Tidakhala ndi atsogoleri ophunzira angapo koma sitidatukike pa cbuma ndi zitukuko ndiye tidzayese mtsogoleri wa form 4
@BwanaGD13 күн бұрын
Tisinthe flag yanthu ilindi mintundu yoyipa ntunduwake mmm ndiwachabe mutundu ya bendera yanthu imagwilitsidwa nthawizabili ndizinthu zakumidima panayenela kuyisintha bas
@Lee-lee-w1r13 күн бұрын
Koma ndipo Simukunama. Taonani flag ya Kenya 🇰🇪 ndi ya malawi 🇲🇼 sizisiyana kwenikweni koma mmene zinthu zilili ku Kenya ndi kuno nzonvetsa chisoni
@user-lw2yp1rf4n14 күн бұрын
Iyiyi nde yandifikapo ndithu big up Hot current 💪💪
@PetersenjMwale13 күн бұрын
Mumapanga ma demo abwino not like born kalindo, thanx TTV
@GiftNyirenda-q9d11 күн бұрын
Koma ma decision makers particularly politicians amamva zimenezi? Uthenga nde ndikwabwino and straight forward. Vuto aliyense angofuna iye ndi abale ake akamachoka, zawo zikhale ziyenda. ie alibe chikondi kwa a malawi koma kuzikonda
@RobertCosmas-bo1uo12 күн бұрын
Massive analysis this is good idea and solution zoonad katangale akhoza kutha zkufunika azitsogoleri odana ndizopusa that's right guys.
@HastingsJonathan12 күн бұрын
Nelson Nelson 🤣🤣ukumaika ma flash et
@blessingsfalamenga457510 күн бұрын
Anyamata inu get ready in 2025 boma lina likubwerari tikonze malawi you are good indeed.
@user-mh7cc8up4i12 күн бұрын
Apankunku ndi ndevi zamwayi mwayamba bho next time muzapose apa apa ndakayika kuti mudadya chikondamoyo we love you lots ❤
@kotking-xg7pp13 күн бұрын
MWALANKHULATU MWAMPHAMVU RELO NDIYAMIKE KWAMBIRI.
@lastonmasoatenganji-bs5gf11 күн бұрын
Tikadali njira, sindazione munthu wa zaka 60 akukakamira kuyamwa bere la amache. Mkakawo udakoma chotani.
@user-sw6rz4tz3z10 күн бұрын
Suzumilani mu MRA muwone zomwe zikuchitika especially in a hot activities eg boarders kkkk
@dumisanimoyo315213 күн бұрын
Amati mwanapiye anawonera make kunyera munyumba nde tiphe mayi wakeyooooo
@OssmanAbubaker-l5s9 күн бұрын
Zoonadi my brothers osaopa osapepesa zaka 4 palibe chanzeru olo chimodzi chimene achita awa a Tonse
@ChettoSongeah10 күн бұрын
impressive guys Ndevu za mwai umaitha ndi nzako yo 🤞
@clintonhodda983013 күн бұрын
Koma a Brown mpinganjira mpaka liti osavomeleza kuti Mulungu sanafune kuti akhale president iiiii
@PetersenjMwale13 күн бұрын
U guys u talking the really truth
@louisgolden13 күн бұрын
Mwauzeso kuti akugulileni track trauser kuti yikhale top and down
@user-sw6rz4tz3z10 күн бұрын
Musogoleri akawoneka wa good future kumapha basi
@user-em3xq2th4g4 күн бұрын
😢 Apa palibezoti bola baja bandani ni same thing those bantu
@xinalungu961612 күн бұрын
Malawi has suffered leaders who kept us in the dark for years. Without water. Leaders that store n cut all rail lines to replace it with mangochi based vehicles. The nation suffered from leaders without teeth who paralized universities for almost a year. If asked, they would go on holiday in the USA. Now, are we promoting such leaders to come back? This is an opposition forum. Not a program that talks reality. None bias reporting is what this nation needs.
@SolokingChimzy-yt7dj10 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂..ati sitidya kwaaaanu eishhhh anyamata anakalowa mu studio ndi mkwiyoo awa...Iman moona mtima ndimopanda mantha ngat Mikaya wa mu Bible yemwe anasutsana ndi mafumu ochuluka pozindikila kut zoyankhula zake ndizo zinali zoona
@christophermukaka740310 күн бұрын
To say the fact ma guys awawa amayankhula zoona koma kumtunda ku mmm
@dysonmasiye573612 күн бұрын
Za katangalezi tinaluza munthu wofunikira kwambiri amene anali ndi masomphenya pa nkhani iyi....SKC 😢 tidzamlila mpaka kale...koma adaferanji?
@gracemkandawire876912 күн бұрын
Brian alikuti Kodi? Amabebetsa
@user-em3xq2th4g4 күн бұрын
❤😂😢 nkhani yagona pa utsogoleli, kwa anthu amene ukuvoteledwao, tinawavotela pachifukwa chiani?😢 Kd tinawavotela chifukwa choti mwaiwo tikuonamo muzimu wa utsogoleli? Kapena chifukwa choti tikumadyanawo? Apa tiwonepo apa, kwa Ife ngati ovota. Kwa iwo amene akhalapo atsogoleli, ndi iwo amene ali atsogoleli, Asanapange chiganizo chofuna kukhala mtsogoleli anayamba azifufuza okha kuti mwaiwo yilimo mphatso ya utsogoleli kapena ayi? Akulu akulu tisaname apa onse amene tawavotela awa ndi amene tikuwavotela awa akungogweramo chifukwa chokakamizidwa ndi anthu ane amene ali atidyenawo, chifukwa cha mzimu uwu uwu, woti tikamuona munthu ndikumuwuza kuti km inuyo kuti mukhale mtsogoleli anthu akhoza kukuvotelani zaziiii, mawa olira ndifetomwe, muMalawi alimo anthu anzelu ophunzira aliso ndi utsogoleli mkatimwao km chifukwa choti ndi osauka palibe munthu amene angawa votele, pano ndi izi zaka 60+ chifukwa chokonda kusankha bakawalala aba tilindicha zero chosangalasa ndichani kumuvotela munthu maba akukufiya pahoroh 😂 kpn kukumanga ndikukakusekera inside kirikiri😮
@nellybruhan583413 күн бұрын
Ine nde kumalawi kwandikwana😭😭😭😭😭😭 thupi lonse likumachita kuwawa ndikuganiza
@user-ec3xh4pc6t13 күн бұрын
Dear bwelani mbalikuno bas
@nellybruhan583413 күн бұрын
@@user-ec3xh4pc6t kutiko kumeneko saka bag yanga ndapakililatu
@user-zo3bf3ec3g11 күн бұрын
Nde mwati amagwila pati anyamata aja
@FosterMatchano12 күн бұрын
I like the conversation
@jelsonmlowoka861113 күн бұрын
Zoti inali times television yooneledwa ndi anthu ambiri pano ndi history chabe hahaha ndaonela ma viewers ndi kuchuluka kwa ndemanga
@EdwinMakwangwala13 күн бұрын
Ambiri amaonela but they reserve their comments but ndawakonda ma guys
The curtain in the temple is about to be torn, we are waiting eagerly
@EdwinMakwangwala13 күн бұрын
The problem of you and us as Malawians we always celebrate when someone fail, this is very bad and ugly kkkkkk
@user-si7po9sd5i13 күн бұрын
Sometimes it's good to understand the message properly,who is celebrating here? If someone is failing to run the affairs of the country,how does that concern me?,he has 23 advisors,What is their job?what are all the advisors doing, this is high level filth,Justice hurts.
@Lee-lee-w1r13 күн бұрын
@@user-si7po9sd5iexactly tell this person the truth
@Lee-lee-w1r13 күн бұрын
@@EdwinMakwangwalait’s not celebrating them. It’s celebration that the truth about them will be coming out
That's why they assassinated malemu mnyamata woganiza boo Adamupha KS and they think we have mastered the crime and they will not be able to be caught and arrested.
@DalitsoulNchengah12 күн бұрын
Ulemu
@Erickasonya-uw8yw10 күн бұрын
Bravo guys mumakwana
@MemoryKamanga-jv4jh13 күн бұрын
Number one brothers
@sulleahmnyimbili136213 күн бұрын
Well spoken
@sungirenikampu863013 күн бұрын
Guys mumatha keep it up
@StevenFombe13 күн бұрын
If yuo steal with sorrounded one day all will 😂😂
@JuuuKomba13 күн бұрын
China chake kuseliku nkumati ndikupeleza 7 kwa ten mfiti 😢
@BlessingsSeleman13 күн бұрын
Zofunika osambisala munda wa mtedza timadabwatu koma apa mwabwera