Bon Kalindo lero pa 11 July kufotokoza mopanda kuopa aliyense - “MUNDIMVA NDIPO SINATI”

  Рет қаралды 30,966

Makosana

Makosana

22 күн бұрын

Пікірлер: 81
@user-ix2ux5ss1b
@user-ix2ux5ss1b 19 күн бұрын
More fire mukutiimilira bwana! Ife timasowa mpata oyankhura zakukhosi kwathu. God bless you and protect you. Amalawi tikuvutika
@EversDman
@EversDman 18 күн бұрын
Bon kalindo wathu wathu 🔥🔥🔥💯
@PeterKasiya
@PeterKasiya 18 күн бұрын
Boniiiiiiiii kalindoooooooooo Mwana owopswa kwambili
@JowasiMasina-fy8ji
@JowasiMasina-fy8ji 19 күн бұрын
Mukazava kuti boma lawanyera ndi zimenezo anavako kuti Koma Malawi ayi ndithu komaso kamuzu samapaga zimenezo ayi amati zithu zikamakwela iyeyo amakambolana ndi anuwake kamphani kuti atsitseko anthu ake alibe ndalama ndiye inu mukuzitega bwanji zimenezo kodi dziko la Malawi mwalitani tamakumbukirani komwe munali azanufeso tikuva kuwawa ngati munkhavera inu muja kuli mulungu kumwamba zonse mukupagazo akuziwona ndithu tsiku lina lidzakwana la 40👏👏
@LuyoloTlhapane
@LuyoloTlhapane 12 күн бұрын
A pule athu ❤❤❤god protect your mr born mmatiimilila
@MomeryPhiri
@MomeryPhiri 18 күн бұрын
❤❤❤❤❤❤❤ love it
@user-kk4uj8ko8k
@user-kk4uj8ko8k 19 күн бұрын
bon kalindo sukunama luchenza. Lijoni ikupanga khazakwambili longopackngi 1ooooo u lube amakumanga kuselo
@user-xm5cq1fb8g
@user-xm5cq1fb8g 18 күн бұрын
Ulemu wanu big❤❤❤❤❤
@DauglassNkhoma-dj9lp
@DauglassNkhoma-dj9lp 18 күн бұрын
😂😂Boni kalindo wangadula kkkkk boooo towopa kubwelako kumalawi
@neemahkapatamoyo9563
@neemahkapatamoyo9563 19 күн бұрын
Kkkk koma abare zowona mchenga omwewo omwe analenga Mulungu mwini nthaka zowona mpaka kumagulitsa ayi zikomo dziko ili 🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌
@user-dj6rc3lc4t
@user-dj6rc3lc4t 19 күн бұрын
Inu ndinu Muthu wankulu kalindo Bon mumakwana
@FarookRaphael
@FarookRaphael 19 күн бұрын
More fire komanso mukuyankhula ngat chinyanja service channel Africa
@Shelifibraheem
@Shelifibraheem 19 күн бұрын
Big up bro
@user-be5fc3ed1i
@user-be5fc3ed1i 19 күн бұрын
Ndipangeso replay pakanyimboko kandisangalasa bwanji kkkk koma uyu ndi pangolin 😂😂😂😂😂😂
@FlorryVugy
@FlorryVugy 19 күн бұрын
A president Bon mumatiyimilira😂😂😂😂😂 Sikusinja ndi gwenembe😂😂😂😂
@UthmanKapungu
@UthmanKapungu 19 күн бұрын
Fire!!!!!!!!!! Bon kalindo nazoni tatopa ife
@AffickChaona
@AffickChaona 16 күн бұрын
❤❤❤❤❤
@user-hx6jl2jq9j
@user-hx6jl2jq9j 19 күн бұрын
Aaaaa yai awawa akufuna kuti tiyiwale kunlankhula za chilima. Agalu a anthu ndithu
@user-lg6ym4hz3w
@user-lg6ym4hz3w 19 күн бұрын
Kkkkkkkkkk ana ofewa odya mipungu nthawi ya mayeso apolice akungosilira
@EllinaBitto
@EllinaBitto 19 күн бұрын
Bulaza wathu❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
@NdawaPhillipfortunePhakatie
@NdawaPhillipfortunePhakatie 19 күн бұрын
Motor 💥 kalindoooo
@user-wm4rs4kd7d
@user-wm4rs4kd7d 19 күн бұрын
@user-zt3gv7md6x
@user-zt3gv7md6x 18 күн бұрын
Zoona amwene
@PrinceBlessings-bv5bs
@PrinceBlessings-bv5bs 19 күн бұрын
😂😂😂😂😂 lero wayaka moto kalindo❤❤❤❤❤ a opposition please chitanipo kanthu awawa aikanika dziko olo manyazi alibe
@user-be5fc3ed1i
@user-be5fc3ed1i 19 күн бұрын
Awa ndi machine poyankhula the DC mwana wowopsya kwambiri 😂😂😂
@nicholasmutano6017
@nicholasmutano6017 19 күн бұрын
Uyuyu ndi mandrax sichamba, akufuna titani tilowele kuti si misala iyi?
@PeterMaulana-qk5uq
@PeterMaulana-qk5uq 19 күн бұрын
Ooh...ambuye dalisani anthu amene akumenyela ufulu m'malawi chonde musalore kt mbava za mcp zilamulire dziko lathuli AMen!!
@FwasanMwenefumbo-zq7sg
@FwasanMwenefumbo-zq7sg 19 күн бұрын
The DC 🔥
@BernadettaTengula
@BernadettaTengula 18 күн бұрын
Koma ine uyu ndimasowa pomuyika ,,ati chifukwa cha udindo😂😂😂
@ericlarks8165
@ericlarks8165 19 күн бұрын
,🔥🔥🔥🔥
@JoyceChitsulo-mw7wg
@JoyceChitsulo-mw7wg 19 күн бұрын
Makosana apa nde mwapita
@FrankMilias-og3js
@FrankMilias-og3js 19 күн бұрын
Kulankhula mosaopa nyooo sss winiko
@user-hq8fw5hz2l
@user-hq8fw5hz2l 19 күн бұрын
Awa ndie mawu
@user-dm6xq6cp1m
@user-dm6xq6cp1m 19 күн бұрын
Ai zikomo 🥱
@HelenamoisésLisboaMoisésLisboa
@HelenamoisésLisboaMoisésLisboa 19 күн бұрын
Ambuye akudalitsen
@benjulius6070
@benjulius6070 19 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂
@gerrardgladstone2473
@gerrardgladstone2473 19 күн бұрын
Akuti kufuna kumangidwaaaaa 🤣🤣🤣
@EdwardMukholi
@EdwardMukholi 19 күн бұрын
Kkkkkkkkkk koma chakwera ndiye ndiye zikuchoka kuti zimenezi
@ChisomoamitoniSauzandeamiton
@ChisomoamitoniSauzandeamiton 19 күн бұрын
bwana ng'alurani ndithu tili nanu nanu
@SmartMoles
@SmartMoles 19 күн бұрын
Zofunikila kulangura mwayangure kumene
@VincentMalika-w7x
@VincentMalika-w7x 19 күн бұрын
Ndipo eeeeee tikudziwona kuno tikulemba mayeso apolici ache akupemphaso dzokudza zakudya zath
@directorkfuture118
@directorkfuture118 19 күн бұрын
Ameneyo asamwe mowa 😂😂😂
@user-tw5iw7gf2v
@user-tw5iw7gf2v 19 күн бұрын
😂😂😂😂 mpaka muchenga license
@RamseyWasi
@RamseyWasi 19 күн бұрын
Blasa, Malawi saadzatheka mpaka kale kale. This is my second SMS to you mr Dangerous Child (DC) My opinion: Kungosiiya utsogoleri wa anthu osawukawu.chfkwa or titatan,kusawukaako sikudzaatha.
@BlessingsKalonga
@BlessingsKalonga 18 күн бұрын
Aliyese ndi wakuba koma kusagwidwa Judgement day tidikire oweruza
@BlessingsKalonga
@BlessingsKalonga 18 күн бұрын
Ubwino wake ukuzimenyera wekha khondo uzalemera wekha
@user-kx4cj7iu9q
@user-kx4cj7iu9q 19 күн бұрын
Dc
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 19 күн бұрын
Mpakana tizigulisana mchenga wamudziko lathu zoona?, kusavukatu uku sopano aati!?, chaza ndiyan choti tizikhala ndi linces yovuwulila mchenga ?, ndepoti amalawi mumkafuna kusintha zinthu , zimene mumkafuna kwa abusa zija mzimenezi😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂❤❤ , mo 🔥🔥🔥🔥🔥🔥 mcp kkkkkk
@HendersonDziwa
@HendersonDziwa 19 күн бұрын
Dzelu zachepa kkkk
@DaudiAbdullah-o5l
@DaudiAbdullah-o5l 19 күн бұрын
Mumatiyimilila
@TshepoModise-xs4qu
@TshepoModise-xs4qu 19 күн бұрын
Koma nkhaza zake mpaka licence ya mnchenga Mmmm zovuta bwanji eeee
@maxwellcaptain3937
@maxwellcaptain3937 19 күн бұрын
Kalindo samaopa😂😂
@PeterGrant-ih1sr
@PeterGrant-ih1sr 19 күн бұрын
Athuawa atakhala alipo okwana 4 ziko muno athuwa atasitha ndithu😂😂😂😂
@CaptainNyenga
@CaptainNyenga 19 күн бұрын
😂😂😂😂😂 koma DC
@D.RJALLI-qo6yd
@D.RJALLI-qo6yd 19 күн бұрын
Ine ndikudana ndi ma opposition akumalawi ndi agalu kobasi makamaka dpp ikungoyang'anila wosalangula khatu kumbonà lamasuso ngati ili ndiye boma adzalipesa bwanji dpp tadzukani ife tampudzilapo ndipo talapa mamisiteki athu bwelani nditu mutiwombole kwa agalu awa
@MathpeterLemon-ls1ns
@MathpeterLemon-ls1ns 19 күн бұрын
Ati kutitola kapena chani
@JuliusMunthali-z7j
@JuliusMunthali-z7j 19 күн бұрын
Awuzeni
@ChrispinEdward
@ChrispinEdward 19 күн бұрын
Bwanawe pafika boma umuthu walimbe akungo funa kumupanikiza Muthu osawuka kut azikhala ndima strees bas komano azidikile kut Pali mwambi waphala lakaka ukaza fika pomva kukoma limakhakut lathamo mupoto
@user-ls5zj8qn6k
@user-ls5zj8qn6k 19 күн бұрын
Koma uyu inu kkkk ati apolice osilila mpunga wa nyama 😂😂😂😂 ayi zikomo
@AnthoniohMazengera
@AnthoniohMazengera 18 күн бұрын
Hahahahahahahahahaha😂😂😂
@Aluwenkareem-ev3ro
@Aluwenkareem-ev3ro 19 күн бұрын
😂🤣😂🤣
@lytonmaseko4534
@lytonmaseko4534 19 күн бұрын
😂😂 kung'alulatu
@pempheroraynnoxmpesi8713
@pempheroraynnoxmpesi8713 16 күн бұрын
😂😂😂😂msusi olo nthuli amatayapotu a dpp
@GiftKulture
@GiftKulture 19 күн бұрын
🤣🤣🤣🤣 mipunga
@AaronLitete
@AaronLitete 19 күн бұрын
Kkkkk boma lopusa
@YonaMartin-kb3do
@YonaMartin-kb3do 19 күн бұрын
😂😂😂😂 akavoterana ndi amawo yemweyo kupuma palibe
@user-yl3lg5fk8f
@user-yl3lg5fk8f 19 күн бұрын
Koma amalawi tinalakwanji kt tizunzike,,,galu uyu wazunza miyoyo ya anthu osalakwa,,chitsiru cha m'busa munthu opanda conscious
@sir-wanton-2001
@sir-wanton-2001 19 күн бұрын
Kkkkk Kkkkk uyu akazankhala president azamujaje nda uyu ndi dolo
@ikmusic-s9f
@ikmusic-s9f 19 күн бұрын
koma nde eeee mpaka licence mchenga
@YohaneMbewe-u4k
@YohaneMbewe-u4k 19 күн бұрын
😂😂😂😂
@user-ky8us1ff5b
@user-ky8us1ff5b 19 күн бұрын
😅😅😅😅
@wangachindeya8577
@wangachindeya8577 19 күн бұрын
Bigiliman naweni
@user-vn1wq6wg6i
@user-vn1wq6wg6i 19 күн бұрын
K.K😂
@PhillipMtonga-g7o
@PhillipMtonga-g7o 19 күн бұрын
🤣🤣🤣🤣🤣🤣 zamanyazi kuntonse alliance
@BenjaminKayembe-j7j
@BenjaminKayembe-j7j 19 күн бұрын
km eeee awawa ndsbwsna gayz mmmmmm amakwana km
@Kachelephiri
@Kachelephiri 19 күн бұрын
Awa.akulila.ayesetse.2025.azawinekwawo.ump.kwawo.kma.ngatiakukanakwawo.ndiakanene.jilose.tingamuvele.galu.wachabechabe.
@ChristopherKawilam
@ChristopherKawilam 19 күн бұрын
Uku nyoza bon kalindo,, zeru ulibe iwe uku Kanika kulemba kumene galu iwe
@ChristopherKawilam
@ChristopherKawilam 19 күн бұрын
Yamba wapita Kaye Ku school ya mkaka uziwe kulemba...... galu iwe
@user-wz6jy3re8n
@user-wz6jy3re8n 19 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂
@MadalitsoManyozo
@MadalitsoManyozo 19 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂😂
@myheartforkids2876
@myheartforkids2876 19 күн бұрын
😂😂😂😂😂
A Michael Usi Inu Si A UTM - Lyton Mangochi
23:13
Nyasa VoiceBox
Рет қаралды 6 М.
Inside Out Babies (Inside Out Animation)
00:21
FASH
Рет қаралды 12 МЛН
Самый Молодой Актёр Без Оскара 😂
00:13
Глеб Рандалайнен
Рет қаралды 12 МЛН
Iron Chin ✅ Isaih made this look too easy
00:13
Power Slap
Рет қаралды 36 МЛН
EXCLUSIVE INTERVIEW WITH BON KALINDO
59:52
Zodiak Malawi
Рет қаралды 48 М.
Wakatolika uyuyu Amutapa posachedwapa😂😂🤣😂😂
14:40
Malawian Cameras
Рет қаралды 70 М.
Times Exclusive featuring Bon Kalindo - 6 January 2024
1:03:20
Times 360 Malawi
Рет қаралды 241 М.
Inside Out Babies (Inside Out Animation)
00:21
FASH
Рет қаралды 12 МЛН