She is a true politician,u can tell by how she refuses some questions
@RobertChisenga-ci2mqАй бұрын
Masten amandiyakhulira bwino kwambir kaya anali loya kaya I love you masten
@user-nf3ik3ff6yАй бұрын
Good Messnge mayi navicha
@johnmpatama1461Ай бұрын
Best interview ever ❤❤
@user-tw3fl7vh7jАй бұрын
Apm my vote
@augustMagАй бұрын
Powerful words mum💪💪
@user-eh1mg3ww6dАй бұрын
Ndipo mai olo mutakhala plesdent dziko likhoza kukhala losangalala mukhale ndi moyo chikhaleli mai❤️❤️
@MrsNankhumwaАй бұрын
APM my vote
@PrinceBlessings-bv5bs20 күн бұрын
Tivomereze Dpp zina sizimayenda koma 85% zambiri zimatheka, Mulungu atiyendere kuti Ngati kuli kotheka Dpp ikoze utsogoleri wake ku conversation then akoze dzikoli popeza Amalawi osauka chiyembekezo chawo ndichomwechi. Let's Beg God to give us maso auzimu
@user-rb9jq2pv2tАй бұрын
big up Mary Navitcha
@CharlesKachipanda-jz9jvАй бұрын
My Favorite radio station
@DeborahHetekereАй бұрын
Mary Navitcha MP Thyolo thava constituency moto unandiiiiii
@user-bs8nk1si4eАй бұрын
Limpopo Radio woyeee.Mai Navicha Woyeeeeee
@IsaacMusa-py2jmАй бұрын
Powerful 👊
@user-pv9uk6sc3wАй бұрын
Mau a mphanvu mai Navicha, ndipo a Malawi tili pa vuto kwambiri. Chakwera walepherela basi.
@MikeKathumbaАй бұрын
Ngakhale chiphatso cha ubatizo chikagwira ntchito pokavota.....
@KennethMpininga-iz2ieАй бұрын
Super ❤
@AmosBandula-up4ybАй бұрын
Okay
@user-fi7ko7bl6fАй бұрын
I salute you Maa
@BaulenChipalaАй бұрын
CHOTI nikuuzeni Inu abale akummwera ndichakut kut mumuve bwino chakwera , muyenera kugwira ntchito, kazilimani kut kukwera kwachimanga kusakuwaweni bcoz kwa amene timalima timasangalara chimanga chikamadula even kugula fertilizer it's easy just sale 2 bags it's enough to buy 1 bags of fertilizer pamene kwa amene Salima namene amakhara patsogolo kudandaula, ife ogwira ntchitozakudula kwazinthu sitikukudziwa bweran central regional man mukamaziva kuchoka ku John ko muchedwa
@user-gu3sp8ci6vАй бұрын
Pali zina zoti muuzane kumbali musanayambe program , mumatichedwetsa
@MustapherLinoАй бұрын
Mau amenewo amai mary Navicha
@user-gl1ev1dw6wАй бұрын
Koma mayiwa amatha kulankhula
@GiftMathewe-fr3knАй бұрын
Ndimakunyadilan mama
@TwalikiWisikiАй бұрын
A Malawi ndiwokonzeka Kuka vota,koma Pali kuthekela Kot MCP ikumana anthu cha unzika, ndiye inuyo a opposition mulimbane nayo nkhani imeneyi
@user-nl5rq9to2sАй бұрын
Congress party inapanga zitheka kuvuta malawi yonse inuyo adpp chimene chikuwavuta ndi chiyani why dont dpp do the same
@Maliko-bp1xnАй бұрын
Mai inuyo ndi loya panokha mukutimvetsa kukoma
@PangolinimwАй бұрын
💙💙💙💙💙💙
@user-lp8wj3vq4xАй бұрын
Mavenda ife ndye tikuliradi mmm zinthu zavuta bola adada aja ndinthu
@user-nl5rq9to2sАй бұрын
mchifukwa chake mcp ikutanga advantage mkumatiopsesa malawi yonse dpp ndi mboni kapena chifukwa choti iwowa akudya bwino