ZOMWE AYANKHULA KU NDILANDE ATUPERE MULUZI NDI FREDOKISS

  Рет қаралды 29,196

HOT 265

HOT 265

Күн бұрын

Пікірлер: 90
@GladysBombeya
@GladysBombeya Ай бұрын
Wabwela lweyoo fredoo 🎉🎉tilipa mbuyoo pako SKC forever in our hearts ❤🎉
@user-wi9pe2hz7e
@user-wi9pe2hz7e Ай бұрын
Atupele akuyenela utsogoler kma ugwilizane nd Dpp coz 2025 Peter akuwina no doubt ❤
@SamKaposa-i5c
@SamKaposa-i5c Ай бұрын
Exactly
@user-qp8kh2hj9o
@user-qp8kh2hj9o Ай бұрын
UTM my vote ❤❤❤SKC forever in our hearts 🎉🎉🎉🎉🎉
@MAPAGASTUDIOS
@MAPAGASTUDIOS Ай бұрын
Good bless Hon ryt atupele the only last hope in Malawi with utm and dpp afford more fire
@rashidlamos3403
@rashidlamos3403 Ай бұрын
God bless you Atupele muluzi
@RoyBanda-d7h
@RoyBanda-d7h Ай бұрын
Atupele is good coz had to manage all the position given as a minister. Mainly Health ministry the guy did well. He never failed
@Freedomchennl47
@Freedomchennl47 Ай бұрын
Ife tikuyang'ana Atupele kaya atitengela kut 2025 tilinao mpaka tikhalowe Boma ❤❤❤❤❤❤❤
@ErnestChansa
@ErnestChansa Ай бұрын
Mcp asaza bweleleso boma paka kale kale chipani Cha mcp chikanango kutha Malawi anthu awa ndakupha fiti za anthu
@chikondichabwera6974
@chikondichabwera6974 Ай бұрын
Fredo alindichikoka but one thing aphunzire bhobho ndale from his father komanso mfundo akunge tili pambuyo pa utm..❤ skc forever in our hearts ❤❤
@AlickChima
@AlickChima Ай бұрын
Atupele Muluzi, a seasoned and mature politician. Mwaiyeyu tsogolo tiliona
@user-dn3gp6yi4y
@user-dn3gp6yi4y Ай бұрын
Tatopa ndi abilimangwe omati lelo ali uku mawa ali uku tikufuna achinyata omwe ali kuthekela kosinda zindu m dziko muno osati ma gogos party Atupele more fire
@emmanueljelemani4203
@emmanueljelemani4203 Ай бұрын
Osaopa, osatopa, osafooka SKC will fight with us..... Let God guide us
@user-ju7vc1uv7m
@user-ju7vc1uv7m Ай бұрын
Atupele it's my vote
@manasemaposa
@manasemaposa Ай бұрын
UTM my vote with no contradiction SKC in my heart forever.
@user-iq5xk6ju7y
@user-iq5xk6ju7y Ай бұрын
Atupele very humble always. Fredokiss achinyamata tikupatsa support. Taona mmene Burkina Faso yikusinthira ndi ulamuliro wa mwana Ibrahim Truore. 2063 ndi ya achinyamata not makolo akukakamilawa
@PrinceKachimanga
@PrinceKachimanga Ай бұрын
fredokiss needs ukali unali ndi SKC...TO sound relevant.avule chigoba cha munthu oyimba
@bridgetmajor3646
@bridgetmajor3646 Ай бұрын
More 🔥 ma gyz❤
@LeviChakwira
@LeviChakwira Ай бұрын
Put much effort kuti anthu akalembetse mwaunyinji
@LuwisKaigwaze-gr6cg
@LuwisKaigwaze-gr6cg Ай бұрын
Ku UTM kukusowekelabe mwini wake sindikuonakoso ntsogoleri wazeru
@user-vm7iz6oz6r
@user-vm7iz6oz6r Ай бұрын
2025 mcp tiyezeka
@khadijailiyasa5315
@khadijailiyasa5315 Ай бұрын
UTM ❤ ipatse moto 🔥 🔥 🔥 tiyenawo makape ang'onawa
@INNOCENTMOFOLO-io8tg
@INNOCENTMOFOLO-io8tg Ай бұрын
❤❤❤ utm together us one OSAOPA guys
@actuarialscience2283
@actuarialscience2283 Ай бұрын
Atupele is the only hope Malawians have. Let me give you the reason why I think so. ATUPELE IS THE ONLY PRESIDENT WHO STOPS DOING POLITICAL CAMPAIGNS AFTER ELECTIONS. Let's try Atupele.
@evancejimu2872
@evancejimu2872 Ай бұрын
I second sir
@SamKaposa-i5c
@SamKaposa-i5c Ай бұрын
We are together bro
@preciousnombo6875
@preciousnombo6875 Ай бұрын
Mmmmmm boza
@actuarialscience2283
@actuarialscience2283 Ай бұрын
@@preciousnombo6875 Mwaonapo Atupele akuuza anthu kuti akafotere UDF zisankho zili kutali? Ine ayi. Koma ndaona kongeresi(=ufiti), DPPigs, UTMiths, and other guys akupanga ndale daily. Koma uyuyu anali bize ndi ma biziness ake. Kwa ineyo ndingavotere Atupele panopa. Think wisely.
@MirriamChakanza
@MirriamChakanza Ай бұрын
Atupele our only hope. #changebegins#
@amoschataika7440
@amoschataika7440 Ай бұрын
Big up Brothers, Njawala, Fredo, Atupere ndi ena nonse let's kick out these idiots of MCP
@Atheeeefire
@Atheeeefire Ай бұрын
Together we can fight guys unity basi
@SamKaposa-i5c
@SamKaposa-i5c Ай бұрын
Unity is power
@user-dn3gp6yi4y
@user-dn3gp6yi4y Ай бұрын
Atupele more fire
@FelixBoss-yn9pe
@FelixBoss-yn9pe Ай бұрын
Wagulu lathu fredo ometa mwamakono ipatse 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
@YamikanGomonda
@YamikanGomonda Ай бұрын
utm udf and dpp tikuybekezela kuti mutithandiza mutati mwagwilizana chifukwa 50 +1 siyophweka kuipeza chipani chimozi
@andrewngowe8836
@andrewngowe8836 Ай бұрын
Wina apenga misala apo ayi wina ayendera wheel chair kunamizira kudwala 2025 kuli ntchito
@mphatsosadiki4983
@mphatsosadiki4983 Ай бұрын
2025 kukhale alliance ya DPP, UTM,UDF,Aford..... Wokha Alliance achoka m'boma basi😂😂😂😂
@user-qs2kr4gl6t
@user-qs2kr4gl6t Ай бұрын
Big up UTM
@tracybennie7783
@tracybennie7783 Ай бұрын
Mulungu atsogolele
@giftsalijeni6962
@giftsalijeni6962 Ай бұрын
Dpp + Udf + aford+ utm we are deleting Mcp in 2025
@leonardkangoma
@leonardkangoma Ай бұрын
President akhala ndani?
@janemanyamba7201
@janemanyamba7201 Ай бұрын
Camera simaonesa bwino bwino mmene tinakunganilana ndilande ❤❤❤❤
@Yusufu-Daudi
@Yusufu-Daudi Ай бұрын
Tayedzeka 😂😂😂
@TemwaMazuma-gs5de
@TemwaMazuma-gs5de Ай бұрын
Sure, we can very much fight
@AdiniKhama
@AdiniKhama Ай бұрын
Don't give up I'm with you people
@MATHEWSMAYIRA
@MATHEWSMAYIRA Ай бұрын
UTM 2025 my vote
@SaeedHurzrut
@SaeedHurzrut Ай бұрын
ndizisilu za nkhanza zimenezi UDF moto moto
@LazaroSinerioSineiro
@LazaroSinerioSineiro Ай бұрын
Limbikirani anyamata muchose nyasizi mbava
@asiyatujuma5507
@asiyatujuma5507 Ай бұрын
Atupele
@giftsalijeni6962
@giftsalijeni6962 Ай бұрын
Candle light mpaka 2025
@user-hb2hr5oc9l
@user-hb2hr5oc9l Ай бұрын
Koma maboma onsewa chipani chimene asangalala amalawi ndi chiti amalawi mugani MCP ndiye mwayiona kuyipa kwake muganize bwino
@AnthonyMhango-e9q
@AnthonyMhango-e9q Ай бұрын
Umakwana bro
@DONNEXKhama-bk1gy
@DONNEXKhama-bk1gy Ай бұрын
😂😂😂😂😂 chakwera unya manyi chakachino nd makape anzakowo
@jaydee1236
@jaydee1236 Ай бұрын
Atupele❤❤❤
@user-pv9uk6sc3w
@user-pv9uk6sc3w Ай бұрын
UTM, UDF, AFORD ndi DPP pangani alliance mutebge bomali, koma pasakhale ophangila ai, President aliyense wa chipani mu alliance apatsidwe udindo mu bomalo.
@jeremiambendera2749
@jeremiambendera2749 Ай бұрын
Morefire MCP out
@macmanyusa8242
@macmanyusa8242 Ай бұрын
😂😂 mcp mmimba bwaaa
@bismarkmhone
@bismarkmhone Ай бұрын
LETS JUST TRY THEM ALL PAJA TIMAKONDA KUYESA🔥
@shotsfired588
@shotsfired588 Ай бұрын
Don’t be fooled by Atupele, he feels entitled to be president that he didn’t want to work with chilima in 2020 but to work with mutharika. He’s not humble enough.
@CardinalDigital
@CardinalDigital Ай бұрын
Chilima felt entitled too
@LeviChakwira
@LeviChakwira Ай бұрын
This must be preached extensively. Anyamata akalembetse mwawunyinji please
@UseniMailosi
@UseniMailosi Ай бұрын
Musamaike maodio. mutikomola skc
@EmmanuelDanitsa
@EmmanuelDanitsa Ай бұрын
Fredokkis akadzitorere mfundo anakalibe
@Stewartchikoja
@Stewartchikoja Ай бұрын
@InnocentMtafya
@InnocentMtafya Ай бұрын
Kkkkkkkk😂😂😂😂😂😂😂 kkkk ine ndidzuke ndikagwire ntchito zanga ndikuona ngati it's what will make me better later, anatilodzayo eeeh! Ndi captain,anakuuzani ndani kuti kusintha sintha nkazi kumathandizila kupeza banja labwino, 😢😢😢mwiniwache Ndi mwiniwache Basi skc😢😢😢😢😢😢😢
@mnnyirongo2934
@mnnyirongo2934 Ай бұрын
Kuswa kuswa UTM madolo kwambili
@eliffagondewe8214
@eliffagondewe8214 Ай бұрын
🔥🔥🔥🔥🔥🔥
@JasonMailos
@JasonMailos Ай бұрын
UDF my vote ❤
@GLABELMW
@GLABELMW Ай бұрын
Osawopadi osafooka simulungu iyeyo
@user-kf3qm3or8l
@user-kf3qm3or8l Ай бұрын
Tikufuna sapato zomwe qnatiwuza adadi ako
@neemahkapatamoyo9563
@neemahkapatamoyo9563 Ай бұрын
Zaziii kusowa zolankhula zikugwilizana bwanji? Osangosiya bwanji Kupanga comment
@JumaKachala
@JumaKachala Ай бұрын
Kkkkkkkkkkk
@actuarialscience2283
@actuarialscience2283 Ай бұрын
@@neemahkapatamoyo9563 Uyuyu ngwa ufit=MCP.
@SamKaposa-i5c
@SamKaposa-i5c Ай бұрын
​Ukufuna chilima osati zopusazo
@user-ri2vi2fd5v
@user-ri2vi2fd5v Ай бұрын
Kupusa kwako iwe uzilimbukila kusaka mwana wa ng'ona iwe
@mswatizumalizwe4
@mswatizumalizwe4 Ай бұрын
Zalowa zibwana
@SheriffDyson
@SheriffDyson Ай бұрын
Yomweyo mchana wamugeto umakwana
@atanasioestevao9707
@atanasioestevao9707 Ай бұрын
❤❤❤
@TroubleMuthala
@TroubleMuthala Ай бұрын
Ng'ona zisazatulukenso m'mabango
@JamesNgwaya-vz1ox
@JamesNgwaya-vz1ox Ай бұрын
Kkkkk mupole moto
@MzikaPhiri
@MzikaPhiri Ай бұрын
MCP paulendo basi
@LindaNkwazi
@LindaNkwazi Ай бұрын
UTM woyeee
@SarahMusama-eu7wt
@SarahMusama-eu7wt Ай бұрын
Njawala moto
@EmmanuelDanitsa
@EmmanuelDanitsa Ай бұрын
Koma za Atupere yekhau ine ay.. alibe mfundo but am strong follower of UTM
@user-gd2kl1fx1q
@user-gd2kl1fx1q Ай бұрын
Utm forever not udf
@thomaschipinda6952
@thomaschipinda6952 Ай бұрын
Uyu mukuti fredokiss pa fair mfundo alibe infact the whole utm
@MAPAGASTUDIOS
@MAPAGASTUDIOS Ай бұрын
Good bless Hon ryt atupele the only last hope in Malawi with utm and dpp afford more fire
EKIVULU KISAZE GRAVITY OMUTUJJU NAWUNGA,AKOLIMIDDE ABA NRM
59:24
Gossip Live
Рет қаралды 55 М.
KUYANKHULA MWA MPHAMVU 10 September 2024
26:48
HOT 265
Рет қаралды 913
Underwater Challenge 😱
00:37
Topper Guild
Рет қаралды 48 МЛН
ДОКАЗАЛ ЧТО НЕ КАБЛУК #shorts
00:30
Паша Осадчий
Рет қаралды 995 М.
❌Разве такое возможно? #story
01:00
Кэри Найс
Рет қаралды 7 МЛН
TIMES TV KUING'ALULA MBC TV - APWETEKANA AWA🙌🙌
30:44
HOT 265
Рет қаралды 17 М.
FREDO MASINTHA
12:07
Fredokiss
Рет қаралды 6 М.
KUSEMPHANITSA KWA ZIZIMBA, ZOMWE ZINAPHETSA SAULOS CHILIMA 🤯😭
35:46
KUYANKHULA KWA GOTANI HARA ndi BRIAN BANDA.🙌🙌🔥
25:20
HOT CURRENT  LERO 8 September 2024 🔥🔥🙌🙌
33:23
HOT 265
Рет қаралды 9 М.
EXCLUSIVE WITH DR MATTHEWS MTUMBUKA
57:49
Zodiak Malawi
Рет қаралды 11 М.
THE COURT..(Malawi )🤔
20:45
Malawi News Update
Рет қаралды 217 М.
POLICE OFFICERS AND A CIVILIAN IN COURT FOR EXTORTION
Newslive SA
Рет қаралды 296
KUYANKHULA KWA BON KALINDO LERO PA 10 September 2024
11:51
HOT 265
Рет қаралды 10 М.