Pali anthu ena amene simumusata munthu yi, please ma post ake sananene kuti president wafa koma anati Ali ku chipatala cha Garden city hospital basi
@ThivadoartistDyson20 минут бұрын
Kunkuyu wachamba, panopa maiko usi akukozekela kunka ku state house, mkadakonda manganya akadantulitsa pasi udindo chimwendo kkkķkkk mimba njuu kulibe kusintha atsogoleleri kwa manu konko
@FatimanickisJaffer3 сағат бұрын
Mwat born kalindo akamamusak saoneka km ndasekatu 😂😂😂😂 man of God glory to God born kalindo pangolin my brother
@AmickKammalele34 минут бұрын
Golf akamenyela kuti muthu wamwalira kkkk tiyeni only 2days
@GideonKodimba4 сағат бұрын
Kkkkk wabodza iwe umati chani uli ndi pakamwa
@EnriqueLemitton9 минут бұрын
Iwe ndi galu kwabasi..izi sizoona lumikiza a Malawi kuti tigwirizane
@FreserAaron16 минут бұрын
👍
@BrightLucianoСағат бұрын
Ntanyiwa sananenepo kuti president wamwalila apo pokha musanamizle
Ntanyiwa umangidwatu iwe ndi bodza lako misleading Malawian ndi za bodza,ngati ulibe zolankhura kumakharako chete pena,ngati momwe amachitirako a Bon Kalindo amazakharako chete pene osati kubwetuka
@rodrickwiskes48 минут бұрын
Pajatu boma ili silimanena chilungamo
@GrecianWyson4 сағат бұрын
Esh osamafaritsi khani ya ifa Koma arimoyo esh zopusa bwanji
Ntanyiwa sadaneneko kuti Chakwera wamwalira mukatelonso amene mukutelonu mukunama, ndatsatira bwino MA vn ake onse kuyambira dzuro atasowa kwa kanthawi koma zomwe ine ndinamva ndi zoti Ali ku chipatala cha Garden city ku south Africa, komanso musayiwale, 2018-2019-2020 mu nthawi ya Peter muthalika ambiri amakambanso nkhani ngati zomwezi president akasowa,nde monga ine sindikuwona cha chilendo choti mpaka Ena azimangidwa nazo, anthu akufuna Baba wa dziko atiwuze kuti wayenda bwanji ku UNGA koma kuli ziiiiiiiiii😢😢😢😢
@ShamimuBisani4 сағат бұрын
Mwayankhula zoona
@MoosaTrouble-o7p3 сағат бұрын
Ine ndamunatu chakwerayo akumwa magagada
@ShamimuBisani3 сағат бұрын
@@MoosaTrouble-o7p broh wationjeza abusatu aja
@MagretDaniel-m8cСағат бұрын
Musamunamizire ntanyiwa munthu wamulungu uyu
@BrightMbewe-fz5zf5 сағат бұрын
Aaaaa mwachedwa nayo,
@LonexWataya2 сағат бұрын
Che macdonald kachala ndi iwe wa mcp eti
@MaxwellMalisawoСағат бұрын
Mumaitha a mtanyiwa
@MemoryMankhwazi2 сағат бұрын
Ntanyiwa mabodza usiye
@TamalaKambanje3 сағат бұрын
Munthu wakulu nthanyiwa
@MacDonaldkachala-cm5gc2 сағат бұрын
If you don't have news, you don't have it's not a crime, if you keep broadcasting false news, you will lose followers, that's my advice