Blasa, Malawi saadzatheka mpaka kale kale. This is my second SMS to you mr Dangerous Child (DC) My opinion: Kungosiiya utsogoleri wa anthu osawukawu.chfkwa or titatan,kusawukaako sikudzaatha.
@BlessingsKalonga18 күн бұрын
Aliyese ndi wakuba koma kusagwidwa Judgement day tidikire oweruza
@BlessingsKalonga18 күн бұрын
Ubwino wake ukuzimenyera wekha khondo uzalemera wekha