Am not Malawian but I love my brother and sisters from Malawi chakwela must go
@FatimaAyami15 күн бұрын
Do you hear what he say
@NEBERTMVULA15 күн бұрын
CHAKWERA, ZIKHALE NG'OMA, MKAKA, CHIMWENDO BANDA, CATHERINE HARA, KUNKUYU be very careful Malawi is watching. MCP WILL COME TO AN END!!!!
@user-uv5rf4zt5q16 күн бұрын
Politics is a dirty game killing innocent people like that its very sad.
@JMB80416 күн бұрын
Eeeeeeh koma Malawi nde wavundilatutu 🙌🏾😭
@georgeaiwa866115 күн бұрын
Comrade Ntanyiwa ndinu amfumu ndipo we are in your favour. May God and ancestors protect you from MCP and it's corporates
@Jafaliwathombo16 күн бұрын
Keep it up abraz,we are on your back and we know more from you
@user-kw2do9wf3c16 күн бұрын
ulura zambiri ndimakunyadilani Mr Ntanyiwa
@user-hq6dq7zr1e16 күн бұрын
Musationongele South Africa timadalira konkuno ife,monga Osauka nde mumuuze nyaniyo,apole moto
@agreementphiri541614 күн бұрын
We are all with you mr Limpopo, Keep it up.
@IgnatiousFote15 күн бұрын
A malawi tikakhl chete kwmbr Chakwela ayambisa nkhondo kuphanso asilikali atatu pamwamba pa ngozi ya ndege ija
@user-kw2do9wf3c16 күн бұрын
utipase ma video onse angozi Mr Ntanyiwa plz
@user-lw9su5om5z16 күн бұрын
Eeesh kma chakwera mmmm
@ruthkundwe74483 күн бұрын
above all this,God is at work
@user-bi5lg8mg9y16 күн бұрын
Best Radio
@ThomsonNyirenda-df9io15 күн бұрын
We really appreciate we know more things from you 😮😮😮
@veronicanyirongo131413 күн бұрын
More fire limpopo we love u our brother for justice ❤❤❤❤
@LonnieGrem16 күн бұрын
Kma abale ufuluwo nde ndutio🤷🤷😭😭
@CostanceLalli16 күн бұрын
Lord have mercy
@JummaSAmick16 күн бұрын
Malawi X mavuto plus mavuto oooh Malawi wanga
@user-ku2fe8nb3j15 күн бұрын
A christu okhaokha kuphana mesa mumati zigawenga ndi Asilamu. Zamanyazi kobasi
@DONNEXKhama-bk1gy15 күн бұрын
😂😂😂thawi dzina ngat useke Pena ngat ulire pena kungokwiya bas eeesh chigawenga cha chikhristu
@user-oc9vl9xz8e13 күн бұрын
Ku malawi kuli anthu ozindikila oziwa kuyankhu komanso a nzeru
@YatoRoy-kt4lh14 күн бұрын
There is a massive American base in Botwana,what are they going to do about it?
@InnocentBabyTurtles-iq4ok15 күн бұрын
no one lipopo fm with comrade mtanyiwa
@LysonMtalika-tb6fk15 күн бұрын
Loud and clear ❤❤
@dysonfysonchifundo228416 күн бұрын
Mukutiyimilila inuyo 🤝
@GetrudeMseteka15 күн бұрын
Palibe chisisi pasziko lapasi. kungade kumachabe basi.. keep it up brother tidziwe zoona.
@KenChitete-pg3ws13 күн бұрын
Poti ku Malawi tilibe muthu odalilika a Malawi adzatsakha Peter Mutharika koma pamenepo pa Peter Mutharika ndimavuto okha okha.
@KenChitete-pg3ws13 күн бұрын
Kodi Peter Mutharika anali muboma athu amadandaula nayo Peter Mutharika plz audzeni a Malawi nfundo dzabwino,,a malawi atsakhe president wina otsati Peter Mutharika chifukwa analephela kale Peter Mutharika ndiponso Peter Mutharika ndi president otsakha mitundu kwambili.
@UsenLashid13 күн бұрын
Congratulation mr limpopo fm dont be afrid
@user-mw3kj4qz7b15 күн бұрын
That was really bad chakwela never liked the vice president evil act mr president that is bad from Zambia
@HalimaDamiano14 күн бұрын
Wabudula ndiwo zagulu. Keep it up bro
@SimonMlangiza-mu9fg11 күн бұрын
Uku ndie kupusa kupanga zosokineza athu Malo mo manga Zilibe phindu kazikambani zokonkholoka
@PetroMatias15 күн бұрын
Ndani ameneo angaiwale nzaifa imeneo zachambazo mcp yathabasi
@FakeAcc-mi4ko14 күн бұрын
Aslikali waphaso chakwela!😮 Akufuna atithamangitse kuno ku south tinathawa kumalawi kamba ka iye,galu kobasi chakwela ndi chimonica chakecho
@MikeMwale-bw1xw14 күн бұрын
Kachipani konunkha. This party must never exist again in Malawi,Chakwera must go we don't need dirty leaders,killers,murders God will punish.
@AiameAdamo-su1nt15 күн бұрын
Live from Mozambique.
@harrisbanda589116 күн бұрын
Chakwela asazunzitse abale athu ku South Africa chifukwa chandale zake zopusazo, leave malawians alone in South Africa, i beg South African government and Rusher government Mr Puttin to deal with chakwela with his crocodile party called mcp please.
@HalimaDamiano14 күн бұрын
Keep it up
@Elvin-dr8tv15 күн бұрын
Timchotse chakwera bcoz tazanu tithera Kuno joni
@peterlowole784115 күн бұрын
South Africa must react before, us Russia did kick out MCP
@user-wp9js5vu6s16 күн бұрын
Zachison 😢😢😢
@user-vb1iq5un5p15 күн бұрын
Komatu zoyankhulazi ma comrades mwachulutsa..mukutisokonezatu..timve ziti kodi?.. zuwoneka kt mukugoyankhula zinthu zomwe simukuuzidziwa, omwe simuli nazo sure.muvi wa chiponyeponye.. apa mukuti mundege munaikidwa spray amene anapatsa dizzy anthu anali mu ndege .😂😂 😂...mukachulutsa zoyankhulatu,,, anthu sakukhulupilirani...siine wa MCP koma ndangokulangizani ma comrade..
AMALAWI UMPHAWI TILINAWO ,KOMA BWANJI WOSAGWIRANA MANJA ,MMATI DZIKO NDI ANTHU ,KOMA NO ACTION . IT'S NOT ONLY DEATH OF CHILIMA ,NO!!!!! ,KOMA IYI YINALI NTHAWI YOTI A PRESIDENT ACHOKE BY FORCE . KOMA KULI ZIIII. TIKUZUNZIKA KUKHALA MAYIKO AKUNJA KAMBA KOTI MALAWI AKUSOWA MTSOGOLERI WOTI ATITSOGOLELE
That’s why I said Chihana & atupele not chakwera & grandpa.! 👴
@afritouch466016 күн бұрын
No MCP no DPP..!! Waste of time.!
@EuniceBauleni15 күн бұрын
Aponyedi
@IssaKapalamula15 күн бұрын
That English is not for a South African citizen 😂😂😂😂
@MichaelWilliamsNyirenda13 күн бұрын
Is for who ?
@IssaKapalamula12 күн бұрын
@@MichaelWilliamsNyirenda Zimbabwean, and it’s a Shona guy
@AndasoniWikisoni15 күн бұрын
Kkkkkk eeeee kwachematu
@Henry-vw2cz15 күн бұрын
Chakwela mbolo yako wamva
@user-lr2wx5xd9d16 күн бұрын
Following
@user-ml9fm2wm1o15 күн бұрын
🍇🍇🍇🍇🍇🍅🍅🍅🍅🍅
@HassanKareem-ck2qj16 күн бұрын
Mumakwana
@SolomonAmon-bu5qc15 күн бұрын
Even in Kenya people are talking
@Aubiekenneth16 күн бұрын
Iwe makutu amako wanva machende ako
@joebrown115816 күн бұрын
Mwana wa njoka wakusaweluzika mwana wa chiwonongeko ulendo ku Gahena
@LamieTiger16 күн бұрын
😂😂😂uvayanayo MCP ada zikolonse lamuoodza chakwera iweyo wekha ndi athu akwanu mudzamuwinitsa chakwera 2025 Bola chakwera akanangokhala abusa m'mene analili kale lija coz apapa nde or kupepherera athu sangakhulupilire
@blessingsbanda103116 күн бұрын
Chitsilu chamunthu iwe
@joebrown115816 күн бұрын
@@blessingsbanda1031 mwana Waipa kwambilri kusangalara ndi M C P MAKOLO ANGA ANA BVUITIKA NDI M C IWEYO NDIKUMASANGALALA CHOTERE MWANA WOIPA KWAMBIRI