BAKILI MULUZI TV 21 JUNE 2024 CHIGAWO CHA USIKU ..Political Prisoners in Chakwera's Police State

  Рет қаралды 51,854

Club Junta

Club Junta

8 күн бұрын

Be active and listen and watch what is happening around the world 🌍

Пікірлер: 113
@rexphiri7242
@rexphiri7242 5 күн бұрын
Zobisika mumatipatsila ndiinuyo wankulu Mulungu azikudalitsani nthawi yose tipatsen mphavu komaso apatsen uthenga anthu oti akwiye zen zen please boss
@YousufKadwala
@YousufKadwala 4 күн бұрын
Number one bakili muludzi tv
@powercharios2087
@powercharios2087 5 күн бұрын
Bakili muluzi TV is a best we always love you
@user-nf3ik3ff6y
@user-nf3ik3ff6y 5 күн бұрын
Bakili TV number one ❤
@DavidJackson-ox4xm
@DavidJackson-ox4xm 5 күн бұрын
I support Bakili Muluzi TV.
@LysonMtalika-tb6fk
@LysonMtalika-tb6fk 21 сағат бұрын
May God bless and protect you comrade, long live Bakili Tv
@NoelLangwani
@NoelLangwani 5 күн бұрын
Zobisika timadziwa chifukwa chainu boss naye chakwela amwalila adzamusata chilima 😭 😭😭😭
@user-pv9uk6sc3w
@user-pv9uk6sc3w 5 күн бұрын
Ndipo a Peter Mutharika adapilila minyozo ndipo mulungu adalitse Mutharika. Sanamange munthu. MCP ndi yakupha, ndipo sitilora dictator.
@giftdulamkalenga7344
@giftdulamkalenga7344 5 күн бұрын
May Allah bless you ine or mutawulura zoipa zichits bambo anga sindingskusiken. Long live The Dcccc mcp amanga Akaluwa to threaten fredokisi
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 6 күн бұрын
Can't wait bro, always listen to ur station alongside limpopo FM ❤
@MisheckAselo
@MisheckAselo 5 күн бұрын
Munthu akamumanga ndiye kuti akunena zoona tasiyeni achina Bon kalindo, mukamamanga anthu choncho simukudziwa kuti mukuonjezela mkwio kwa malawi, choti mudziwe mudzachoka pamenepo, nanunso adzakumangani 😮
@user-ku3gk4fz5i
@user-ku3gk4fz5i 3 күн бұрын
Ndipo inu bakili muluzi,ine pemphero langa ndiloti musadzafe mpaka ambuye adzakupezeni muli moyo, muwelenge yohene 11:25-26 kuti muchite umboni
@cynthiakananji1608
@cynthiakananji1608 5 күн бұрын
Koma ineyo azikhalewa andisekesa,😂😂😂😂akut anaoneka bwino atawaika makutu afisi😂😂😂😂😂
@sharonicier001
@sharonicier001 5 күн бұрын
🤣🤣🤣🤣😂😂😂
@ChikuMega
@ChikuMega 4 күн бұрын
Big up brother pitixan kutiphuzisa achinyamatafe ngt mne amatiphuzisira achilima❤💪
@marryphili5419
@marryphili5419 5 күн бұрын
Iwe wukutukwana apa zeru wulibe ngati ndiwe WA MCP tangokhara chete anthu akupha inu zisiru
@Anthonymendos
@Anthonymendos 5 күн бұрын
Zonse paja greci Chinga adayankhula zokhuza zokhuza kulanda u plezident, ndi asatanic a MCP
@cephasnkhoma2301
@cephasnkhoma2301 4 күн бұрын
Powerful TV
@marygoza1205
@marygoza1205 5 күн бұрын
Mu kuononga ndalama za anthu osauka zomwezi mpaka kuyitanitsa anthu from mapiko kunja kuti azafufuze are you serious Mr minister? Bakali muluzi ndi Munthalika akhala akujambulidwa a cartoon komanso kuyimbidwa mu nyimbo sanayambe amangapo munthu. Even Jacob Zuma mwakhala akutukwanidwa even kupangidwa cartoon but sanamangepo anthu. Osayiwala kuti ukakwera pa nsanga pa njovu osamati kunja kulibe mame. God is watching at Malawi one day is one day
@MussaAsidi
@MussaAsidi 5 күн бұрын
I pray for you God bless you
@MalikiAlex-wn8jc
@MalikiAlex-wn8jc 5 күн бұрын
Yeah Kodi osamadzitenga ngati madolo amenetu muli mu bomatu yeah ❤😂🎉
@user-pv9uk6sc3w
@user-pv9uk6sc3w 5 күн бұрын
Awatutse a Kamlepo Kalua ndi Bon Kalindo, tili mu democracy. Chakwera ndi boma lake la MCP lalephera, tatopanawo.
@JoybJohn-s6t
@JoybJohn-s6t 5 күн бұрын
Ku Malawi kulibe freedom of expression 😢
@user-gg6uh2wo4x
@user-gg6uh2wo4x 5 күн бұрын
Best tv
@sanuhabdullah5998
@sanuhabdullah5998 5 күн бұрын
Anduna awa di ambutuma kuyitana anthu kucha za nkhani imeneyi malo molimbana Dziko litukuke cmc
@brightcharlie2396
@brightcharlie2396 5 күн бұрын
Angoni analakwanji km RIP legend chilima 😭😭😭
@alexmkolongo3089
@alexmkolongo3089 5 күн бұрын
Awa zimene akudziwa ndikugwetsa kwacha basi
@shayrafernandeslatif9556
@shayrafernandeslatif9556 5 күн бұрын
MTSRIP 🌹,we are all mourning with you the families ifeso takhudziwa kwambiri,imfa yosayiwalika😢
@user-cu8wy9rz3b
@user-cu8wy9rz3b 5 күн бұрын
Boss you should be making your own vids koma. Leave bakili tvs videos to his channels, thus the problem yaife ku malawi...we take someone's song n put pa channels yathu😊....it's not own
@DinopianoVascoPianoVasco-m3g
@DinopianoVascoPianoVasco-m3g 5 күн бұрын
Otukwana bakili muluzi tv simuthu ndi satana komanso ndi khumba
@DizayaLikhunye
@DizayaLikhunye 4 күн бұрын
Kkkkkk ifeyo tiripo mr kkkkkk akunama
@NoelKhwimba-bh3ts
@NoelKhwimba-bh3ts 5 күн бұрын
Inutu akumanga bakiri muluzi TV sinu mungofuna ma views
@ChisomoKandikole
@ChisomoKandikole 4 күн бұрын
My God prossed keep kuti muzitiuxa zambiri
@user-vm7iz6oz6r
@user-vm7iz6oz6r 5 күн бұрын
Maiko USi wamupereka chilima mm zimu wa chilima use mutendere😭
@sharifujoe7633
@sharifujoe7633 5 күн бұрын
Kkkkkkkkkk Skelton ngoma😂😂😂 yahhhh Malawi wanga ine
@user-hx6ly3cl8m
@user-hx6ly3cl8m 3 күн бұрын
Apato Boma Ngati lamanga kamulepo kaluwa ndiye Kuti nawoso nkulu wasilikali amangidweso sinanga kamulepo amumanga dzimene ananena
@Yungjoe786
@Yungjoe786 5 күн бұрын
Malawi on 🔥 🔥 🔥 🔥
@AngellahPhiri-wy6xl
@AngellahPhiri-wy6xl 5 күн бұрын
Ambwiyewa tidawavulira kare chipewa
@eliaskachali-xn2ve
@eliaskachali-xn2ve 5 күн бұрын
Chakwera tamusiyeni kamulepo kaluwa ndi boni kalindo, chakwera uziwe Kuti una Wana vamachero vikumanyikwa Yai , Wana wako chakwera wazamuwa pa suzgo musogolo tizamuwa Landa Chuma chose Dtn without Try, ziko ili lapasi likuzungulira .uzalira Lazarus takusungila mawng
@Yungjoe786
@Yungjoe786 5 күн бұрын
We belong to Allah and to Him we shall return 😥😥😥
@MorganBanda-oc2jx
@MorganBanda-oc2jx 5 күн бұрын
koma siwonse angakhukonde ayi. anthu ena njoka ndthu ndipo bambo chilima anafera zaini
@johnmiselo2230
@johnmiselo2230 4 күн бұрын
😢😢😢😢😢😢 continue giving us good news 🗞️ like this
@chimwemwemorris6827
@chimwemwemorris6827 5 күн бұрын
Zoonadi usi analinthira kuwiri kwamwalira kwachilima sitinanvepo chomwe anayakhura kaporoamenei
@user-co3wr3rn4h
@user-co3wr3rn4h 6 күн бұрын
Iwe watukwana bakili tv naweso pathako pako nyawu mwapha chilima ndinu ndipo ziko likusawuka zinthu zamuvutani mu kuwona ngati anthu azakuvotelani palibe never never munthu, akamakususani basi mwayamba kumutukwana basi nyawu inu 2025 kuphana kuphana mu kuwona ngati tukuwopani iyaa
@AladenKachewere
@AladenKachewere 6 күн бұрын
👍
@ArabJames-de7fx
@ArabJames-de7fx 5 күн бұрын
@user-ku3gk4fz5i
@user-ku3gk4fz5i 3 күн бұрын
Ndizoodi mwanenazi achimwene
@Thewarrior7093
@Thewarrior7093 5 күн бұрын
Agalu amenewa aonjeza
@kondwamlungu8384
@kondwamlungu8384 5 күн бұрын
Vyachitima chomene titimalenge tosa
@eliaskachali-xn2ve
@eliaskachali-xn2ve 5 күн бұрын
Chakwera uzamuli pulika kuwawa ziko lapasi tizakulanda Chuma chose ndi nduna Zakozonse
@MasterAkidu-cz4fb
@MasterAkidu-cz4fb 5 күн бұрын
Malawi defence Army ikungoyang'ana?...zachamba zokha zokha... Malawi ikhala ngati Sudan...zoona akulu akulu andale akungoyang'ana zimenezo
@DennisDonework
@DennisDonework 5 күн бұрын
Koma bakili muluzi tv mmmmm usazafe sanga
@Trancy-xt4py
@Trancy-xt4py 5 күн бұрын
Chakwera asatirat chilima ngat akuona ngat iye ndiwa panazare tiona achakwera thawi yanu ikafika mufera nyumba inuyo
@user-co3wr3rn4h
@user-co3wr3rn4h 6 күн бұрын
Panji nikuyowoyele muchitumbuka pamatako pako ulichindele chomene nkhana vimavi vako we love bakili muluzi tv our best Chanel ise luta waka uko kutali ungatikwitiska
@rachelkaunda
@rachelkaunda 5 күн бұрын
Akulu Inu kutuka nthena yayi please fear God musanayulutse Mau mkamwa mwanu think about God first there is judgement day after this life your words are too much before it is too late receive Jesus Christ
@Extratremendouszeus
@Extratremendouszeus 5 күн бұрын
Mumatenga ma audio mochedwa Iyi inatuluka dzulo,inu mwapanga upload lero
@ChipilipiroMtsukwamwale
@ChipilipiroMtsukwamwale 5 күн бұрын
Big mutipatsireko mbiiri ya asing'anga abwino kumalawi kuno, mwina tiyeseko matsenga abwino. 14:36
@MackCent-ee8ys
@MackCent-ee8ys 5 күн бұрын
Zimenezo ndie zoona bwana
@user-pl8kw3dc9d
@user-pl8kw3dc9d 5 күн бұрын
Kod chakwera ndi mubusa otani wankhaza chonchi??
@augustMag
@augustMag 5 күн бұрын
Chilungamo chokha chokha Bakili Muluzi TV ndiyokhayo imatiuza zoonadi zokhazokha kuposanso Ndipo pitilizani osaopa kuyima pachoona Mulungu Ali kumbali yanu nthawi zonse kukutetezani mpaka kuyitanisa anthu Kuja kuti azakucheni kuti kodi angakupeze kuti sangaone kuti Mulungu samalira kuti anthu amene amayima pachifuniro Cha Choona Samawapereka mmanja mwa adani awo? Amphunzirepotu pamenepo sangakupezeni kapena kudziwa kumene Inu muli Ambuye wazatheka bwanji apitilize kuchitisa khungu mmaso mwao amenewa
@WilliamChunga-jv5lm
@WilliamChunga-jv5lm 5 күн бұрын
Kkkkkk
@SelemaniAlie
@SelemaniAlie 5 күн бұрын
Osadandaura wakulu mulungu alinanu thawizonse
@user-vm7iz6oz6r
@user-vm7iz6oz6r 5 күн бұрын
Afit mwachuluka et ndin mwapha vc takuonan mulungu achita nan
@YasinMusa-ym8lp
@YasinMusa-ym8lp 5 күн бұрын
Chakwera wakupa wapa chilima palibeso kubisanaso apa
@webstermbewe8395
@webstermbewe8395 5 күн бұрын
Club junta don't imitate bakili muluzi tv you are down grading yourself and you not go far
@user-xj9uy6wz7b
@user-xj9uy6wz7b 5 күн бұрын
😢😢😢
@johnlameck8366
@johnlameck8366 4 күн бұрын
😭😭😭😭
@JaccobMwenye
@JaccobMwenye 4 күн бұрын
Malo mopanga zitukuko ntchito Ku manga anthu bas
@webstermbewe8395
@webstermbewe8395 5 күн бұрын
Is this real
@user-oq5rg5mz7q
@user-oq5rg5mz7q 5 күн бұрын
Manganya ndi amene waphetsa chilima
@laurentbutao4084
@laurentbutao4084 5 күн бұрын
Politics so evil,nobody is clean in politics
@WisdomBlack-uu7zt
@WisdomBlack-uu7zt 5 күн бұрын
Ulemu wanu bigy mumati tsekula maso 🤔🤔
@GreenBadani
@GreenBadani 5 күн бұрын
🤦😢
@user-yj2dz5ej7r
@user-yj2dz5ej7r 5 күн бұрын
Osaphunzila uyu chimidzinso chili momcho
@PreciousPhiri-jr4sd
@PreciousPhiri-jr4sd 5 күн бұрын
Kma dzkolanthu ili😅
@omarjustin5518
@omarjustin5518 5 күн бұрын
MCP yazaza ndi mbuli ndi mphamva
@emiliaumali8360
@emiliaumali8360 5 күн бұрын
Akusowa zochita awa
@KelvinJpchimphepo-sh6nc
@KelvinJpchimphepo-sh6nc 5 күн бұрын
Koma bomali mmmm ayi zikomo
@MaggieChiomba
@MaggieChiomba 5 күн бұрын
🤣🤣😂😂😂azikhale andisekesa
@petrokagona1708
@petrokagona1708 5 күн бұрын
Mukumatenga zomwe a bakili muluzi TV akamba kale inu mkumapangirapo ndalama. Izizi tamva kale kuseriku, inu mwangopanga repost. Fotseki. Sakani nkhani zanu mutiwuze
@user-lv9vf6rf8r
@user-lv9vf6rf8r 5 күн бұрын
Boma ili lititha m'thambo aliko adziwe kuti watiika m'mavuto poika boma ili m'boma.
@user-mz8nw6nx6p
@user-mz8nw6nx6p 5 күн бұрын
Inuyo ndiye big man ndimakutsatani not enawa akuti Athanyiwa amangopanga za nonsense
@user-dp7bc7yy6s
@user-dp7bc7yy6s 5 күн бұрын
Eeeeeeeee km abale kd inu aboma munthu uyu amamuti Azikhale Ng'oma munamutenga kt? iiiiiii edit mpaka kuidabwa. Kd tiziti smartphone mwayamba kuigwiritsa ntchito ndi Mcp yomwe km zinaz mukumatichitisa manyaz
@EmanuelMlenga-sb5kw
@EmanuelMlenga-sb5kw 5 күн бұрын
Uziwuza amako zimenezo galu lwee
@CiprianoBindissone
@CiprianoBindissone 5 күн бұрын
Choka iwe galu
@SharifahWillardChampionn-rn8cm
@SharifahWillardChampionn-rn8cm 5 күн бұрын
Mmm watibwanji iwey pls ngat sukumafuna kumavera bakili muluzi TV pls just skip don't talk nonsense respect yourself manyi akwanu mbuzi
@SharifahWillardChampionn-rn8cm
@SharifahWillardChampionn-rn8cm 5 күн бұрын
Mmm watibwanji iwey pls ngat sukumafuna kumavera bakili muluzi TV pls just skip don't talk nonsense respect yourself manyi akwanu mbuzi
@SharifahWillardChampionn-rn8cm
@SharifahWillardChampionn-rn8cm 5 күн бұрын
Mmm watibwanji iwey pls ngat sukumafuna kumavera bakili muluzi TV pls just skip don't talk nonsense respect yourself manyi akwanu mbuzi
@zimmekapachika6784
@zimmekapachika6784 5 күн бұрын
Stupid president 🙄
@chadreckchibwithala1493
@chadreckchibwithala1493 5 күн бұрын
LIMPOPO USANAMIZE ANTHU IWE ULI GALU FOSEKI ISE KU NORTH NO DPP UWONASO TILIBE NTHAWI YA CHIPANICHA SANKHO . ALOMWE MKHAUKA
@AleksaWilliams-qc6cn
@AleksaWilliams-qc6cn 5 күн бұрын
Ingosiyani kumvera palibe yemwe amakukakamizani
@user-eh1mg3ww6d
@user-eh1mg3ww6d 2 күн бұрын
​@@AleksaWilliams-qc6cnsure
@robsontyg3928
@robsontyg3928 6 күн бұрын
Pathako pamako muluzi tv watsala ndiwe kumangidwa, mmadzitcha anthu omenyela ma ufulu, ufulu wa kumatako kwa Munthalika dzitsilu nyelo zanu
@Musa1828-l5d
@Musa1828-l5d 5 күн бұрын
Mukhaula agalu inu mudziwaso simunati, pathako pabambo ako galu iwe
@EllahChikwatu
@EllahChikwatu 5 күн бұрын
Opepera iwet ukuwatukwana amako osat amuthalika koma ukuzitukwana wekha manyaz ulibe
@robsontyg3928
@robsontyg3928 5 күн бұрын
@@EllahChikwatu you what iweso panyelo pamako, kodi inu ma refugees mmafuna mudzitisowetsa mtendele mudziko lathu why
@EllahChikwatu
@EllahChikwatu 5 күн бұрын
Ziko lake liti lomwe ukusowa tenderero kapolo iwe ... Akusowa tendere ndamene akuyakhula cilungamo kumagidwawo ndpo bambo opanda zeru iwe
@CeniaMayeni
@CeniaMayeni 5 күн бұрын
Eeeeee akulu mwamasukatu,zonse zomwe watukwana zipite kwa azibale ako uwagawanisa wekha, kukhala nyau ndi mavuto ndithu ntchito yozola manyi
@FrynessMoyo-to2du
@FrynessMoyo-to2du 5 күн бұрын
Zovesa chisoni Malawi wafika Pena pale zinthu sizikuyende kungovutika
@ChiyembekezoPhiri-sv8nw
@ChiyembekezoPhiri-sv8nw 5 күн бұрын
Tikumvera ndithu, mutesi atitha mkutinjata
@GreenBadani
@GreenBadani 5 күн бұрын
🤦😢
@gladysbonongwe1038
@gladysbonongwe1038 5 күн бұрын
Zoonadi ndithu, ife timadabwa kuti, oipawo amadziwa bwanji mapulani achilima
GWEDE-GWEDE PA 27 June 2024🙌🙌🙌
25:27
HOT 265
Рет қаралды 9 М.
Malawi President Lazarus Chakwera Demands The West Pay Full Price For African Resources
10:06
Final muy inesperado 🥹
00:48
Juan De Dios Pantoja
Рет қаралды 18 МЛН
She ruined my dominos! 😭 Cool train tool helps me #gadget
00:40
Go Gizmo!
Рет қаралды 58 МЛН
⬅️🤔➡️
00:31
Celine Dept
Рет қаралды 48 МЛН
Дибала против вратаря Легенды
00:33
Mr. Oleynik
Рет қаралды 3,3 МЛН
Zamalove Episode 10
27:13
Mibawa Studios
Рет қаралды 3 М.
Adaferanji olemekezeka bambo Sidik Mia?
25:14
Bakili Muluzi TV
Рет қаралды 140 М.
Chakwera wayamba nkhondo yolimbana ndi social media
7:45
Bakili Muluzi TV
Рет қаралды 67 М.
Comrade Lwara Lero pa 27 June Kugadada MCP mosaopa
24:21
Club Junta
Рет қаралды 12 М.
KUCHIPANI CHA UTM CHADABWITSA ANTHU🤔🤔
49:16
HOT 265
Рет қаралды 67 М.
BAKILI MULUZI TV  📺, CHIYAMBI CHA TSIKU LA VALENTINE🩷
12:10
ҚАЙНОНАСИГА ПРАНК 😨
0:15
BOBUR ALI
Рет қаралды 6 МЛН
Жизнь КОМАРА (смешное видео, юмор, приколы, поржать)
0:59
Натурал Альбертович
Рет қаралды 3,5 МЛН