Eyadi .Akuphawa azipita akawruzidwwe ndi Ambuye Yesu mnkhristu..kuphatikizaponso.Inspector geneal of police Merylyn Yolamu agwere limodzi cos she is soo wicked.May God punish them all .refer Jeremiah 32 vs 26 amen
@abdullahmalinga14452 ай бұрын
Zikomo kwambiri ine ndimachinyadira chanel chanu chomwenso tsopano tinenetse kuti ndi chanel chenicheni cha amalawi. pitilizani kuchita support Bon Kalindo, president wa ine ndi anthu tonse osauka muno mu Malawi. ndipotu moti nawonso aja onse olemera aja nawonso akusilira kuti Bon Kalindo the D.C. Atakhalanso president wawo. Azingopemphera mwina n'kudzaterodi zikomo.😂😂😂😂😅😅😅
@MemoryLikaka-to7ho2 ай бұрын
DC ❤❤❤
@GanieAlidih-gu7no2 ай бұрын
✊🏻✊🏻✊🏻✊🏻✊🏻 THE DC mumakwana
@bonfacemoyo51712 ай бұрын
We are with you
@AlexanderBilliat2 ай бұрын
Following the DC
@SostenPiyo2 ай бұрын
Uh uh Kodi Bon kalindo lero wasanduka wamisala,kt MCP ilowe mboma wamisalayu anatenga nawo mbalitu,mwayiwala? Okay ndiye kt nchifukwa chake zinthu zakezi zkyenda mwa misalamisala eti,ndimadabwatu, the DCccccccc more fire wina akomoka
@ChristopherChakometsa2 ай бұрын
Tiuzeni zoona Mr DC
@samanthamuller76432 ай бұрын
The DC ❤❤❤❤❤❤ only you is best of malawi
@enerstmakochera39562 ай бұрын
Kudos dziwe TV to keep us posted every day
@cacksygustarf62602 ай бұрын
DC❤
@CharityChanzah2 ай бұрын
Always wishes de best for his motherland
@BlessingswazaDyress2 ай бұрын
Auzen Mr DC
@EmmanuelMalata-r4j2 ай бұрын
Pangolin wathuwathu DC mufune musafune azaimabe pa chilungamo ❤❤❤
@Noel-y6t2 ай бұрын
Mr Kaindo plz push for Malawi to go into partnership with Russia.The EU and the West will never do good for. Africans.Plz my big brother push for this agenda it will help Malawi and Africa at large.
@JunaKananji2 ай бұрын
❤❤❤❤❤❤Dc
@ChristinaSimwaka2 ай бұрын
Bad to be done
@PrinceBlessings-bv5bs2 ай бұрын
DC kuswa kuswa basi❤❤❤❤
@Elson-cf1gy2 ай бұрын
D C yakuthebay osaisiyla pangila boma ililieee nd lopanda nchison menyelani ufulu m' tunthu wanu presdent wa aliyese D C❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
@HafizaMussah2 ай бұрын
Nkadakonda phiri limenelo litakhala uyo akuzitchura kut mtsogoleriyo. I mean chakwela
@VictoriaKumwenda-k6o2 ай бұрын
Ukufa ndiwe kalindo koma iwe kalindo ukafa ukafikila kuti ndi maboza ako wo ndi ufiti wakowo
@IssaLazack-ij1gf2 ай бұрын
Wamabosa ndiwe namapwala osadulao amako
@JohnfosterNkusengwa2 ай бұрын
Takangazani kuno tizanvere limozi
@williamdaka792 ай бұрын
Chikangawa out
@UremuSimon-w3w2 ай бұрын
Nice
@IshmaelDenzo2 ай бұрын
Oyipa awa
@BakaliYassin2 ай бұрын
Exactly moya
@DamaliceWamalanguluko2 ай бұрын
Babiloni agwesedwe kkkkk
@DeborahHetekere2 ай бұрын
Zama scale pa thyolo ndizoona ndithu ine ndi mboni
@MaryKassim-vw9kv2 ай бұрын
Zoona zake
@CatimboJosé2 ай бұрын
Th Dc
@VosterMkandawire-u8p2 ай бұрын
Good speach
@blessingchimunda56392 ай бұрын
Dziwe tv❤❤❤❤❤
@Benjamin-h4k2 ай бұрын
Koma MCP ndi yankhaza
@MosesMkandawi-e2v2 ай бұрын
Zamphamvu the DC
@HendrickBanda2 ай бұрын
♥️♥️♥️
@BaulenichimenyayohaneYohan-n9p2 ай бұрын
the dc makwana timavera inu phiri rigwe basi auzeni ine bauleni watikwa chikangawayu
@PaulMalunga-i5i2 ай бұрын
Bwana DC...there is sense in you..simisala iyiyi....work more
@samanthamuller76432 ай бұрын
Ndipo mr chikangawa aziwa chaka chino
@NtchindiChirwa-l8o2 ай бұрын
Chosecho umachipangira kampen ndimwe 😂😂😂😂 wamisaladi iwe
@MikeEvason-rx4qf2 ай бұрын
Guys.changu D C wafika
@InnovativeSealing2 ай бұрын
❤
@phillgatoma48572 ай бұрын
Umakwanila Moya
@DavidJackson-ox4xm2 ай бұрын
The DC'S mwana woooopsa kwambiri
@KelvinSamboSambo-m1q2 ай бұрын
Zopanda tchito
@GraceLimani-zw7dx2 ай бұрын
A nalibe chakudya a police akugona ndi njala ndipo zola da ndalama zo a aphuzitsa apolice ndi Ken zikhale kubera anthu ama business
@JohnConar-kq4hi2 ай бұрын
The DDDDDDDDDCCCCCCCCCCCC bon kalindo 🇲🇼 ✊️
@NancyNyelenda2 ай бұрын
Osafowoka osatopa the DC
@GeshoMwakitwile2 ай бұрын
Anthu akamanena kut bon kalindo ndi mbuli ndimayesa akungomunamizila koma ndi mbuli yeniyeni
@BlessingsTembenu2 ай бұрын
Phili lake ndilitilo please tilidziwe likufuna kugwalo
@Daniel-cf4tu2 ай бұрын
Amzanu akuthamanga pa ground inu muli busy pa social media daily Ndinunomweso mumasogolela athu kuyenda pa mseu mkumaononga zithu
@UTHMAN-WAYA2 ай бұрын
Sono iweyo umabwera kuzamvera iyeyu fukwa chani? 🤣🤣🤣
Tsopano ku dpp ko kulibe anthu a ku southern region ? Tidaiwala paja Arhur Peter wamutharika ankachita tsankho.loopsya kusiyana ndi mkulu wake uja Bingu wamtharika.Him..must also quit let God in Jesus name reign us / rule Malawi nation .one who is not tribalistic and regionalisation get off peter mutharika
@PatrickMangochi2 ай бұрын
Meaningless
@AhmadumkomaTambala-lr9gp2 ай бұрын
Emen my broo akumudzi kwathu
@HaroonMKWANDA-r4x2 ай бұрын
Tangokerulani phiri lo tilidziwe
@VictoriaKumwenda-k6o2 ай бұрын
Zaziii boza basi bola iweyo kalindo kufa tilibe nawe ntchito kambwe iwe