Kuomba manja kusonyedza apule akulakhula dzazelu koma Malawi wazaza ndi dzipukwa dzawathu dziathu dzovala masuti dzongosamba ndindalama dzakuba ska lapamalawi
@user-yn4ee1qn2j20 күн бұрын
Akuluwa ndiabonza zedi
@user-gx5ht9gm3z25 күн бұрын
NO PAIN NO GAIN PLEASE NYAN IWE YAKULA CHIZUNGU AKUVE AMELIKA KUTHI AKUBANESO NAWE
@giftjamali820425 күн бұрын
Mr president you need to know kuti American peaple don't love corruption 😊
@user-gs7wc3nx3q25 күн бұрын
Chakwera mapazi ako iwe mbava iwe sataniki ingokhara chete paribe chazeru chomwe ukunenapo kamboro kako kodura ni sowo
Kuyankhula mopusa uku ukutiudza kut katangele kumalawi Kuno anthu tizipanga za umbava ndi kuba ndi mifuti chifukwa America imapanganso ndikanakutukwana wamva
@NditajiMaxwell-cz8ir24 күн бұрын
Inu munawalanda mphavu a vice anu kamba koganizilidwa pa zakatangale asanagamulidwe kt ndi olakwa nde zikusiyana pati ndi Americayo
@nahayopaulkim909725 күн бұрын
Agriculture mukuti yayambibwino???? So why last month munadandaula zoti kuMalawi kwagwa njala
@dianajobe416224 күн бұрын
Mmmmm akulunu mutiphetsa. America mukumuputayo amfunseni anzanu they'll tell u
@user-dk6yc8pl2m25 күн бұрын
Ukafna kuzuzula uzyakhula chizunga azkuva mbuz iwe
@IbrahimMatias-te1kc25 күн бұрын
Kkkkkkkk
@ChikondiChauma-ib9pg25 күн бұрын
Akut tinve zomwe awerenge pa chipepala kkkkkkk koma hot 265😅😅😅😅
@lymonmanda-cd8ol23 күн бұрын
He could address in English so that the US citizen themselves could hear or understand him properly, why he is addressing in chichewa today? Something is hidden. He is complaining about the American behaviour in a local language that's a sign of corruption hidden and defending which has taken place in Malawi
Chakwera kutumbu kwako wamva America ikunama mesa ukungokhalira kuba
@thulanimpphiri687325 күн бұрын
America no 1 ku Africa kunu mumadama ndi America chifukwa anakuzindikirani kuti ndinu akatangale. Alakwisa kulesa anthu 4 okha koma akanalesa nose muzikhala kumalawi komweko. Nose atsogoleri akanakupanga chimozimozi.