Akuzakhala running met wa APM MUZANDISIMIKIZA IYI N MISSION mark my wards
@PharrohmagawaZimba230Ай бұрын
100%
@PharrohmagawaZimba230Ай бұрын
100%
@isaihmagani5697Ай бұрын
Nde runningmate azayimira chipani chanji poti ku UTM azayimira Mary Chilima
@actuarialscience2283Ай бұрын
He is our president at UTM. Wachoka kuchipinda kupita pa seating room. UTM and DPP we are one.
@hamischikalimba6626Ай бұрын
Welcome to our beloved party UTM osaopa, osafooka osatopa SKC ndi ineyo ndi iweyo ndi ifeyo
@user-hm9nc7lz6eАй бұрын
Akabambe amafuna uprezdent ndiye mmene inangocitika ngodzi ya kuchikagawa achilima mkutisiya mumtima mwawo.amakondwa kuti atenga uprezdent ku utm akuluwa musavutike nawo asiyeni akaimire ku utm
@thokojames5231Ай бұрын
Musaiwale naenso anali gulu lofuna kuba chipani la kondwani nankumwa ,komanso after kuionera patali kuti sangamake pa adad basino kuthawira ku UTM KUMENEKO MPATA AKAUUPEZA ayende bwino usazabwerenso ku dpp
@jeremiahmalikebu2393Ай бұрын
Dalitso was a favourite wa adad, he is the only one amene adad amamukhulupilira kuti atha kumupanga endorse. Believe me, iyiyi ndi movie ma guys wa(adad ndi Kabambe) akudziwana.
@user-st6bt5vv9cАй бұрын
Mwana amalira ninkodzo wake asiyeni ayende bwino both him and others are not settled kutha kwamunthu kumeneko
@thokojames5231Ай бұрын
Komano movie imenei zitengera kuti akupitako akakhaladi president
Musapusitsike inu izi ndiye amati ndale zenizeni akungofuna kutipusitsa awa ,iyi ndi plan yoti dpp yonse idakhalilana pansi kuti ipangidwe ndicholinga choti utm ija ijoyiniletu ku dpp ndiye kabambe watumidwa ngati nthumwi kuchokela ku dpp kulowa utm.woooo!
@yassinn5634Ай бұрын
Pitani ku UTM.We want energetic leaders in UTM
@leonardmalirana7423Ай бұрын
Pamene zafikapa sip
@user-nu1dj3jh7bАй бұрын
Njomba zimenezo kufuna kupusitsa a Malawi 😂, adakali ku dpp komweko koma akufuna apusise wanthu apite ku utm akatero akasankhidwa kukhala president wa utm kenako azapange n'gwirizano ndi DPP ndiye ku dppko azakhala VP wa peter akatero peter azachita resign ndiyekuti kabambe azasala nkukhala president wa DPP. Izi nzomwe amadananazo achina Nankhwa aja , peter waku Thyolo, kabambe waku thyolonso.akufuna azasiilane mpando anthuwa akuziwa chomwe akuchita
@user-gp10.10Ай бұрын
Apa mwaganizo mozama bro,zitha kukhaladi chomcho
@user-qp8kh2hj9oАй бұрын
Aaaa palibe ubwino wake mnzeru za alliance ife a UTM tadzidziwa ndipo tikudzidziwa takula nazo mpaka taluza president wathu palibe angavotere izi mukunena iwalani
Apa nde akufunadi kuimaliza UTm cholinga akasakhidwe kudzakhala Vice president kuti UTM itheretu iyi ndi plan
@FarookStambuliАй бұрын
Welcome Mr kabambe to utm
@isaihmagani5697Ай бұрын
Welcome to UTM monga ngati member chabe osati President
@paularasonАй бұрын
Welcome to UTM Mr
@ChifundoChiwanda-ru3pgАй бұрын
Ngati akufuna kupita ku UTM apite koma tione kaye performance yake Ali ku reserve bank and also ku DPP. sometimes timakhala ndi anthu oti atha kugwila ntchito bwino dziko ndikutukuka koma amalephera chifukwa sapatsidwa mpaka bwinobwino or kuwagwiritsa ntchito mosiyana ndi mbali yomwe iwowo amayiziwa and atha kupanga deliver mosavutikira if they given the necessary resources. So I believe ngati anagwirako ntchito ngati nkulu wa reserve bank nzeru zilimo, he can be useful ku dziko lathu
@RobertLuka-wy9clАй бұрын
Wayiwonera patali sangamake pa Apm
@isaihmagani5697Ай бұрын
Osapusisika inu uyu ndi Cousin wa APM pachi bale chawo
@PatrickMtiraАй бұрын
Mwapusa mr mukanangokhara komweko bwezi trem inayo akanakupatsani kuti mudzaimire km apa palibe mwachita
@robertkalima874Ай бұрын
wachita bwino kusiya chipani cha kubanja
@JasonMailosАй бұрын
Muuzeni akalowe Ku MCP asati nyatsa
@AbdulrahimoMassambaАй бұрын
A UTM musanyadire,woteroyo ngwa dyera
@user-vx5kv8dz3dАй бұрын
Wachita bwino akalowe UTM . Vote yanga azaipeza
@user-ru1mm7bf4pАй бұрын
Wadabwitsa ndani munthu olo chipani alibe
@BrianJoe-z7uАй бұрын
Aaaaakabambe kabambe
@user-jj1zv2rs7fАй бұрын
Munalibe impact iliyonse mwainu yen Danish bwino
@user-kq6rp6hn7yАй бұрын
Welcome to UTM
@user-jj1zv2rs7fАй бұрын
Go well
@AndreaSignala-hk2ygАй бұрын
DPP 2025 boma muzakumbuka
@yassinn5634Ай бұрын
Kabambe akuthawa chani ku DPP? Kapena Biden wa Malawi?
@amonfrancisautotune2073Ай бұрын
Kkkkkkkl😂😂
@user-qp8kh2hj9oАй бұрын
Akuthawa chipani cha family watopa nacho
@ChrifordBizielАй бұрын
Zakhara bwino chipan cha banja ichi
@eliaskachali-xn2veАй бұрын
Pitani ku aford basi
@SaidiMbawa-st6bjАй бұрын
Ku Dpp usogoleri kulibeko koma dyela kukakamila udindo gogo imeneija osapasako mpata achinyamata
@DalitsoMatopeАй бұрын
Achinyamata ngati inu alepheratu
@MzadziWangaАй бұрын
Chakwera wapasa ndani mpata?? Mesa nae wakakamira 😅
@DalitsoMatopeАй бұрын
@@MzadziWangaakufuna amalizitse kudya misokho ya malawi
@SaidiMbawa-st6bjАй бұрын
@@DalitsoMatope zikugwilizana bwanji usogoleri ukufunika kwa Ana chakwela so ndi wachikulire bola awa not gogo ngati Peter kabambe kuti achoke kuli vuto kumeneko uzavomereza mochedwa
@GanizaniKamvazaanaАй бұрын
Ali ndi tsoka ameneyo
@hamischikalimba6626Ай бұрын
Peter Mutharika sangasiye mpando once voted into power unless death takes him. So l salute that decision Kabambe has made
@user-qp8kh2hj9oАй бұрын
Ndipo zoona Peter Munthalika sangasiye mpando wa chipani cha achimwene ake zoona
@user-nw6ie3xx8bАй бұрын
Prophet liyabunya analankhula za utm Zana kuti ayigula, liyabunya is not just a prophet like others no he is Elijah of our generation, love u prophet, bless me my name is Paul kheche mvuma
Catholic zoonadi ndi church ya pamalo pose koma mulibemo choonadi, like praying for the dead, Christmas, forgiving sins like God himself,kubatiza ana,ubatizonso wabodza,kuletsa kukwatila,kumafuna kupanga control boma pomwe church and state siziyenera kuphatikizana, kusintha sabata from surtuday to sunday,tsiku kumayamba usiku kuthanso usiku mmalo moti tsiku liziyamba kulowa kwa dzuwa kuthanso kulowa kwadzuwa ndi zina zambili bible likuti turukanimo mmenemo anthu anga babulo wagwa wagwa amayi wa a chigololo wa zonyasitsa za dziko ndipo mpingo umenewu uli ndi ana ake omwe amaitsatira zochita zakezo monga sunday keeping and all things that are out side the bible these practices are from pagan the chief of all paganism is the enemy of God called satan thanks for understanding ❤❤❤❤