KWANUNKHA MWAZI KU MCP.

  Рет қаралды 39,209

LIKI-LIKI TELEVISION

LIKI-LIKI TELEVISION

15 күн бұрын

Пікірлер: 123
@user-un6qv6sj3h
@user-un6qv6sj3h 13 күн бұрын
❤❤❤iyiyi mwanena zogwila mtima lero mwaonetsa u independent wa times keep it up
@rosekaliwo5547
@rosekaliwo5547 13 күн бұрын
Ulamuliro wa nkhanza inde pano school fees anthu tikulephera kulipira ndiye Ana aphunzire motan mmmm ambuye atithandize
@user-zq3li3qw1m
@user-zq3li3qw1m 13 күн бұрын
Zoonadi
@xinalungu9616
@xinalungu9616 12 күн бұрын
For the first time Malawi can see great roads not just miyala ya madziko. I pray that Malawi wakes up. We should wake up n balance our forums
@rameckmauranagerald9783
@rameckmauranagerald9783 11 күн бұрын
Kuyakhula mopanda mantha. Komaso mwaphawi zofunikira kwaose amalawi pabwino mkuyamikirana. Poipapo dzuzurani, rangizani akapanda kumva arekeni!!!!🎉
@ElizabethMajiga
@ElizabethMajiga 13 күн бұрын
Apa ponkhapa mwawalakhulila amalawi🎉🎉🎉🎉🎉🎉
@IshumaelMbewe-d4t
@IshumaelMbewe-d4t 13 күн бұрын
Tidakhala ndi atsogoleri ophunzira angapo koma sitidatukike pa cbuma ndi zitukuko ndiye tidzayese mtsogoleri wa form 4
@BwanaGD
@BwanaGD 13 күн бұрын
Tisinthe flag yanthu ilindi mintundu yoyipa ntunduwake mmm ndiwachabe mutundu ya bendera yanthu imagwilitsidwa nthawizabili ndizinthu zakumidima panayenela kuyisintha bas
@Lee-lee-w1r
@Lee-lee-w1r 13 күн бұрын
Koma ndipo Simukunama. Taonani flag ya Kenya 🇰🇪 ndi ya malawi 🇲🇼 sizisiyana kwenikweni koma mmene zinthu zilili ku Kenya ndi kuno nzonvetsa chisoni
@user-lw2yp1rf4n
@user-lw2yp1rf4n 14 күн бұрын
Iyiyi nde yandifikapo ndithu big up Hot current 💪💪
@PetersenjMwale
@PetersenjMwale 13 күн бұрын
Mumapanga ma demo abwino not like born kalindo, thanx TTV
@GiftNyirenda-q9d
@GiftNyirenda-q9d 11 күн бұрын
Koma ma decision makers particularly politicians amamva zimenezi? Uthenga nde ndikwabwino and straight forward. Vuto aliyense angofuna iye ndi abale ake akamachoka, zawo zikhale ziyenda. ie alibe chikondi kwa a malawi koma kuzikonda
@RobertCosmas-bo1uo
@RobertCosmas-bo1uo 12 күн бұрын
Massive analysis this is good idea and solution zoonad katangale akhoza kutha zkufunika azitsogoleri odana ndizopusa that's right guys.
@HastingsJonathan
@HastingsJonathan 12 күн бұрын
Nelson Nelson 🤣🤣ukumaika ma flash et
@blessingsfalamenga4575
@blessingsfalamenga4575 10 күн бұрын
Anyamata inu get ready in 2025 boma lina likubwerari tikonze malawi you are good indeed.
@user-mh7cc8up4i
@user-mh7cc8up4i 12 күн бұрын
Apankunku ndi ndevi zamwayi mwayamba bho next time muzapose apa apa ndakayika kuti mudadya chikondamoyo we love you lots ❤
@kotking-xg7pp
@kotking-xg7pp 13 күн бұрын
MWALANKHULATU MWAMPHAMVU RELO NDIYAMIKE KWAMBIRI.
@lastonmasoatenganji-bs5gf
@lastonmasoatenganji-bs5gf 11 күн бұрын
Tikadali njira, sindazione munthu wa zaka 60 akukakamira kuyamwa bere la amache. Mkakawo udakoma chotani.
@user-sw6rz4tz3z
@user-sw6rz4tz3z 10 күн бұрын
Suzumilani mu MRA muwone zomwe zikuchitika especially in a hot activities eg boarders kkkk
@dumisanimoyo3152
@dumisanimoyo3152 13 күн бұрын
Amati mwanapiye anawonera make kunyera munyumba nde tiphe mayi wakeyooooo
@OssmanAbubaker-l5s
@OssmanAbubaker-l5s 9 күн бұрын
Zoonadi my brothers osaopa osapepesa zaka 4 palibe chanzeru olo chimodzi chimene achita awa a Tonse
@ChettoSongeah
@ChettoSongeah 10 күн бұрын
impressive guys Ndevu za mwai umaitha ndi nzako yo 🤞
@clintonhodda9830
@clintonhodda9830 13 күн бұрын
Koma a Brown mpinganjira mpaka liti osavomeleza kuti Mulungu sanafune kuti akhale president iiiii
@PetersenjMwale
@PetersenjMwale 13 күн бұрын
U guys u talking the really truth
@louisgolden
@louisgolden 13 күн бұрын
Mwauzeso kuti akugulileni track trauser kuti yikhale top and down
@user-sw6rz4tz3z
@user-sw6rz4tz3z 10 күн бұрын
Musogoleri akawoneka wa good future kumapha basi
@user-em3xq2th4g
@user-em3xq2th4g 4 күн бұрын
😢 Apa palibezoti bola baja bandani ni same thing those bantu
@xinalungu9616
@xinalungu9616 12 күн бұрын
Malawi has suffered leaders who kept us in the dark for years. Without water. Leaders that store n cut all rail lines to replace it with mangochi based vehicles. The nation suffered from leaders without teeth who paralized universities for almost a year. If asked, they would go on holiday in the USA. Now, are we promoting such leaders to come back? This is an opposition forum. Not a program that talks reality. None bias reporting is what this nation needs.
@SolokingChimzy-yt7dj
@SolokingChimzy-yt7dj 10 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂..ati sitidya kwaaaanu eishhhh anyamata anakalowa mu studio ndi mkwiyoo awa...Iman moona mtima ndimopanda mantha ngat Mikaya wa mu Bible yemwe anasutsana ndi mafumu ochuluka pozindikila kut zoyankhula zake ndizo zinali zoona
@christophermukaka7403
@christophermukaka7403 10 күн бұрын
To say the fact ma guys awawa amayankhula zoona koma kumtunda ku mmm
@dysonmasiye5736
@dysonmasiye5736 12 күн бұрын
Za katangalezi tinaluza munthu wofunikira kwambiri amene anali ndi masomphenya pa nkhani iyi....SKC 😢 tidzamlila mpaka kale...koma adaferanji?
@gracemkandawire8769
@gracemkandawire8769 12 күн бұрын
Brian alikuti Kodi? Amabebetsa
@user-em3xq2th4g
@user-em3xq2th4g 4 күн бұрын
❤😂😢 nkhani yagona pa utsogoleli, kwa anthu amene ukuvoteledwao, tinawavotela pachifukwa chiani?😢 Kd tinawavotela chifukwa choti mwaiwo tikuonamo muzimu wa utsogoleli? Kapena chifukwa choti tikumadyanawo? Apa tiwonepo apa, kwa Ife ngati ovota. Kwa iwo amene akhalapo atsogoleli, ndi iwo amene ali atsogoleli, Asanapange chiganizo chofuna kukhala mtsogoleli anayamba azifufuza okha kuti mwaiwo yilimo mphatso ya utsogoleli kapena ayi? Akulu akulu tisaname apa onse amene tawavotela awa ndi amene tikuwavotela awa akungogweramo chifukwa chokakamizidwa ndi anthu ane amene ali atidyenawo, chifukwa cha mzimu uwu uwu, woti tikamuona munthu ndikumuwuza kuti km inuyo kuti mukhale mtsogoleli anthu akhoza kukuvotelani zaziiii, mawa olira ndifetomwe, muMalawi alimo anthu anzelu ophunzira aliso ndi utsogoleli mkatimwao km chifukwa choti ndi osauka palibe munthu amene angawa votele, pano ndi izi zaka 60+ chifukwa chokonda kusankha bakawalala aba tilindicha zero chosangalasa ndichani kumuvotela munthu maba akukufiya pahoroh 😂 kpn kukumanga ndikukakusekera inside kirikiri😮
@nellybruhan5834
@nellybruhan5834 13 күн бұрын
Ine nde kumalawi kwandikwana😭😭😭😭😭😭 thupi lonse likumachita kuwawa ndikuganiza
@user-ec3xh4pc6t
@user-ec3xh4pc6t 13 күн бұрын
Dear bwelani mbalikuno bas
@nellybruhan5834
@nellybruhan5834 13 күн бұрын
@@user-ec3xh4pc6t kutiko kumeneko saka bag yanga ndapakililatu
@user-zo3bf3ec3g
@user-zo3bf3ec3g 11 күн бұрын
Nde mwati amagwila pati anyamata aja
@FosterMatchano
@FosterMatchano 12 күн бұрын
I like the conversation
@jelsonmlowoka8611
@jelsonmlowoka8611 13 күн бұрын
Zoti inali times television yooneledwa ndi anthu ambiri pano ndi history chabe hahaha ndaonela ma viewers ndi kuchuluka kwa ndemanga
@EdwinMakwangwala
@EdwinMakwangwala 13 күн бұрын
Ambiri amaonela but they reserve their comments but ndawakonda ma guys
@francismungu7749
@francismungu7749 12 күн бұрын
Guys mwasiya kugawa ma sweet ulemu wanu. Timayesa nanuso akudyesani chibansi
@mustafahassan9128
@mustafahassan9128 11 күн бұрын
Koma ndiye mwanena mosanyengeleratu
@stevephiri1043
@stevephiri1043 12 күн бұрын
Mmoziyi ndamene amalakwisa program amakonda kuwatchinga azinzakewo kuti asamasuke
@GraceZumazuma
@GraceZumazuma 13 күн бұрын
Keep it up times musalore akupatseni ma banz mudzitiimilira chonchi
@sparkdymon3429
@sparkdymon3429 13 күн бұрын
Iyi koma mwang,alulandi makosana abwana kutundako azizifusa makamaka achekwela ndimbava ndifukwa akopa ACB
@user-un8yq1gg2i
@user-un8yq1gg2i 12 күн бұрын
Hahahaha koma iyiyi nde ndiyong'alura kuyipatu kkkkkkk
@user-no5eb7rp1o
@user-no5eb7rp1o 13 күн бұрын
Eeeeee anyamata relo mwatokota kkkkkk muli bho kwambiri mwaveka ❤❤❤
@khwimamtonga954
@khwimamtonga954 13 күн бұрын
Mmmm Zikhale Ng'oma nawoso akufuna u Vice President ku MCP? Mmmm awa ai body structure
@eliffagondewe8214
@eliffagondewe8214 13 күн бұрын
Kkkkkkk 🔥🔥
@obviouskedson6483
@obviouskedson6483 13 күн бұрын
Ife timamva nanu kukoma chifukwa mumayankhula chilungamo ,ndipo nthawi ya program yanuyo muionjezele mabwana
@user-pv9uk6sc3w
@user-pv9uk6sc3w 13 күн бұрын
Yeah! This is hot for sure.
@augrinngunga8031
@augrinngunga8031 12 күн бұрын
Mwalakhulako zazerutu, mukamadya ma bazi guys times izakhala Ngati MBC yoonera achakwera okha
@user-ux8bc6wy1i
@user-ux8bc6wy1i 12 күн бұрын
Iyi ndye hot current yen yen 🔥🔥🔥
@dysonmasiye5736
@dysonmasiye5736 12 күн бұрын
Hahahaha akuti 👇 "Sitidya kwanu!" 😅😅😅😅
@DalisoulThom
@DalisoulThom 13 күн бұрын
Chanzelu apha chilima+anthu 8 kumphatizapo kasambala
@amosmuluwane4182
@amosmuluwane4182 11 күн бұрын
Lelotu anyamata mwawalankhulila amalawi pitilizani
@user-to5of3ks3g
@user-to5of3ks3g 13 күн бұрын
Nice message
@user-si7po9sd5i
@user-si7po9sd5i 13 күн бұрын
The curtain in the temple is about to be torn, we are waiting eagerly
@EdwinMakwangwala
@EdwinMakwangwala 13 күн бұрын
The problem of you and us as Malawians we always celebrate when someone fail, this is very bad and ugly kkkkkk
@user-si7po9sd5i
@user-si7po9sd5i 13 күн бұрын
Sometimes it's good to understand the message properly,who is celebrating here? If someone is failing to run the affairs of the country,how does that concern me?,he has 23 advisors,What is their job?what are all the advisors doing, this is high level filth,Justice hurts.
@Lee-lee-w1r
@Lee-lee-w1r 13 күн бұрын
@@user-si7po9sd5iexactly tell this person the truth
@Lee-lee-w1r
@Lee-lee-w1r 13 күн бұрын
@@EdwinMakwangwalait’s not celebrating them. It’s celebration that the truth about them will be coming out
@EugeneChiyenda
@EugeneChiyenda 13 күн бұрын
Kma iyiyi mwang'alula🥳
@jamusnamwino-br2iz
@jamusnamwino-br2iz 13 күн бұрын
anyamata musamale muphedwatu mcp sifuna anthu oyankhula chilungamo
@raytavares2256
@raytavares2256 13 күн бұрын
That's why they assassinated malemu mnyamata woganiza boo Adamupha KS and they think we have mastered the crime and they will not be able to be caught and arrested.
@DalitsoulNchengah
@DalitsoulNchengah 12 күн бұрын
Ulemu
@Erickasonya-uw8yw
@Erickasonya-uw8yw 10 күн бұрын
Bravo guys mumakwana
@MemoryKamanga-jv4jh
@MemoryKamanga-jv4jh 13 күн бұрын
Number one brothers
@sulleahmnyimbili1362
@sulleahmnyimbili1362 13 күн бұрын
Well spoken
@sungirenikampu8630
@sungirenikampu8630 13 күн бұрын
Guys mumatha keep it up
@StevenFombe
@StevenFombe 13 күн бұрын
If yuo steal with sorrounded one day all will 😂😂
@JuuuKomba
@JuuuKomba 13 күн бұрын
China chake kuseliku nkumati ndikupeleza 7 kwa ten mfiti 😢
@BlessingsSeleman
@BlessingsSeleman 13 күн бұрын
Zofunika osambisala munda wa mtedza timadabwatu koma apa mwabwera
@fatimautilah5648
@fatimautilah5648 13 күн бұрын
Ati sitidya kwanu kmatu Mr wonder
@eliffagondewe8214
@eliffagondewe8214 13 күн бұрын
Watopera akanganya amenewa.
@user-zq3li3qw1m
@user-zq3li3qw1m 13 күн бұрын
Every day kusokesa uniform ya police zovuta zedi
@PrinceBlessings-bv5bs
@PrinceBlessings-bv5bs 12 күн бұрын
😂😂😂😂😂 apa mwatha manthatu
@ShagaFologonya
@ShagaFologonya 13 күн бұрын
Mmakwana uzo ndi mzao
@Benson-cf6qd
@Benson-cf6qd 13 күн бұрын
Aaah koma ma boys inuyo mumakwana 😅
@StevenFombe
@StevenFombe 13 күн бұрын
Why big people wear tinted sun glasses
@user-im7sc2my4w
@user-im7sc2my4w 13 күн бұрын
Komadi ma junior police akuvutika ,srs
@abunaseem6866
@abunaseem6866 11 күн бұрын
Ku painter eti?
@yamiecharles
@yamiecharles 14 күн бұрын
Mmmmm tiyeni ticheze bwino
@shephardlonex3371
@shephardlonex3371 13 күн бұрын
Koma zikhale ng'omayo nde ayi aaaaa
@lucianogeoffrey4275
@lucianogeoffrey4275 13 күн бұрын
Vuto lolandililatu zanu tinkhope tanuto nditamanyaziii😢
@user-qe3iu7jy4h
@user-qe3iu7jy4h 13 күн бұрын
Ayi palibe chabwino kulibwino undindo asiyile wena
@mathewsmakina7845
@mathewsmakina7845 13 күн бұрын
Mukamatero tililimodzi pamenepo
@dumisanimoyo3152
@dumisanimoyo3152 13 күн бұрын
Iyayi bomali linaziyipisila kale
@madsondzintchira9831
@madsondzintchira9831 10 күн бұрын
Abodza awa sanena zoona komaso oopa kwabasi bwanji analephela kutuuza zoona nthawi ya maliro anyamata wanthu skc timakubukila zbs isakudziwa ndalama pa imfa ya bingu atolankhani amakwela mu tengo kuti anene zoona Koma pano mmmmmmmmmma radio ake cabbage oneka oliba koma mkati madzi okhaokha
@Yamikaniwalasi
@Yamikaniwalasi 13 күн бұрын
😂😂😂😂
@ThomsonmbiziGwazafupa-rr6zg
@ThomsonmbiziGwazafupa-rr6zg 13 күн бұрын
Brilliant idea 💡
@user-ce8ud5ed5y
@user-ce8ud5ed5y 13 күн бұрын
Mumakwana gayez
@EllenChione
@EllenChione 13 күн бұрын
Ndakutayilani kamtengo guys
@RuthMkangala
@RuthMkangala 13 күн бұрын
Koma kumeneko
@McstanleyChalema
@McstanleyChalema 13 күн бұрын
Mtsogoleri yekhayo adali ndi kuthekera koteroko adali Akamuna a Bingu seconded by Akamuna Dr Saulosi
@RitaKainga
@RitaKainga 13 күн бұрын
Exactly!
@JimmyGenda
@JimmyGenda 13 күн бұрын
Hello Guys. Please continue hitting the nail on the head.
@user-wi8xw9qh7n
@user-wi8xw9qh7n 13 күн бұрын
Chakwera must go before September pls God is looking for us
@RitaKainga
@RitaKainga 13 күн бұрын
Thanks you 2 guys there,Komano kod mmesa achakwera anatiuza Kut adzamanga aliyense ochita katangale m'boma lawo? Ndy chilowele amenebanamuona mkumanga ndi achilima okha? Plz plz t mkwabwino kusangalatsa Mulungu than munthu mzako
@RemaniNkhoma
@RemaniNkhoma 13 күн бұрын
bora bingu ndi ng'ono wake pta osati uyuyu chakwerayu ndimbzi
@ChiccoDzikolo
@ChiccoDzikolo 13 күн бұрын
More fire gentlemen, Malawi wathu ndiyemweyu,Osaopa kuzilangiza nkhutukumve ndi mbala zimenezi
@ChifundoNinje
@ChifundoNinje 13 күн бұрын
Chilungamo chimamasula, azibambo inuyo mulungu azikudalisani ndikutetezani mukugwila tchito, from cape town
@EnockBwaila
@EnockBwaila 13 күн бұрын
Apapa ndiye mwabwera madolo ulemu wanu that is democracy
@DavieKalonga-y5j
@DavieKalonga-y5j 13 күн бұрын
Pitilizani kumatiyakhulira chilungamo pa hot current
@INNOCENTMOFOLO-io8tg
@INNOCENTMOFOLO-io8tg 13 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂😂 ndemvu zamwayi apolice akumadula zikhadabo atavala nsapato kkkkkkkkkk
@CalvinThomson-ys5zf
@CalvinThomson-ys5zf 13 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂 uyu ndiwamwano ati kuwenga zikhadabo autavala nsapato
@INNOCENTMOFOLO-io8tg
@INNOCENTMOFOLO-io8tg 13 күн бұрын
@@CalvinThomson-ys5zf kkkkkkkkk akutero kuli kutha kwa nsapato kkkk
@juliochiwalo
@juliochiwalo 13 күн бұрын
Pamene apolisi akusowa nsapato nawo ma pensioners sakulandira ndalama zawo ena mpaka zaka panopa katangale mbona wa chulukadi
@PetersenjMwale
@PetersenjMwale 13 күн бұрын
Mumapanga ma demo abwino not like born kalindo, thanx TTV❤
@PetersenjMwale
@PetersenjMwale 13 күн бұрын
Mumapanga ma demo abwino not like born kalindo, thanx TTV
@PetersenjMwale
@PetersenjMwale 13 күн бұрын
U guys u talking the really truth
@user-dc7qq9yz3v
@user-dc7qq9yz3v 13 күн бұрын
Matha
@RuthMkangala
@RuthMkangala 13 күн бұрын
Koma kumeneko
@PetersenjMwale
@PetersenjMwale 13 күн бұрын
Mumapanga ma demo abwino not like born kalindo, thanx TTV
@GiftNyirenda-q9d
@GiftNyirenda-q9d 11 күн бұрын
Vuto lanu lopanga compare anthu awiri osiya, zolinga zosiya, koma kulephela kusiyanitsa.
@PetersenjMwale
@PetersenjMwale 13 күн бұрын
Mumapanga ma demo abwino not like born kalindo, thanx TTV
Full speech: Donald Trump speaks on final night of RNC
1:33:11
NBC News
Рет қаралды 180 М.
ЧУТЬ НЕ УТОНУЛ #shorts
00:27
Паша Осадчий
Рет қаралды 6 МЛН
Mom's Unique Approach to Teaching Kids Hygiene #shorts
00:16
Fabiosa Stories
Рет қаралды 9 МЛН
Donald Trump’s full speech at the RNC
1:32:16
ABC News
Рет қаралды 435 М.
Special report: Major computer outages occur worldwide
7:14
NBC News
Рет қаралды 1,7 МЛН
MUNTHU WAMULUNGU kuling'alura boma la CHAKWERA...lalephera
4:43
LIKI-LIKI TELEVISION
Рет қаралды 26 М.
CRUISE 5 WITH BYSON KAULA PART 2 - 20 JUNE 2021
59:55
Joab Frank Chakhaza
Рет қаралды 48 М.