If he was clever enough he should start this in Central Region! Opusa Michael Usi. When did you spoke to PS 😂😂😂😂😂 Manganya!
@itubiz15012 ай бұрын
inuyo ochenjera? a Malawi muthu achite chabwino mumuloza zala apange zoipa ndiye worse...tonse stingayendese dziko man even amene mungafune inuyo eyendeseo papezekabe ena osawakonda. muona koma kuti mutaani
@henryphiri61002 ай бұрын
Malawi immigration office ndi dimba la nick chakwera ndi zikhale ng"oma motsogozedwa ndi Lazarus. Yankhulani chichewa akulu palibe nzungu amene akukuvetsa nyasi ya chizungu chimenecho.yankhulirani munthu wakudzi ave.
@@petroszgambo9949 bwino nthawi yatha iyi yesu akubwera muchimwa nazo zambili muziwone ndi maso a uzimu zikutsegulani maso kuti yes chofunika kukonza mtimawu siziyenda momwe tikufunila kaya ndi economy,njala,matenda,nkhondo ma floods,ananena kuti zidzachitika mu nthawi yakumapeto zikomo kumbukilani sodomu ndi gomola ndi momwemu angakhale mu nthawi ya nowa
@Chilinga_P2 ай бұрын
Akungolongolola ..phokoso basi....system ya ku immigration yakupeta and he likens it to medical / treatment system
@patiencechangole98252 ай бұрын
Apite ku capital hill akayankhule kumeneko ngati ali serious
@JamesKhengemussa-t1d2 ай бұрын
Kuno nku Malawi basi tizidikila tsiku lakufa
@AbunthiMtambo2 ай бұрын
Zaziiiiiii 😂
@CharityChikomo-hl1gz2 ай бұрын
I wish I can speak to him in person asatiyese ife opusa ndale iziii
@MakupeWekha2 ай бұрын
Waste of time and resources
@CharityChikomo-hl1gz2 ай бұрын
Za ziiiiiiiiiiiiiii musatipepeletse ife mukudziwa zomwe mukupanga anyani Inu munalonjeza kuti ma passport mwayamba kupanga lero kuli ziii zili zabodza amalawi mmationa ngati opepela eti agalu Inu Ali ndi #ya Micheal manganyayo andipatse ndimuimbile pompano mxieeee
@VictorKachulu-y3n2 ай бұрын
Nenani ndinu zennizeni anthu abwino amzanu a nyani good for you
@kumbukanikafwafwa2 ай бұрын
@@VictorKachulu-y3n kkkkk palibe wabwino padziko lapansi. The guy is trying hard. Akulubwawa ndi ana oti sakuona chabwino pa chilichonse. Zimaoneka bwino Muthu uja akachokapo. See the Presidency trend bwana. Komaso iweyo moti sukuona zomwe akupanga. I support usi. Other wise enawo nde Ali trush