there is no way you can beat MACOPA.
@josephgabriel1016Ай бұрын
Timothy sangatinamize for the second time.....
@alickkachepa3801Ай бұрын
Move
@BrightNyoni-yd4ipАй бұрын
Mumakwana a hot 265 watching you from lusaka Zambia twatotela sana
@user-jn9tz3li3vАй бұрын
Mtambo mpaka kumuziwa Mulungu kkkkkkkkk ndale ndizovuta
@user-wk7ut7ld1xАй бұрын
Mtambo you are Malawian julias malema and your party aford you get 9% of the votes that is my prediction
@BestonChagalaАй бұрын
Vuto ndiloti ena pa imfa ya chilima afuna kutchukirapo.Aford yakhala zaka 30 but no progress koma pano they are claiming to be friends of chilima just to capitalise on the direction less supporters of utm.Ku AFORD kuli ndani odziwa ndale kuposa kaliati?And in terms of popularity utm ili pa mwamba kwambiri kuyerekeza ndi AFORD
@MercyNkhoma-b6hАй бұрын
Koma a Mtambo akunena zoona kuti samafuna mpando? kkk
@PangolinimwАй бұрын
🫡🫡🫡🫡🫡🫡
@HappyAntenna-sf9qxАй бұрын
iweyo ukumenyela ufulu wako ndalama zakuthela
@emmanuelsambo1158Ай бұрын
It was only SKC
@samdiverson9733Ай бұрын
Kkkkk mtambo sungatunamize adah ndife a utm we are together with DPP
@spargomwАй бұрын
I agree with you 100%❤❤
@MercyNkhoma-b6hАй бұрын
Koma chaka chino ziliko ndithu.
@MosesNyalugwe-ll8hhАй бұрын
Maloto achumba
@chrispinechirwa2655Ай бұрын
Ili ni lirombo yayi 😂😂😂😂
@VungaQueenАй бұрын
Kkkk😂😂😂😂😂
@chrisgremu740Ай бұрын
Ndiye Chakwera akawinaso 2025 Mutani?
@petertaulo8014Ай бұрын
Sangawine mark my words
@TiyesNayumaАй бұрын
Chitsilu iweyo you failed as a minister
@user-eh1gn1nj9dАй бұрын
Kodi imfa ya Chilima mukupangira campaign Mulungu akukanthani ndithu
@MercyNkhoma-b6hАй бұрын
Koma a Mtambo akunena zoona kuti samafuna mpando? kkk