Uyu chimwendo mnmm he is full of himself. May God punish him
@mishecksipolo7153Сағат бұрын
Ok
@HenryKeyala16 минут бұрын
Ngati wafa nde zilibwino bwanj❤
@cmsanyama2002 сағат бұрын
Honourable Mtanyiwa you really have shown maturity here as a journalist,bravo to you!
@OwamThoko2 сағат бұрын
Tipephelele kuti asafe chakwela pls,ali ndi ma answer oti atiyankhe pa nkhani ya imfa ya olemekezeka late Dr saulos chilima.bcz ngati angafe ameneyo onse onkhuzidwa pa nkhani imeneyi azangoti ndi a chakwela anatiuza.popeza iyeyo wapita Mapeto ake pazakhala opanda omboni.
@YasenYasen-q9g2 сағат бұрын
Kuti asowe kkkkk
@RuthMkandawire-l8d2 сағат бұрын
Iweso zachani nawe
@RashidPiano2 сағат бұрын
Wafa bs Or Abise km Timukwilila Bs Uku Tikusekelela Ndipo Malilo Amene ndi olila Anthu Okha Okha Akubanjia Osati ife😂😂
@RahimLuembaСағат бұрын
Bravo comrade u real deserves
@TimeAbilu2 сағат бұрын
M'mati yimilira comrade mtanyiwa Allah bless you all the time, to fighting freedom
@SusanaMakangaСағат бұрын
Mmmm Malawi Basi kumangoganizirana zoipa basi Mulungu Akadalitsa wadalitsa 🔥 All the best Mr President
@PhahlaniMugaba-e8r27 минут бұрын
Justice delayed is justice denied
@SilenceChepiano2 сағат бұрын
Ngati alimoyo akanaveka mawu
@lyiemanganjira97083 сағат бұрын
Comrade Ntanyiwa umatimilira,, viva comrade viva
@ElizabethFatch-o3w39 минут бұрын
Zikomo Mr ntanyiwa timakukondani Mr ndipo mumakonda mtundu wa mfuko lanu ambuye adzikudalitsani chikufa kwa amene akanatha kufa imfa yosalakwa kathu koma Ili ndi chenjenzo lanu
@shavickmzulamzula701220 минут бұрын
Mulungu si Muthu achira😢
@melnisachagwamnjira60822 сағат бұрын
Kulibe kumwalira ataaa boma ndilomweli mpaka 2030
@MadalitsochristopherMagalasi2 сағат бұрын
😂😂😂😂
@RUNBWOYСағат бұрын
😢
@RhodaJere-f7o2 сағат бұрын
Zikomo kutiyimilira zose tivera Kwa mthanyiwa
@StanleyChamasowa2 сағат бұрын
Ndipo akamwalila chinwendo kunkuyu ndi team nyamazikukuzikulu akonzekele
@SaidMkonongo2 сағат бұрын
PAlibe kumupepherera azipita kumanda basi misonzi ya mary chilima iyankhidwe basi
@MakabaBauleni-c2iСағат бұрын
Ambuye ikani zanja lanu la machilitso kwa mtsogoleri wathu L M Chakwela 🙏🙏
@LoleniShabani-mt7nzСағат бұрын
Let him go
@VeraBeab38 минут бұрын
Nyapako iwe apite ameneyu
@FeliaNgunga2 сағат бұрын
Bisani matenda maliro atipeza pasanathe week, wapita wapita, no wat wat bon voyage 😂
@MikeLodzi2 сағат бұрын
pa inu amtanyiwa timadekhatu
@UthmanKapunguСағат бұрын
Anthu ndi masooooo kuchokera Ku hospital kufikira Ku golf
@AnaphWanjaСағат бұрын
Km mukuti zowonadi za chakwera
@JerieWytonTenganiСағат бұрын
A Michael Utsi osawanamiza anthu tinned kuti character ichi chikubwelachi Chakera akusiilani kuti mukhahle pa upresident poti panali mgwirizano popeza a chilima anaphedwa? Inu Muima? Osamawanamiza anthu a UTM bwelelani mmbuyo Mathieu asanathe .Chakwera Singapore ndi pang"ono pomwe, ndiye waupodatu bwanawe.
Mwati bwanji pamenepo bisani matenda koma chaaaa.......😂
@BairdThomas-c2kСағат бұрын
ngt alimoyo ine ndiye zindinyasa chifukwa zisangaralo tinayambapo pa c z pa m and m pano amtanyi tafufuzani kachikena mutiuze zoti wafa tipitilize kukondwela
@FatimaAtibuСағат бұрын
Malawi will change, imagine chakwera waduwa then 😂😂
Unya uona alikuno uyu ku South Africa kulibe moyo kuno ndangoyandikana nayeso chipatara chake 😂😂😂 akupitaso kwa america apa akapangidwe Zina ndi Zina kkkk
@xinalungu9616Сағат бұрын
Koma mabodza amalawi tidzawasiya liti?
@AlfredsencoSeleman3 сағат бұрын
Akasewela bwanji golf ndidzanja limodzi??
@eliffagondewe82142 сағат бұрын
Mposo inu
@ivymakiyi3 сағат бұрын
Cry cry until you cry no more
@YasmeenYalabi-b2c3 сағат бұрын
Inu achakwera kulibe wapita kukapangidwa embum komwe anali kuja kwa America tsegulan Alhazeera mumvere
@lyiemanganjira97083 сағат бұрын
Mmmmmh serious
@giftsululu42743 сағат бұрын
Maganizo asatana
@Randy-er2xo3 сағат бұрын
Serious
@OssmanAbubaker-m5u2 сағат бұрын
Bola akanafa chakwera yo watikwana kwambiri Satana kumupha mzake iyesoafe
@RusselleStanley2 сағат бұрын
2030 woooo!
@AbrahamManyenga-v1gСағат бұрын
The sole reason I don't follow your stories, full of speculations based on fiction
@McshonWilliam2 сағат бұрын
No scrate under the sun 🤣🤣🤣🤣dj song done by chimangeni