Good Evance Meleka. Anthu akusowa zolemba. Name basi
@SameSamliu-u7h8 күн бұрын
🎉
@Littlefair713 күн бұрын
Ine kuyimba nyimbo kapena kuyankhula za kukhosi, wa police kudzandiamamga adzatsanzike kwawo chifukwa sadzabwerera, ine sindingalole kundimanga zopusa.
@isaacmanjele648713 күн бұрын
Anthu ambiri Ali busy kufalitsa maudani than kufalitsankhani yachikondi
@harrisphambana429913 күн бұрын
Ndiye mulandu wake ungakhale oti chani popeza nyimboyo anayimba ya lucious Banda komanso ndi zabodza watsutsa kale pa clip
@TaweniChavulaKamwendo13 күн бұрын
Eee
@user-tl9xg4fg9x13 күн бұрын
Dpp ikulowa pati
@MejarYusuf13 күн бұрын
Ndi ma kadeti awa akufuna kuononga mbili ya boma sanamange
@Kamdeukezimbabwesoko13 күн бұрын
Nice to hear this
@hopekamanja540713 күн бұрын
It's a lie
@SaidiMbawa-st6bj13 күн бұрын
Dpp ndi choncho
@inessmsiyambiri851713 күн бұрын
Aaaa itinso kkkkk dpp yo
@SaidiMbawa-st6bj13 күн бұрын
@@inessmsiyambiri8517 amene akufalisa nkhani zabodza zimenezo ndipo iye wakamba kuti ubale wake ndi Boma uli bwino kwambiri ndiye amene Sali boma ndi a dpp