Chakwera kupha munthu kamba ka udindo? Ayi ndithu Mulungu akukhathe.
@user-pv9uk6sc3w11 күн бұрын
Nkhani imeneyo ndi yabwino, koma Manganya awatangwanikitsa chabe, mwamunva mzimai uja, Usi ndi wa independent, awapusitsa chabe apa.
@UsenLashid12 күн бұрын
Ulemu wanu akaliyati team yonse ya UTM pitiliza kusunga ulemu wanu komaso ndi kukweza mbendela ya Malawi komaso mokomela amalawi chezezo la ndilakuti samalani kwambiri musagulitse chipani chanu Ku MCP Ayi foundation ya UTM chakwela sakuyidziwa Ayi, chomwe akudziwa iye tonse alayasi koma zofetsa chisoni Kuti chakwela Anantchola bridge yowolokela tonse alayasi zomwe zikutathauza Kuti chakwela sakuwelengaso Za tonse alayasi chonde chonde ndalama zimene akukoza a MCP including president Kuti akupatse inu ndikuopa mulungu wanu Musalandile Ayi chifukwa zimenezo sindalama ayi Koma ndi mwazi wa president wanu komaso Kuti Ife amalawi tipitilize kukusapotani , ndi mbili ya bwino inuso mukuona amalawi ndi Mene alusila musakhale mu gulu lonyozedwa ndi amalawi chifukwa cha ndalama mudzakhala wosowa mtendele Moyo wanu , tikumbukile Kuti silikali wa kuzomba uja Anati ine ndinali komweko Ku chikangawa ndipo tibapatsidwa ma 10,000000 Koma ine ndenkha ndikulemphela kudya ndalama iyi chifukwa cha mwazi wa chilima Muthu wosalakwa god bless UTM party including all the members