💙💙💙APM you're my vote today. Kaya upanga kampeni kapena ayi. Ndidzabwera ku Malawi only to vote for you. But now start looking for a successor to maintain the party.
@user-uc1pd1tc2xАй бұрын
Me too i will vote for him Ndipo ndikuona kuchedwa❤❤
Koma ndiye, kukakamira mtunda wopanda madzi- za zii!
@user-gq6nj6yo6fАй бұрын
❤❤❤❤
@PatrickViyacheАй бұрын
Ulemu wanu adad?
@bysongeorge3243Ай бұрын
Yes , he is our hope but he is surrounded by some ill mannered individuals who also participated in bad behaviours during their past rule of government. They are quietly hiding behind him..
@tasmania527Ай бұрын
Very true brother and they're the main beneficiaries of APM's presidency. We don't need a leader who is as good as senile and who is being controlled by selfish minds. His time is past.
@user-oc9vl9xz8eАй бұрын
A professor nawonso analephela zinthu zina kuzikomza zimene Chakwela wazikwanilisa padzuko palibe wabwino Maka a ndalewa onse ndi zunkhanila zikha zika...
@user-oc9vl9xz8eАй бұрын
Munthawi yawo Magetsi amavuta vuta kwambili lero ndi mbili yakale ikakhala njala pa Malawi ndi culture yaba Malawi no wonder
@LamseyLazarous-dl5qdАй бұрын
Suka. Wen uthetha kaka
@ShelifibraheemАй бұрын
Dzikolathu ndilomweli ena akuesela kung'amba koma bwana mulisoka
@Randy-er2xoАй бұрын
Adzalowanso amcp ayamba kusanza😂😂😂😂😂😂😂
@BwanaGDАй бұрын
Ndilipano daaaa
@martinsailesi1731Ай бұрын
Please when you upload the videos make sure you take the shit sound out, doesn't sound sense.
@MaggieMuhone-r7mАй бұрын
Tikukudikililani. Apm
@SaidiMbawa-st6bjАй бұрын
Azikoza munjila yanji ngati sadali mu boma koma malubino kumangofa ngati nkhuku
@user-vl8uw8mc3uАй бұрын
Chiyembekezo cha amalawi chokhachi basi
@WhiteRichard-cw2foАй бұрын
Athu. Akudikila inu adad
@user-ez1kc7zp9mАй бұрын
Sizikumveka ntaaa
@MynessChirwaАй бұрын
Boma iloo
@ImranAlisen-zb9szАй бұрын
amalawi taphuzira sitidzayesanso
@spargomwАй бұрын
Ndipo tachimina😂😂😂 komaso tachilàpa, boraso kuika munthu osapemphera pa mpando😂😂😂😂😂.. Adad my vote❤❤❤❤❤