The great historian. Man u r a good narrator ever, sending some from Lusaka Zambia 🇿🇲🇿🇲🇿🇲
@CHINDEBVU Жыл бұрын
We will remember him like Malawian Yudas
@actuarialscience2283 Жыл бұрын
He always stood for evil. He supported one-party system during Kamuzu. During Bakili he supported 3rd term just to fight Gwanda Chakwamba.
@GwazaGomuzy Жыл бұрын
😂😂😂u are right 👍
@CHINDEBVU Жыл бұрын
Mu history yathu tili ndi nthawi yokumbukira achina John chilembwe Ndi gulu lake Achina Sangala Gadama Ndi ena Otero Osati anthu amene sanapindulire amalawiwa Tilibe ubwino wawo ndithu Kwa munthu amene anasatapo kapena kumva za mcp bwino lomwe Palibe angaifunire Rest in peace gulu limeneli Asogoleri ambiri ankalimbana ndi Asamunda nkumaika anthu awo pasogolo koma anthu awa amazuza anthu awo osusna nawo nkumaphedwa Zooona mmalawi weni weni Rest in peace Kwa zigawengazi Osaisunga bwanji misoziyo tizalire pa chilembwe day either kumukumbukira Bingu better than this crimals
Please give us history of Gwanda Chakwamba and why kamuzu choose him over John Tembo to be success of MCP
@rosseshaibu1576 Жыл бұрын
John tembo no rest in peace wakumoto basi
@staceycossam5933 Жыл бұрын
Kkkkkkkkk
@daviemafunga Жыл бұрын
Kkkkkkkkkkk
@TakosaGideon-ho6ng11 ай бұрын
Nobody knows it's only God who can judge...
@cheruartsofficial Жыл бұрын
You are a powerful researcher. I like how you put pieces together. I have learnt a lot of historical facts for malawi. My father is zambian but mother is malawi. Great documentary.
@husseinmoffatt Жыл бұрын
Muluzi TV ndi number One tchanelo of Malawi utube I like you man
@MasudiMatenje Жыл бұрын
Timakonda kumvela khani zanu big course mumaikamo chilungamo chokha chokha. Big up broh
@tisuhmakhwah7085 Жыл бұрын
Kip doin de good work bro God is and will protect u. Munthu ochita zabwno amalandila madaliso. Upitilize kusegula anthu maso.
@ChristinaMdeza21 күн бұрын
Mulungu wathu azikudalisani ndikuksamani. Bakili Muluzi tv your are the best brother❤❤❤❤
@user-ux3ed3ni1p Жыл бұрын
Chipepeso kwa mabanja omwe sawona chilungamo pamilanduyi. Apume mumtendere. Thank you for documenting our history.
@JacksonDamiano-ko8ui Жыл бұрын
Our own interpreter ❤️🔥🔥 Rest in peace Mr Tembo🙏🙏
@rashidsaid2232 Жыл бұрын
It's very complicated to remember this man his death when we remember our parents who died through him and Kamuzu Banda Cecilia Kazamila eish munthu amakoma akamwalira only God knows rest in peace
@gregchisuse83011 ай бұрын
Akazipedza ntchito zake zoipazo
@martinkalaka2667 Жыл бұрын
Resting In Piece Mr Tembo we don't want unnesessary history please only God judges the problem
@eunicemoyo6024 Жыл бұрын
Nanga osasiya kumveselako bwanji hiyaaa
@DanJohn-ws5gl27 күн бұрын
Woipa Tembo munthu wamagazj
@mataxsimon1737 Жыл бұрын
penatu I just like your voice, koma kanyimboko mopempha ndimayesera kukasewera pa keyboard, I wish simudzandipanga sue?
@abisalomchunga6695 Жыл бұрын
Thanks brother 🙏
@AshrafuBwanali-qi3my Жыл бұрын
Ànzanu atulusatso mbili yake koma sitinamvele kudikla inu inu Mulungu anakupasan nyota yakayankhulidwe mukamayankula munthu amamva sekeseke
@ibrahimmeemzy9754 Жыл бұрын
Original bakili muluzi tv ❤❤❤
@christophermkhize1991 Жыл бұрын
Ndimakhala ndikudikilila kuti no matter what muyiponya imeneyo big up bro mulungu adzikhala nanu nthawi zonse my brother
@staceycossam5933 Жыл бұрын
Kkkkkkkk this guy yooo
@ChomeNgondolo-uh5mu Жыл бұрын
Mwanena mwanena basi chilungamo chimawawa but anyway ndimamukonda John tembo moti nkhata yanga ndiyo ili patsogoloyo ndukapeleka 🔥
He can rest in piece wat can we say Salute wa Bakili muluzi TV.
@edsonndalama233411 ай бұрын
We can't remember him without remembering the death of Aaron Sangala, Gadama, Dick Matenje and some other people who were sent to their early graves because of politics.
@DumisaniMhango-e4i Жыл бұрын
My king ❤
@Cr7bianca Жыл бұрын
I love you bro
@BenjaminKamanga-p8w Жыл бұрын
Imfayi osatengakoso amene akutizunza lerowa bwanji apite onsewa basi
@YusufRahimu-be9hu Жыл бұрын
Big man❤❤❤❤
@KanguwoGift Жыл бұрын
Nah I can't say rest in peace coz I know that he is not going to rest this guy did alot there rest for people who did murder
@TakosaGideon-ho6ng11 ай бұрын
Nobody knows it's only God who can judge.
@user-tg8ye9yp8p Жыл бұрын
Ndimupemphe mulungu kuti amukaniretu ameneyi pansi pompano asanamukwilire. Galu wa sankho ameneyi, anabalitsa umasiye ku mtundu wa amalawi, Nsaname ankhanza asamamveredwe chisoni. 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥Apserere ku gehena akupitako
@christopherbottoman9131 Жыл бұрын
Congratulations bro everything else is good
@edwinrobert5346 Жыл бұрын
Rest in peace Mr Tembo
@williamsmanda8592 Жыл бұрын
Ichi ndi chigawenga chomaliza Cha MCP kukaliwa ku gahena. Chakwera adzakhala chimtseka khomo ku gehenako
@BenjaminKamanga-p8w Жыл бұрын
😂😂😂😂
@actuarialscience2283 Жыл бұрын
Tidzamukumbukira ngati mfiti. Kupha ndi chikhalidwe cha MCP. Pano ikupha a Malawi ndi njala.
@LUCIUSCHARLES-ei5vu Жыл бұрын
Yeah salute big
@ZioneMkwanda-y6i11 ай бұрын
Rest in the 🔥🔥🔥 John Tembo , Kadzamila will join you later 👉🔥🔥🔥
@LUCKYM4787 Жыл бұрын
Thank you bg mn respectful
@BenissoneErnesto-kn9bd11 ай бұрын
Mai mulungu wanga ine Joni tembo nde panopo Ali kuti siwafaso mulungutu simunthu
Go's round comes round palibe wamuyaya anayiwalazimenezo
@alfredbanda886 Жыл бұрын
Ndipo Kaya Yehova amasunga Bwanji chimunthu choipa chonchi Ndimoyo zaka zonsezi???? Ena mwaagalu akutizunza Amalawi Achina Chakwela osawapha Bwanji Dziko Lamalawi lipeze Ntendele koma akufa ndiokhulipilika kwa inu Mulungu kusiya Afitiwa
@BenjaminKamanga-p8w Жыл бұрын
Ndipo😂😂
@ziyamporoma377 Жыл бұрын
Kodi iweyo ukakhala nawo pa chiweluzo kuti udziti John Tembo sakalowa kumwamba? Do u know the the relationship he had with God at the time of his passing? Sitiyankhula chonchi pa nthawi ya maliro galu iwe opanda khalidwe ndi mwambo
@rickiez Жыл бұрын
In time like this, sikwabwinodi. Any way pakuti ndi nthawi ya demon class
@frezarphiri348023 күн бұрын
Tsiku line muzatipaseko history ya Esmay chafukili pliz chafukila anaphedwa movesa chisoni
@sharifujoe7633 Жыл бұрын
Exactly madder case Brah
@joegibsonzulu2599 Жыл бұрын
Munthu wankhanza, wakupha, opanda chisoni
@TakosaGideon-ho6ng11 ай бұрын
Nobody knows it's only God who can judge.
@shaik4123 Жыл бұрын
Akuti Nyimbo ikhale Nzimu wa Agadama
@ChikumbutsoPumani Жыл бұрын
Rest well Mr murderer
@BrightonPhiri-ug3gk Жыл бұрын
Let Malawians mourn Tembo peacefully than br br br
@KamusonCun Жыл бұрын
Good
@DaudBonomali Жыл бұрын
Ndiyenso choti aziwe zikhale ng'oma pano sikuseli kwa 2000 kuti anthu abadwa nthawi ya bakili muluzi kuti zithu zonse zinali chonchi kuseli kwa 2000 kunalibe tv kunalibe ma Radios komanso ukangoyelekeza ku chula zina la kamuzu amakuuzakuti ankhwazi akukumvani ku sanjika kukhala ngati malawi yonse anayi microphone everywhere anthu amaletsedwa kupanga mabissines bottom line John tembo tizamukumbukila ngati munthu mmodzi oipa kwambiri kuno ku malawi John tembo kamuzu banda anali anthu oipa kwambiri Ndiye pano mmalo mwa john tembo akufuna akhale mulowammalo wake zikhale ng'oma munthu oipanso kwambiri
@victorbanda9039 Жыл бұрын
Ndiwe chitsiru wabodza iwe Tembo anabadwira kukhola ntcheu osati Dedza
@inkprokasungu9287 Жыл бұрын
There's no need to remember him is only cruel people who support mcp like chilima joice banda lucius banda
Akalowa kuthako kwa make mbuzi imeneyi. Ndisaname I don't even want to hear the name of joni tembo. Munthu oyiiipa zedi.
@sihalimwasama753011 ай бұрын
Gahena is waiting for him
@johnchavula3282 Жыл бұрын
Ndimadabwatu😂 kuti zikuphonyani bwanj
@giftevans2957 Жыл бұрын
Yes
@daviekamanga1417 Жыл бұрын
inu munthu omwalira amakhala ndichilango kumwamba komaso simukuziwa ubwezi pakati pa iye ndi Mulungu
@declarembukwaАй бұрын
🎉
@harrispheleni2205 Жыл бұрын
Chodabwitsa nchakuti aliyese amakhala ndi zofooka koma sitimangoyang'ana zoipa zokha muli ndi vuto akulu mpaka muli ndi nkwiyo ndi munthu omwalira nde Nanu ndi munthu ouma mtima
@ZioneMkwanda-y6i11 ай бұрын
Tembo bwanji sunakhale wamuyaya wekha?? Wasatira kamuzu wamuyaya yo Cclia mmbuyo akubwera next week
@MrGodwinSambo Жыл бұрын
Eeee kwachema apo 😢😢
@khaikgotso156422 күн бұрын
😮
@Yahiya-wm8nd Жыл бұрын
Yah its not fair
@TonyBanda-ch6vo11 ай бұрын
Kkkk ndye mwati akumudikilira kuti akayankhe
@EdwinPhiri-k1w Жыл бұрын
He will be remembered for his satanic dids
@Lizzie-h1k Жыл бұрын
Zikhale will not be a minister forever, that he must know..
@Qiraa.m Жыл бұрын
Aise umatha kufufuza ndi kutsanthula Pitiliza ndipo ambuye azikusunga ndikukutsogolera
@HusseinMachemba Жыл бұрын
Za atembowa chilango awapase ndi mulungu koma sindinganene kt ause mumtendele
@ShadrackMsitweni-sr2uo Жыл бұрын
Ulemu upite kwainu big ulibwino big serious
@ashberiwlmariamejofe1885Ай бұрын
Atembo anali muthu oyipa kwambili
@costerrobert1519 Жыл бұрын
Amawona ngati mmene amawaphawo iye ndiye wamuyaya lero ndiye akawapeza komweko basi